This song remains one of the best campaign songs ever! I am not affiliated to any political party koma every time I hear this song I can't help but dance 🎉
A malawi tisapusitsike Dan Lu wayimba bwino koma zitukuko zose zomwezikuwoneka munyimbo anapanga ndi malemu bingu zimuwake uwutse mumtende chitukuko cha APM Chawonekapo ndi kutsengulila mwala wamaziko basi ambili mutha kundiyikila umboni komaso angoyiwala kuwonetsa majenileta chifukwa ndichitukuko cha Dpp basi a malawi tiyeni tilembetse mukalembela wazisakho 2019 kukasakha mwazelu.
Aja amanena kt chakwela sali boma pano ali boma tikuti ....... tikudikililabe ife kt aloze zawo ndi 2024 iyi kuli ziiiii ....... mmmmmm km gyz a dad omwewo 2025
Am inluv with this song DPP ndi kawawa amwene 2019 Boma.........asakufuna asiye ......my vote is already for you peter...count my vote.........wina alira....Big up Dan Lu....
Dan Lu wadya kale ndalama za Pitala chifukwa cha nyimboyi, koma pitala sakuzindikila kuti dan lu akunena iyeyo kuti aloze zake yomwe ndi ma generator ndi miseu yophotchoka. Kkkk koma Dan Lu achezele bwino apitala
I can't comment this,even Dan lu he start to sing politicians song this is enough now and too much think about it and think about your fans Dan lu who listening your song each and everyday,how they feels now?
Up to now lozani zanu remains one of the best campaign songs❤ who agree?
Of course it's a masterpiece koma angwazi senderani is greatest
This song remains one of the best campaign songs ever! I am not affiliated to any political party koma every time I hear this song I can't help but dance 🎉
Ur right bra
Kungoti dpp have good songs for campaign 🔥🔥🔥
Sound well composed
Coming back after loosing our only hope skc😢 adad tabweraso ife Ana anu
Osafooka Dan lu we need u now campaign
Yomweyo bas 🤣 😂💪💪💪🔥🔥🔥
Inde iwe❤❤2025 ddp boma❤
We still inlove this video DPP 2025💙💙
😊😊😊APM woyeee
This masterpiece never gets old🔥
Basitu come here to refresh my Day...🤣🤣 Koma DPP naikonda ine eh eh
Eeee we are here to take wat belongs to us😢🎉🎉🎉🎉alozedi zawo😢🎉🎉🎉
Ndipo inu
A malawi tisapusitsike Dan Lu wayimba bwino koma zitukuko zose zomwezikuwoneka munyimbo anapanga ndi malemu bingu zimuwake uwutse mumtende chitukuko cha APM Chawonekapo ndi kutsengulila mwala wamaziko basi ambili mutha kundiyikila umboni komaso angoyiwala kuwonetsa majenileta chifukwa ndichitukuko cha Dpp basi a malawi tiyeni tilembetse mukalembela wazisakho 2019 kukasakha mwazelu.
Kkkkkkkk ndaonaso kuti zitukuko akuonetsazi zayeni
Nkhani ndiyokut inapanga DPP
Akuti DPP
Akuti isabwere Dpp
Guy is talented...respect his hustle whether you don't agree with his opinion....
Arrangement of the song on point despite whatever 👏👏👏
Big up to Dan.music is about hustle.make money bra n grow big in music.DPP ndi boma
Anyone still 2024 listening notify
The guy on 3:04 is a whole vibe! 👏🏽👏🏽😃😃😅😅❤️❤️ Great Song Dan Lu! 👏🏽👏🏽💯💯💯
Mulibe kanthu munyimboyi coz what I am it's all about Bingu. I think as the sounds itself akut aloze zawo, I could see Peter's works in this video..
That ShakuShaku a beg! A bi cool like cucumber and salt!
Siine wa DPP kma ichichi chinaipweteka🔥🙌
Ndipo tiripotu ambiri though sine wa DPP koma ichi chinyimbo still outstanding 2024
Anapha iyiyi@@user-fn3ep2dh7m
this was the best campaign song ever. Bravo Dan Lu
Danlu ulibe nzeru ukuwona ngati tikuvotera wawupoda walemba m,madzi. UTM patsogolo zinazi ndi zopanda pake , Iwe danlu ngat ufuna kuti uwine bwera ku UTM .
Watching this after seeing adad dzulo ku maliro
DPP more fire,,,the winning team 🔥🔥🔥🔥🔥
peter utsampatse ndalama Dan lu tsanga Ku votere ndi wa utm ameneyo akufuna akudyareni
Rooney Master akungofuna Dolla ada awa
Kkkkkk Kkkkkk zoonadi2 Koma... Coz sindikuona wachinyamata akusapota APM
Joni mutipukuta misosi a malawi mukubwela bho❤
My late father loved this song..
adan uyu ndeye aaaa. kuchenjela ayi chenjelani 2b quaint is very enough 4 everything.
Aja amanena kt chakwela sali boma pano ali boma tikuti ....... tikudikililabe ife kt aloze zawo ndi 2024 iyi kuli ziiiii ....... mmmmmm km gyz a dad omwewo 2025
1:53 we are here to take what belongs to us 🔥🔥🔥🔥
Musatinyase a Dan lu mwangovutika mukuona ngati akuponyelani la fanta.Musavutike ovota ndi ife ndipo amalawi pano anachengela sizoika khalamba komaso mbava kapena kuti apumbwa mmipando mukhaula mkuona 2019 UTM BOMAAAAAAA
This is still the best song for campaign till today 30 December 2023🎉
Chimoto buuuu!
Iwe umatii 🔥🔥
bro Dan LU ndinu dolo ngat siwakwathu kumangochi mwaveka a bro pa dziko lose koma MMMMMM ndale aleche wawo
Am inluv with this song DPP ndi kawawa amwene 2019 Boma.........asakufuna asiye ......my vote is already for you peter...count my vote.........wina alira....Big up Dan Lu....
wow what a nice song dan we love you ☺☺☺☺
Tikadalibe pa mbuyo panu adad love u dan lu
The best campaign song ever ♥️♥️
Nyimbo iyi hit sizaguga🎉🎉
The best one campaigning song ever and forever
Nyimbo unayimenya bwino kwambiri.....
Today is 12 may 2024❤❤
Lovely tune🔥🔥🔥
2023 we're still here
Love mpaka pano 💙💙💙💙
Dan lu akufna ponyera et zitukuko zimene akuonesa ndza bingu
kachaso ndiwamafilu ndipo boma livomereze kut jada ali khenge osat kumamanga anthu ogulisa kachaso chifukwa kachaso ndamene amabweresa nzeru
Mukutionesa zitukuko zomwe anapanga Bingu
But those development are still under dpp...it doesn't matter that its bingu or peter who built them.....dpp ndi motto!!!!!!
Izi ndi zipaso Za chipani cha DPP nanga munganene KT ndi zipaso za ulamulilo wa MCP?
dan LU ANAPHA NYIMBOYI....EEEHHHH SALUTE
ndichitsilu Dan lufan
AFUNE WINA APETAR OOOO WOYIMBAOO ASATI IWEE NDIWAMINYAMA IWE
Kma ichi campaign nde inaipweteka🥳🥳🔥♥️
Nice nice @Dan lu
Dan Lu wadya kale ndalama za Pitala chifukwa cha nyimboyi, koma pitala sakuzindikila kuti dan lu akunena iyeyo kuti aloze zake yomwe ndi ma generator ndi miseu yophotchoka. Kkkk koma Dan Lu achezele bwino apitala
I can't comment this,even Dan lu he start to sing politicians song this is enough now and too much think about it and think about your fans Dan lu who listening your song each and everyday,how they feels now?
Man inu anthu amakukondani kom zandalezi mupepela nazo
👍
Zonadi mani awa asachedwe ndi zimenezi zandalezi
Hit song until now 2024
This song is a classic!
Waimba bwinotu nyimboyi koma zoona ungamamunenenso pitala kuti aloze zake chonsecho ukudziwa kuti palibe chomwe wapanga???? Ndiwe olakwa ndithu Dan Lu coz Chakwera sangaloze coz sali m'boma koma pitala Ali m'boma koma ayi ndithu miyala basi.Bingu anali machine ndithu m'mimba ndi mchipaladi sure nanga izi ndiziti???? Mmalo mopitiliza zomwe mzako anapanga iwe kungobwera kudzaononga chipani.Mulungu akuone mwapadera ndithu fisi iwe.
racheal jamu
kkkk
More fire😜😍😍😍😍
❤grate🎉❤❤😊
Dan lu ndilaka umandivesa kukoma
Mmmmmm ndne wa MCP but iyiyi anaika mmm
Dpp woyeee!!!!!!!
Ine nyimbo iyiyi imandiwaza ndipo sinzasiya kuikonda
this song still hit bg up dan
Dpp bomaaaaaaaaaaaaaaaaaa
Eat the money bra. Much respect to Bingu though...
Next year tivine basi.
Serious
APM my vote🔥🔥🔥🔥
nyimbo yabwino koma sitingavotele achina Dausi chifukwa cha iwe
anthu akuba amenewa
Fadah😂🔥🔥
Mr dan-Lu you really rock big man continue to be humble yourself and God fearing #i sylute you always mr
Masala eti
APM my vote 💙
Hozaaaaa
Dan lu zachamba mayambizi mupuza nazo
Lonzani ZANU, makape inu .DPP .boma
Dolo ka 1,000
E-Classic respect bro
U re there bro
#RespectAkumvapainmaster
Za uchitsiru basi a dan lu anthu ozindikila ngati inu kutsatira nkhalambayi
Mumakwana mani😅😅😅
Inu guys ngt mmatha kuimba inuso osangoimba bwanji???ameneyo alindi ndalama zake kale kd amalawi munakhala bwanji??mukaona kt munthu wapangapo mzeru zake???aliense alindi ufulu opanga zomwe akufuna ,ky munakhala bwanji ky? Akakhala munthu oimba zauzimu mukt ndi wasatanic,aimbe za secura mukt akufuna amudyere muntharika ,kd zina simmatha kungoyang'ana ????inuyo ngt mumatha osangoimba bwanji?mumva myeyo anakuletsani??kuimbako ???kumeneku ndie kusatukuka @all amaganizo opiaaaaaaaaaaa,izi ndie zakupansituuuuuu
mmm
Nyimbo iyi inakoma pa njamba 😂😂
ndale sopano mwafuse akasa manyazi pano akayima uyu manja mmwamba uyu mmwamba pano eeeeee ndevu zokha pwiiii kusowa kopita wasala iwe mphaka
Tell him idiot
APM my vote
Adad takusowani 😭😭😭😭
Uyuyu anali dada
Wachinyamata iwe watani kodi, ndinkayesa kut ukuona nawo mavuto tilinawowa. Shame poor mind Dan lu. Tidzalila mpaka liti kodi osaukafe
Apa Nde mwaliradi 😂😂😂
APM my vote 🔥🔥🔥 2026😂😂
Dan Lu apa nde waonetsapo uchitsirutu , peter muntharika alibe chomwe wapanga dzamalemu dzimenedzo hahaha
2025 boma
Is true that
Best song
Nyimbo yako ndi ya bho koma wayilakwitsa wayimbira zipan
akufunadi Dollar
Inunso lozani zanu koz zonsezi mukuonetsazi ndi za malemu bingu, may his soul rest in peace
Zabhoza dani Lu wayimba bho kwabasi eeeee alozani zanu kkkkkkk
Lozani zanu wosamangolubwalubwa wina alira 2019 zidazonse zili ready zophera mwana wa mwano
Yomweo
My lovely song