Kodi Mulandu Wa Chilima Ndekuti Watha? Bon Kalindo
ฝัง
- เผยแพร่เมื่อ 22 เม.ย. 2024
- On Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo is asking if the trip taken by Right Honorable Saulos Chilima, Vice President of Malawi to Tanzania signifies the end of Chilima’s corruption trial.
Ku Nyasa Voicebox, Bon Kalindo akufunsa ngati ulendo womwe Right Honourable Saulos Chilima, wachiwiri kwa President wa dziko la Malawi kupita ku Tanzania ukuonetsa kutha kwa mlandu wa Chilima.
#malawi
Good job
True man of Malawi 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥we love you Mr bon
Mawu! Mawu!
Mwana ooopsa kwambili 🔥🔥🔥🔥🔥
Bad Bone.. ❤GET UP Stand Up Malawi yoyoyoyo
Bon Kalindo Double salute
The DC rast man standing on true kunkhadxulu kunkhadxula The DC bon kalindo
We're follow you bwana DC ipondeni fadar congress yatikwana koopsa
Malawi tikufuna anthu ngati bone
Poyamba ndimaona ngati chilima ndi oona patali koma ayi ndithu, khwangwala weniweni
Go ahead boss
We are here bcoz of our economic depression.
Mr Bon Kalindo mumakwanila inuyo 😂😂...
Salute
Akungomubwadika chilimayo ndi munthu osaona patali monga anthu ena , mwachidule ndi osaganiza ngakhale pangono za zaka zonsezi anabanidwa ndi chakwera , amuoma kupusa chilima akanangokana osapitako
Akudziwana awa aaaa
Bon kalindo big of the biggest
Bonnie kalindo 🔥🔥🔥🔥
I wish I could meet you DC
Moto moto moto bwana zowona
A president anthu, problem after problem.
😅 kalindo the 1
Pangolin akatakwe
The DC mwana owopsa kwambiri umatiyimilira ife amphawi ife
The DC ❤❤❤❤
Neabor moto moto go ahead
Milandu ikudzigamula yokha apa basi....Chilima ndi machine bambo siza m'busa ofooirazi apa zonse akudzipanga apazi a MCP akummenyera Chilima Campaign ndithu
Palibe akumenyeredwa Campaign apa bwana koma akudzikoleka onse kuti wina asaoneke ngati ndi wabwino..nkhani ijatu ikukhudza onse nchifukwa Chilima amapempha kuti immune ya President ichotsedwe.
Koma yaaaah Nyanja yalandidwadi ndi Tanzania?????😢😢😢😢😢😢😢
Fuso lilipo kut kodi, Abon Kalindo, mwathandizapo athu agati omwe mutawadziwa kuti amalawife tikuvutika ndi njala, tikuvutika ndi uphawo osowa ndalama,
Monga inu a president athu ifeosawukafe mwationetserako chithandizo chanji popatul kutiyakhirirak kuboma?
AMalawi pepani boma likukomera Anthu womwe ali kustsogolo ,Malawi wanga tikanalipo kuzunzika ndi Anthu andalewa
Kalindo makwanira kwambri
Pangolini Bon Kalindo
A NEW THINKER WILL GOVERN OUR LAND SO HELP ME GOD
MCP and tonse alliance manyaka enieni
Azibabo 2:56
Apa zikusonyeza kt chilima alibe mulandu 🤣🤣🤣
Kalindo huma kwanaaa
Uyu ndiwamisalad
Ndie chirima azizati sindkuramura nawo ndgaru chirima
Pangolini eeeee
Chi Pangolin Bamboo Lastman Standing 🤣🤣🤣
Awa anabwela kuzatipha bas
Sinditha kugona osamumvera DC ndipo ndendimamva Naye kukoma nkamamumvera Kalindo ndipo osamasowa baba 😂😂😂
Pamenepo ndipo we mungadziwe kuti Chilima alibe mulandu ndizongopeka akanakhala ndi mulandu so Bwenzi atapasidwa ulendo ngati umenewo komanso zachita kuoneseratu kuti Chakwera akumuopa Chilima that's why nkhani yatero SKC 2025 BOMA ❤❤❤❤
The DC mwana oophya kwambiri.....Chakwela ndi Chilima ndi mbuzi za anthu
Go deeper the DC
Justice Kapindu ndidolo analamumula kuti passport ya Chilima asunge kumpanda pano watumima Chilima ku Tanzania 😅😊😮
The DC
Ana amuna obadwa masiku okwanira munthu opanda mantha kulankhula true story
😂😂😂 mr bon mmakwana
Akalindo ine ndimakhala kuno ku TANZANIA.. Koma zomwe zirikuno mwina CHIRIMA akanafkila pantete anthu akanamugenda chifukwa ASWAHIRI amadana ndi munthu okuba.. nde anthu akuno ndi okwiya kwambiri ndikubwela kwa CHIRIMA.. akuti kwabwela mbava yakumalawi kuno
Mmmm nanga Chocho athu oipa ameneo osamawalandila m,thamangitseni ndi miyala
Akulu kukhara mbava Chilima sakadatumidwa ndi boma ai komanso ndindale izi nanu tamazitsatani......Chilima akanatha kumutuma ku America ndipo zikanatheka koma eishhhh palowa ndale apa
I think n I bliv kut munthu uyuyu ndichitsiru chazitsiru zonse m'malawi muno
pangoline katundu waboma ndweyo born kalindo
Munthu opanda mantha uyu 😂😂
President wa anthu osauka kuno kumalawi. Boooon kalindo. The pangolin
😂😂😂 khaaaaa khoooo
Our pangolin 🔥 The DC mwana Woopsa Kwambiri BON ELIAS KALINDO 👍🔥
Zomvesa chisoni angowononga ndalama
Abusa opanda chiyembekezo awa
Matchine bambo
the Dc...ulemu wanu😅😅😅😅😅😅😅
Guys ndimatsuleni za Nyanja yathu pls, Mukufuna muzindiuza kuti Nyanja ya Malawi yalandidwadi basi ndi Tanzania?????😢😢😢😢😢😢😢 Pls reply me fast if it is possible
Ndimomwemo m,bale basi tiyeni tingosamuka m, Malawi muno kkkkk
@@user-eh1mg3ww6d 😃😃😃😃😃Eishiiii koma Tri ndie ndafooka nditanva Izi wanva mmmmm ndie tisamukire Kutiko m'bale wanga kuonera???😃😃
@@user-uc1pd1tc2x kwa amelica m,bale wanga bolasotu ngati passport uli nayo ngati ulibe wanya basi kkk chifukwa nao ma passport anasiya kupanga tili ku bagamoyo tu paja osaiwala kkkk
Yes
@@frankbanda7333 Koma MCP abale Anga inu ndi chani???? Ziwanda kapena chani??? Mmmm😭😭😭😭😭😭
Drama yokhayokha
Kalindo udzafa ndi nsanje. Keep fighting for DPP until 50 yrs if you will still be alive. Ndiwe munthu wokwana, wongobwebweta ngati galu wankutu. Pangani za phindu ku family kwanu osati kulimbana ndi atsogoleri. Mulungu adzakukanthamula. Ukuwanamiza a Malawi kuti ukuwamenyera ufulu and yet it's about your stomach now and then, and if DPP would win which is an impossibility. You lost your soul through anger and bitterness so watch yourself Mr Kalindo.
i hope ndiwe mulendo ku Malawi, coz uthenga uwu ukanawawuza a Timothy Mtambo ndi anzawo a Gift Trapence, who lied to multitude of people to vote for Tonse alliance as a game changer, yet the alliance is failing to organize themselves. so musiyeni kalindo aziyankhula. Malawians have opened their eyes. sangaputsitsidwenso
Ngt uli foreign usatinyase ndi nonsense ukukambazi
@VincentNgabuhvincent Ukunyasa ndiwe ndi umbuli wakowo ongosatira munthu without reasoning. Kalindo is being used by a political party coupled with his frustration in the Tonse government, which didn't provide what he expected as a personal gain. Now, what is making Kalindo hate the idea of Chilima going to Tanzania? Is he the judge and the jury? Does he have presidential powers? The fact is he's just another bitter dog trying to score a point from his sponsoring party and blind followers like you. Otherwise, akukamba zamanyi and zotsathandiza a Malawi. Kalindo is always negative even when something looks positive and worth the praise-a testimony to his bitterness and hatred of the leadership. Ngati Chakwera kapena Chilima amakunyasani , palibe adzakukakamizeni kuvotera iwowo, zavotereni Adadi anuwo. Choti mudziwe ndi chakuti anthu akuziwa za mkwiyo wa Adadi anuwo ndipo alibe chance chozawina chisankho, mark my words bro. Vuto ndi loti mumakonda ndale za mtundu, and that's a disadvantage to DPP in 2025; do not say I didn't alert you on the impending loss of your party in 2025.
Dc anakonza
Chofuntha ichi
Ofuntha ndiweyo ukumvera bwanji Za munthu ofuntha.
Ofuntha ndiweyo ukumvera bwanji Za munthu ofuntha.
🤣🤣🤣
😂😂😂 chisilu chakwela akuwona ngati ife amalawi ndife Ana ake stupid Lazaro iwe
Kulepheraso chizungu kkkk
😂😂😂😂 pangolin
This guy speaks for he's on benefits not Malawians I still remember the video window made saying amalawi siwowafela and what ever this guy does it's for he's own good
Komatu kalindoyi nsanje ikumupweteka,
Iwe ukuganiza Kuti boma litakupeza ndi chifukwa chokwanila silingakumange
😂