Zifukwa zomwe Brian Banda anachoseredwa ntchito

แชร์
ฝัง

ความคิดเห็น • 42

  • @wadilikasingini500
    @wadilikasingini500 5 หลายเดือนก่อน +9

    The way I know and follow Brian he is a man of integrity and he can't do that, Ife a Malawi tinazolowela kuipisa dzina la mzathu akamachita bwino

  • @salimmkumakumakitombi-yc7pw
    @salimmkumakumakitombi-yc7pw 5 หลายเดือนก่อน +10

    Nkhani yanuyi ndikukupatsani 15% .Kanakondwa kuti mukayambire kawili kufufudza .... zikanakhara kuti Brian amapanga ziphuphu Brian bwedzi atamangwidwa kalekale kutengera ndimmene Brian amachitira polidzudzura boma .. zotiso kunyumba kwake kumakhara apolice zabodza.zoti kunyumba ya mayi mpaka a police 6 zabodza .iyeyo anali IG ndani .

  • @ruzuwanmoyenda23
    @ruzuwanmoyenda23 5 หลายเดือนก่อน +4

    MFUNDO zomuchotselazi sizikundigwira mtima zikumandimvekela mwabodza

  • @paulmakaula4937
    @paulmakaula4937 5 หลายเดือนก่อน +2

    Brian ndi president wa Malawi wa mtsogolomu! Brian chipempherere ichichi

  • @BannetChaduka-ei7qq
    @BannetChaduka-ei7qq 5 หลายเดือนก่อน +2

    Mukuti anachotsedwa nchito mosatsata malamulo,kusonyeza kuti Munthuyu amayeneradi kuchotsedwa koma motsata malamulo?

  • @macdonaldkufankomwe
    @macdonaldkufankomwe 5 หลายเดือนก่อน +3

    People wake up please! These issues or stories will not take you anywhere in life. Focus on your daily business for your success.

  • @UssenCobra
    @UssenCobra 5 หลายเดือนก่อน

    Mumakwana 👌

  • @johnynamano3862
    @johnynamano3862 5 หลายเดือนก่อน +6

    Achimwene ine ndimachokera ku Chileka kufupi ndi agogo ake koma kunalibe a police amalondela kunyumba kwake

    • @LukeshadrickShadrick
      @LukeshadrickShadrick 5 หลายเดือนก่อน

      Sakuti kwa agogo akeyi. Akuti kwa mai ake

    • @johnynamano3862
      @johnynamano3862 5 หลายเดือนก่อน

      @@LukeshadrickShadrick akamanena adziti kwa agogo ake osati mai ake ayi alibe mai

    • @macleanwazalanyirenda4994
      @macleanwazalanyirenda4994 5 หลายเดือนก่อน

      Muveseni bwino

  • @user-hb9sm9hn9g
    @user-hb9sm9hn9g 5 หลายเดือนก่อน

    Chilungamo chiyende ngati madzi

  • @ConfusedAtv-bs4gc
    @ConfusedAtv-bs4gc 5 หลายเดือนก่อน

    Koma kumeneko ndalama andale ananyambitamo umu mboma azizitenga kuti zoti aziwapasa anthuwa ayambanso maulendo opita kunja kuti akayambe kupemphaso tikumakamba mobweleza kuti aliyense amene akudziwa kuti wadya misonkho yamalawi tsiku likubwela zonsezo muzazosanza ngati muli ndinzelu pano zingobweza nokha ndalamazo

  • @hakeemQadango
    @hakeemQadango 5 หลายเดือนก่อน +2

    wakupasa ndalama zingati chakwelayo Kuti ukambe zimenezi iwayo ndi chakwele 🐕🐕🐖🐖

  • @moseskavalo3304
    @moseskavalo3304 5 หลายเดือนก่อน

    Mbanva zokhazokha iziz.. We know these people

  • @user-wy8lk7ns7i
    @user-wy8lk7ns7i 5 หลายเดือนก่อน

    Mulungu alowelerepo

  • @ChikuCharlie-bf4nj
    @ChikuCharlie-bf4nj 5 หลายเดือนก่อน

    K103 000 000 new blazer in town 😊

  • @user-jn9tz3li3v
    @user-jn9tz3li3v 5 หลายเดือนก่อน

    Ayenera kulipila Chakwela ndi amene anali SPC, mmene zinalili za APM ndi Mhura

  • @user-xh1ve5ym3l
    @user-xh1ve5ym3l 5 หลายเดือนก่อน

    Brian Banda ndi munthu wamkulu alandire ulemu wake.

  • @VeronicaSekobi-is6dk
    @VeronicaSekobi-is6dk 5 หลายเดือนก่อน +4

    You never disappoint your people with information keep up the good work 🎉🥰

    • @LINNLYMBETA
      @LINNLYMBETA 5 หลายเดือนก่อน +1

      😊😅

  • @user-vh9uk1jy7w
    @user-vh9uk1jy7w 5 หลายเดือนก่อน

    Osokonenza kwambiri

  • @petermtema5241
    @petermtema5241 5 หลายเดือนก่อน

    Umatha samu mavitha keep it up

  • @paulmakaula4937
    @paulmakaula4937 5 หลายเดือนก่อน

    Zonama zimenezi kuba nduku kukupitililaku

  • @NumbDee
    @NumbDee 5 หลายเดือนก่อน

    Ampase zake basi

  • @GiftMULOMOLE-sd7wc
    @GiftMULOMOLE-sd7wc 5 หลายเดือนก่อน +2

    Sam uchite improve pochita compile komaso uzichita Kaye practice kuwerenga ma story ako before releasing your Video. Komaso uzifufuza bwinobwino before releasing your Video.

  • @user-bz7iv1rq2f
    @user-bz7iv1rq2f 5 หลายเดือนก่อน

    Kkkkkk

  • @christopherstosherchimbuwi676
    @christopherstosherchimbuwi676 5 หลายเดือนก่อน

    Of course zamveka ndiye ndichifukwa chani aboma amakanika kukaonekela??? +

  • @randolphkazembe229
    @randolphkazembe229 5 หลายเดือนก่อน

    Ndikuyamiken blo potipatsa satanetsatane wa nkhani yokhudza Brian koma ndipemphe kut muziyesako kugwilitsa ntchito chichewa chabwino ,mwati akhothi anangokhadzula kut,pamenepa mupaunikile.

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r 5 หลายเดือนก่อน +2

    Ndiye chifukwa chake pano brian akulimbana kwambili ndi achakwela akukhala ngati sintola nkhani

  • @user-kv4cs1ot3x
    @user-kv4cs1ot3x 5 หลายเดือนก่อน

    Amupase zake basi

  • @CharlsChiyembekezo-xu4wk
    @CharlsChiyembekezo-xu4wk 5 หลายเดือนก่อน

    timakunyadila pitilizani

  • @BishopMagalasi-wp9ii
    @BishopMagalasi-wp9ii 5 หลายเดือนก่อน

    Mpaka ma body guard kwa Mai ake ? It is tit for tat.

  • @lawrenceblacktealyson8015
    @lawrenceblacktealyson8015 5 หลายเดือนก่อน

    Mbava iyi

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r 5 หลายเดือนก่อน +1

    Kuzitukumla abriani

  • @user-md5uv2cg6i
    @user-md5uv2cg6i 5 หลายเดือนก่อน

    Analiso wachamba bwanji koma akamalankhula ngati wanzelu

  • @lawrenceblacktealyson8015
    @lawrenceblacktealyson8015 5 หลายเดือนก่อน

    Mbuzi ya mumthu iyi

  • @giftblack7690
    @giftblack7690 5 หลายเดือนก่อน

    Chakwelatu mukunena zowoona chakwela ndi mbuzi yamunthudi ndipk ndimbavadi komaso garu satana

    • @DanielNamate-nk9so
      @DanielNamate-nk9so 5 หลายเดือนก่อน

      Mbuzi ndi iweyo, makolo ako, abale ako komanso amzako onse

  • @user-hb9sm9hn9g
    @user-hb9sm9hn9g 5 หลายเดือนก่อน

    Brian ulemu wako