ไม่สามารถเล่นวิดีโอนี้
ขออภัยในความไม่สะดวก

Dan Lu Ft. APM - Winanso Ayi (Official Music Video)

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 22 พ.ย. 2018
  • New Music Video Winanso Ayi Featuring His Excellency The President Of The Republic Of Malawi Professor Arthur Peter Mutharika. Produced And Directed By Pesi Nyasa

ความคิดเห็น • 169

  • @ISHMAELSHAIBU-kn4on
    @ISHMAELSHAIBU-kn4on 3 หลายเดือนก่อน +5

    Kunena chilungamo. Peter uja zinthu nde ankaonetsadi. Boma lililonse anayesetsa kupanga zofunika. Za kuba ndi izo koma let's see mmene Munthuyo adagwirira ntchito. Sizikufanana ndi Chakwera tu nkomwe.
    Tikafika kumbali ya nyimbo yi. Ai ndithu bwana Dan Lu katundu mudakwapula. Well talented

  • @preciousmaononga
    @preciousmaononga 19 วันที่ผ่านมา +1

    Here is 2024🌈♥️♥️waiting fo 2025

  • @TPSQUAREsqure
    @TPSQUAREsqure 4 หลายเดือนก่อน +3

    Dany lu, tinasowa nyimbo zako za kapeni tikudigila za 2025

  • @siphiek6312
    @siphiek6312 5 ปีที่แล้ว +3

    ineyo siine wa DPP. ndayesetsa kumukwiyila Dan lu kuti akuimbila za ndale, koma nyimbo iyiyi ndi maifila, beat ili bhoo.. and u r so talented Dan Lu. Koma suti ndingavotele DPP. izi zanyimbo basi.

  • @priscillachimango8962
    @priscillachimango8962 5 ปีที่แล้ว +14

    Hate him or love him, guy is talented and give him respect for that...love the composition despite everything 😘😘

  • @Mervic-vm8eo
    @Mervic-vm8eo 28 วันที่ผ่านมา

    Boma ilo❤❤❤❤🥳🥳

  • @williamslahman8998
    @williamslahman8998 5 ปีที่แล้ว +3

    ife amalawi tili ndivuto losowa chikondi mmalo moti tikhale athu awumodzi vuto mkunyozana palibe yemwe adzakonzeso dziko lathu ngati tilibe chikondi tikuyenera kuyamikila pazithu zina zomwe ena akuchita ndikuwalimbikitsa kuti dziko lipite pasogolo . Dan Lu kwake mkuyamika pazithu zomwe ena apangapo kutukula dziko adzabweraso ena adzayamikila muthu paiye yekha sangakwanise kuthandiza onse mkusangalala tiyeni tikhale athu okondana kuti dziko lathu likhale chitsanzo kwa ena

  • @RemitterFlik1130
    @RemitterFlik1130 วันที่ผ่านมา

    Apm my vote

  • @BlakRedGrin
    @BlakRedGrin 5 ปีที่แล้ว +2

    Koma nyimbo umakutumula mophyesa mtima ayise..

  • @rosemagombo359
    @rosemagombo359 29 วันที่ผ่านมา

    Dan lu ndi dolo❤

  • @user-tl9bj2fm8m
    @user-tl9bj2fm8m หลายเดือนก่อน

    This song is so good really love it ❤

  • @arnoldfungulani9800
    @arnoldfungulani9800 5 ปีที่แล้ว +2

    Zilibho more fire dan lu more fire dpp APM akulamulanso mpaka 2024 wooooo

  • @dysonthindwa4697
    @dysonthindwa4697 5 ปีที่แล้ว +2

    Big up Dan DPP Niboma ufune usafune Peter yomweyo wina alira .

  • @francisbwerera9975
    @francisbwerera9975 5 ปีที่แล้ว +6

    bola inu mumatha kuimba,,,apapa kuteleko akupatsani ndalama (gawo la ma tax athuwa)malawi mukuimva kukomer.. ife nde tatopa ndikumangonamizidwa ndi andale!!! mtendele si msima yokha!!

  • @kachalaphoebe4480
    @kachalaphoebe4480 5 ปีที่แล้ว +5

    Massive Dan Lu.. 2019 APM boma!!!!

  • @Alex-vr1yb
    @Alex-vr1yb 4 หลายเดือนก่อน

    Nyimboyi inaimbidwa mwa luso koma the message Aaaa zanu izzo

  • @user-bn4tx6th1z
    @user-bn4tx6th1z หลายเดือนก่อน

    Vote yanga bas

  • @user-bo9df6cw7d
    @user-bo9df6cw7d 5 หลายเดือนก่อน

    Eeeh kunena chilungamo Dan lu umatha, komañso peter amatha,,, but time tells,,, zonsezo kulibe lero ulemu wapadziko uli ndi limit

    • @user-qs4qd6py4d
      @user-qs4qd6py4d 5 หลายเดือนก่อน

      Ndiposo zonsezi kusowa umuthu wa muthu Ali tilibe chilungamo kmaso stitha kumanga umodzi

  • @smartchitimbe2450
    @smartchitimbe2450 ปีที่แล้ว +1

    despite it's a political song but I have much feeling with this song well composed, good melodies, so danceable.

  • @lovenessbanda9762
    @lovenessbanda9762 5 ปีที่แล้ว

    Hayibooo!!! no comment God will choose by himself for nobody is perfect

  • @billiechunda8786
    @billiechunda8786 5 ปีที่แล้ว +2

    Ayise ugwanayo mmadzi 2019 , APM palibe chochitika usogoleri sitikuuonamo ,

  • @beinhardkausiwa7107
    @beinhardkausiwa7107 5 ปีที่แล้ว +3

    Winanso ayi Ife tufuna APM basi.....chitukuko chipitirire.Bravo Dan lu

  • @leymaskeva5820
    @leymaskeva5820 5 ปีที่แล้ว +5

    Kuyaruka Dan kusowa ma plan sopano apitara ake ati,ndalama zathu zomwezi misonkho yamthumba mwanthu zimenezo uchisiru uzakupha

    • @starmondaychikwax1277
      @starmondaychikwax1277 5 ปีที่แล้ว

      Dan lu if u keeping hitting studio lyk diz loool.u wll lose more fans.any 1 agree

    • @brown8350
      @brown8350 5 ปีที่แล้ว

      These are our taxes indeed man! So what is this guy saying?? Crazy man. Singing sin! ati bwana!

    • @sintasintchaya5020
      @sintasintchaya5020 5 ปีที่แล้ว +1

      Mungoona kuti mupanga bwanji truth be told Muntharika ngwachitukuko zina kambu

    • @olivelikwaya785
      @olivelikwaya785 5 ปีที่แล้ว

      Musova

    • @user-nf3ik3ff6y
      @user-nf3ik3ff6y ปีที่แล้ว

      Muyisova pa nyasa apo Dan lu lekawaka Kuyimbila Agogo awo Anthu akuchoselapo waka mano

  • @beniekamoto8227
    @beniekamoto8227 5 ปีที่แล้ว +5

    Udali kale Daniel Lufani iwe.....pano ndiye aaaaa ukubowa

  • @sarahmugawa249
    @sarahmugawa249 5 ปีที่แล้ว +1

    Chomwe timadziwa a Malawi ndi kupanga complain basi!!!!......if you are not part of the solution you are part of the problem....osamapaka boma chilichonse. Everyone has potential to make a change......we citizens don't love our country that's y we end up cheering maiko a anzathu nkumanyoza lathu lonwe.....APM kaya MCP kaya SKC....palibe wabwino and wabwino sadzakhalapo mpaka tizaphunzile kukonda dziko lathu....Amen mpingo.....

    • @nellietsonga4609
      @nellietsonga4609 5 ปีที่แล้ว +1

      Louder for those at the back .Mawu ndithu 😍

  • @mavuschitseko7757
    @mavuschitseko7757 ปีที่แล้ว +1

    Watching from Durban, apitilize ,peter, Dan Lu 🔥

  • @wilsonmudaudi
    @wilsonmudaudi 5 ปีที่แล้ว +3

    APM kasupe wachitukuko 2019 akupitiridza kutukula Malawi.

  • @OscarChris-jn1wo
    @OscarChris-jn1wo 2 หลายเดือนก่อน

    Mwalowaso bwana💪💪💪

  • @sarahmugawa249
    @sarahmugawa249 5 ปีที่แล้ว

    Zipani mbweee!!!......everyone tryna take down and pull down the other kuti akhalepo iyeyo dziko litukuka bwanji??.....mmalo mopangana support wina akakhala pampando koma mwati ayi tiipitse ameneyu asazawineso timuonele kuti zitha bwanji.. shaaaa!!!....Malawi wanga mayooo hehe

  • @husnahaslam6
    @husnahaslam6 5 ปีที่แล้ว +3

    U are number1 malawi♥♥

  • @mphatsomtoso2506
    @mphatsomtoso2506 2 ปีที่แล้ว

    Ineyo nyimbo iyiyi ase sinxasiya kunvera ngakhale ndili wa MCP, imandiwaxa hvy, ndipo unafatsilila, nde padxima speaker dxogunda bwino iwee

  • @JohnMsimango-b5s
    @JohnMsimango-b5s 22 วันที่ผ่านมา

    ❤❤❤❤🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉

  • @ajilukalitendere105
    @ajilukalitendere105 5 ปีที่แล้ว +1

    Winanso ayi dpp woyeee😗

  • @manhaj5743
    @manhaj5743 5 ปีที่แล้ว +2

    Winaso ayi zoona Dan Lu APM yemweyo 2019 kuti moyo buuuuu

    • @ajallan7051
      @ajallan7051 5 ปีที่แล้ว

      follow me i will follow u

    • @inuragreen7387
      @inuragreen7387 5 ปีที่แล้ว

      Ayi zilibwino ena amene akubwelawo ndiwozaba koma pita eyemweyo basi Dan uli bcoz pali anthu ena odana ndi PETA koti ntchito yawo yodula ziwalo inayima pano

  • @billiechunda8786
    @billiechunda8786 5 ปีที่แล้ว +1

    Utm bomaaaaaa manyadzi akugwila

  • @wellocenjobvuyalema6456
    @wellocenjobvuyalema6456 5 ปีที่แล้ว +1

    Za zii,, ife pambuo pa SKC 2019 BOMAAAAAAA

  • @user-tl9bj2fm8m
    @user-tl9bj2fm8m หลายเดือนก่อน

    Nyatwa I wish DPP can take over the government again 🔥🔥🔥

  • @chawingamanase4790
    @chawingamanase4790 5 ปีที่แล้ว +2

    That’s you Dan Lufan i like your mingoli keep it up bru listening 👂 you on TH-cam all the way South Africa 🇿🇦

  • @RemitterFlik1130
    @RemitterFlik1130 วันที่ผ่านมา

    2025 boma iloooooooooooooooo

  • @lindahchisemphere9220
    @lindahchisemphere9220 4 ปีที่แล้ว +1

    Personally lov&love this song

  • @danielkawoza9255
    @danielkawoza9255 5 ปีที่แล้ว +1

    Kweni ivo wayamba vwachipani tikutinkhenge DPP palije ichoyikuchitapo vileke chonde vachipani lutilila nyimbo zawo ziweme not politics

  • @coollovelyk314
    @coollovelyk314 5 ปีที่แล้ว

    Akunama, ukubwera boh Dan my Brother. 😘

  • @frezarphiri6141
    @frezarphiri6141 5 ปีที่แล้ว

    APM woyeeeeee thax Dan lu cop motomoto

  • @user-nn7kh5oe1h
    @user-nn7kh5oe1h ปีที่แล้ว

    We remember that time things are going well where are you peter mtalika😢😢😢

  • @kingsleymsampha2260
    @kingsleymsampha2260 2 หลายเดือนก่อน

    This guy I talented sure

  • @lucasnanjalla4385
    @lucasnanjalla4385 5 ปีที่แล้ว

    Blue for ntendere kawa Bravo

  • @marthamwenelupembe1188
    @marthamwenelupembe1188 2 ปีที่แล้ว +1

    Nice song 🔥🔥

  • @jessymkwala5812
    @jessymkwala5812 5 ปีที่แล้ว

    yoooooooo ziliko liko

  • @jameskavina197
    @jameskavina197 5 ปีที่แล้ว

    Ofunika kukushuta bas , ngati ukufuna dolla
    Peza njira Ina , anthu akufa ndi njala ku mamidzi ndi peter wakoyo muli kuti

    • @tiyabanda7555
      @tiyabanda7555 5 หลายเดือนก่อน

      Yakhulaninso lero😂

  • @rooneymaster4861
    @rooneymaster4861 5 ปีที่แล้ว +4

    Onama iwe magamoto anatipatsa ndi dziko la China otsanamiza anthu iwe uli madzi ndi dpp yakoyo utm 2019 bomaaa

    • @olivelikwaya785
      @olivelikwaya785 5 ปีที่แล้ว

      Can we sit down and laugh together now?

  • @mwayimasina8050
    @mwayimasina8050 5 ปีที่แล้ว +2

    The beat 100%%%%%%

    • @ajallan7051
      @ajallan7051 5 ปีที่แล้ว

      follow me i will follow you

  • @ireendanbwanali3938
    @ireendanbwanali3938 4 ปีที่แล้ว

    Came here after Peter kuluza kkkk. Koma zoopsa

  • @jambokhembo67
    @jambokhembo67 2 หลายเดือนก่อน

    Boma oyeee 2025❤❤❤❤

  • @FatimaChagunda
    @FatimaChagunda 2 หลายเดือนก่อน +1

    2025 apm boma🎉

  • @marianyati7003
    @marianyati7003 5 หลายเดือนก่อน

    Big up Dan lu nakubaĺi sana sana natamani kufanya colabo na wewe

  • @wizziemasamba9385
    @wizziemasamba9385 5 ปีที่แล้ว +3

    Ai tazionela thokha mene APM akuchitira DPP 2019 boma bax

  • @CollinsPhatama
    @CollinsPhatama 2 หลายเดือนก่อน +1

    Tadzizowa

  • @GanizaniBalon-ie2oq
    @GanizaniBalon-ie2oq 4 หลายเดือนก่อน

    🔥🔥🔥🔥🔥

  • @winniemfunda8618
    @winniemfunda8618 4 ปีที่แล้ว

    Umaimba bwino mmakukonda though chipanichi smmachikonda am still ur fan hommie

  • @jackiempulula3670
    @jackiempulula3670 5 ปีที่แล้ว

    Nkona anakutibula anthu akuchilobwe iwe kusamva

  • @frezarphiri6141
    @frezarphiri6141 5 ปีที่แล้ว

    Zoona Dan lu tawina APM woyeeeeeeee

  • @justicekandaoje2255
    @justicekandaoje2255 2 ปีที่แล้ว

    Yeee

  • @Chiku723
    @Chiku723 11 หลายเดือนก่อน

    Very talented man

  • @HeliodaCostaMario
    @HeliodaCostaMario 4 หลายเดือนก่อน

    Boa musica

  • @williamnkhoma6245
    @williamnkhoma6245 ปีที่แล้ว

    for sure 👍

  • @ImranSande
    @ImranSande 2 หลายเดือนก่อน

    Ndipo tikulowanso muboma

  • @stewartkamwendo735
    @stewartkamwendo735 5 ปีที่แล้ว

    Anthu ena anangobadwa otsutsa ndipo azafa ali otsutsa ndiye sitikukudabwani choti muziwe palibe tsogoleli angakhale 100% ndiye olo ntsogoleli atakhala ambuyani kapena bambo anu pali anthu ena azati sizilibwino ndipo enanu kuti tifufuze mukuchita kulephela kuyendetsa mabanja anu deile kuyambana

  • @RobertChidothe-ei2qh
    @RobertChidothe-ei2qh 10 หลายเดือนก่อน

    awa ndi akamuna awa palibe wopikisana nawo

  • @MyPhone-gf2ks
    @MyPhone-gf2ks ปีที่แล้ว

    Ndani lu

  • @benjaminmtima9360
    @benjaminmtima9360 5 ปีที่แล้ว

    Dan lu mofireeeee

  • @chimwemwekasambe4353
    @chimwemwekasambe4353 5 ปีที่แล้ว

    Dan lu aonetse mwina alindikhungu

  • @yamiechikhola6705
    @yamiechikhola6705 5 ปีที่แล้ว

    Koma ngati galu amenei angawineso amalawi tizalira kwambir sitikukonda dziko lathu

  • @frederickskamphonje1410
    @frederickskamphonje1410 5 ปีที่แล้ว

    Zankutuuuuu basi

  • @waishansambo79
    @waishansambo79 5 ปีที่แล้ว

    Big up Dan Lu tili pambuyo pa Adadi.....2019 APM,Dpp Boma.....Wina Alira..winanso ai ....peter yekha basi

  • @user-cq8hs7zd8s
    @user-cq8hs7zd8s 3 หลายเดือนก่อน

    Tikulowa 2025🇲🇼❤❤❤❤❤

  • @serasera8492
    @serasera8492 5 ปีที่แล้ว

    More fire

  • @michaelchibambo3832
    @michaelchibambo3832 5 ปีที่แล้ว +2

    I like your songs Dan.......and i know that reality is that u even know the message in ur song is totally wrong palibe chomwe akupangapo mdala wakoyo. I respect his brother who did great job to Malwians and iyeso akuloza za brother wake.

  • @IsaacFranciscoPedro-wn8yb
    @IsaacFranciscoPedro-wn8yb ปีที่แล้ว

    Zoona bg

  • @thewzg3433
    @thewzg3433 5 ปีที่แล้ว

    Dan Lu apandewanamatu man

  • @mouricesaidi5348
    @mouricesaidi5348 5 ปีที่แล้ว

    I love Dan Lu ,and the music but not thr message in the song, and l can't hate him coz of his choice,,,,,,,Aliyese amathilira msipu wake

  • @tickabdulkhadija9859
    @tickabdulkhadija9859 5 ปีที่แล้ว

    ife ndiye sitimazisata zazipanizi kwathu ku chance dollars 💸💵 basi....

  • @jamesngalande4345
    @jamesngalande4345 5 ปีที่แล้ว

    cHAKA CHA MAWA SUZAYIMBANSO CHIFUKWA CHA MANYAZI AZAKUTENGETU MBUYAKOYO AKAMAPITA KWAWO KU US CHITSIRU SUMATHANSO KUYIMBA

    • @ajallan7051
      @ajallan7051 5 ปีที่แล้ว

      follow me i will follow u

  • @jameskamanga628
    @jameskamanga628 3 ปีที่แล้ว

    Nyimboyi udakwapula man koma ndine wa Chakwera sorry

  • @montharrilson4556
    @montharrilson4556 5 ปีที่แล้ว

    MLI nyatwa man

  • @thombanda8318
    @thombanda8318 5 ปีที่แล้ว

    Chipatara chankhatabay sip itara wakoyo ukunama

  • @eltonmaseya6511
    @eltonmaseya6511 5 ปีที่แล้ว

    Dan ataaa

  • @jameskamanga628
    @jameskamanga628 3 ปีที่แล้ว

    Moti nyimbo zabwinozi udangoyimba zabule adad pano akuwedza somba kumangochi ngati kumalototu😂😂😂😂😂😂😂😃

  • @fosterjames2985
    @fosterjames2985 5 ปีที่แล้ว +2

    Keep it up Dan lu pitilizani zitukuko a Peter kukasungu north tikusalira kuno please

  • @mbwanaidi2844
    @mbwanaidi2844 ปีที่แล้ว

    Sikepe chimo

  • @karenijames5538
    @karenijames5538 5 ปีที่แล้ว

    ukati Malawi yese mwagwirizana ndi ndani uziti banjarako mwagwirizana. misewu yake itiyo mesa ndalama zamisokho ndizomwe timalipira musewu zinja ndizomwe amamangiraso misewu... ukanenaza misika timadura ziphaso kulipira misikayo,, za sugar ndiye pilara sizakumukhuza ... ukawone kwanu kwachiyenda usiku. ukamayakhura munyimbo zakozo uzionaso komwe unachokera azichemwari ako alimbuuu nyumwa ngati kuchimbuzi ndiye uziti pitara pitala hahahaha chiyenda usiku kulibeko zazeru wapangako magesi ndiye wesi usatinyaseso ,,, chisilu chowonesa mbolo ...

    • @dysonthindwa4697
      @dysonthindwa4697 5 ปีที่แล้ว

      Ulibe mfundo umadziwa kutukwana APM Boma

  • @mercymatchado6438
    @mercymatchado6438 2 ปีที่แล้ว

    Umaimulira

  • @changausyayao3111
    @changausyayao3111 5 ปีที่แล้ว

    Komanso awa fuc all around APM×10000

  • @LeoC-in6um
    @LeoC-in6um 5 หลายเดือนก่อน

    Mumakwana APM ndi one

  • @dumelohashim7362
    @dumelohashim7362 5 ปีที่แล้ว

    koma zoti chuma sichikuyendabwino mukuziziwa musamakomedwe achisilu inu auzeni athu zona zokha zokha osamaimba zopsesa mtima athu tikuthawa ziko lathu lomwe

    • @obrianbanda3863
      @obrianbanda3863 4 ปีที่แล้ว

      A dpp chamba chikuwapweteka zakuziwa chomwe akuchita la 40 days lizakwana siku ndi lamulungu

  • @mouricesaidi5348
    @mouricesaidi5348 4 ปีที่แล้ว

    Dan Lu,,, ndyele mdalayo adzaona ngat Ayao ndi mazoba,,,, uzimupopa uku ukumuyamwa klkkkkkkkk l kno kut sunamuvotele kkkkkk

  • @shareefrabson8259
    @shareefrabson8259 5 ปีที่แล้ว

    Sowona mn zimukuna sofeza chison izi mn

  • @amandamajomeka3839
    @amandamajomeka3839 4 ปีที่แล้ว +1

    are we kids we dont know Ft.......or you mean everyone can sing?

  • @everlardngwira2112
    @everlardngwira2112 5 ปีที่แล้ว

    Kuziphwekesatu kumeneku! Mpaka kukunyngererani apitala?

  • @laymanchirwa8026
    @laymanchirwa8026 5 ปีที่แล้ว

    more fire Dan.... 2019 DPP mbomaaaaaaaa

  • @markseniorkamoto4844
    @markseniorkamoto4844 5 ปีที่แล้ว

    A Malawi kodi ndiliti tizaziwe Mulungu? Dan Lu akulephela kungowauzako amalawi chilungamo zoona,, boza ili lamtundu wanji abale? Sibwino koma. Am'pwetekesatu bwana wakeyu.......

    • @ajallan7051
      @ajallan7051 5 ปีที่แล้ว

      follow me i will follow u