ขนาดวิดีโอ: 1280 X 720853 X 480640 X 360
แสดงแผงควบคุมโปรแกรมเล่น
เล่นอัตโนมัติ
เล่นใหม่
The way I know and follow Brian he is a man of integrity and he can't do that, Ife a Malawi tinazolowela kuipisa dzina la mzathu akamachita bwino
Nkhani yanuyi ndikukupatsani 15% .Kanakondwa kuti mukayambire kawili kufufudza .... zikanakhara kuti Brian amapanga ziphuphu Brian bwedzi atamangwidwa kalekale kutengera ndimmene Brian amachitira polidzudzura boma .. zotiso kunyumba kwake kumakhara apolice zabodza.zoti kunyumba ya mayi mpaka a police 6 zabodza .iyeyo anali IG ndani .
MFUNDO zomuchotselazi sizikundigwira mtima zikumandimvekela mwabodza
Brian ndi president wa Malawi wa mtsogolomu! Brian chipempherere ichichi
Mukuti anachotsedwa nchito mosatsata malamulo,kusonyeza kuti Munthuyu amayeneradi kuchotsedwa koma motsata malamulo?
People wake up please! These issues or stories will not take you anywhere in life. Focus on your daily business for your success.
Mumakwana 👌
Achimwene ine ndimachokera ku Chileka kufupi ndi agogo ake koma kunalibe a police amalondela kunyumba kwake
Sakuti kwa agogo akeyi. Akuti kwa mai ake
@@LukeshadrickShadrick akamanena adziti kwa agogo ake osati mai ake ayi alibe mai
Muveseni bwino
Chilungamo chiyende ngati madzi
Koma kumeneko ndalama andale ananyambitamo umu mboma azizitenga kuti zoti aziwapasa anthuwa ayambanso maulendo opita kunja kuti akayambe kupemphaso tikumakamba mobweleza kuti aliyense amene akudziwa kuti wadya misonkho yamalawi tsiku likubwela zonsezo muzazosanza ngati muli ndinzelu pano zingobweza nokha ndalamazo
wakupasa ndalama zingati chakwelayo Kuti ukambe zimenezi iwayo ndi chakwele 🐕🐕🐖🐖
Mbanva zokhazokha iziz.. We know these people
Mulungu alowelerepo
K103 000 000 new blazer in town 😊
Ayenera kulipila Chakwela ndi amene anali SPC, mmene zinalili za APM ndi Mhura
Brian Banda ndi munthu wamkulu alandire ulemu wake.
You never disappoint your people with information keep up the good work 🎉🥰
😊😅
Osokonenza kwambiri
Umatha samu mavitha keep it up
Zonama zimenezi kuba nduku kukupitililaku
Ampase zake basi
Sam uchite improve pochita compile komaso uzichita Kaye practice kuwerenga ma story ako before releasing your Video. Komaso uzifufuza bwinobwino before releasing your Video.
Kkkkkk
Of course zamveka ndiye ndichifukwa chani aboma amakanika kukaonekela??? +
Ndikuyamiken blo potipatsa satanetsatane wa nkhani yokhudza Brian koma ndipemphe kut muziyesako kugwilitsa ntchito chichewa chabwino ,mwati akhothi anangokhadzula kut,pamenepa mupaunikile.
Ndiye chifukwa chake pano brian akulimbana kwambili ndi achakwela akukhala ngati sintola nkhani
Ndimamudabwadiii
Amupase zake basi
timakunyadila pitilizani
Mpaka ma body guard kwa Mai ake ? It is tit for tat.
Mbava iyi
Kuzitukumla abriani
Analiso wachamba bwanji koma akamalankhula ngati wanzelu
Mbuzi ya mumthu iyi
Mbuzi ya munthu ali ndani??
Chakwelatu mukunena zowoona chakwela ndi mbuzi yamunthudi ndipk ndimbavadi komaso garu satana
Mbuzi ndi iweyo, makolo ako, abale ako komanso amzako onse
Brian ulemu wako
The way I know and follow Brian he is a man of integrity and he can't do that, Ife a Malawi tinazolowela kuipisa dzina la mzathu akamachita bwino
Nkhani yanuyi ndikukupatsani 15% .Kanakondwa kuti mukayambire kawili kufufudza .... zikanakhara kuti Brian amapanga ziphuphu Brian bwedzi atamangwidwa kalekale kutengera ndimmene Brian amachitira polidzudzura boma .. zotiso kunyumba kwake kumakhara apolice zabodza.zoti kunyumba ya mayi mpaka a police 6 zabodza .iyeyo anali IG ndani .
MFUNDO zomuchotselazi sizikundigwira mtima zikumandimvekela mwabodza
Brian ndi president wa Malawi wa mtsogolomu! Brian chipempherere ichichi
Mukuti anachotsedwa nchito mosatsata malamulo,kusonyeza kuti Munthuyu amayeneradi kuchotsedwa koma motsata malamulo?
People wake up please! These issues or stories will not take you anywhere in life. Focus on your daily business for your success.
Mumakwana 👌
Achimwene ine ndimachokera ku Chileka kufupi ndi agogo ake koma kunalibe a police amalondela kunyumba kwake
Sakuti kwa agogo akeyi. Akuti kwa mai ake
@@LukeshadrickShadrick akamanena adziti kwa agogo ake osati mai ake ayi alibe mai
Muveseni bwino
Chilungamo chiyende ngati madzi
Koma kumeneko ndalama andale ananyambitamo umu mboma azizitenga kuti zoti aziwapasa anthuwa ayambanso maulendo opita kunja kuti akayambe kupemphaso tikumakamba mobweleza kuti aliyense amene akudziwa kuti wadya misonkho yamalawi tsiku likubwela zonsezo muzazosanza ngati muli ndinzelu pano zingobweza nokha ndalamazo
wakupasa ndalama zingati chakwelayo Kuti ukambe zimenezi iwayo ndi chakwele 🐕🐕🐖🐖
Mbanva zokhazokha iziz.. We know these people
Mulungu alowelerepo
K103 000 000 new blazer in town 😊
Ayenera kulipila Chakwela ndi amene anali SPC, mmene zinalili za APM ndi Mhura
Brian Banda ndi munthu wamkulu alandire ulemu wake.
You never disappoint your people with information keep up the good work 🎉🥰
😊😅
Osokonenza kwambiri
Umatha samu mavitha keep it up
Zonama zimenezi kuba nduku kukupitililaku
Ampase zake basi
Sam uchite improve pochita compile komaso uzichita Kaye practice kuwerenga ma story ako before releasing your Video. Komaso uzifufuza bwinobwino before releasing your Video.
Kkkkkk
Of course zamveka ndiye ndichifukwa chani aboma amakanika kukaonekela??? +
Ndikuyamiken blo potipatsa satanetsatane wa nkhani yokhudza Brian koma ndipemphe kut muziyesako kugwilitsa ntchito chichewa chabwino ,mwati akhothi anangokhadzula kut,pamenepa mupaunikile.
Ndiye chifukwa chake pano brian akulimbana kwambili ndi achakwela akukhala ngati sintola nkhani
Ndimamudabwadiii
Amupase zake basi
timakunyadila pitilizani
Mpaka ma body guard kwa Mai ake ? It is tit for tat.
Mbava iyi
Kuzitukumla abriani
Analiso wachamba bwanji koma akamalankhula ngati wanzelu
Mbuzi ya mumthu iyi
Mbuzi ya munthu ali ndani??
Chakwelatu mukunena zowoona chakwela ndi mbuzi yamunthudi ndipk ndimbavadi komaso garu satana
Mbuzi ndi iweyo, makolo ako, abale ako komanso amzako onse
Brian ulemu wako