Komaso vuto amabungwe nanu si muli serious . Ena amabungwe andapereka masiku kuti ma passport sakutulukwa mokwabila minister wa immigration zikhale ng'oma atule pasi udindo koma mupaka pano akugwirabe ntchito only bon kalindo munthu wolimba mutima boma ili latitenga amalawi ngati zisilu.mcp ikanatha amene munayibweresa mitu ndiyo zungulira kwabasi anatizuza from 1964-1994 akutizuzatso 2020 -2025 hmmmm chipani choipa kwabsi sichizasintha
chabwino takuvani ife tidikira inu amabugwe Bola zimenezo mwanenazi muzikwanirise kodi mulipo mungomuyang'ana chakwera akuononga zikomo ayi takuvani
Siyinu nokha amene mwakhumudwa inoso zandinyasa kwambili
Komaso mulandu wachilima waumbavawo wawuthetsa bwanji mlanduwo chanukhayo nayeso ndiwakuba
Galu amene akuthesa milanduyo ndi mbavanso akulandila ndalama
Mukulu ameyu amaziva ngati wazeru ndiyenkha kuti azithesa milandu yakuba motere osapereka zifukwa wandikwiyisa kwabasi si munthu woti azikhala paudindo
Komaso vuto amabungwe nanu si muli serious . Ena amabungwe andapereka masiku kuti ma passport sakutulukwa mokwabila minister wa immigration zikhale ng'oma atule pasi udindo koma mupaka pano akugwirabe ntchito only bon kalindo munthu wolimba mutima boma ili latitenga amalawi ngati zisilu.mcp ikanatha amene munayibweresa mitu ndiyo zungulira kwabasi anatizuza from 1964-1994 akutizuzatso 2020 -2025 hmmmm chipani choipa kwabsi sichizasintha