Amene amaiziwa M fucken CP sanavotere chipani chopanda chisoni ichi. Chinapha anthu ofunikira,anthu alephera school because of fucken MCP. Kodi njoka ukaiphwanga diso mkuthawira ku mphanga pakapita five months imazakhala njoka kapena buluzi??? Chipani Cha Richard Amestrong ichi
Ngati zithu sidzitsika,tionana pa 2025, alliance ichoke, Anthu akuba kupotsa dpp,tionana pa May pano.ndipo,kulozedwa kuba vote yanga,tikutyolani ma kosi one by one.
Munkauzidwa za MCP Koma kusamva lero mukulira ndiye akutitu mpaka 2025 ndipo adzawinadi mwachinyengo ngakhale mudzapite Ku khothi mudzaluzanso chifukwa akhothi wo nso adawagula
Eeee komatu apa ndiye olo azayitanise MDF yose koma kungochitika chibwana chimenecho sitizamayendaso misewu komano makomo mwawo, komaso ma khothimo kukawapasa war yomwe iwowa akhala akuipepha kwa nthawi yaitali and they will get it if they try such nonsense
Amalawi vuto lake timavota ndi emotions chifukwa choti chakwera ndi Chilima wakugulirani nthumba lachimanga, wakupasani tindalama toti simungadye even in two days inu mwati uyu ndiye ndi deal azatisunga osadziwa kuti akukutchelani matchela, kuvota kotereku kwa wonongesa Malawi lero kodi muzayamba liti ku vota ndi dzeru? Onena adanena, olakhula anakuuzani musapatse chiongolero munthu yemwe sakudziwa za m'boma inu mukamuseka kumuona ngati ndi mwana komaso chitsilu lero ndi izi mawu akulu amakoma akagonera. Malangizo anga ndi oti tamavotani ndi dzeru please osati mwa emotions chifukwa mukatero inuso muli gulu lovuladzitsa amalawi ndipo ndi zija amakuyakhani kuti ine sindinakutumeni kapena kukukakamizani kuti mundivotere.
Government is composed of three categories 1 Reason(rulers) 2 Guardians(soldiers, Judiciary etc) 3 Appetites ( civilians) It is the responsibility of the rulers to come up with reasonable decisions and actions to see to it that the needs(Appetites) of the citizenry are timely addressed .... The guardians ( soldiers, judiciary) have a responsibility to see to it that the rulers are protected... Sugar is a one of the most important basic nutritive food value that the body needs daily for it's energy source and sound functioning Denying energy to the citizenry is akin to almost killing them...life is energy ...one can not act or think well without energy It's confusing to understand what this gvt is priotizing on This leadership is insensitive to the needs of it's people and doesn't deserve to continue being on the driving seat of government affairs
The same courts that helped u ascend into power u now blaming them. Why do u NGOs comment when MCP is being disadvantaged?? Courts are always favouring Nankhumwa for leader of opposition in parliament but u are not commenting. U have to be impartial for people to put trust in you. Otherwise fighting Illovo is fighting against your own fiscal that allow for price elasticity. I have noted with regret that DPP has been losing almost 100% of their court cases, most oftenly unfairly but none of the NGOs stood for DPP. I f u need people to stand with u, stand with DPP first to remove Nankhumwa as leader of opposition.
Koma mose muja tayambila mpaka pano sakutsika sugar ngati kulibe president abale ai zikomo .mesa president akalakhula zithu zimatheka pompo pompo koma ai ndithu kuli ziiii
I as a Malawian am very sure that this sugar crisis is politically influenced. There certain people who are behind this crisis so that MCP should be blamed. ILOVO should be inquired.
I don't think so...your assertion would be reasonable if we could have seen gvt taking some serious steps to work hand in hand with the responsible companies on how skyrocketing of these prices could be contained or cushioned...but i am sure you can agree with me that government is just quiet as if nothing is happening... This explains the weakness and insestivity of this Onse Alliance Gvt
Sugar wadula ndithu kuno ku South Africa 2kg R50 imene kumalawiko ndi 5000kwacha koma kumalawi 1kg 4000 it's too much
All these days where were you??? We already lost hope in all government and non governmental organisations in Malawi 😢
Amene amaiziwa M fucken CP sanavotere chipani chopanda chisoni ichi. Chinapha anthu ofunikira,anthu alephera school because of fucken MCP. Kodi njoka ukaiphwanga diso mkuthawira ku mphanga pakapita five months imazakhala njoka kapena buluzi??? Chipani Cha Richard Amestrong ichi
A malawi sitimva agalu awa anaziwika paka mpain kuti sangakwanise ndiizi lero anthu tikulira muzaonaso 2025 MEC ikupanga chinyengoso
Iwe ndee wanena zoonadi
Sugar Peter Munthalika anali pa K700 😂😂😂😂😂😂 koma panopa Ali pa K4000😂😂 my Malawi 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 MCP ai zikomo tiyeni nazoni😂😂😂 Bagamoyo party
Amalawi ife ndife anthu opusa kwambiri,osaziwa zimene tikuchita anthu akuononga ziko tikumawa yang,anila, tiphesa ana amalawi zukani osagona
Ngati zithu sidzitsika,tionana pa 2025, alliance ichoke, Anthu akuba kupotsa dpp,tionana pa May pano.ndipo,kulozedwa kuba vote yanga,tikutyolani ma kosi one by one.
Amalawi amakhalira kuthamanga daily atii Peter Muntharika achoke lero, chimanga 60 thousands kwacha thumba by Chakwera nthawi ya Peter Munthalika chimanga Thumba linali 3500 basi chimanga kumapezeka paliponse kubwera sugar Anali mbweeeee Koma panopa amalawi munkafuna zija ndizimenezizi ndithu 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Keep it up amalawi anthu otseketsa inu😂😂😂😂 ndi Chakwera wanuyo komanso Chilima wanuyo 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Mumati chakwera chakwera si zimenezo
Ineyo ndine walilongwe koma chakwwla achoke galu kwambili
2020 Chakwera akazati ndibweletsa nkhondo kungoti sindinatenge bomaa😂😂😂😂😂😂 Lero ndiizi anthu akufa ndi njala mmmmm 😂😂
Mcp ndiyoyipadi apa takhulupirira asatanatu amenewa
Ndipo compain ya MCP imkachitika ngakhale m'Mipingo😂😂😂😂😂 ndizimenezo Ambuye adayankha.
Nice talk bakili muluzi TV simanama
Malawi okomera tonse uja ndi ameneyu.. Tankhala tikumulilira uja ndi ameneyu
That's what you wanted malawians! You know that mcp is a party of vilombo.
Mumafuna kuona zina ndizimenezi
Koma ndipo
Zowonadi shuga wakwera kwambili chilichonse m'malawi Chakwera ndithu ndiye amalawi yesesani kuchitapo kanthu..mapeto ake anthuwa akungofuna kuti pochoka M'mipando afuna azatisiye pamoto
President wanthu ndichisilu kwabasi
Kumakweza zinthu ngati wagwa manyii
Iwe Lazarus iwee
Munkauzidwa za MCP Koma kusamva lero mukulira ndiye akutitu mpaka 2025 ndipo adzawinadi mwachinyengo ngakhale mudzapite Ku khothi mudzaluzanso chifukwa akhothi wo nso adawagula
Eeee komatu apa ndiye olo azayitanise MDF yose koma kungochitika chibwana chimenecho sitizamayendaso misewu komano makomo mwawo, komaso ma khothimo kukawapasa war yomwe iwowa akhala akuipepha kwa nthawi yaitali and they will get it if they try such nonsense
Ndizomwe mumafuna amalawi.. mademo Anu aja ndi amenewa munaika anthu okuba
Eti eti akulira chani?
Ndinu nomwenso azimayi mukutengeka ndi ma k2,000.00 akugawidwa ndi zitsiru za mcp.
Ndipo palibe muthu opwetekesa mtima ngat mzimayi, mmmmm
Eti sukunamadi nda usiru azimayiwa amangotengekq
Satana ali nkati mwaomo mwa atsogowo 😢
Azimai inu ndi ausiru busy nditima 2000 kwatcha
Athu tikuvutika ku malawi chifukwa cha president chakwera
Thanks so much keep getting please its too much
Amalawi vuto lake timavota ndi emotions chifukwa choti chakwera ndi Chilima wakugulirani nthumba lachimanga, wakupasani tindalama toti simungadye even in two days inu mwati uyu ndiye ndi deal azatisunga osadziwa kuti akukutchelani matchela, kuvota kotereku kwa wonongesa Malawi lero kodi muzayamba liti ku vota ndi dzeru? Onena adanena, olakhula anakuuzani musapatse chiongolero munthu yemwe sakudziwa za m'boma inu mukamuseka kumuona ngati ndi mwana komaso chitsilu lero ndi izi mawu akulu amakoma akagonera. Malangizo anga ndi oti tamavotani ndi dzeru please osati mwa emotions chifukwa mukatero inuso muli gulu lovuladzitsa amalawi ndipo ndi zija amakuyakhani kuti ine sindinakutumeni kapena kukukakamizani kuti mundivotere.
Boma ilili ndi agalu okhaokha angokumana
Sitilowelela mayi muphuzile
Allahuma yarabii amiin ,mpangen kakanthu chakwela musasiyesiye mupange kanthu
Sugar waduladi kaya timwanso tea yo kaya?
Chonchi nkumakakamira itsogoleri mbava zimenezi
Government is composed of three categories
1 Reason(rulers)
2 Guardians(soldiers,
Judiciary etc)
3 Appetites ( civilians)
It is the responsibility of the rulers to come up with reasonable decisions and actions to see to it that the needs(Appetites) of the citizenry are timely addressed ....
The guardians ( soldiers, judiciary) have a responsibility to see to it that the rulers are protected...
Sugar is a one of the most important basic nutritive food value that the body needs daily for it's energy source and sound functioning
Denying energy to the citizenry is akin to almost killing them...life is energy ...one can not act or think well without energy
It's confusing to understand what this gvt is priotizing on
This leadership is insensitive to the needs of it's people and doesn't deserve to continue being on the driving seat of government affairs
Zokhumba moyo kuzuza sure
Sugar wa malawi ali ku Zimbabwe koma ali wochipa,kodi akupitista sugar kunja ndindani???
Pathumbo pawo anyani amenewa
Chakwera why 😢😢😢😢
kkkkkkkkkk akwefule ndani iwowo ndizomwe akufuna. ndizomwe amalawi amafuna
Vuto ndi usogoleli nothing else. even ma passport kulibe
Zikomo chakwera
Khani ndiyakuti amalawi adziwe kuti chakwela ndibuzi kwambili chitsilu akapanga zobela mavote koma akunama sawina ziona komaso akangoluza amangidwa aziona
Kuvotera gure wankuru kuyipa kwake nkumeneko
Zimene mumkafuna amalawi simunati munakalira Inu ndithu kuvotera mcp
Eeeee koma nkhani ya sugar tiyang'aneni ma bwana.
Sounds like Malawi is more of a capitalist economy than a socialist economy
Chakwera mchilima pathumbo panu
mwayamba kukamba zopusa sopano mesa ndizomwe mumafuna? pano PETER akufuna abweleleso mukuyankhulaso zopusa kusonyeza kuti kuti kumalawiko dzinthu zikuyenda bwino
The same courts that helped u ascend into power u now blaming them. Why do u NGOs comment when MCP is being disadvantaged?? Courts are always favouring Nankhumwa for leader of opposition in parliament but u are not commenting. U have to be impartial for people to put trust in you. Otherwise fighting Illovo is fighting against your own fiscal that allow for price elasticity. I have noted with regret that DPP has been losing almost 100% of their court cases, most oftenly unfairly but none of the NGOs stood for DPP. I f u need people to stand with u, stand with DPP first to remove Nankhumwa as leader of opposition.
Chakwela akufuika musamuvoteleso ndi galu kwambili chitsilu kwambili machende ake ameneyu
Unya manyi sumathi ukufuna kusinda dziko kwachosa adad
Amalawi saziwa kuvota
Chakwera mbava chimwendo mbava mkaka mbava kunkuyu mbava agalu inu mwaononga Malawi
Zoonadi sizikuyenda ayi
Kkkk alipheee chakwela zosamukhuza olo half kod akukweza sugar kulibeko
Vuto amalawi timadziwonongela tokha...kukonda kulemekeza chibwana
President uyuyu
Akupanga zithuzopusakwambili athuamanamizilanji alangidwebasi agalu opusa
Koma mose muja tayambila mpaka pano sakutsika sugar ngati kulibe president abale ai zikomo .mesa president akalakhula zithu zimatheka pompo pompo koma ai ndithu kuli ziiii
Deal ndi yake akumakagulitsa kunja apeze ma dollars adziba bwino nde angalankhule chani???
Mukamuvotera mfiti ameneyo mmmmmm mudzalira kuposa pamenepa akuti anali m,Busa wanji ameneyu
Mayo mowa ujaso wakwera bc
Sugar akhale pa mk900
Bagamoyo mcp 😂
Akapito a CAMA ati ziiii bwanji adya chibazi?
Kkkkkkk paja adati boma ili ndilosamva, mwina atopa nalo
💪💪
Atsitse basi
Tiyenipaground
Very sad situation.
😂😂 😂
I dont like Mcp,
I as a Malawian am very sure that this sugar crisis is politically influenced. There certain people who are behind this crisis so that MCP should be blamed. ILOVO should be inquired.
I don't think so...your assertion would be reasonable if we could have seen gvt taking some serious steps to work hand in hand with the responsible companies on how skyrocketing of these prices could be contained or cushioned...but i am sure you can agree with me that government is just quiet as if nothing is happening...
This explains the weakness and insestivity of this Onse Alliance Gvt