Mafuta osinthanitsa ndi asilikali ku DRC; MCP yayambapo kubera chisankho

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 9 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 218

  • @joshuasamuel-vq2be
    @joshuasamuel-vq2be 5 หลายเดือนก่อน +4

    Am following you from Pretoria 🎉❤❤

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 6 หลายเดือนก่อน +12

    Poti asilikali a Malawi ndiopusa ndikale alolelanso zopusazo .
    But MCP never repeat on 2025

  • @johnmiselo2230
    @johnmiselo2230 6 หลายเดือนก่อน +2

    I love bakili muluzi tv news 📰 they tell the truth we are following you from Zambia

  • @HopefulCoralReef-tx4vx
    @HopefulCoralReef-tx4vx 6 หลายเดือนก่อน +4

    Thanks ulemu wanu big God bless you because you make us happy

  • @KondwaniChikapula-o5l
    @KondwaniChikapula-o5l หลายเดือนก่อน

    Thank you boss,,,we always appreciate you

    • @Outi-p7d
      @Outi-p7d 3 วันที่ผ่านมา

      Brothers n sisters tiyeni tigwilane manja Kuti ziko lathulino😢😢😢😢

  • @JailosDavie-sd3wq
    @JailosDavie-sd3wq 6 หลายเดือนก่อน +5

    Anthu amat akumangani ifeee kudandaula

  • @user-co7ut2zp2q
    @user-co7ut2zp2q 6 หลายเดือนก่อน +1

    Following mwachidwiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiii, you're genius keep it up

  • @DBF390
    @DBF390 6 หลายเดือนก่อน +10

    Make History ya abraham Lincoln

  • @abisalomchunga6695
    @abisalomchunga6695 6 หลายเดือนก่อน +1

    Good work .... amalawi chakwela akutisewelesa kwambili watikwana

  • @user-ov4wt4qs3x
    @user-ov4wt4qs3x 6 หลายเดือนก่อน +2

    Always your talking the truth story God bless you big man ❤

  • @LUCKYM4787
    @LUCKYM4787 6 หลายเดือนก่อน

    We are proud of you bg man, only you our hope

  • @StuartMlomboji
    @StuartMlomboji 2 หลายเดือนก่อน

    Keep it up our jenius

  • @MathewsMANDUTU-lh6oo
    @MathewsMANDUTU-lh6oo 6 หลายเดือนก่อน +1

    Amalawi chakwera wationongela dziko uyu,,,,, ndipo inu amene mukutaya nthawi pomuwombera manja ndinu opusa,,, anzakeawenga zokha zokh

  • @Emmy-y9f
    @Emmy-y9f 6 หลายเดือนก่อน +2

    Zikhale ng'oma anakufikapotu😂😂😂😂

  • @webstermbewe8395
    @webstermbewe8395 6 หลายเดือนก่อน

    Thanks for the update we have been waiting for this
    Confirm that

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h หลายเดือนก่อน

    ❤❤ chakwela basi dziko wayigulisa palibe za Malawi apa 😢😢

  • @masebermsanga7623
    @masebermsanga7623 6 หลายเดือนก่อน +1

    Always respect

  • @thumbikonkwawazingwe4334
    @thumbikonkwawazingwe4334 6 หลายเดือนก่อน +2

    "a Malawi akufuna kumwa Tea" 🔥🔥😂

  • @user-md2nf8gl9r
    @user-md2nf8gl9r 6 หลายเดือนก่อน +2

    Big up💪✊

  • @Arnoldkatunga-rg4gq
    @Arnoldkatunga-rg4gq 2 หลายเดือนก่อน

    Am following you, please may you Also teach us about Hutu and the Tutsi of Rwanda as Paul kagame is president of Rwanda

  • @user-oy2bu8vm4t
    @user-oy2bu8vm4t 6 หลายเดือนก่อน

    Best tv in africa

  • @johnkatapeh7182
    @johnkatapeh7182 6 หลายเดือนก่อน

    Respect brother❤

  • @LuciusByson
    @LuciusByson 6 หลายเดือนก่อน

    Respect to u brother

  • @user-hq6dq7zr1e
    @user-hq6dq7zr1e 5 หลายเดือนก่อน

    Yaaa Chakwela ndi dolo,
    Thank br for letting us know 😂

  • @EphilidaMtengabvumba-ld4df
    @EphilidaMtengabvumba-ld4df 6 หลายเดือนก่อน +1

    Kuyendetsa dziko mumawona ngati limayendetsa ndi dziko limodzi, amathandizana chinchilla ndithu

  • @user-tu5yi4oo7s
    @user-tu5yi4oo7s 6 หลายเดือนก่อน

    Salute big man

  • @jameskimu3961
    @jameskimu3961 6 หลายเดือนก่อน +1

    Best TV

  • @user-fd7fg1bx4y
    @user-fd7fg1bx4y 6 หลายเดือนก่อน

    God bless you boss please musamasowe chonchi

  • @silvainiesta3583
    @silvainiesta3583 6 หลายเดือนก่อน

    Thank you big wathu true story 🙏🏼🙏🏼☀️☀️☀️

    • @user-ko1lk3br4r
      @user-ko1lk3br4r 6 หลายเดือนก่อน

      Aaaa ine adzakambe za masambuka death paja peter muthalika akukhudzidwa

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x 6 หลายเดือนก่อน

      ​@@user-ko1lk3br4rBaai waikamba iweyo mesa ukudziwapo kanthu

  • @raymondchilimba7010
    @raymondchilimba7010 6 หลายเดือนก่อน

    I support good deal....
    Deal ili bwino kwabasi

  • @kubengovender6996
    @kubengovender6996 6 หลายเดือนก่อน

    We are together big man!!

  • @user-zh9kb2sj2i
    @user-zh9kb2sj2i 6 หลายเดือนก่อน

    Thank you blather ❤❤❤❤❤

  • @franciscochizimbi3398
    @franciscochizimbi3398 6 หลายเดือนก่อน

    Good documentary

  • @user-om7ol2mp6z
    @user-om7ol2mp6z 6 หลายเดือนก่อน +1

    Popanda bakili muluzi TV bwezi a malawi 🇲🇼 tili mu mdima

  • @user-si7po9sd5i
    @user-si7po9sd5i 6 หลายเดือนก่อน

    Our own legendary

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 2 หลายเดือนก่อน

    Chakwela you mast go Galu

  • @daniloahawadi4803
    @daniloahawadi4803 5 หลายเดือนก่อน

    Mumakwa
    I am Fom Moz 🇲🇿

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire หลายเดือนก่อน

    Kukatenga anthu ku D R C kudzaphera mu malawi,ndekuti ku malawi nde koimitira magadzi aanthu nde wafikapo mbusa ,

  • @davidkadyakapita8836
    @davidkadyakapita8836 6 หลายเดือนก่อน

    Respect Bossa yama Bossa

  • @SinsaKachale
    @SinsaKachale 6 หลายเดือนก่อน

    Ulemu wanu bwana ❤

  • @FrancisBanda-g9v
    @FrancisBanda-g9v 2 หลายเดือนก่อน

    Afunika kukamba president ngat ayenda aut or akabwela afunika kukamba, comwe comwe amacita nako Keanu kumawi mwacita over mudziko murivisisi but muri umphawi

  • @user-vh9uk1jy7w
    @user-vh9uk1jy7w 6 หลายเดือนก่อน +1

    Ndie ayaluka kwambiri

  • @AmandaConstance-fx8cr
    @AmandaConstance-fx8cr 6 หลายเดือนก่อน +1

    Pastor ameneyo eeeeee
    God protect our country malawi 😢😢😢😢

  • @sanlakedickson6780
    @sanlakedickson6780 6 หลายเดือนก่อน +1

    uyu si president ayi kodi kuno ku malawi kulibe asilikali tipange order captain ibrahim traore azatenge boma lathu

    • @neemahkapatamoyo9563
      @neemahkapatamoyo9563 6 หลายเดือนก่อน

      Koma mposoo Kuno asilikali tinakwilila ndithu

    • @user-qv4ko6ps4j
      @user-qv4ko6ps4j 6 หลายเดือนก่อน

      I am on your point

  • @jussaMulupa-iq9gv
    @jussaMulupa-iq9gv 6 หลายเดือนก่อน

    Best tv

  • @RobertChipatala-ow9vn
    @RobertChipatala-ow9vn 6 หลายเดือนก่อน

    Tonsefe tinaripo pomwe APM ndi DPP amalamura dziko la malawi ndipo tikudziwa momwe iwowa ankayendetsers dziko, ndiye tikudabwa kuti TV imeneyi imangowona zorakwa za boma lapanori, kapena tiziti ndinu murendo ku malawi kuno?

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 2 หลายเดือนก่อน

    Palibe chomwe akulakwisa....
    Opusa ndi asirikaliwo....they supposed to protect us all not to be cheaply manupulated by stupid dumb leaders...
    Ngati leader akupanga zopusa...atsilikali ndamen amamuthamangisa not just following nonsese

  • @JOHNSANGWALI-ox8mu
    @JOHNSANGWALI-ox8mu 6 หลายเดือนก่อน +1

    I was miss you

  • @KingDaniel-xc2qn
    @KingDaniel-xc2qn 2 หลายเดือนก่อน

    Bodza bodza asilikali achitezo cha african union kuli south africa Tanzania Malawi kenya moti asikali awiri a ku South Africa aphedwa week yomoino bodza bodza

  • @user-jy5sl8yr5n
    @user-jy5sl8yr5n 6 หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤❤❤❤❤❤❤you brother

  • @MphasoGift
    @MphasoGift 6 หลายเดือนก่อน +1

    Chakwela ndi buzi yamuthu Yona uyu atipha

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 6 หลายเดือนก่อน

    Ulemu wanu brother

  • @RomeoPrecious
    @RomeoPrecious 2 หลายเดือนก่อน

    Komaso ngozi iyi ndiopsa kwambili bwanji akanaika pamozi china chavetsa chison china chomaliza galimoto tomwe ikunyamula malilo a chilima vp president zoona ikhale iyi kuboma kulibe galimoto zapamwamba chakwela akuonjeza inu

  • @austinkadzuwa7273
    @austinkadzuwa7273 6 หลายเดือนก่อน

    What then shall we do . ?

  • @user-hy6gc6ld9w
    @user-hy6gc6ld9w 6 หลายเดือนก่อน

    Ayaruka garu ameneyi mbuzi kapuku

  • @user-ml9fm2wm1o
    @user-ml9fm2wm1o 6 หลายเดือนก่อน +1

    akulu ndinu apaderadera, god bless you,

  • @LuckyKhonyongwa-pt7ck
    @LuckyKhonyongwa-pt7ck 6 หลายเดือนก่อน

    This guy mmm atipha

  • @daudyassin1920
    @daudyassin1920 6 หลายเดือนก่อน

    Kkkķkkkkkkk umphawiwu mpaka tipatseni mafuta ife tikupatsani asilikali

  • @AaAa-qy9id
    @AaAa-qy9id 6 หลายเดือนก่อน

    Chakwera mbuzi yeniyeni
    Zikharr Mbuzi yeniyeni
    Asilikari nawonso angoona zinthu zikuonongeka. Bwanji osangopha Chakwerayo basi tione zina

  • @chamiyuna.siraji
    @chamiyuna.siraji 6 หลายเดือนก่อน

    Uremuwako❤❤

  • @user-lw2hu9hx4x
    @user-lw2hu9hx4x 6 หลายเดือนก่อน

    Maboza toooo

  • @FosterChinzimuBanda
    @FosterChinzimuBanda 6 หลายเดือนก่อน

    Chipani chimenechi chatitopesa chzipita,chatidzunza nkhanza zachuluka.

  • @JEVICO-MW
    @JEVICO-MW 2 หลายเดือนก่อน

    Ku mulanje machine amodzi koma kulibe ma form😅😅😅😅

  • @daydayjosephf.chigamane220
    @daydayjosephf.chigamane220 6 หลายเดือนก่อน

    Muthire fire🔥

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire หลายเดือนก่อน

    Kamunthu kodzungulira mutu ka chakwera bwanji otsapeleka ana ako mkadziwako nda bare ako ndi wamisala inu uyoyo komaso zikhare chinkhope kunyasako ndi mtima momwe

  • @AhmadumkomaTambala-lr9gp
    @AhmadumkomaTambala-lr9gp 6 หลายเดือนก่อน

    Tikuynela kukhala anthu ochenjela stidzalola tizavotanso kawili

  • @user-xw6ic1gj1p
    @user-xw6ic1gj1p 2 หลายเดือนก่อน

    ❤ Live

  • @YONA-v5o
    @YONA-v5o 2 หลายเดือนก่อน

    Kupusa Kwa asilikali a malawi

  • @lusolawo73
    @lusolawo73 6 หลายเดือนก่อน

    Best 1

  • @user-yj5xv4cy8x
    @user-yj5xv4cy8x 5 หลายเดือนก่อน

    Ndiwamisara chakwera

  • @user-vq9zj1fw1y
    @user-vq9zj1fw1y 6 หลายเดือนก่อน

    Anthu amat akumangani bg

  • @Hasaninussa
    @Hasaninussa หลายเดือนก่อน

    Tiphwetekanaa

  • @MonicaThocco
    @MonicaThocco 6 หลายเดือนก่อน

    Kumapha mtundu wa a Malawi pofuna kulowetsa ndalama thumba mwawo ,Koma akulu awawa ndi Mulungu yekha awapange sorted ,Mulungu anachokera nzeru anawachotseranso

  • @joemlelemba6572
    @joemlelemba6572 6 หลายเดือนก่อน

    Tinasankha njoka

  • @cassimyusuf6683
    @cassimyusuf6683 6 หลายเดือนก่อน

    Ndimasangalala ndimomwe mumalankhulira mwawukali, galu chakwera ameneyu ndimunthu osanva

  • @user-mz4tk1pw3f
    @user-mz4tk1pw3f 6 หลายเดือนก่อน +1

    Ulemu wanu big ❤❤❤❤❤❤

  • @mercychirwa2147
    @mercychirwa2147 6 หลายเดือนก่อน

    This country mmmmmm 🙌💔 silidzatukuka . Lili mmanja mwa afalao

  • @molicieeosama8877
    @molicieeosama8877 6 หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire หลายเดือนก่อน

    Kuchikamwa kwa chuleko

  • @shonmike-su7qk
    @shonmike-su7qk 6 หลายเดือนก่อน

    Atiganizireko zokha za ku imigration boma litengepo ngawo plz plz tikumva ululu kwambiri kokha ku ma passport

  • @KingDaniel-xc2qn
    @KingDaniel-xc2qn 2 หลายเดือนก่อน

    Koma izi ndiza boza kuno ku South Africa timonela news😊 ku SABC amanena kuti asilikali A South Africa mothandizana Malawi Tanzania Kenya akumenya as peace keeping force moti Asilikali awiri a South Africa A mwalira

  • @VincentChikopa-mm6ig
    @VincentChikopa-mm6ig 2 หลายเดือนก่อน

    Chakwela amalawi sopepela uoona ngati ungawine

  • @KanyengaMatress-kg4wt
    @KanyengaMatress-kg4wt 6 หลายเดือนก่อน

    Chakwela ndi president wamisala Komaso
    Ziwanda zakumidima zikumuvuta kwambili ndipo Ngati amalawi tingalole kulamulidwa ndi chakwela 💯% zilala milili ikhala yambili kwabasi

  • @REXCHARLESKAJAWO
    @REXCHARLESKAJAWO 2 หลายเดือนก่อน

    Zomvesa chisoni kwambili

  • @giftevans2957
    @giftevans2957 6 หลายเดือนก่อน

    🙏🙏🙏🙏

  • @user-pi4kg9jn4c
    @user-pi4kg9jn4c 6 หลายเดือนก่อน

    Umakwana bg😂😂😂😂😂😂

  • @user-hr4wt3fm4w
    @user-hr4wt3fm4w 3 หลายเดือนก่อน

    Ndipo pa za machine eeee ai akuonjedza tizavotatu koma

  • @LazaroSinerioSineiro
    @LazaroSinerioSineiro 2 หลายเดือนก่อน

    Mbuzi ya presidente iyi

  • @user-zn8bl9ic6x
    @user-zn8bl9ic6x 6 หลายเดือนก่อน

    Uremu wanu🙏🙏

  • @moyo77777
    @moyo77777 6 หลายเดือนก่อน

    Uthu oipa chakwera😅

  • @lastonkandiyado4526
    @lastonkandiyado4526 6 หลายเดือนก่อน

    Malawian people amene angazavotele MCP in 2025 ndiwotembeledwa basi Muthu ameneyo mpaka moyo wake onse

    • @user-ko1lk3br4r
      @user-ko1lk3br4r 6 หลายเดือนก่อน

      Adatisithanitsa km ku Israel tikulandila 4 million mpabwino bwanji

  • @patricgama4788
    @patricgama4788 6 หลายเดือนก่อน

    ife dzobeladzo tinadziwakale kut akufuna kuba ma vote mungila yama passport amati sistm ama nama

  • @user-dl8xl4nq1v
    @user-dl8xl4nq1v 5 หลายเดือนก่อน

    Osowa cholankhila iwe,ndie mwaluzatu kale ikhale nkhani imeneo zopusa 3:01

  • @user-sy9bl6sb2m
    @user-sy9bl6sb2m 6 หลายเดือนก่อน

  • @replacefruittreenursery
    @replacefruittreenursery 6 หลายเดือนก่อน

    Nice

  • @user-to4lf5cr5v
    @user-to4lf5cr5v 6 หลายเดือนก่อน

    Ife amalawi sitikufuna chakwera tisavotera Peter mutalika

  • @emmanuelmukondia3568
    @emmanuelmukondia3568 6 หลายเดือนก่อน

    Bambo wa dpp wabodza.Otsati chakwera say your president

  • @kashindijohn5145
    @kashindijohn5145 6 หลายเดือนก่อน

    KAGAME tu ndi chilombo, amalawi samalani ndithu.tufunsani ife aku DRC tikuuzeni khani zo badwitsa za KAGAME.

  • @user-cg1vm5fl8l
    @user-cg1vm5fl8l 6 หลายเดือนก่อน

    Vomerani kuti mulibe anthu oti akuvotereni. Mwakhala mukuononga dziko lino amalawi adatopa Nanu.

  • @user-uz4lk5cv6r
    @user-uz4lk5cv6r 6 หลายเดือนก่อน

    Mbava zachabechabe