KU HOT CURRENT KWATENTHERATU

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 6 ก.ค. 2024

ความคิดเห็น • 45

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 8 วันที่ผ่านมา +4

    Hee bwanji pamaliro achilima munalephela kusegula mlomo chochi bwanji simunena kuti chakwera ali ndi dyela loipa mpaka kupha munthu sure chifukwa cha 5years😢😢😢 machende ake

  • @user-lb6ek3ee6d
    @user-lb6ek3ee6d 8 วันที่ผ่านมา +2

    Malawi ndi chitsazo chabwino cha kusauka koma zikukhala zovetsa choni kwambiri mpaka pano ma President adakalibelabe a Malawi ndi President yekhayo yemwe amandisangalatsa Professor Dingu wa Muthalika zimu wawo ukuse mu ntendere adasitha zithu kwambiri osati izi tikuziona panozi manyaka enieni the must go out stupid Government

  • @stevenchirwa5028
    @stevenchirwa5028 8 วันที่ผ่านมา +3

    Don't just talk we need action to change Malawi 🇲🇼

  • @yusufbakali
    @yusufbakali 8 วันที่ผ่านมา +3

    Nduna zaboma zosezakuba zimangidwe it only one way katangale akhoza kuta akamangidwa no belo ndende basi akagwire

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 8 วันที่ผ่านมา +2

    🙏🙏🙏🙏🙏🙏Anyamata lero muli bwino kwambili 🙏🙏🙏🙏🙏🙏

  • @JustinChiwale
    @JustinChiwale 8 วันที่ผ่านมา +1

    Khoswe akakhala pakhate sapheka Malawi we can't fight against corruption

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h 8 วันที่ผ่านมา +1

    Kkkkkk anyamata inu leroli ndakupatsani 100 pa 100 ❤❤❤ guys iyiyi ndiye hot current

  • @SamukLungu-zg7fl
    @SamukLungu-zg7fl 8 วันที่ผ่านมา +1

    Talk guys we are together but don't eat baz from chakwera

  • @ahmedmsume1489
    @ahmedmsume1489 8 วันที่ผ่านมา

    Akuonesana zikwanje inu lero mwatasa 😂😂😂😂

  • @RaymondKaumba
    @RaymondKaumba 8 วันที่ผ่านมา

    Vuto ndale zanthu zimapatsa mphanvu president.koma democracy parliament ndiyomwe imakhala ndi mphanvu yolemba ACB director azipanganso report Ku parliament basi

  • @g_forcemusician4242
    @g_forcemusician4242 8 วันที่ผ่านมา +2

    2025 we choose wisely

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 8 วันที่ผ่านมา +1

    Abida mia wapelekera bwino kwachakwera😂tiona dzinthu yakumbuyo😂😂

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 8 วันที่ผ่านมา +2

    Kuti katangale kuti athe muphe chakwera ndi chimbava choipa kuchokela kumpingo that's why he kill chilima

  • @paulpaseli6310
    @paulpaseli6310 8 วันที่ผ่านมา +1

    Lelo mwayakhula zokomela athu osaukano. Osati zachamba zanu zinja.

    • @williamdaka79
      @williamdaka79 6 วันที่ผ่านมา

      Apo mwanena ndithu omva amva

  • @user-wx1jt5fd2j
    @user-wx1jt5fd2j 8 วันที่ผ่านมา +3

    We need to change this leadership

  • @SheenahMwalabu-iz3pr
    @SheenahMwalabu-iz3pr 8 วันที่ผ่านมา

    Ajona mwamvatu malango anga kkk cz ndeumabowa bolako lero ❤

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 8 วันที่ผ่านมา

    Kumalawi tili ndivuto katangale sangathe. Chifukwa ndi culture. Katangale ngati mukufuna kuti athe choyamba president akhale oopa Mulungu komaso akhale osanama chachiwiri azikhala ndinthawi yotendera ma office mwazizuzi osawawuza anthu ogwira ntchito. Chachitatu a police a traffic army ikhale yachilungamo ndipo asavere boma pankhani za katangale. Simungathane ndikatamgale pamene oteteza ziko ndi amene akuchita katangale ndiye mukugani anthu angasiye katangale

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 8 วันที่ผ่านมา

    Nkhani ya police kuti alibe uniform sapata zili bwino ngati akuvutika choncho chifukwa apolice wo ndi amene akumanga anthu akamazuzula boma so azivutika motero

  • @Moses51
    @Moses51 8 วันที่ผ่านมา

    Chakwela ndigalu kwabasi

  • @SaukaniMbiliyawanda-ur7zb
    @SaukaniMbiliyawanda-ur7zb 8 วันที่ผ่านมา +1

    Amene sanachimweko ayambe kumugenda miyala

  • @TarPoor-ye9jx
    @TarPoor-ye9jx 7 วันที่ผ่านมา

    Lero ndaziwa kut anthu chilungamo akuchziwa koma mantha mcp ndi chakwera anthu atopa nawo kkkk 😂😂anthu amaba koma tonse yalepera pazonse kuba kuli pa high too much

  • @user-cf9yz3ei5o
    @user-cf9yz3ei5o 8 วันที่ผ่านมา

    we shall be singing like this for how long

  • @StevenMjMbama
    @StevenMjMbama 8 วันที่ผ่านมา

    Guys big up kwinako muzitchulako mayina aaaanthu amene akumapanga katangale

  • @AustinNkhula-j6y
    @AustinNkhula-j6y 8 วันที่ผ่านมา

    Ttv awunikileni anthu aziwe zenizeni tatopa ife ndianyapapiwa

  • @IssacMateyo
    @IssacMateyo 8 วันที่ผ่านมา

    Chakwela akufunika kuti achoke ndimuthu wakuba komaso dzikoli linalo bwino koma chakwela waononga kwambili zedi koma 2025 aona nyekhwe

  • @paulpaseli6310
    @paulpaseli6310 8 วันที่ผ่านมา

    Bon kalindo anayakhula kt aku prison akudandaula kt iwo palibe amapita muziwaganizila km mukati wamisala

  • @Austinyonah
    @Austinyonah 8 วันที่ผ่านมา

    Kuyankhula kwabwino

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py 8 วันที่ผ่านมา

    Ambuye mulungu wanga mudapereka mwana wanu modzi yekha yemweyo kufera ifeyo ochimwa kudzuzika yesu chifukwa chaife , kodi ngat mudalora mwana wanu modzi yekha kufera ife ,simungalore yehova wina osakhala mwana wanu kuti angofa yekha kutulo osadwara ai kuti afere ifeyo amalawi tatopa naye ndiy skhale Chakwerayu ambuye ndimvereni mbuye wanga Chakwerayi atifere ife chifukwa wanyañya tikumvutika musadzuze ndimatenda ai akangogona apitilirekonko kuti tipume mbuye wanga ndimvereni yehova chskwerat akutidxuza musakhare chete yehova akhoza kumayesa ngat mulibe phamvu ngat safera kutola koma afeeee chakwera kuti nduna zake ziziwe kuti inuyo mdinu owopsa yehova

    • @AustinNkhula-j6y
      @AustinNkhula-j6y 8 วันที่ผ่านมา

      @@Trancy-xt4py eee koma yaa

  • @HarryMsudzula
    @HarryMsudzula 8 วันที่ผ่านมา

    Sinanga ntchito zina akanatha kugwira aprison like kugadira mayeso ameneb anaipereka ku mdf omwe sizimayenera kutero malinga ndi nature yantchito yawo

  • @Moses51
    @Moses51 8 วันที่ผ่านมา

    Aphana 🤣🤣🤣🤣

  • @IssacMateyo
    @IssacMateyo 8 วันที่ผ่านมา

    Aona nyekhwe 2025

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu 8 วันที่ผ่านมา

    Lelo maimatu pachilungamotu kunenachoona chomwe ngakhale ife akumudzi tikuziona masomu boma ili linangolowelamo Kuba basi, chifukwa chilima anangomunamizila kuti apeze mphata Obama bwino, after kuona kuti bodza anapangila chilima kunamizila Kuba, anaona kuti kubako otsogolela anali chakwela chifukwa anatetsa mulandu cholinga amuphe chifukwa anadziwa kuti chilima amadziwa zonse. Chakwela chakwela iweyo mulungu azikupangila za bwino

  • @KanjoIsaac-u1w
    @KanjoIsaac-u1w 8 วันที่ผ่านมา

    Kkkkkkkkkkkk

  • @DalitsoulNchengah
    @DalitsoulNchengah 8 วันที่ผ่านมา

    Ulemu wanu

  • @user-wx1jt5fd2j
    @user-wx1jt5fd2j 8 วันที่ผ่านมา

    Anthu ena anagontha ku makhutu chifukwa cha matemberero

  • @peterchikwakwa8476
    @peterchikwakwa8476 8 วันที่ผ่านมา +1

    Kikikikiki

  • @MusaManati-ho4zf
    @MusaManati-ho4zf 8 วันที่ผ่านมา

    😂😂😂😂😂😂😂

  • @SandramKambalame
    @SandramKambalame 8 วันที่ผ่านมา

    Boma ilili ili ndi manyaka

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 8 วันที่ผ่านมา

    In Malawi we consider corruption as a problem.It is not a problem but the result of something.Therefore,to end corruption in Malawi we must list down main causes of corruption and get rid of them.

  • @giftmwango3214
    @giftmwango3214 8 วันที่ผ่านมา

    You don't know what you are talking about

  • @IssacMateyo
    @IssacMateyo 8 วันที่ผ่านมา

    Chakwela akufunika kuti achoke ndimuthu wakuba komaso dzikoli linalo bwino koma chakwela waononga kwambili zedi koma 2025 aona nyekhwe

  • @IssacMateyo
    @IssacMateyo 8 วันที่ผ่านมา

    Chakwela akufunika kuti achoke ndimuthu wakuba komaso dzikoli linalo bwino koma chakwela waononga kwambili zedi koma 2025 aona nyekhwe