We need him back kaya mulankhula bwanji koma just know kuti we are going to vote for him,amene akuti anyamatawo apanga chani pa unyamata waowo? Peter my vote
Peter Munthalika he's really educated guy who can improve our country as hr did before, president sikuti azilimayi nkhani ndi nzeru zamunthu basi. APM my vote ❤❤❤❤❤❤
Zoti okalamba sangalamule dziko nzabodza. Maiko ena akuchitabwino pa ulamulilo wa anthu okalamba kuposanso muthalika. Anthu akulankhula chonchiwa ndiongotumidwa ndi MCP cholinga anthu agwe mphwayi pa za Peter muthalika.
As amalawian Peter Muthalika he has lights to be a president again if he tied on the way he will give the one he trust that his not going to disappoint Malawians we need peter back
Policy for presidency period in Malawi is 2 terms which is 10 years, it doesn't denie the aged to stand, lets not confuse With Pension Age, these are different things to compare. Let him stand and See what the majority will choose.
Pieter Atha kuwinaso Anthu akumu3ra heavy mukanena zakukula osadanda pazakhala Achinyamata othandizira A pita Ali phe pa mpando wa ndarema 2025 DPP Boma 💪💪💪
Mulekeni munthu ndi ufulu wake kudzaima . Ngati anthu sakumufuna idzaweruze ndi vote. Inu dzavotereni munthu wakukhosi kwanu. Ife amene tikumva kuwawa ndi BOMA la tonse, tizavotera peter muntharika.
Kukalamba kwa chani anyamatawo akuchitapo chani mumangoganiza mutalankhula eti osamatero aliyense Ali ndiufulu musiyeni ndiufulu wake Mesa anyamata amati azasintha zinthu pano zasintha anthutu sakudana ndi chakwera koma ulamuliro wao anthu tikuzunzika or ulamuliro wa amutarika fertilizer anafikapo 100000 iwowatu ankati ndi anzeru lerobwa abale ukakhala pa kariyalaa umati driver satha kuyendetsa koma yendetsatu goo
We need him back kaya mulankhula bwanji koma just know kuti we are going to vote for him,amene akuti anyamatawo apanga chani pa unyamata waowo? Peter my vote
Yes nomata kut ndinkhalamba
We really need our president peter muthalika❤
The man is so loved and needed by Malawians, his old age is a sign of wisdom. Those that claim to be young are doing nothing to the common Malawians.
Leadership is not the old age, but the reposibility.
Peter Munthalika he's really educated guy who can improve our country as hr did before, president sikuti azilimayi nkhani ndi nzeru zamunthu basi. APM my vote ❤❤❤❤❤❤
APM ayimenso basi anyamata zithuzi zawamvuta basi. Kulamula boma amadikilana pamene mitsonkho akutolera tsiku ndi tsiku
@@ThomasMaulidi Ndipo brother Thom, anyamatawo zikuwakanika kaaaah uwone katundu wakwelera ndipo anakwelera APM atangochoka kumeneko 2020, mmmmmm thumba la cement linali pa 6 pin nthawi ya APM. Chakwera kungolowa kukaika pa 29 pin. Thumba la fertilizer APM linali 17 pin mwamavendor ndipo Chakwera kungotenga 110 pin. Ndie chomakakamira Kuti Nyamata Nyamata Ndi chain????? Muone mmene Chakwera yo panopa Malawi wamuonongera mmmm
Alamule bas Apeter
Zoti okalamba sangalamule dziko nzabodza. Maiko ena akuchitabwino pa ulamulilo wa anthu okalamba kuposanso muthalika. Anthu akulankhula chonchiwa ndiongotumidwa ndi MCP cholinga anthu agwe mphwayi pa za Peter muthalika.
Inuyo mukulankhura chabe kod anyamawao apanga chan akagwere uko chakwera ndi chilima ife tifuna adad amuthalika
Inuso bodza limenero bweretsani chitsanzo cha maiko omwe akulamulidwa ndi nkhalamba
Palibeso apa piter muthalika yemweyo
Koditu omwe akuyakhula zimenezowo sikuti azika vota ndi iwowo ayi Ovota ndi ife nde APM my vote💙💙💙🔥🔥🔥
Peter Mutharika has a vision,,not that omuzungulira akumukakamiza,,but the masses want him.
amen mukuti peter sazawina vote yanu nd banja ranu muzapange zotheka koma ife adad oyee
Chikuni chachikulu kusunga moto❤❤❤❤❤❤
Akuyima apm akufuna kt asayime ndicholinga aziba panyo panu
Ameneyo akuyimabe or atanena bwanji
l am still ❤❤❤❤ Ada zakukarambazo ukuziwa ndiwo bs Ine chakwera ndamuda ndikanamutukwana popeza mwaresa pachakwera pake 🎉🎉🎉😅😅😅
❤athu oyakhulilapo pandale akulakhula Fundo zomveka ❤kma kunena zoona ,zithu pano zakwera kwambili ,end revolution it's too high from 7 percentage to 44 end boma lawo labweleka loan it's 9 tillion kwa 3years ,,,,ma loan mu dziko ndiyamene amapangisa kut ziko lizikweza revolution end of that katundu amakwera mtengo ,,,,mamvuto amakhala athu akumudzi ...... So ifeo sitikufuna Muthu wamkulu kapena mwana aiiii tikufuna Muthu ositha zithu basi ,.
panopa sitikufuna achintamatanso ayi alutibera ndalama zathu zamisonkho ife tikubvutika kwambiri ngati mudziko muno mulibe ndalama zambili akuteng ndalama kumakagawa kumisonkhano mmalo moti akanapita kukapereka ku makampani kuti mitengo ya zinthu itsike lero akuswerwtsa anthu akubvutika chonchi peter muthalika wooyeeeeee 2925 enawa alephela kuyendetsa dziko
Wokalambayo ndamene amatudyetsa bwino mufune musafune God will fight for us
Ayimeso adadi ❤❤ Allah bless you pitha 🎉🎉
We need him back as soon as possible, we really love him so much ♥♥
Ife tikufuna Peter Mutharika ayimeso.bas
💙💙💙APM adzasitha zinthu. Afiti a MCPigs mukufuna mupitirire kupha anthu.
Anyamata kumba beta dadi ❤
Kod ukaswiri wanuo anakupasani ndani? Anthu opusa inu eti. APM is my vote thanks.
We still love ❤️ him
Palibe zimenezo kod Mesa anali mboma momwemo amalephela bwanji akagwele 😢uko
Ife tikufuna utsogoleri wabwino osat president wachinyamata koma mbuli dziko likungoonongeka lopanda president
We need Big boys.
APM my vote✅
In 2020 rate it was 45%❤
From 2021 to 2024 rate 145%😢
imagine???? 😮
DPP pachiongolero wina afune asafune❤❤❤❤❤
As amalawian Peter Muthalika he has lights to be a president again if he tied on the way he will give the one he trust that his not going to disappoint Malawians we need peter back
Straight Professor a Kula...
Akuluakulu ake ati zopusa agalu inu mufuna muzibaeti
We need our own responsible president petert arthur muthalika
APM bas....akuluakulu andaleo bwanji apite ku mcp ndi ukuluukulu wawoi azikaba limoz....
Mantha awo
Zowona big
Ayime adad imani
Amusiye Peter mutalika ayimile amalawi akasankha sogoli yemwe akufuna yene ndi sa voter Peter mutalika
weather u like or not apm is coming into power
APM my vote apoayi bola osavota
Nkhani ndiyoti malamulo akuwalola kuyimila ??
Osati ndi okalamba
Ameneyo wayankhula bwino kwambiri,anthu azavote okha.
I love peter 2 much is the one who save malawi
We need him no matter his age but his love
Mufune musafune Apm akuyimaso ndipo azawina osat mbuzi zomwe zilipo panoz zikapitirize kuvala nyau
Ngati wakalamba bwanji anyamatawa zikuwabvuta?
Akuyenera kuzaima osat omuzugulira ayi
Agogo wo akapume ....kodi kulibe anthu ena ku dpp?
Ameneyo waboza wamutumayo akunama ine ndimuvotela
We love him Amp ❤
Peter Munthalika vote ndiyako basi❤90 %
Akaswiri olankhulira za ndale enawa ndi a mcp eti?
Policy for presidency period in Malawi is 2 terms which is 10 years, it doesn't denie the aged to stand, lets not confuse With Pension Age, these are different things to compare. Let him stand and See what the majority will choose.
Peter muthalika will win no matter what
Abwerereso Peter ❤
We love you Mr president
Sinzolakwika Peter Munthalika aimenso.
Dpp oyeee
3:35 Achaima inu ndinu agulu la nankumwa inu zainu tikuziwa kale, anthu ngti inu ndiamene mukumasokoneza chifukwa chazolankhula zanthu zaziii zongofuna kuwasokoneza amalawi asiyeni apange zomwe iwo akufuna ngt anthu azawakonde ndie kuti azawavotera
He is a rigth person and a presdent to malawians
My vote dpp❤
If God says yes who can say no,,, we want change, we need APM
Tikufuna Peter Mutalika abwelere mboma
Akumuopa Peter Muntharika yo kkkkkkkk ndiufulu wake kuyimanso
Komatu muyambitsa nkhondo inu, iweyo amene ukunena zoti sangayendese zinthu bwino chifukwa chakuti wakalamba machende ako 2025 boma ndipo ndidzabwera kuzavota
Apm my vote chakwera wandililisa sugar mpakana 3600😢😢😢 chimanga 50 pin ayi malaulo ndithu dpp imatisamala potchipisa xithu osati kutivesa pain
Achinyamatawo, Chakwera ndi MCP apanga zonyansa zambiri.
Ndipo ndiye timuvotera
My vote adad
How old is current Nigeria president, American president and Donald Trump?
We need him here nomuter wat ppl can say
Ngt amunthalika akula ndye kutiso palibe cifukwa chowakakamiza acikulile anthu mmamidzimu kukavota nthawi ya zisankho
Zimenezo ndizopanda nzeru. Ngati Peter sangasinthe, ndekuti ndi uti amene achepetse mavutowa?
Awa si anthu oona zoona ayi.
Osamatokosa dala anthu mwava wakula wakula nde kuti chani za chamba basi Peter akuyimaso komaso awinaso💪💪💪💪💪💪💙💙💙💙💙🔥🔥🔥🔥🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼
APM my VOTE
APM my vote ❤❤❤❤❤❤
APM my vote
Pieter Atha kuwinaso Anthu akumu3ra heavy mukanena zakukula osadanda pazakhala Achinyamata othandizira A pita Ali phe pa mpando wa ndarema 2025 DPP Boma 💪💪💪
Mulekeni munthu ndi ufulu wake kudzaima . Ngati anthu sakumufuna idzaweruze ndi vote. Inu dzavotereni munthu wakukhosi kwanu. Ife amene tikumva kuwawa ndi BOMA la tonse, tizavotera peter muntharika.
Ayamba kale Dad ipatseni moto ❤❤❤❤❤❤
Akuluwa sangamangidwe even atalakwa
My vote
Ernest inuyo palibe chomwe ukuyakhula apa Garu wachabe chabe, ngati ukudya ndalama zabomazo usamanene za age limit apa
Akumuwopa muthalika awina
Apm ndigwero lopulumutaa amalawi pa mabvuto akukumananawo mdziko muno anthufentizimuyamika peter muthalika zinthu zinali zochipa kwambiri kusiyana ndi pano amalawi tonse tikutha kusiyanitsa tokha kumanena chilungamo ndibwino mulungu akutha kunonso ndi chifukwa anthu akufuna peter muthalika kuti a were so mboma Apm my vote 2025 wooyeeeeee
Kukalamba kwa chani anyamatawo akuchitapo chani mumangoganiza mutalankhula eti osamatero aliyense Ali ndiufulu musiyeni ndiufulu wake Mesa anyamata amati azasintha zinthu pano zasintha anthutu sakudana ndi chakwera koma ulamuliro wao anthu tikuzunzika or ulamuliro wa amutarika fertilizer anafikapo 100000 iwowatu ankati ndi anzeru lerobwa abale ukakhala pa kariyalaa umati driver satha kuyendetsa koma yendetsatu goo
Mutharika ndiye yankho,inuyo ndi acongres.
Pali funso pa nkhaniyi adzakoza bwanji pakuti mavuto anabwela ndi iwowa mmmm zikufunikadi kuganiza kwambiri
Adada omweo peter tikufuna chitukuko osati kumaphana ngat a mgalu
Aimilebe Apm palibe chowalephelesa kamba kakukula kwawo Apm my vote
Amusie alephere ekha president samaendetsa dziko ekha
Ukunama chakwera amene aononga dziko
Vote muthalika
Kukaramba sivuto zikufunika ndi zeru zoyendesera dziko tikuwafunabe adadi mwina fertilize wungazasike mtengo chomwe tikufuna ndi nsima basi wosati tizigonera batata tatopa mkazi wumamuziwa wubwino wake wukakhara Kuti wamuthamangisa watenga mkazi wina ndiye akasiyana zochita pamene wumalingalira kuti ndikadaziwa sindikanapanga zimenezi
Palibe zokalambazo muziziwa ndiinu, ndi anthu akumufuna akumuzi osati inu , mwamva
Amusiye APM adzaime, Palibe chifukwa chomukhomelela nayeso Ali ndi ufulu oyimaso
Akalamba ndichani zausilu akalamba amusiye zaisilu apm oooooooyeeeee chamba
Akalamba ndambuyawo Kodi mufuna anene kuti okalamba sazaponya nawo voti
Za ziii Angadzasithe chaniso Amuthalika zinawakanikakare
A George chaima alephera kulankhula, chifukwa mavuto omwe alipo siomwe akunenawo ai. And akuyankhula monga otumidwa ndi anthu ena. APM ndi mtsogoleri yemwe angapangitse zinthu zitsinthe
Undule ndi wa MCP
I love him so much
❤iyimeso
Apm my vote ..MCP anyamata oganiza BHO akagwere uko mbanva zokha zokha DPP boma