Zaululuka kuti Chakwera wapha Chilima

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 17 มิ.ย. 2024

ความคิดเห็น • 187

  • @BridjetFrank
    @BridjetFrank 27 วันที่ผ่านมา +11

    Wayankhulawe yehova akukuyang'na pa khani imeneyi

  • @MumbaPlayson
    @MumbaPlayson 27 วันที่ผ่านมา +3

    Condolences to you and the family.may the Grace of GOD be with you all.amen.

  • @Mpikamezo20-nt5dv
    @Mpikamezo20-nt5dv 27 วันที่ผ่านมา +1

    Kkkkk freedom of speech...from Mulanje

  • @user-tg3bl5ey9v
    @user-tg3bl5ey9v 27 วันที่ผ่านมา +3

    Koma akuyakhulawo siwangopeka coz mawuwo sakunveka mwa ndalama 😅😅

  • @mafukenimasangwi5487
    @mafukenimasangwi5487 27 วันที่ผ่านมา +2

    Onse akwiya apa ndi A MCP okha okha tiziona

  • @user-lr2wx5xd9d
    @user-lr2wx5xd9d 27 วันที่ผ่านมา +3

    Muziwe kuti mcp basi yatha mwapita ndipo tikumangani

  • @thondoyaenterprise3795
    @thondoyaenterprise3795 27 วันที่ผ่านมา +1

    The beuty of freedom of speech 😂😂

  • @DevidsamZikacha
    @DevidsamZikacha 27 วันที่ผ่านมา +5

    Ineyo ndikuona kuti m c p ingothetsedwa bass

    • @acklaschintowe
      @acklaschintowe 27 วันที่ผ่านมา +1

      Yes ayambe chipani china zoonadi

    • @jackiemayanika
      @jackiemayanika 27 วันที่ผ่านมา +2

      Isadzanvekenso mcp ipite ndi ma minister ankhanza onse asadzalowenso chipani chilichonse

  • @Wittie0505
    @Wittie0505 27 วันที่ผ่านมา +1

    Uyuyu ndiwabodza uyu😂😂 zochita kukonza izi😂

  • @LilyMbewe
    @LilyMbewe 7 วันที่ผ่านมา

    Munthuyu akubisa voice yaku kkkkk

  • @JustinLipipa
    @JustinLipipa 27 วันที่ผ่านมา +1

    Kkkkkkk komatu guys muzikhala serious

  • @user-im7sc2my4w
    @user-im7sc2my4w 27 วันที่ผ่านมา

    Kuyankhula zosamveka ,AMalawi ali ndi njala yofuna kumva zowona zosatira za imfayi .So try kubwelesa zinthu zomveka kwa anthu 😅😅😅😂😂😂

  • @Donvaga
    @Donvaga 27 วันที่ผ่านมา

    Chizungu chakecho eeeee😂😂km guys mumathatu kkkk😂

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 27 วันที่ผ่านมา +1

    longosola Fadah osawopa😅😅😅😅😅😅😅😅😅

  • @johnkambala692
    @johnkambala692 27 วันที่ผ่านมา

    Wait for investigation. Don't rush.

  • @user-zf9xs3zj9b
    @user-zf9xs3zj9b 27 วันที่ผ่านมา +2

    😂😂 Awa sanadye sizikuveka zomwe akuyankhula

    • @user-hm9nc7lz6e
      @user-hm9nc7lz6e 7 วันที่ผ่านมา

      Usakumva ndi iweyo ambiri tikumva ndipo zamveka bwino

  • @AngungaThatcherNgoma
    @AngungaThatcherNgoma 27 วันที่ผ่านมา

    Za boza izizi mumvere bho bho conversation yi. 😂

  • @user-ru8xm6sk2n
    @user-ru8xm6sk2n 27 วันที่ผ่านมา

    Kkkkkkkk mangidwa nazo izi

  • @wilbroadm
    @wilbroadm 27 วันที่ผ่านมา

    Ndapanga subscribe,.you will update us more.

  • @HalistarStreet
    @HalistarStreet 27 วันที่ผ่านมา

    Nice greys❤

  • @fidelixdezembro4599
    @fidelixdezembro4599 27 วันที่ผ่านมา

    Deus proverá

  • @ElizabethMaononga
    @ElizabethMaononga 27 วันที่ผ่านมา

    Mmmm lindani ofufuza .phuma bwanji?

  • @MustaphaImuran
    @MustaphaImuran 27 วันที่ผ่านมา

    😅😅😅😅😅😅😅😅 Nyasaland ayi zikomo

  • @enockdaisi1306
    @enockdaisi1306 27 วันที่ผ่านมา

    Aaaaaa choka iwe nawe. The way you are speaking uiungoganiza

  • @user-gg9hw4oj2v
    @user-gg9hw4oj2v 27 วันที่ผ่านมา

    🔥🔥🔥

  • @christophergibson72
    @christophergibson72 2 วันที่ผ่านมา

    Anthu mukangokhuta malo momakanyela basi busy tima voice zopusa

  • @BensonChizenga
    @BensonChizenga 27 วันที่ผ่านมา

    😮

  • @BrownMainje-sh7hj
    @BrownMainje-sh7hj 27 วันที่ผ่านมา

    agalu kkkkk musiyeni president

  • @noahmshanga-rb1xc
    @noahmshanga-rb1xc 27 วันที่ผ่านมา

    Oh! No! This is serious.

  • @user-rz6xh8qg5r
    @user-rz6xh8qg5r 27 วันที่ผ่านมา

    Ndiye apa akuti bwanji. Kikikkkk

  • @user-or7ng3fj8f
    @user-or7ng3fj8f 27 วันที่ผ่านมา

    Inu kodi mwadya chani kodi palibe chimene chikumveka apa 😢😢😢

  • @Donvaga
    @Donvaga 27 วันที่ผ่านมา

    😂😂😂 hahaha km guys et

  • @knacktricky8521
    @knacktricky8521 27 วันที่ผ่านมา

    😅😅😅 bodza lakeso nde yayitu

  • @marypatriciamakuru226
    @marypatriciamakuru226 27 วันที่ผ่านมา

    Mwayaluka basi, mu Chikangawa munali Mulungu si mutiuza bodzaaaaaa

  • @sokojane4015
    @sokojane4015 27 วันที่ผ่านมา

    Kkkkk zoyenda eshiii

  • @SildaKatundu
    @SildaKatundu 27 วันที่ผ่านมา

    Kalikonse tikaona ,muyaluka

  • @YamzyAmos
    @YamzyAmos 27 วันที่ผ่านมา

    Koma 😂iweyo amene wapanga audio iyiyi anakupanga

  • @rholingssambale8274
    @rholingssambale8274 27 วันที่ผ่านมา +1

    Lankhulani chilankhulo choti muthe kukamba zomveka bambo. Nkhani yanu ndi yoti chani yomwe mwabweletsa???

  • @burtonjere-wn3qu
    @burtonjere-wn3qu 27 วันที่ผ่านมา +11

    Kodi ukuti chani iwenso ??? Tayankhula zonveka apa asah !! Ngat ulibe zonena osangokhala bwanji ..

    • @mcsellahntv6896
      @mcsellahntv6896 27 วันที่ผ่านมา

      Zimenezi sizinanveke?

    • @user-im7sc2my4w
      @user-im7sc2my4w 27 วันที่ผ่านมา

      Waboza uyu

    • @usseintomasbacar8612
      @usseintomasbacar8612 27 วันที่ผ่านมา

      Munthuyutu sakuuza inu alipo amene amamuuza nde angotibenthulira

    • @alexanderntephea8706
      @alexanderntephea8706 27 วันที่ผ่านมา

      Chitsilu iwe iweyo ndi ndani? Watani Kodi? Sakunveka😮

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d 27 วันที่ผ่านมา +1

      Ife tikumva amene sanave zake zimenezo

  • @user-ry9ql9jv3y
    @user-ry9ql9jv3y 27 วันที่ผ่านมา

    Bozailo mukulephera chizungu kikkk

  • @WilliamKawaza
    @WilliamKawaza 27 วันที่ผ่านมา

    Akuyakhulayo ndindani kodi, sizochezeratu izi

  • @user-ty4pq5ub3q
    @user-ty4pq5ub3q 27 วันที่ผ่านมา

    😂😂😂😂 Koma abale....

  • @LinessdorisScot
    @LinessdorisScot 27 วันที่ผ่านมา

    Mwamupha wapita basi,, kwasala muziphanano nokhanokha, ife as time goes tilimba mtima

  • @AbelPeter-mm9fz
    @AbelPeter-mm9fz 4 วันที่ผ่านมา

    Akulu lankhulani zomveka mukuzilumaluma bwanji

  • @RitaKainga
    @RitaKainga 11 วันที่ผ่านมา

    Palibe Chinsinsi padziko lapansi, Mulungu amavumbulutsa zinsinsi zobisika angakhale pa nsi panyanja

  • @GwejeNundwe
    @GwejeNundwe 27 วันที่ผ่านมา

    Ngati ndimtukwane namachende ameneyu mxxx zaziiii

  • @VioletMaseko-ys4cu
    @VioletMaseko-ys4cu 27 วันที่ผ่านมา

    Koma bodza lakelo😊

  • @OFG-th3st
    @OFG-th3st 27 วันที่ผ่านมา +1

    😢😢😢😢

  • @user-ox6rc2wn1p
    @user-ox6rc2wn1p 27 วันที่ผ่านมา

    Boza iwe

  • @sfelanchirwa4190
    @sfelanchirwa4190 27 วันที่ผ่านมา

    Mmmu Kodi ndani amenei?😮

  • @Christopher-xc2ey
    @Christopher-xc2ey 27 วันที่ผ่านมา

    Tayakhulani zomveka man mukuti chani kodi

  • @SmartJumbe
    @SmartJumbe 27 วันที่ผ่านมา

    Machende tazirankhura zinthu zazeru Machende ako wanva ukumuyikira kumbuyo chakwera bwanji

  • @user-ty5wq9js8f
    @user-ty5wq9js8f 27 วันที่ผ่านมา

    My heart is totally broken due to Mr chilima's death, but I can see that this guy is lying. Uyuyu asatipusitse pano. Nthawi zina chilungamo chimadziulura chokha.

  • @laureenshaibu
    @laureenshaibu 27 วันที่ผ่านมา

    Voice of poor person iyi

  • @ivymakiyi
    @ivymakiyi 27 วันที่ผ่านมา

    Umbuli at its best,,,,you want to hear what you think,,,,,,,

  • @ElizabethMaononga
    @ElizabethMaononga 27 วันที่ผ่านมา

    Za ziii.mungoliubwa lubwatu apa

  • @andrewchiusiwa3487
    @andrewchiusiwa3487 27 วันที่ผ่านมา

    Musokosa chabe apa

  • @jackmuhura1797
    @jackmuhura1797 27 วันที่ผ่านมา

    Koma chizungu chavutapo apa

  • @chifundocharles2348
    @chifundocharles2348 27 วันที่ผ่านมา

    MCP mudziwaso 😂😂

  • @efkayshaun890
    @efkayshaun890 27 วันที่ผ่านมา +2

    😅😅palibe2 chmene chikuveka mwadya koma

  • @user-tw9nl6ks9d
    @user-tw9nl6ks9d 27 วันที่ผ่านมา

    Mau a maluzi sasowa kmb edit yo mwaesesa ndithu

  • @Lloyd-gd6pu
    @Lloyd-gd6pu 27 วันที่ผ่านมา

    Tadzingodyani gwada opanda tomatoyo inu

  • @LilyMbewe
    @LilyMbewe 7 วันที่ผ่านมา

    Chidzungulilere 😅

  • @fidelixdezembro4599
    @fidelixdezembro4599 27 วันที่ผ่านมา

    Basitu apano zonse zaululika

  • @user-cj1nw7bi1k
    @user-cj1nw7bi1k 27 วันที่ผ่านมา

    Chitsilu cha munthu iwe ambuye akuone ndipo akuyendere ndithu

  • @ElizabethMaononga
    @ElizabethMaononga 27 วันที่ผ่านมา

    Osamaoneka kuchenjera pa gulu dekhani

  • @adamashrafi5875
    @adamashrafi5875 27 วันที่ผ่านมา

    Ukasuta uzingolima zitsiru inu

  • @MacBanda-df5zk
    @MacBanda-df5zk 27 วันที่ผ่านมา

    Kafukufuku ameneyo akhala opanda chilungamo ,this is Malawi ndikafukufuku uti unaphulapo kanthu kanzeru?wait and see.

  • @ReginaMhango-zn2iy
    @ReginaMhango-zn2iy 27 วันที่ผ่านมา

    Ayi tamva nawo zakuchipinda .. Ife tili chete kutchela nkhutu. Iponde fadaaaaa

  • @SteveZale-pf1gk
    @SteveZale-pf1gk 27 วันที่ผ่านมา

    kkkkkkk agalu awa

  • @NellxXebo
    @NellxXebo 27 วันที่ผ่านมา

    Mulungu oziwa kuweluza akupaseni madaliso ochuluka .

  • @sylviachitseko397
    @sylviachitseko397 27 วันที่ผ่านมา

    Kodi can't we wait for investigation to finish first? Stop this please aaah

  • @FelixMhango
    @FelixMhango 27 วันที่ผ่านมา

    Palibe funds yomveka apa timawona ngati muli ndi zinthu zogwilika. Komatu izi muzitenge bwino

  • @user-xx4jb9se3z
    @user-xx4jb9se3z 27 วันที่ผ่านมา

    Mukufuna mudziwe mau ake eni eni kut mumuphenso wadya koma akuopa kufa mcp kkkkkk

  • @user-cd4df3vg4y
    @user-cd4df3vg4y 27 วันที่ผ่านมา

    Mcp khalidwe lonyasa sangasiye awa dzigawenga zawanthu izi Mulungu akukantheni nonse amene mwachotsa miyoyo yabale athu asanu ndi anayi

  • @IssacMateyo
    @IssacMateyo 27 วันที่ผ่านมา

    Bodza lanulo mudzinama bwino big mani

  • @user-dp4lv6lo2o
    @user-dp4lv6lo2o 27 วันที่ผ่านมา

    Iwe

  • @tendaimakamabviko5916
    @tendaimakamabviko5916 27 วันที่ผ่านมา

    Iwee wasowa zochita eti .....kagone !! Palibe chomwe chikumveka zomwe ukulankhula....ndiwe Cadet takudziwa iiiiiiya ....ungoti kukamba Ichi kusiya kukamba Ichi kusiya kagwere uko shatapu !!!!!

  • @stevenghambi3471
    @stevenghambi3471 27 วันที่ผ่านมา

    Nde UTM mchita chiyani ndi chakwela???????

  • @ZungeniBanet
    @ZungeniBanet 27 วันที่ผ่านมา

    Washoke chakwel please matogo yake

  • @MarthaMbewe-uk5nn
    @MarthaMbewe-uk5nn 27 วันที่ผ่านมา

    Mudziona simunati aphwanga mfiti Inu akapolo inu

  • @khwimamtonga954
    @khwimamtonga954 27 วันที่ผ่านมา

    Chizungu chake

  • @MarvellousTech-kz6no
    @MarvellousTech-kz6no 27 วันที่ผ่านมา

    Za ziiii kusowa zochita ,

  • @FOSTERLUPIYA-zc1xv
    @FOSTERLUPIYA-zc1xv 27 วันที่ผ่านมา

    Pepani,God is with Malawi.U are trying to who?

  • @noelchitimbe
    @noelchitimbe 27 วันที่ผ่านมา

    Kape iwe

  • @Royhauya-uw2kr
    @Royhauya-uw2kr 27 วันที่ผ่านมา

    A government of national unity is possible but it will simply be to ransack the economy and go home.

  • @greymitomoni4047
    @greymitomoni4047 27 วันที่ผ่านมา

    kwachema😆😆

  • @AlexSymon-he1vt
    @AlexSymon-he1vt 27 วันที่ผ่านมา

    Zosaveka izo kubwebweta nenani zoona apa

  • @PaulMalemba-pp8hk
    @PaulMalemba-pp8hk 27 วันที่ผ่านมา

    Foolishness at it's best. Tiyeni tikalime kuminda uku andale asiyeni sugar anapanga kale

  • @DivalaKaphaka
    @DivalaKaphaka 8 วันที่ผ่านมา

    mcp nituvi malawi

  • @ChifundoChicco
    @ChifundoChicco 15 วันที่ผ่านมา

    Za nziii

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9o 27 วันที่ผ่านมา

    Zaziii kodi mukumsowa nkhani yoti mutchukire pano???

  • @franciscoduartie5762
    @franciscoduartie5762 27 วันที่ผ่านมา

    Chizungu chimenecho ungakumane ndi president...?😂😂

  • @user-lb8xz9lt3z
    @user-lb8xz9lt3z 27 วันที่ผ่านมา

    Kodi wamwa ambuye ntengeni akuyankhula apayutu

  • @williamsalexmbonga
    @williamsalexmbonga 27 วันที่ผ่านมา +2

    People of Malawi, greetings. How are you feeling? I know for most of you the pain of death is in your hearts, including Our President Dr Laz M Chakwela . Please let's take this time to unite and to console one another. Stop the blame game. It will not help us and our beautiful country. My fellow African brothers and sisters, I am also aMalawian citizen who loves his country deeply . Take the path of peace and stop destroying our beautiful country. The right honorable vice president will never return to earth. Just know that. Please honor his legacy by uniting your country. I am praying for the late vice president's family, our dear President and for the people of Malawi. Love is the way to go right now. I love you and will continue to pray for you . Williams Alex Mbonga

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 27 วันที่ผ่านมา

    Koma ndiye zawo Zada basi panopa aliyese waziwa Kuti MCP ndi ya kumpha ndipo yizakhara history mupaka kalekale

  • @user-us5hw4uy3t
    @user-us5hw4uy3t 27 วันที่ผ่านมา

    Iwe ndi kape fada wayaluka.

  • @DavidMtambo-zm8ne
    @DavidMtambo-zm8ne 27 วันที่ผ่านมา +3

    Achoke chakwera atinyasa kumpha vise wawo, nanga tikaasiya ampha angati.

    • @DavidMtambo-zm8ne
      @DavidMtambo-zm8ne 27 วันที่ผ่านมา

      Enafe timadabwa anayàmba kumamupasa tima trip osaziwa amamuikira mbeza kuti akodwe, ngongore timabweza achakwera simukanawina zisankho panonkha popanda saulos ,,

  • @NEBERTMVULA
    @NEBERTMVULA 27 วันที่ผ่านมา

    CHAKWERA, KUNKUYU, ZIKHALE NG'OMA, CHIMWENDO BANDA, MKAKA, CATHERINE HARA be careful Malawians are watching. MCP HAS ENDED; IT WILL NEVER EVER BE AGAIN!!!!

  • @festusmhango
    @festusmhango 27 วันที่ผ่านมา

    Za boza izi comfused cump ndi yomwe yikukoledzera moto