Kuyakhula mosaopa Chakwera wamupha Chilima. Chifukwa cha udindo

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 23 มิ.ย. 2024

ความคิดเห็น • 180

  • @user-fm8ed7eo3i
    @user-fm8ed7eo3i 4 วันที่ผ่านมา +10

    Akulu eeee apa pa kanakhala kuti Pali anthu 10 ngati inu ayi dziko bwenzi likuyenda bwino. I like your style brother ❤

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 5 วันที่ผ่านมา +6

    Mizimu ya wonse omwe adawapha pa ngozi ya ndege ija iwanzunzedi anthu amenewa

  • @VeronicaChirwa-ct4os
    @VeronicaChirwa-ct4os 13 วันที่ผ่านมา +14

    Mwandiyankhulira bwino kwambiri. Ama radio onse sakuthandiza a Malawi. Kulephera kunena chilungamo zoona??? Amalawi muzichangamuka please!!! Ku Church ko mumapemphera chani? Ama Wailesi simunathandize or pang'ono, ndipo tataya nanu chikhulupiliro ma Radio 📻 oyipa panokha.

    • @manfredzalirabetha2440
      @manfredzalirabetha2440 4 วันที่ผ่านมา +1

      Ma radio osathandiza a mmalawi muno bola limpopo basi iyaa

    • @user-be5fc3ed1i
      @user-be5fc3ed1i 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Bora Limpopo FM yoha basi komanso ndi imene inasegula maso amalawi kuti ndege yagwera kuchikanga komaso anthu amwalira shame mawayiesi oyima panokha Lero ndimasiya kalekae kunvera hot current.yanga ndi Limpopo FM, Bakili muluzi tv ndi Boooorn kalindo ndi okha amene akutiuza chiungamo

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py 13 วันที่ผ่านมา +11

    Posatengera CHIPANI chilima adachita kuphedwa kumene achakwerawo akudziwa Koma pot CHOIPA chimakanidwa sangamvomere Koma MULUNGU akudziwa

    • @DorrahBanda
      @DorrahBanda 5 วันที่ผ่านมา +1

      Zoona

  • @LamieTiger
    @LamieTiger 13 วันที่ผ่านมา +10

    Vuto ndilot athu ena akuikira kumbuyo athu afitiwa athu ot akudalira mitsokho yathu Kut antchedwe olemera mipando akupheranayo nditimisokho tathu toja deleri kuzolowela Moyo osagwira ntchito Moyo opatsidwa zaulele chakwera wayetsa Kuno Ku church Kut udzilandila chakhumi mabatile ako

  • @OsmanBakali-s5x
    @OsmanBakali-s5x 5 วันที่ผ่านมา +2

    💔💔💔💔mpaka pano ineyo ndmangoona ngati a CHILIMA alipo sanamwalire ai.. I will still missing him in my heart ❤️ forever 😭😭😭

  • @MercyKachenje
    @MercyKachenje 13 วันที่ผ่านมา +10

    Mau amphavu awa vuto anthufe nsanje too
    Mulungu apitilize kitiululira zinsisi

  • @ThomasKaphwiti
    @ThomasKaphwiti 10 วันที่ผ่านมา +6

    Ndipo manganya siwakuno mayi ake ndi aku Zimbabwe muzikaona kuchenjera ngt akuba nkhuku😅😅

    • @samueljuma4452
      @samueljuma4452 4 วันที่ผ่านมา

      Kkkkkkk ngati akuba nkhuku???koma ndaseka

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 13 วันที่ผ่านมา +16

    Manganya ndi mfiti yotheratu ndagwilizana nazo

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du 5 วันที่ผ่านมา +4

    Amene anapha chilima panya pake 😢😢😢

  • @PaulMinofu
    @PaulMinofu 13 วันที่ผ่านมา +8

    On point❤❤❤❤

  • @GiftKananji
    @GiftKananji 13 วันที่ผ่านมา +8

    But how manganya did this? he looks like a sheep but he is a bad person, here Boni Kalindo is being punished because of this man eish that's very sorry

  • @cacksygustarf6260
    @cacksygustarf6260 12 วันที่ผ่านมา +3

    Voice ya nzeru❤

  • @Aisha-db6ds
    @Aisha-db6ds 4 วันที่ผ่านมา +2

    Iponden fadah 🎉

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du 5 วันที่ผ่านมา +3

    Manganya ndi fiti panya pamake plus chakwera 😢😢

  • @InnocentMlowoka-ew4lo
    @InnocentMlowoka-ew4lo 13 วันที่ผ่านมา +8

    Chilungamo kuwawa

  • @ThomasKaphwiti
    @ThomasKaphwiti 10 วันที่ผ่านมา +3

    Ndipo zoona tatiyeni a Malawi tionetse mkwiyo wathu Maliro ndiye tinayika kwa tsalano tithane ndizigawengazi😢😢😢😢

  • @mollymasangano473
    @mollymasangano473 22 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Well spoken my brother we can't keep Quite on what happened in our National, we are still mourning all who died on that day ,it SAD.

  • @BensonChilundu
    @BensonChilundu 4 วันที่ผ่านมา +2

    Micheal Usi ndi munthu ozikonda kwambiri.zoona zake zaoneka zokha chifukwa iyeyu sakadalolera kukhala Vice President.Koma abale ndalama zovuta ndithu

  • @YusufuKaifa-fr4wt
    @YusufuKaifa-fr4wt 5 วันที่ผ่านมา +2

    ❤❤❤❤❤❤my point president chakwera out

  • @user-dp7bc7yy6s
    @user-dp7bc7yy6s 11 วันที่ผ่านมา +4

    Muli speech yamphavu ndipo boma ili Mulungu achite nanu

  • @user-yo9rw8tr4s
    @user-yo9rw8tr4s 13 วันที่ผ่านมา +7

    Dosanama munthu Uyo walankhula mau wogwilika kwambile

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 4 วันที่ผ่านมา +1

    Osaopa osafooka tizafera mbendera yathu😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @ChimwemweBottomani-hc5ju
    @ChimwemweBottomani-hc5ju 2 วันที่ผ่านมา

    I was wondering how mr michael usi allow to bi a vice president as he was a vice president to late chilima😢😢 we was all.shocked to bi honest usi sanaganize bwino ...indeed they need to comfess ngati amakhulupiliradi Mulungu ....i salute you my brother n may u always bi protected

  • @paulinekayuni1621
    @paulinekayuni1621 5 วันที่ผ่านมา +1

    As for radio and tv extension I can agree I was expecting too for them kupangitsa conference yofusa mafuso representing people mafuso amene akufusa. Koma zinazo kaya

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 5 วันที่ผ่านมา +2

    Sanayankhuleponso amangophwisa mkhutu wa udindo usi

  • @GodisoneNoel
    @GodisoneNoel 13 วันที่ผ่านมา +4

    Zoona ❤❤❤❤❤❤❤

  • @HameedahMasambuka
    @HameedahMasambuka 13 วันที่ผ่านมา +8

    Ndipo kukumangan inuyo. Ndizakhala numbar one kusonkha ndalama yokuombolelan mmmmmmm

    • @user-jn2oc3cn3q
      @user-jn2oc3cn3q 5 วันที่ผ่านมา +1

      Kkkk km support iyi

    • @user-be5fc3ed1i
      @user-be5fc3ed1i 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      ​@@user-jn2oc3cn3qkkkkkkk kwachema

    • @user-be5fc3ed1i
      @user-be5fc3ed1i 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Chilungamo chiyende ngati madzi 😂😂😂

  • @AmandaConstance-fx8cr
    @AmandaConstance-fx8cr 13 วันที่ผ่านมา +2

    Not all days are Sundays
    God is watching and may there souls rest in peace 🙏

  • @ibrahimalfred6539
    @ibrahimalfred6539 12 วันที่ผ่านมา +1

    The power of massage and the power of prayer indeed

  • @ackimChiumia
    @ackimChiumia 7 วันที่ผ่านมา +2

    U are talking sense

  • @ruthkundwe7448
    @ruthkundwe7448 9 วันที่ผ่านมา +1

    Yesu anapelekedwa chifukwa cha ndalama yochepa,God have mercy

  • @LovelyBlini-cu3iu
    @LovelyBlini-cu3iu 13 วันที่ผ่านมา +6

    Mau amphamvu

  • @user-mw3kj4qz7b
    @user-mw3kj4qz7b 13 วันที่ผ่านมา +2

    So heartly broken dear

  • @user-ml8lk9dr7t
    @user-ml8lk9dr7t ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Yes may God perform wonders that the truth must prevail

  • @FelisterNgwira-op7rr
    @FelisterNgwira-op7rr 11 วันที่ผ่านมา +2

    Deotoronomy 29 ; 29 verse the secret things belong unto the Lord our God: but those things which are revealed belong unto Us and to our children ever, that we we may do all the words of this law

  • @user-mw3kj4qz7b
    @user-mw3kj4qz7b 13 วันที่ผ่านมา +3

    It's true my brother that's sad

  • @lyiemanganjira9708
    @lyiemanganjira9708 11 วันที่ผ่านมา +1

    Mulungu akuona zonse,,, ndipo samagona tulo. 😭😭😭😭😭

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 12 วันที่ผ่านมา +1

    Inu ndiye mwanena zoona brother mmmmmh ulemu wanu Inuyo shaaaa Ndamva nanu kukoma zedi❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @WellingtonHowahowa
    @WellingtonHowahowa 4 วันที่ผ่านมา +1

    Basi poti kulibe mulandu okupha ndimphezi ...mudiyeni chakwelayo azasowa omusumila

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma 4 วันที่ผ่านมา +1

    Manganya mpando kumeneko sanjoya akachita chibwana mkwiyo wa Mulungu umukantha koopsa tikupempheratu magazi a Chilima aja ayankhula usazione ngati wachenjera

  • @user-er7ub4ug7y
    @user-er7ub4ug7y 12 วันที่ผ่านมา +1

    Osaopa osafooka tiime pa chilungmo dziko lino nditose ndopo mbendera yake ndiii🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼situkukuopami😢😢😢😢

  • @FelixBoss-yn9pe
    @FelixBoss-yn9pe 10 วันที่ผ่านมา +1

    Enanu mudakangosiya kucommenter Ngati sizikukumvekelani bwino Ife nde tikumva kusekemela chipepeso chathu timachipeza kuzela kwaanthu amenewa chilima wathuuuu tizamfela

  • @georgejere2922
    @georgejere2922 13 วันที่ผ่านมา +2

    You will pay for it, what's wrong did our SKC do to you😭😭😭😭😭 the day will come 😢😢😢

  • @NaomieBanda-t6g
    @NaomieBanda-t6g 5 วันที่ผ่านมา +2

    Ndava chisoni

  • @Sabina-hw4js
    @Sabina-hw4js 13 วันที่ผ่านมา +2

    Ndi Ana omwe akudziwa

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma 4 วันที่ผ่านมา +1

    Koma izizi tu we are praying kuti Mulungu alange aliyense amene anatenga gao lokupha chilima pompano asadikile chiweluzo

  • @MtokomaYohane
    @MtokomaYohane 4 วันที่ผ่านมา +1

    And is true chakwera akukhunzidwadi and i have more questions

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 9 วันที่ผ่านมา +1

    Ambuye tipheleni Chakwera 😂😂😂😅😅😅

  • @YamikanChirwa
    @YamikanChirwa 9 วันที่ผ่านมา +2

    Ndpo mabala akutiwaw

  • @mariamahamadu8402
    @mariamahamadu8402 5 วันที่ผ่านมา

    Nawoso mayiko usi mbusi yamunthu kukonda ndalama kumeneko mpaka kulolela Kuti munthu ampedwe ndalama abale God bless you mukutidzegula mithu

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 5 วันที่ผ่านมา +1

    Chi Michael usi manganya that why amuika pa mpando iyeyo kuthamanga kukakwera pa mpando pakamaso gwaaaaa manganya

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 5 วันที่ผ่านมา +1

    Eyadi ndemweyooooo

  • @MirajiYusuf-vx5ux
    @MirajiYusuf-vx5ux 12 วันที่ผ่านมา +1

    Zoonadi brother ife tikulira ndithu esh infa ya chilima mmmm😢😢😢😢 mulungu 😢😢😢😢

  • @NoelLangwani
    @NoelLangwani 5 วันที่ผ่านมา +1

    Ndipoh zoonadi mwalakhula bwino ndithu broz man

  • @Marymahendra
    @Marymahendra 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    That’s true brother if it was khozi ya ndeka suit no trousers no shoes my

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 5 วันที่ผ่านมา +1

    Komad manganya anatidabwitsatu palibe chimene anayankhula pa za imfa ya Chilima an angokhala pheeee ngt sizikunkhudza zombvetsa chisoni kwabasi Mulungu yekha ndamene akudziwa zonse

  • @samsonpadiwa9185
    @samsonpadiwa9185 23 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Ndipo inu ka pangolin kamakhala chikwama mpaka kumugwira ndege ikulu ikulu osayipeza😂😂😂

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 13 วันที่ผ่านมา +2

    Zoonadi manganya ndi munthu oipa sanayakhulapo za imfa ya chilima

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e 2 วันที่ผ่านมา

    Ameni amen misonzi ya wanthu osalakwa simapita pachabe

  • @user-gk6bf7xe9g
    @user-gk6bf7xe9g 13 วันที่ผ่านมา +3

    manganiso anu ameneyo okay alibwino

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 4 วันที่ผ่านมา

    Chichakwera chakupa galu wacha be chabe kupa andu osa lakwa chaka chamawa ndipa fup mtikumana mbusi simenesi achakwera 😢😢

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py 13 วันที่ผ่านมา +2

    Atola khani afikapodi apasidwat ndalama kut akhale chete ndipo mulungu agwesere mulili mkabudura mwawo Kuti zokozera zawo zinyenyeke kuti AZIWE phamvu ndiukulu WANU mulungu wanga chilimat sadakwake ,osalakwq kwambili ndiuyu chakwerayi

  • @user-fm8ed7eo3i
    @user-fm8ed7eo3i 4 วันที่ผ่านมา

    Zoona awa ndiye mau bro end I love you so much brother ❤🎉🎉

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du 5 วันที่ผ่านมา +1

    Amalawi ndi amantha size😢😢😢

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 4 วันที่ผ่านมา

    Inu ndiye mwandilizaaaaa ineeeeeeeeee maliro awa ,A chilimaaaaaa inuuuuuuu😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw 13 วันที่ผ่านมา +3

    Zoonadi inenso ndikusiwa cho cho

  • @AjudantFombe
    @AjudantFombe 8 วันที่ผ่านมา +1

    Mudziwa bwanji chilungamoa Malawi ambili ndi osaphuzila ndipovuta

  • @user-wl4nd7ic1s
    @user-wl4nd7ic1s 13 วันที่ผ่านมา

    ❤❤

  • @MabvutoMichaelPanagona
    @MabvutoMichaelPanagona 11 วันที่ผ่านมา +1

    Bambo ndithu mwapeleka mitu akanakhala kuti amawelenga kapena kumvela ma media mwina akanaphuzira zina

  • @user-so7wg6ii5m
    @user-so7wg6ii5m 6 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Bambo inuo ambuye akutetezeni mwayankhura mau amphamvu kwambili ndipo mizimu yanthu amene anamwalira pangozi imeneija iwazuze achakwera komaso onse amene anatenga po gawo ambuye muchite nawo

  • @InnocentnMbale-zq8pk
    @InnocentnMbale-zq8pk 13 วันที่ผ่านมา +1

    Ndipo Inu eee ziko ili likupita kuti ndipo ine zundiwawa ndisaname ngati ndikufa ndife koma kumalawi anthu tili ndi mantha kwambiri

  • @PraiseCedar
    @PraiseCedar 13 วันที่ผ่านมา +2

    Unali bho koyamba kuja koma zalowa nsanje kwinako

  • @lyiemanganjira9708
    @lyiemanganjira9708 11 วันที่ผ่านมา

    Ili ndi pemphero la Ana a Mulungu,, ndipo akuona ndi kumva msozi wa aliyense... Mudzalira nonse munatenga gawo pa imfa Ya anthu amenewa 😭😭😭😭

  • @LoveHawabwa
    @LoveHawabwa 3 วันที่ผ่านมา

    Inu mwayakhula mawu ife tikuwopa kuyakhulapo mwatilakhulira mulungu awakanthe kopotsa

  • @AbnormalMk
    @AbnormalMk ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Nkhani ya Straight 200%

  • @RaymondKaumba
    @RaymondKaumba 5 วันที่ผ่านมา +1

    Ufulu umeneu wa anthu a misala

  • @ChilangoNdalama
    @ChilangoNdalama 9 วันที่ผ่านมา

  • @jamessheki4293
    @jamessheki4293 4 วันที่ผ่านมา

    Iwe ndiye munthu, Malawi tulo anthu kutipusitsa chonchi,tingoyang'anila ngat nkhuku mkhola ikaphedwa imodzi zina zimangoyang'ana. Mmmmm

  • @user-gi1gh9ry6h
    @user-gi1gh9ry6h 12 วันที่ผ่านมา +1

    Zoona anthu oyipa kwambiri magazi alimanji mwawo 😅😅😅

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 5 วันที่ผ่านมา +1

    Koma nde zoonadi ndithu watsala iyeo akuwona ngt sadzafa

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg 3 วันที่ผ่านมา

    Ndpo zoona zake bro 💥

  • @user-wl4nd7ic1s
    @user-wl4nd7ic1s 13 วันที่ผ่านมา

    🔥🔥🔥

  • @user-rk4ch1ly3z
    @user-rk4ch1ly3z 4 วันที่ผ่านมา +1

    Iwe ndiye walasa!

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 9 วันที่ผ่านมา +1

    Kulankhula chilungamo mopanda kuopa

  • @patrickndojime1632
    @patrickndojime1632 13 วันที่ผ่านมา +1

    Ndifiti Manganya mwana oyipa kwambiri chisilu chamunthu ichi galu kwabasi nkhankhankha uyuuuuuuuuuuu ndimapulani awo opusawo abvutika okha mitima mwawomo

  • @SebastianSauwa
    @SebastianSauwa 8 วันที่ผ่านมา +1

    Akuopa kumangidwa

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 12 วันที่ผ่านมา

    Yes ambuye atithandize abale eesh💔💔so sad

  • @user-rk4ch1ly3z
    @user-rk4ch1ly3z 4 วันที่ผ่านมา

    Pokhapo pokakamila u president next term, munawonesa kuti chilima simumamufunila zabwino.mukayakha kwa jahjah.

  • @HopeSaka
    @HopeSaka 12 วันที่ผ่านมา

    Mwatilankhulila father 😢😢😢

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Manganya umuziwe yesu ndiukachenjede wakoyo kupusa kwako Michael usi Mzimu wa chilima ukusate ndikukantha kwambiri

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e 2 วันที่ผ่านมา

    Zimenezi amalawi onse akuziwa zimenezi koma akuopa kuyankhula chilungamo monga chimenecho Mulungu akuteteze kuti upitilize kutiya khulila ku Mtundu wathu..

  • @GRACEKUMWEMBE-rv2se
    @GRACEKUMWEMBE-rv2se 3 วันที่ผ่านมา

    Aaaaa ndinu ophwasula ingopitani ku police mukanene umboni wanuwo

  • @IssahAluba
    @IssahAluba 4 วันที่ผ่านมา

    Koditu Ku Malawi kuyambira ama Radio komaso aa police angalu achabe,chabe alibe nzeru athu amenewo ndamene akuonoga dziko rathu

  • @FelixBoss-yn9pe
    @FelixBoss-yn9pe 10 วันที่ผ่านมา

    Kkkkk mimba zilikhutchu Ngati ogulitsa tomato oola kkk Koma big man

  • @Mervic-vm8eo
    @Mervic-vm8eo 5 วันที่ผ่านมา

    Osawopa osatopa osafooka 💪🔥🔥🔥

  • @SellarKasiya
    @SellarKasiya 12 วันที่ผ่านมา +1

    Or zbs yomwe tinkadalira PANO ili zii or tuzwen zoona program adangot duu

  • @Spaw-BTheGogoBoy
    @Spaw-BTheGogoBoy 3 วันที่ผ่านมา

    Like fact mau amanganya kukamba or kudabwa zammene chilima anamwalilira sananeneko ayi ithink izi ndi zoona

  • @HamidavioletYassin
    @HamidavioletYassin 4 วันที่ผ่านมา

    Akuti pangolini imakhala chikwama koma mumayigwila kukanika kuyipeza ndege koma yayikulu ngati imeme ija eshiii malawi walila ndithu

  • @AliceChipeta-pc3nb
    @AliceChipeta-pc3nb 3 วันที่ผ่านมา

    TTV ineso ayamba kundidabwisa mmmm simene analili something is happening ndalama inapha yesu