New Music Video Winanso Ayi Featuring His Excellency The President Of The Republic Of Malawi Professor Arthur Peter Mutharika. Produced And Directed By Pesi Nyasa
Kunena chilungamo. Peter uja zinthu nde ankaonetsadi. Boma lililonse anayesetsa kupanga zofunika. Za kuba ndi izo koma let's see mmene Munthuyo adagwirira ntchito. Sizikufanana ndi Chakwera tu nkomwe. Tikafika kumbali ya nyimbo yi. Ai ndithu bwana Dan Lu katundu mudakwapula. Well talented
ineyo siine wa DPP. ndayesetsa kumukwiyila Dan lu kuti akuimbila za ndale, koma nyimbo iyiyi ndi maifila, beat ili bhoo.. and u r so talented Dan Lu. Koma suti ndingavotele DPP. izi zanyimbo basi.
bola inu mumatha kuimba,,,apapa kuteleko akupatsani ndalama (gawo la ma tax athuwa)malawi mukuimva kukomer.. ife nde tatopa ndikumangonamizidwa ndi andale!!! mtendele si msima yokha!!
Chomwe timadziwa a Malawi ndi kupanga complain basi!!!!......if you are not part of the solution you are part of the problem....osamapaka boma chilichonse. Everyone has potential to make a change......we citizens don't love our country that's y we end up cheering maiko a anzathu nkumanyoza lathu lonwe.....APM kaya MCP kaya SKC....palibe wabwino and wabwino sadzakhalapo mpaka tizaphunzile kukonda dziko lathu....Amen mpingo.....
Zipani mbweee!!!......everyone tryna take down and pull down the other kuti akhalepo iyeyo dziko litukuka bwanji??.....mmalo mopangana support wina akakhala pampando koma mwati ayi tiipitse ameneyu asazawineso timuonele kuti zitha bwanji.. shaaaa!!!....Malawi wanga mayooo hehe
Ayi zilibwino ena amene akubwelawo ndiwozaba koma pita eyemweyo basi Dan uli bcoz pali anthu ena odana ndi PETA koti ntchito yawo yodula ziwalo inayima pano
I like your songs Dan.......and i know that reality is that u even know the message in ur song is totally wrong palibe chomwe akupangapo mdala wakoyo. I respect his brother who did great job to Malwians and iyeso akuloza za brother wake.
Kunena chilungamo. Peter uja zinthu nde ankaonetsadi. Boma lililonse anayesetsa kupanga zofunika. Za kuba ndi izo koma let's see mmene Munthuyo adagwirira ntchito. Sizikufanana ndi Chakwera tu nkomwe.
Tikafika kumbali ya nyimbo yi. Ai ndithu bwana Dan Lu katundu mudakwapula. Well talented
Here is 2024🌈♥️♥️waiting fo 2025
Dany lu, tinasowa nyimbo zako za kapeni tikudigila za 2025
ineyo siine wa DPP. ndayesetsa kumukwiyila Dan lu kuti akuimbila za ndale, koma nyimbo iyiyi ndi maifila, beat ili bhoo.. and u r so talented Dan Lu. Koma suti ndingavotele DPP. izi zanyimbo basi.
Hate him or love him, guy is talented and give him respect for that...love the composition despite everything 😘😘
Fact and true
Boma ilo❤❤❤❤🥳🥳
ife amalawi tili ndivuto losowa chikondi mmalo moti tikhale athu awumodzi vuto mkunyozana palibe yemwe adzakonzeso dziko lathu ngati tilibe chikondi tikuyenera kuyamikila pazithu zina zomwe ena akuchita ndikuwalimbikitsa kuti dziko lipite pasogolo . Dan Lu kwake mkuyamika pazithu zomwe ena apangapo kutukula dziko adzabweraso ena adzayamikila muthu paiye yekha sangakwanise kuthandiza onse mkusangalala tiyeni tikhale athu okondana kuti dziko lathu likhale chitsanzo kwa ena
Apm my vote
Koma nyimbo umakutumula mophyesa mtima ayise..
Dan lu ndi dolo❤
This song is so good really love it ❤
Zilibho more fire dan lu more fire dpp APM akulamulanso mpaka 2024 wooooo
Big up Dan DPP Niboma ufune usafune Peter yomweyo wina alira .
bola inu mumatha kuimba,,,apapa kuteleko akupatsani ndalama (gawo la ma tax athuwa)malawi mukuimva kukomer.. ife nde tatopa ndikumangonamizidwa ndi andale!!! mtendele si msima yokha!!
Awapatsako za cash gate
Zako zimenezo
Massive Dan Lu.. 2019 APM boma!!!!
Nyimboyi inaimbidwa mwa luso koma the message Aaaa zanu izzo
Vote yanga bas
Eeeh kunena chilungamo Dan lu umatha, komañso peter amatha,,, but time tells,,, zonsezo kulibe lero ulemu wapadziko uli ndi limit
Ndiposo zonsezi kusowa umuthu wa muthu Ali tilibe chilungamo kmaso stitha kumanga umodzi
despite it's a political song but I have much feeling with this song well composed, good melodies, so danceable.
Hayibooo!!! no comment God will choose by himself for nobody is perfect
Ayise ugwanayo mmadzi 2019 , APM palibe chochitika usogoleri sitikuuonamo ,
Mbola
Winanso ayi Ife tufuna APM basi.....chitukuko chipitirire.Bravo Dan lu
Dpp morefire
Kuyaruka Dan kusowa ma plan sopano apitara ake ati,ndalama zathu zomwezi misonkho yamthumba mwanthu zimenezo uchisiru uzakupha
Dan lu if u keeping hitting studio lyk diz loool.u wll lose more fans.any 1 agree
These are our taxes indeed man! So what is this guy saying?? Crazy man. Singing sin! ati bwana!
Mungoona kuti mupanga bwanji truth be told Muntharika ngwachitukuko zina kambu
Musova
Muyisova pa nyasa apo Dan lu lekawaka Kuyimbila Agogo awo Anthu akuchoselapo waka mano
Udali kale Daniel Lufani iwe.....pano ndiye aaaaa ukubowa
Chomwe timadziwa a Malawi ndi kupanga complain basi!!!!......if you are not part of the solution you are part of the problem....osamapaka boma chilichonse. Everyone has potential to make a change......we citizens don't love our country that's y we end up cheering maiko a anzathu nkumanyoza lathu lonwe.....APM kaya MCP kaya SKC....palibe wabwino and wabwino sadzakhalapo mpaka tizaphunzile kukonda dziko lathu....Amen mpingo.....
Louder for those at the back .Mawu ndithu 😍
Watching from Durban, apitilize ,peter, Dan Lu 🔥
APM kasupe wachitukuko 2019 akupitiridza kutukula Malawi.
Mwalowaso bwana💪💪💪
Zipani mbweee!!!......everyone tryna take down and pull down the other kuti akhalepo iyeyo dziko litukuka bwanji??.....mmalo mopangana support wina akakhala pampando koma mwati ayi tiipitse ameneyu asazawineso timuonele kuti zitha bwanji.. shaaaa!!!....Malawi wanga mayooo hehe
U are number1 malawi♥♥
Ineyo nyimbo iyiyi ase sinxasiya kunvera ngakhale ndili wa MCP, imandiwaxa hvy, ndipo unafatsilila, nde padxima speaker dxogunda bwino iwee
😂😂😂
❤❤❤❤🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉
Winanso ayi dpp woyeee😗
Winaso ayi zoona Dan Lu APM yemweyo 2019 kuti moyo buuuuu
follow me i will follow u
Ayi zilibwino ena amene akubwelawo ndiwozaba koma pita eyemweyo basi Dan uli bcoz pali anthu ena odana ndi PETA koti ntchito yawo yodula ziwalo inayima pano
Utm bomaaaaaa manyadzi akugwila
mulipobe? ndi tonse yanuyi?
Za zii,, ife pambuo pa SKC 2019 BOMAAAAAAA
Nde iti imeneyi
Congratulations
Nyatwa I wish DPP can take over the government again 🔥🔥🔥
That’s you Dan Lufan i like your mingoli keep it up bru listening 👂 you on TH-cam all the way South Africa 🇿🇦
2025 boma iloooooooooooooooo
Personally lov&love this song
Kweni ivo wayamba vwachipani tikutinkhenge DPP palije ichoyikuchitapo vileke chonde vachipani lutilila nyimbo zawo ziweme not politics
Akunama, ukubwera boh Dan my Brother. 😘
APM woyeeeeee thax Dan lu cop motomoto
We remember that time things are going well where are you peter mtalika😢😢😢
This guy I talented sure
Blue for ntendere kawa Bravo
Nice song 🔥🔥
yoooooooo ziliko liko
Ofunika kukushuta bas , ngati ukufuna dolla
Peza njira Ina , anthu akufa ndi njala ku mamidzi ndi peter wakoyo muli kuti
Yakhulaninso lero😂
Onama iwe magamoto anatipatsa ndi dziko la China otsanamiza anthu iwe uli madzi ndi dpp yakoyo utm 2019 bomaaa
Can we sit down and laugh together now?
The beat 100%%%%%%
follow me i will follow you
Came here after Peter kuluza kkkk. Koma zoopsa
Boma oyeee 2025❤❤❤❤
2025 apm boma🎉
Big up Dan lu nakubaĺi sana sana natamani kufanya colabo na wewe
Ai tazionela thokha mene APM akuchitira DPP 2019 boma bax
Tadzizowa
🔥🔥🔥🔥🔥
Umaimba bwino mmakukonda though chipanichi smmachikonda am still ur fan hommie
Nkona anakutibula anthu akuchilobwe iwe kusamva
Zoona Dan lu tawina APM woyeeeeeeee
Yeee
Very talented man
Boa musica
for sure 👍
Ndipo tikulowanso muboma
Anthu ena anangobadwa otsutsa ndipo azafa ali otsutsa ndiye sitikukudabwani choti muziwe palibe tsogoleli angakhale 100% ndiye olo ntsogoleli atakhala ambuyani kapena bambo anu pali anthu ena azati sizilibwino ndipo enanu kuti tifufuze mukuchita kulephela kuyendetsa mabanja anu deile kuyambana
awa ndi akamuna awa palibe wopikisana nawo
Ndani lu
Dan lu mofireeeee
Dan lu aonetse mwina alindikhungu
Koma ngati galu amenei angawineso amalawi tizalira kwambir sitikukonda dziko lathu
Zankutuuuuu basi
Big up Dan Lu tili pambuyo pa Adadi.....2019 APM,Dpp Boma.....Wina Alira..winanso ai ....peter yekha basi
Tikulowa 2025🇲🇼❤❤❤❤❤
More fire
I like your songs Dan.......and i know that reality is that u even know the message in ur song is totally wrong palibe chomwe akupangapo mdala wakoyo. I respect his brother who did great job to Malwians and iyeso akuloza za brother wake.
Koma Chakwera okweza zithuyuu aaa mbola
Zoona bg
Dan Lu apandewanamatu man
I love Dan Lu ,and the music but not thr message in the song, and l can't hate him coz of his choice,,,,,,,Aliyese amathilira msipu wake
ife ndiye sitimazisata zazipanizi kwathu ku chance dollars 💸💵 basi....
cHAKA CHA MAWA SUZAYIMBANSO CHIFUKWA CHA MANYAZI AZAKUTENGETU MBUYAKOYO AKAMAPITA KWAWO KU US CHITSIRU SUMATHANSO KUYIMBA
follow me i will follow u
Nyimboyi udakwapula man koma ndine wa Chakwera sorry
MLI nyatwa man
Chipatara chankhatabay sip itara wakoyo ukunama
Dan ataaa
Moti nyimbo zabwinozi udangoyimba zabule adad pano akuwedza somba kumangochi ngati kumalototu😂😂😂😂😂😂😂😃
Keep it up Dan lu pitilizani zitukuko a Peter kukasungu north tikusalira kuno please
Sikepe chimo
ukati Malawi yese mwagwirizana ndi ndani uziti banjarako mwagwirizana. misewu yake itiyo mesa ndalama zamisokho ndizomwe timalipira musewu zinja ndizomwe amamangiraso misewu... ukanenaza misika timadura ziphaso kulipira misikayo,, za sugar ndiye pilara sizakumukhuza ... ukawone kwanu kwachiyenda usiku. ukamayakhura munyimbo zakozo uzionaso komwe unachokera azichemwari ako alimbuuu nyumwa ngati kuchimbuzi ndiye uziti pitara pitala hahahaha chiyenda usiku kulibeko zazeru wapangako magesi ndiye wesi usatinyaseso ,,, chisilu chowonesa mbolo ...
Ulibe mfundo umadziwa kutukwana APM Boma
Umaimulira
Komanso awa fuc all around APM×10000
Mumakwana APM ndi one
koma zoti chuma sichikuyendabwino mukuziziwa musamakomedwe achisilu inu auzeni athu zona zokha zokha osamaimba zopsesa mtima athu tikuthawa ziko lathu lomwe
A dpp chamba chikuwapweteka zakuziwa chomwe akuchita la 40 days lizakwana siku ndi lamulungu
Dan Lu,,, ndyele mdalayo adzaona ngat Ayao ndi mazoba,,,, uzimupopa uku ukumuyamwa klkkkkkkkk l kno kut sunamuvotele kkkkkk
Sowona mn zimukuna sofeza chison izi mn
are we kids we dont know Ft.......or you mean everyone can sing?
Kuziphwekesatu kumeneku! Mpaka kukunyngererani apitala?
more fire Dan.... 2019 DPP mbomaaaaaaaa
A Malawi kodi ndiliti tizaziwe Mulungu? Dan Lu akulephela kungowauzako amalawi chilungamo zoona,, boza ili lamtundu wanji abale? Sibwino koma. Am'pwetekesatu bwana wakeyu.......
follow me i will follow u