A Malawi Ukani ku Umbuli and fight for a good Cause..Chilima was Malawi's only Hope 😭😭😭...Jac up go and protest..Wise Words Sir..Go People Go We behind you
Acorrin Zambia ndalama zathu angogula mipango yadzaza ma suitcase koma mene a alibe ndalama kaya amai amene wa amaoneka ngati mwamuna tu ndi zikhale ng'oma amaoneka kaya ngati chani
Amalawi ndi amatha koopya,kaya kofunika titenge, anyamata ndi asikana aku Kenya kaya,kunena,zoona andale,anatitola,mumalawi muno.munthu,akusainila kuti zikwele muziko amalawi tinangoti chete.ku Kenya uko,kungolankhula asanamalidze,anatuluka, anthu.lero,akumufuna,achoke.
Inu,for example,ku south Africa uko,ana asukulu ndi omwe anasitha ziko lija.ku, Kenya uko kusitha, chifukwa,cha, anyamata ndi asikana.inuyo,mukaope kufa,iyaaa ndichifukwa mukulamulidwa ndima America,ndi ma rwanda.ma,china awa angoba, gold ndi diamond kumapita,nazo kwao.chifukwa,cha anthu ngati inu.demo sikuyenda,ngati mukupita,ku ukwati, imeneyo ndi demo?iyaaa.tikhala, nawo pa demo ikubwelayo mudzaone.
Zowona zake zimenezo anthu aku Malawi tikugona kwambiri osadzuka pa ifa ya vice president eeeeeeeeesh analoza ife anakwanisa eeeeee mabvuto tili nawo osayamba
Osatopa, osaopa osafooka tiyeni guys tiyimwe ngati anthu aku Kenya,Viva SKC Viva
More than 💯 agree iweyo walowa mmaganizo mwanga ndikuonjezanso... Thank you very much. I love it ❤️❤️❤️❤️❤️ TIYENI TIKAPANGE ZOMWEZO BASI
Iwe ndiye wanena zoonadi what we waiting for, Chakwera mtiti yokupha uchoke pita udzikaba chopekeka ku church
Guys let's go let's go am coming from Zambia chakwela out
Its Chakwela Ndi Cibwenzi cake cimakhala monyasa cisilu cija for me
A Malawi Ukani ku Umbuli and fight for a good Cause..Chilima was Malawi's only Hope 😭😭😭...Jac up go and protest..Wise Words Sir..Go People Go We behind you
100 percent correct lets go out guys
Acorrin Zambia ndalama zathu angogula mipango yadzaza ma suitcase koma mene a alibe ndalama kaya amai amene wa amaoneka ngati mwamuna tu ndi zikhale ng'oma amaoneka kaya ngati chani
Zoona zake,
Usazafe aise wandisengura kwambiriiii 👍👍👍
MUMUUZE CHAKWERA PANYO PAMAKE SITIMUFUNASO KU MALAWI KUNO MIKE UYU TIMUSOWESE KENAKO ZIKHALI MKAKA KABINETI YOSE KUIPONDESA KASIPA MOZI MOZI CHAKWERA WAKUFAYU UYU CHAKA CHINO MZIMU WA CHILIMA UMUGWILA PAKHOSI, CHAKWERA PA MTUMBUPAKO KOMWE ULIKO WAVA
Pepani president ameneyi ndi wa MCP...enafe tilibe
❤❤ zowona tituluka
Angakadye ku Parliament anthu akamapanga ma demo ndiye iwowo amaotcha katundu wa Malawi azawo osawotcha katundu wa boma ndi ma nyumba aminisry
Zoonadi Brother inuyo ndizoona ndithudi
Ndipo mene aphwera ngati galu saulosi chilima
But what is it that you have done apart from talking come we do together
Anthu muli ndimatha hvy ndiye kut abro wa sadalankhure zanzeru?
Amalawi ndi amatha koopya,kaya kofunika titenge, anyamata ndi asikana aku Kenya kaya,kunena,zoona andale,anatitola,mumalawi muno.munthu,akusainila kuti zikwele muziko amalawi tinangoti chete.ku Kenya uko,kungolankhula asanamalidze,anatuluka, anthu.lero,akumufuna,achoke.
Nthawi imeneyo mudali kuti boss kuti mutisogolere ziwawazo
Also you you are Malawian so you can start demostration 8:05 8:05
Vuto ndi ku Malawi kuno ifeyo ndihogona Kwambili
Akulu akulu bomali likutipweteka misokho phwi phwi. Wina nkumati zandale sizindikhuza . Akuluakulu andale atigulisa ku Azungu Kodi ndalama yathu yatha mphamvu bwanji . Asamunda akadatilamulira
Mautu awa
Zooonadi mau mphamvu kwambiri
Not Ali kutali aye inuyo tengane uthengawo wosati muone munthu kt akulankhulila kt chilungamo ndichimenecho kuotcha zosezo sanganene kt taononga katundu wathu mayazi
@@MartinKapanga-q6mimeneyo ndiye yofunika basi tidzaomba manja,mpaka liti.
Ulemu timapeleka kwa bambo kalindo enanu mukungokuwila kutali uko and ife titaphedwa kuno inuyo or mwana wanga simungamgulile ndi boxer yemweyi. Bwelani tidzayendele limodzi osati zongolubwa muli kunjako ayi
Inu,for example,ku south Africa uko,ana asukulu ndi omwe anasitha ziko lija.ku, Kenya uko kusitha, chifukwa,cha, anyamata ndi asikana.inuyo,mukaope kufa,iyaaa ndichifukwa mukulamulidwa ndima America,ndi ma rwanda.ma,china awa angoba, gold ndi diamond kumapita,nazo kwao.chifukwa,cha anthu ngati inu.demo sikuyenda,ngati mukupita,ku ukwati, imeneyo ndi demo?iyaaa.tikhala, nawo pa demo ikubwelayo mudzaone.
Chakwela ndi fiti
Tiyeni tikaotche konko
Amwene ndukhulupilila kuti muli kutali nde zisiyeni zidachitika basi palibenso angabwenzeletse miyoyo ya azibale aja. Inu mudalikuti?
Manyi akenso hule ameneyo
Zowona zake zimenezo anthu aku Malawi tikugona kwambiri osadzuka pa ifa ya vice president eeeeeeeeesh analoza ife anakwanisa eeeeee mabvuto tili nawo osayamba
Amwene ndukhulupilila kuti muli kutali nde zisiyeni zidachitika basi palibenso angabwenzeletse miyoyo ya azibale aja. Inu mudalikuti?
Tiye uko iwe nthaw zonse umakhara kumbuyo kwa mcp osaganizila zowawa zomwe zikuchitika mdiko muno