KU CHIKANGAWA NDIYE KWACHEMA UKU / ZINTHU ZAKE ZOVUTA🙌🙌

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 5 ก.ค. 2024

ความคิดเห็น • 392

  • @RiannahKaliat
    @RiannahKaliat 9 วันที่ผ่านมา +27

    Pempho langa ndilakut ngat chilima anaphedwa ndi anthu ndikut mzimu wake uwakathe ndipo asowe mtendere mpaka kare uwakathe

  • @RiannahKaliat
    @RiannahKaliat 9 วันที่ผ่านมา +34

    Imfa ya chilima mpaka lero ikumandivetsa mutu 😢Rip legend

  • @user-fd1tu6ku1r
    @user-fd1tu6ku1r 9 วันที่ผ่านมา +64

    The problem with Comrade Timothy Mtambo is that He's after Money so He has nothing to do with the development of this Country. He started as an Activist while His aim was to benefit something.

    • @sithandanechirwa6376
      @sithandanechirwa6376 9 วันที่ผ่านมา +8

      I also don't trust Timothy but if I overthink about the dearth of SKC makes me think that maybe Timothy lost direction because of the ruling gvnt. His mouth was shut by other elites who takes Malawi to their own hands

    • @HamiltonwaNamuwah
      @HamiltonwaNamuwah 9 วันที่ผ่านมา +5

      Ndi galu kwabasi ameneyi Timothy Mtambo

    • @MarthaJafali
      @MarthaJafali 9 วันที่ผ่านมา +3

      Timothy mtambo is a betray cos he was betrayed the who malawians some years ago I really don't like this gu

    • @user-nw6ie3xx8b
      @user-nw6ie3xx8b 9 วันที่ผ่านมา +2

      I love this brother but dyela

    • @user-zk7jw9up6m
      @user-zk7jw9up6m 9 วันที่ผ่านมา

      Zikomo mtambo

  • @emmanuelmukondia3568
    @emmanuelmukondia3568 9 วันที่ผ่านมา +16

    THE best way is you to prepare yourself with God. So that you are right with God.

    • @jamesgondwe6669
      @jamesgondwe6669 8 วันที่ผ่านมา

      God, how many times have we consulted God? How come that God fearless countries are more progressive than Malawi? Do you think we really survive death to claim heaven?

  • @jogechawa6192
    @jogechawa6192 9 วันที่ผ่านมา +5

    For the first time I agree with Mtambo .Sitimayenela kusangalala 6th July. Palibe chikukoma

  • @HarlodAndrewbanda-vf2rd
    @HarlodAndrewbanda-vf2rd 9 วันที่ผ่านมา +9

    We're still crawling to get there!! Rest in peace Dr SKC, UTM is a movement

  • @mishecksipolo7153
    @mishecksipolo7153 9 วันที่ผ่านมา +13

    That's too bad,and it's evident kuti chilima anachita kuphedwa,it just needs the youth to clean up this mess

    • @AbelSinoya
      @AbelSinoya 9 วันที่ผ่านมา +1

      Khala chete God knows ungatenge tsoka😂😂

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 9 วันที่ผ่านมา +12

    Mtambo thanks for the vital words.
    We now needs actions against these idiots in the government

    • @rexphiri6951
      @rexphiri6951 8 วันที่ผ่านมา +1

      powerful words Mr Mtambo

    • @ancientnkhata1137
      @ancientnkhata1137 8 วันที่ผ่านมา

      Only stupid people with commend the selfish and greedy Timothy Mtambo

  • @EdoJohn46
    @EdoJohn46 9 วันที่ผ่านมา +17

    Antambo 😂😂😂 ndikukutengeni ngati ndinu amene mudasongezera dzikuni dzamoto kuti tipse Malawi muno ndiwe galu kwabasi

    • @ThomasShuga
      @ThomasShuga 8 วันที่ผ่านมา

      Very true 😢😢

    • @MatiasMbaula
      @MatiasMbaula 7 วันที่ผ่านมา

      Very true

    • @MaggieCement
      @MaggieCement 6 วันที่ผ่านมา

      Ndipo Inu alibe umuthu uyu za ziiii mesa iye emweyi ndiamene anapangitsa kuti tilowe mudima akuonapanowo galu zedi

    • @wakisamsukwa9918
      @wakisamsukwa9918 5 วันที่ผ่านมา

      No matter how long you have gone the wrong road, turn back.
      Turning back isn't an offence

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus 9 วันที่ผ่านมา +10

    Amtambo...ngat mukufuna kut ife tikukhululukireni ...pitani ku mademo mutibwenzere dziko lathu...anthu akuopa mademo chifukwa alibe support...mabungwe onse chakwera adasiya abale ake mmaudindo

    • @LOKAMJ
      @LOKAMJ 8 วันที่ผ่านมา

      Exactly

    • @ancientnkhata1137
      @ancientnkhata1137 8 วันที่ผ่านมา +1

      DPP could have finished us . He did the right thing to rescue some of us from DPP. It was oppressing us

    • @InnocentMmanga
      @InnocentMmanga 8 วันที่ผ่านมา

      😂😂😂

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus 8 วันที่ผ่านมา +1

      @@ancientnkhata1137 oooooh ...May the curse of Almighty befall who is a lier...and make them the wood of hell fire

  • @dhaoudhiabedinegomaseko2363
    @dhaoudhiabedinegomaseko2363 4 วันที่ผ่านมา +1

    Mtambo mseu wa Rumphi Nyika Chitipa munawukana mesa munkaguba nkumaphwanya zinthu kuti musinthe utsogoleri

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 9 วันที่ผ่านมา +4

    SKC forever in our hearts 💔🔥 powerful words Comrade Mtambo Osafooka kms Osaopa Dziko ndi lanthu ife kuno Ku Ntcheu tili mbali yanu...

  • @user-te4ii6sz2v
    @user-te4ii6sz2v 9 วันที่ผ่านมา +5

    We quote more political speeches than prayers. This was not a political rally

    • @JosephHill-fy1bb
      @JosephHill-fy1bb 8 วันที่ผ่านมา

      Ntambo is not a pastor.... Just watch pastor's preaching time...

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023 9 วันที่ผ่านมา +9

    Ndikakumbukila ifa yaathu amenewa mtima umawawa

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj 9 วันที่ผ่านมา +5

    Mtanbo akuyakhula za ndale zikugwilizana bwanji ndi mwambowu

    • @ErickIssah
      @ErickIssah 9 วันที่ผ่านมา

      Ndipo inu

  • @user-ro1pl7rv7z
    @user-ro1pl7rv7z วันที่ผ่านมา +1

    Sometimes I wish Bakili Muluzi to come back again....
    Ligongo apano indu yayi itupile Draft kwabasi. 😅😅 Yangajenda Ata panondi

  • @JohnSingano-f1p
    @JohnSingano-f1p 9 วันที่ผ่านมา +2

    The voice of a lion always brings confusions

  • @user-bq5ev7de1l
    @user-bq5ev7de1l 9 วันที่ผ่านมา +4

    Apm my vote ✊

  • @user-zf9xs3zj9b
    @user-zf9xs3zj9b 9 วันที่ผ่านมา +3

    Wakuba mtambo akutiona ngati amalawi ndife galu anthu mwa sandutsa ndale ndi maliro a Dr saulos chilima 😂😂😂

  • @YohanePatrick-lc2lq
    @YohanePatrick-lc2lq 9 วันที่ผ่านมา +4

    Man ife amalawi tikufuna dpp enawa abodza ngati iweyo Timothy anakuchosa ku mcp chifukwa cha katangale

  • @LloydLuwis
    @LloydLuwis 9 วันที่ผ่านมา +4

    Keep morefire mr tman

  • @AndrewLanken-v3u
    @AndrewLanken-v3u 8 วันที่ผ่านมา +1

    He has got nothing to give malawians never

  • @emmanuelmukondia3568
    @emmanuelmukondia3568 9 วันที่ผ่านมา +11

    Idol worship

    • @user-jx8us9bc1o
      @user-jx8us9bc1o 9 วันที่ผ่านมา

      I totally agree with you

    • @user-nj1pv8hj2x
      @user-nj1pv8hj2x 9 วันที่ผ่านมา

      Ndipo live i agree with you big time 👍👍👍

    • @amourvido8027
      @amourvido8027 8 วันที่ผ่านมา

      And they don't realize it, they blindly do it💔

    • @hendrixchimalizeni750
      @hendrixchimalizeni750 8 วันที่ผ่านมา +1

      Usaweluze pakuti kuweluza ndikwake namalenga

    • @blessingskutchuwi8635
      @blessingskutchuwi8635 7 วันที่ผ่านมา +1

      Take it if it was your DAD.... 😔 Bwez iliso Idol worshipping

  • @JosephJosab
    @JosephJosab 9 วันที่ผ่านมา +4

    Mtambo ndi kape

  • @DannielOnions-fy3dc
    @DannielOnions-fy3dc 8 วันที่ผ่านมา

    Thanks so much 🙏 keep it up please we need people like 👍 u

  • @SteveKumwenda-t3d
    @SteveKumwenda-t3d 9 วันที่ผ่านมา +2

    Chitsiru ichi, ndiponso uku sikumapemphero

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 9 วันที่ผ่านมา +8

    mtambo walankhula za mzeru kuposa namachende chakwera

  • @user-ub1mw7ce5p
    @user-ub1mw7ce5p 9 วันที่ผ่านมา +4

    Well spoken, comrade Mtambo.

    • @KondananiNjakwa
      @KondananiNjakwa 7 วันที่ผ่านมา +1

      He has missed the trail. Uyu watha. Ndipo akamati ngati wina amawona ngati wayimisa agenda, atanthawuza kuti munthu wina anachita kuphedwa? Kulankhula kopanda nzeru

    • @KondananiNjakwa
      @KondananiNjakwa 7 วันที่ผ่านมา

      Nanga munthu angati anyamata oganiza bwino akumanena wena Lwarwa aaaah guys Mtambo anaganiza bwanji?

  • @ConfidenceBanda-g8k
    @ConfidenceBanda-g8k 9 วันที่ผ่านมา +4

    Koma ndipo poletsa kupepherapo ndie nduchitsiludi,mobwereza amene amaletsa kupepherayo nchitsiru

  • @cassimyusuf6683
    @cassimyusuf6683 8 วันที่ผ่านมา

    Well spoken comrade mtambo criticism singalephere as Malawian we were born like that, keep it up comrade

  • @TnmMpamba
    @TnmMpamba 9 วันที่ผ่านมา +1

    Watching live from Salima, Khombedza

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo 9 วันที่ผ่านมา +3

    That's true they is nothing to celebrate 60 years, it's like we help chakwera, kumkuyu ndi zikhale ng'oma kudya mitsonkho yanthu. Ayi momwemo 😂

  • @jonathanmalanda7742
    @jonathanmalanda7742 8 วันที่ผ่านมา +1

    A Mtambo ikani za mapemphero kuti mzimu wa skc uuse mumtendere

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 9 วันที่ผ่านมา +9

    More fire mtambo chakwera machende ako😂

    • @PhillspicJere
      @PhillspicJere 9 วันที่ผ่านมา +1

      You will gain nothing bro potukwana munthu wankulu, matsoka agwa pakutu panu

    • @LukeMkandawire-cr7en
      @LukeMkandawire-cr7en 5 วันที่ผ่านมา

      Watan😅

  • @SakanjiraRose
    @SakanjiraRose 8 วันที่ผ่านมา +1

    I'm getting confused, he is the man who mobilized people to fight a government that was to me far much better than the this one he helped to form.

  • @RitaKainga
    @RitaKainga 8 วันที่ผ่านมา

    Zikomo Inu nonse amene mwalimbabe mtima kupanga mwambo uwu though asatana akutchinga,Mulungu wathu ndwabwino,sanalepherepo,imfa iyi ndyovuta kuiiwala

  • @LunnahMtambo
    @LunnahMtambo 9 วันที่ผ่านมา

    More fire bro ,love from ccter namtambo cp

  • @LulezLele
    @LulezLele 9 วันที่ผ่านมา +2

    Kapolo uyu guyz akulubwa chani, mesa udapanganso ufitiwo at dat time kape

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 9 วันที่ผ่านมา +2

    LUWALA ANGASINTHE CHANI MBAVA YA MNTHU

  • @KenChitete-pg3ws
    @KenChitete-pg3ws 9 วันที่ผ่านมา +2

    Vote yanga yikupita kwa afford

  • @arthurmanyozo1289
    @arthurmanyozo1289 9 วันที่ผ่านมา +2

    Give your life to Jesus.The owner of your soul is Jesus

  • @AlinafeMuleso
    @AlinafeMuleso 6 วันที่ผ่านมา +1

    Ndipo ngati chilima anachita kuphedwa ndi anthu adzakhala osowa ntendere mpaka Ndipo ngati mizimu imakantha yakanthe anthu amenewa

  • @ChiletsoChembe
    @ChiletsoChembe 6 วันที่ผ่านมา +1

    Amalawi please! Let's pray to God forgive us and punish those who mudder saulos chilima

  • @vinceynyone6693
    @vinceynyone6693 8 วันที่ผ่านมา

    Viva mtambo Viva🔥👏👏

  • @AbdulKhan-j2h
    @AbdulKhan-j2h 9 วันที่ผ่านมา +1

    Mpava iyi atidye bawo bwanji Sumatuluka uli nduna pano abakuchosa ukufuna kodwela amalawi timaiwala

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani4921 9 วันที่ผ่านมา +2

    A ndale ndabodza kumene. Ndi chifukwa chake olo akuba ndalama zambiri-mbiri akavala amangokhala ngati avala chithumba chaku chigayo

    • @user-io2uw2me9f
      @user-io2uw2me9f 8 วันที่ผ่านมา

      😂😂😂😂😂😂😂

  • @ChilangoNdalama
    @ChilangoNdalama 9 วันที่ผ่านมา +2

    Big mtambo timakunyadiran

  • @WisdomMaseko-fi5sv
    @WisdomMaseko-fi5sv 9 วันที่ผ่านมา +9

    Koma tizikukhulupirirani ndithu a Timothy???

    • @DeliaKaduya
      @DeliaKaduya 9 วันที่ผ่านมา

      My question too 😢😢

  • @chrisschikozera7271
    @chrisschikozera7271 8 วันที่ผ่านมา +1

    Osaoopa ai......ku Malawi kulibe president

  • @EdwinMakwangwala
    @EdwinMakwangwala 7 วันที่ผ่านมา +1

    Only God is our rest not this politicians. God help Malawi

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 8 วันที่ผ่านมา

    Good Messnge Mr Mutambo

  • @AustinBornface
    @AustinBornface 8 วันที่ผ่านมา +1

    Malawi timakhala ngati tili pa stage tupanga drama kma ayi ndithu ndi action

  • @taombeedward5026
    @taombeedward5026 6 วันที่ผ่านมา +1

    The biggest problem mtamboyu

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 9 วันที่ผ่านมา +1

    Akulesa bwanji ma pephelo akuopa chani tiyeni nazo pephelo ndi chida

  • @JohnAsendi
    @JohnAsendi 9 วันที่ผ่านมา +1

    Antambo vuto chinthu chimozi mumafuna ndalama Chonde muzikhala ngati Born Kalindo chifukwa amati pavute pasavute asayimira amalawi ndipo akuti imila amangidwa amangidwanso pomwe enanu mumatifuna pomwe zakuvutani tikukukuwerenganitu INEYO NDIKUCHALENJA zoti wina aliyese aime payekha kuyambira Apita. Tupele. Raz. Nankhumwa. Shahana. Osati Chakwera Amayi Joyce banda ndi phulezdent Kalindo. Ndiye tikavote masankho mawa mwachilungamo mopanda kubela angawine ndi Kalindo chifukwa ndi amene akuoneka kuti angatithandize osati Ena inu 😁😁😁😁😁😁😁😁😁

    • @inessmsiyambiri8517
      @inessmsiyambiri8517 9 วันที่ผ่านมา

      Inuyo

    • @user-ww4ei5fb7d
      @user-ww4ei5fb7d 9 วันที่ผ่านมา

      Kalindo ndiolimba mtima, ofunika kumuvotera. 😂

    • @JohnAsendi
      @JohnAsendi 8 วันที่ผ่านมา

      @@user-ww4ei5fb7d zoonadi sister osati enawa akuoneka ngati akuti konda koma mmitima mulibe chikondi

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 8 วันที่ผ่านมา

    Exactly Andale akale achoke boma achinyamata alamulire dziko nkhalamba ndi mfiti komaso ndiankhaza

  • @VincentAndrew-jz2gf
    @VincentAndrew-jz2gf 8 วันที่ผ่านมา +1

    Atambo ,Ulibe Zelu unaphetsa Athu Ambili

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg 9 วันที่ผ่านมา +1

    Mtambo 💥💥💥💥

  • @user-ie5pc4ox8i
    @user-ie5pc4ox8i 4 วันที่ผ่านมา

    Ada awawa bwenz Ali MUNTHU wapamwamba kwambir kma Anapanga zausiru ngat akufuna timukhulukire ayambise mademo

  • @AndersonChiponola
    @AndersonChiponola 5 วันที่ผ่านมา

    Mtambo ndamene anapangitsa zonse izi palibe chomwe angayankhule Mutu wake sumayenda bwino ameneyo chifukwa anamuchotsa unduna wagwa nayo Mbuzi iyi

  • @Josehimba
    @Josehimba 6 วันที่ผ่านมา

    More fire comrade

  • @kamangamathias2001
    @kamangamathias2001 9 วันที่ผ่านมา +2

    What's the reason of kuwaletsa anthu ku phiri. Kiphiri kuli chani?

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani4921 9 วันที่ผ่านมา +1

    Dziko la Malawi likuyenda cham'mbuyo

  • @Anordchatha
    @Anordchatha 9 วันที่ผ่านมา +1

    Apm my vote

  • @user-wz1or9ud9i
    @user-wz1or9ud9i 8 วันที่ผ่านมา

    Mzimu wa chilima awasowetse mtendere anthuwa mpaka anfe amene anapha chilima.

  • @WiscotDzombe
    @WiscotDzombe 3 วันที่ผ่านมา

    Uku ngat kunari kumapemphelo ngat uyu anari compain amtambowatu safuna Bata Malawi koma kusokoneza

  • @markjames-v1f
    @markjames-v1f 3 วันที่ผ่านมา

    Chomwe mkukanikila kutiyimilira ndichan boss wanga

  • @SaeedHurzrut
    @SaeedHurzrut 8 วันที่ผ่านมา

    chilima wakuba ngati amwalira sangakhale wabwino Ife tonse tikuziwa zimenezo aphana pa gwilozano wawo

  • @CharityKangulero
    @CharityKangulero 9 วันที่ผ่านมา

    ❤❤❤ Exactly

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 7 วันที่ผ่านมา

    Good Messnge

  • @MagretIdimu-u7w
    @MagretIdimu-u7w 5 วันที่ผ่านมา

    We're heart broken 💔 SKC still remains in our hearts 😢😢😢

  • @PeterThomas-lw3io
    @PeterThomas-lw3io 9 วันที่ผ่านมา

    Rest in peace 🕊️ chilima anagwira chito yaikulu DPP mu
    2014 ikanafela giya komano chilima anapanga zotheka kuti Peter akhale tsogoleri muchomwechotso mu 2020 wayigwira ntchito yathangata kumuyika Crazy Chakwera akulamulila koma njilu ndikupanga mission plane yakumupha yooohhh Chakwera ngoyipa

  • @WilliamChopika
    @WilliamChopika 4 วันที่ผ่านมา

    God is our side nthawi zonse

  • @omarajibu860
    @omarajibu860 9 วันที่ผ่านมา

    Ndipo takonzeka kuchotsa masewerawa

  • @LimbikaniMakwandu
    @LimbikaniMakwandu 8 วันที่ผ่านมา

    Only chilima not you mtambo RIP CHILIMA

  • @nafejonga972
    @nafejonga972 9 วันที่ผ่านมา

    Rest in peace, my president .. we are still fighting

  • @GevinalaVictor
    @GevinalaVictor 5 วันที่ผ่านมา

    God still be my vote

  • @stevenchirwa5028
    @stevenchirwa5028 8 วันที่ผ่านมา

    Unatinamiza ndiwe tuu kut MCP 2019

  • @AnordNjoya
    @AnordNjoya 9 วันที่ผ่านมา +1

    ❤❤❤

  • @AlinafeMuleso
    @AlinafeMuleso 6 วันที่ผ่านมา

    Imfa yachilima ine sinfidzaiwala mpaka pano ndikulirabe ngati kuti anali bambo wanga amene anabereka ine koma sichoncho Ndipo mzimu wachilima ukuyendayendabe pakati pathu mzimu wachilima ambuye muulandire kumpando wanu wakumparadise

  • @YahayaUndiya
    @YahayaUndiya 9 วันที่ผ่านมา +1

    Mpira amauona ndi akunja big bolani osaiwala zimene mukuyankhulazi antambo

    • @jelsonmlowoka8611
      @jelsonmlowoka8611 8 วันที่ผ่านมา

      Anali momwemo mu galawundi bwanji zinamukanika

  • @GibsonBakha
    @GibsonBakha 8 วันที่ผ่านมา

    Andale inu musamatiwawitsemutu muma gofuna ndalama agalu inu

  • @user-bq8gb7tb1l
    @user-bq8gb7tb1l 9 วันที่ผ่านมา +2

    Viva mtambo

  • @tiwongehojaney5873
    @tiwongehojaney5873 8 วันที่ผ่านมา

    Amtambo naye ine ndinakhumudwa naye ndipo ndinataya chikhulupiriro mwaino mwatulukirano nthawi yonseyi munali momwemotu mu Timbaland wakudayo ndiye pano mukutinamizaso chani apaa iyaaa😊

  • @MorrisMapiri-d6z
    @MorrisMapiri-d6z 7 วันที่ผ่านมา

    It's not over until it's over. We shall shut up when we will be satisfied.

  • @AlinafeMuleso
    @AlinafeMuleso 6 วันที่ผ่านมา

    Munayambira kukonaza dziko mudzamaliza liti komanso palibe chimasintha mumaona ngati umphawi wamalawi ndiye podyera panu komanso polemerera panu palibe chanzeru chkmwe wayankhula mtambo apa

  • @HenriqKwilasi2022
    @HenriqKwilasi2022 8 วันที่ผ่านมา

    Iwenso ndi mfiti chifukwa ukupanga za ndale mtambo

  • @limbanikamanga7514
    @limbanikamanga7514 8 วันที่ผ่านมา

    A Minister of National Unity aja

  • @user-qs2tx7wt6g
    @user-qs2tx7wt6g 8 วันที่ผ่านมา

    Achinyamata ake ati angavele iweyo pathako Pako iweyo unakakhala wa mzelu unakakana undunaaa

  • @YasinAmidu-b7b
    @YasinAmidu-b7b 8 วันที่ผ่านมา

    The problem with us is that we are the ones that took evil to lead us

  • @HenryKeyala
    @HenryKeyala 9 วันที่ผ่านมา +1

    Mtambo mbuzi ya munthu

  • @user-ev3hl4hv4e
    @user-ev3hl4hv4e 9 วันที่ผ่านมา +1

    Akutitu ndi afana osata ngini mwana wapa Chitipa .moooooo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @user-lz4kc5ob1t
    @user-lz4kc5ob1t 8 วันที่ผ่านมา

    inetu ndimangokuveran anyamata a mcp ndimaziwa kt simunakumane nazo uyo mtambo ngat ndinu madolo kkkkk

  • @iqrahchikwenga8991
    @iqrahchikwenga8991 9 วันที่ผ่านมา

    Serious reverse gear ineed

  • @MACKDADFFDANIEL
    @MACKDADFFDANIEL 5 วันที่ผ่านมา

    Vuto athu kumalawi safuna kumenyela athu ovutika kom mimba zawo zomwe akuyakhula uyu ntambo ngati Ali ndi nzeru chonsecho momwe anali nduna samayakhula PAno anamuchotsa wayamba kuwalalatila athu omwe anawasiya a kugwila ntchito mbuzi ya muthu uyu ndipo ndipo ndiyemwe anapangitsa kut athu azivutika mpaka lelo

  • @AngellachifundoMwale
    @AngellachifundoMwale 7 วันที่ผ่านมา

    Mumatipangisa ndinu omwe muli ndikuthekela kolamula dzikoli koma chonsecho simutithandiza and iwee ntambo uli nkuyankhula koma osakwanilisa mxiii unduna uja unali pheeeee ife tikuvutika pano fukwa cha nzerru zomwe unatilimbikisa ife kuti tikavotere mcp yet lero ukuti usintha ziko mub 2025 yet wakanika zaziii

  • @GoodluckMwenifumbo-dk8jk
    @GoodluckMwenifumbo-dk8jk 8 วันที่ผ่านมา

    Anthu ambiri osutsa pano ndi a MCP
    Zoona mpaka kuwaopseza amipingo,a MCP mwafikapotu

  • @Patricenkhoma09Tricia
    @Patricenkhoma09Tricia 8 วันที่ผ่านมา

    Imfa yachilima imandidwalisa Bp daily😢

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 8 วันที่ผ่านมา

    Timothy ugwilizire utm please za u vuce uzisiye

  • @josephmsyali
    @josephmsyali 7 วันที่ผ่านมา

    Mtambo is the man