iwe ndi mbuzi ku brantyle yake iti ine kwanthu ndikumeneko ameneyo wapanga chitukuko iwe wabodza kwambili unene Malo amene wapanga chitukuko nosenu ndi mbudzi musamanamize anthu
DPP my vote from Cape Town Stellenbosch south Africa...ine sindinaluzepo , DPP ikulamulila..... amalaw mwaziyonela yokha zomwe abusa anu akuchita....Alimbe mphatso ya utsogoleli chakwela,Koma
Kkkkkkkkk Koma walankhula mopanda Mantha Kuma kachulungamo kayenda ngt madzi mwakumbukila malemu Bingu achakwera angot ndwiiiiiii
Dziko la democracy ndichonchotu anthu saopa
Ndani angavotere zigawenga zakuphazi
Kkkkkkk ngat zomwe ana ronjeza paribe or chimozi chomwe wapangapo nde zomwe mkunturirazo apanga km marawi ndi ziko ronvesa chisoni kwambiri
APM my vote
Lazalo ali masaya vwapa kutsinkha misokho yathu. Waononga dziko Lazaro.
Kulankhula kwachamuna brother ndinu mamuna ❤❤❤❤
Mwalankhula bwino chikangawa akumva ekha
Apm my vote
This is good kumpatsa munthu apeleke madandaulo ake direct kwa president dziko litha kusintha sizabwino Kunamiza plesident
Bingu a man of legacy 👏👏👏
MCP my futu
😂😂😂
Ndagwilizana nazo pankhani yapansewu atrafic akunyanyila kuvutisa masewu
Machende ako .iweyo ungayelekeze BINGU ndi NAMACHENDE chakwera
😂😂😂😂
Mukulakwitsa akulu respect our leader 👑
😂😂😂
Grace Chinga Mofati i quote muzabwera chipani cha magazi Kodi ndi chiti Lazaro anakhetsa mwazi Kuti apezeke mamene Ali clueless presedent
a Mwamlima APA MUKUTETA.....😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
From Pretoria palibe chimene panga chakwela feteleza panopa tima Gula. 100 ,000 atipha.ameneyo my vote Peter basi, anati namiza Ngati ana ife
Dpp is my vote
I my vote is MCP
Kkkk nsonda wazimvera wekhat😅😅😅 nkhani ndi bingu
Reality wise men
iwe ndi mbuzi ku brantyle yake iti ine kwanthu ndikumeneko ameneyo wapanga chitukuko iwe wabodza kwambili unene Malo amene wapanga chitukuko nosenu ndi mbudzi musamanamize anthu
My vote dpp ❤❤❤❤❤
From Don yen mukukhonga chiyani ife sitikumusowa chikwera nkhwangwacho
Nothing will change , bcose MCP has come to destroy malawi ,
Wait DPP on 2025 to continue the development
Kkkkk uyuso waiwala, kuti masakho akubwera zakeyo ndi maplan
Yea yes ndili More more mr present!.
Apm my vote 🗳
Dpp ikulowanso take my word
Fake
Asonda mpaka Tay kkkkk nthawi yomweyi
Osangomutotola bwanji ndi chipolopolo galu ameneyu
A P M my vote
Chisiru presidenti wanu
This guy is so wise 🙊
Zapamsewu...wayakhula...bho traffic...imanyanya heavy
Chakwera my vote🎉
Zikakoma kumayamika....Mwayankhula mwanzeru mkulu wa Mavenda udindo ndiwanudi
Atumbuka paja kuyamikira manyii galu
Mp opusa kwambiri .....ngotukwanitsa kwambiri ndipo anthu sitichedwa kuiwala mphutsi imeneyi yazunza ndipo ikuzunza amalawi kwambiri mpka zoona mp nkuima kumayankhula zopusa chonchi? Kodi or atapanga zitukukozo anthu kutha kufa ndi njala plus kukwera kwa zinthu azapindulire ndani zitukukozo ana opusa kwambir chiuzeni chitsiru chanucho ndi nduna zake zoonandi anyani achabechabe
Ufunse e mp wanu
Atumbuka ndinu omvetsa chisoni wapanga chani chakwera
DPP my vote from Cape Town Stellenbosch south Africa...ine sindinaluzepo , DPP ikulamulila..... amalaw mwaziyonela yokha zomwe abusa anu akuchita....Alimbe mphatso ya utsogoleli chakwela,Koma
Chakwela ndi mbunzi yeniyeni
Pa apolicepo walasa sikokhakuno olo Ku luchenza tikuvutika ndi anthu amenewa Zina aziziona kukugwira mpaka katatu galimoto imozi yomweyo
Ase uzitipatsa khani zeni zeni nanga apopo chalakwika ndi chani ngat wina watukwanaaa
Chakwera anamenya back summer kuyimila ndevu😂😂😂😂
Mukuganiza azakonza zimenezo
😂😂😂😂😂😂😂😂😂 chitukuko chikuyenda koma kumubisa mmaso muthu tuuuuuuuuuuu
Vote dpp
Atidye nawo ndiyamene amayipitsa zina la president kuti mbiri zide
Dpp ndi chipani chamtendele
Dziko la Malawi likufunika anthu ngati awa opanda mantha
Mkuzeni mmwamba agwemo ekha chifukwa chauchitsilu wake pakuti saatha kuona ekha koma kunamizidwa ndie ,,,,2025 uziona galu iwe!
Koma Chimwendo ndi mbuzi kobasi ati amenewo ndie ma Vendor amafuna zakukhosi zomse zithere2 mutha kuchezera koma Richard Chimwendo ndi mfiti ndithu
Mfundo alibe uyu,,, kmaso molaro yake 😢😢😢zachisono
Wise man
Athu akumuzuzu ndinu ozungurila mitu njala ili chiriiii Eshìii koma athufe mavuto sazatha
AISE ukuwuza Chiwanda cha munthu, Chakwera tatu, Ndi Chiwanda mzimu woipa Ndi umene umamu lamulira taonani wangoti ndwiii nkhope yake Ngati kanga use, Chitsiru cha munthu Chakwera kusowa chikondi Ndi amzake Munthu womvesa manyazi,mbava Wanthu akufa Njala Dziko lonse la Malawi, chenjerani amalawi musagone muzaliranso Ngati Wanthu A Mu Babeloni
A police amafuna paper pass( ndalama)
Zovuta kwabasi
Koma mkuluyo zinthu akuziona kuti zikuvuta mumalawi .
Chakwera watitengera ku bagarmoyo.
Amsonda mpaka kuyiwara imfa yamzukulu wawo ali bize ku chipani kkkk
This munthu is very foolish zitukuko zake ziti i hope mwina akunena ku chikangawa chopha anthu 😢😢
Iwe machende ako bingu anali machine sungafanizile ndi namachende chakwela mbolo yake galu mbuzi
Achitsiru aja akt president omva zawanthu utiyo, kupusa ettt
Ndi chitsiru chotheratu galu ameneyi...asiyeni azipusisana chonchi zioneka
Aribe manyazii
Ntumbuka uyu ndiwopepela waiwala kale siwomwewo akadya usipa misika achina chipisi kukwela maminibasi lelo ndiawa alibize ndikugwilagwila tomato wazimayi misika koma iwe siungalankhule ngati vendayo kodi kolelayo wayambila mbado wachakwela
Library ya peter mutharika koma mbuli izi
😂😂🤣🙌
Kulankhula uku ikanakhala nthawi ya DPP , ma cadet akanampondaponda munthuyu
Ndipo amatha kurakhula mwazeru kuposa inawa amayakhula zomukomesa purezideti km uyu wayakhula bwino kwambili
Palibe chodabwitsa apa pulesident aziyankhulidwa
nde uyu ndi president omva madandaulo a wanthu???😂😂😂😂😂
Chisilu chaunthu chakwera
Amakataniko ku mzuzu Lazaro maglass ngati chiwala👺😔
Vitukuko vikwenda ,vikwenda kutiko?kumazinamiza pomwe choonadi mukuchodziwa zaziii amalwai ndifedi ombwambwana
Aaaa mwakumana iwe veendele wabhodza
Iwe mbudzi azingofika no without notice ndikwawo
Enawo akunamizan bwana
Kodi a chakwera wo bwanji manjawo tatingo'no
a tumbuka kodi munatani????simungamupatse mpata ENOCK CHIHANA koma basi busy ndi nyau z..
Nsonda Ali mutu biiiii satana wina wokalamba
Iwe suzawinaso basi kuyamikira zopusa basi wapangako chani chakwera ku mpoto kuno
Ukanangonasula kut kuwapatsa licence yachmanga akut ai akufna 20 pin apolice anyanya
Time is counting down
Apm more fire
Akufuna vote ka kkkkkk
kwizakoso kwithu Kono yayi 😌😌😌😌
Iwe wolankhulawe mutu wako iwe,,,,,..........kodi zimeme akuchita chakwera wakoyo sukuona mwina ukufuna ndrama ,...machende ako wamva,umuuzeso muzakayoasabwereso ku mpoto kuno azathawa
Koma chaka chamawa awuth
Munthu opanda umunthu chakwera, zithu zikukwera mtengo ngt kulibe mtsongoleri akunaminza akulakhulayo chilungamo udzachiona 2025 ngt ukuyesa kt anthu akukondwera nawe
UTM my VOTI
Kuyankhula kwa boh👊
Palibe chomwe angapange ngati dzomwe analonjedza olo chimodzi ndiye mukungotha mau man
Wayankhula bwino kwambiri munthu yu😂😂😂😂
Koma ndindani wachipewayo?
Dziko limafunika anthu ngati amenewa kulankhula mosabisa
AAA satana uyu iwe wapasidwa badzii kapena chani
banja la muthalika ndilachitukuko amalawi enieni osati galuyo ayi
Mr msonda kungoti chete chete kuona maso ankhono ndi kudekha kkkk
😂😂😂😂 ichi ndicha wise
😂😂😂😂
anthu ndiovuta mmmmm amangoyamikila zili zonse
Tikulya vitukuko yaye
ntchito pali maboma angati angomanga mbali yakwanu komweko
Kodi Ken nsonda wafunda skuff