CDEDI PRESS BRIEFING LIVE TODAY - NAMIWA WAPEMPHA PRESIDENT CHAKWERA KUTI ALANKHULE A MALAWI LERO

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 9 ก.พ. 2025
  • CDEDI PRESS BRIEFING LIVE TODAY - NAMIWA WAPEMPHA PRESIDENT CHAKWERA KUTI ALANKHULE A MALAWI LERO

ความคิดเห็น • 268

  • @afritouch4660
    @afritouch4660 หลายเดือนก่อน +10

    Malawi should support Israel because the land was owned by Israel before Palestine claimed it & bible can teach you better. We don’t support terrorists. Shame on you

    • @catherinec1861
      @catherinec1861 หลายเดือนก่อน

      Uku ndikusamvetseta history and Bible.
      These are Jews fighting and killing Christians.

    • @WakuMalawi
      @WakuMalawi หลายเดือนก่อน +6

      That bible that you're referring to says it's ok to kill innocent women & children...? I thought killing was one of the commandments "not to do"...? Please exlplain.

    • @Accountants615
      @Accountants615 หลายเดือนก่อน +6

      Mwapupulumatu kunena kuti Shame on you, 😂😂😂😂😂😂😂😂, Killing is not a good act, Thy shall not murder! Komanso ndiwe wa MCP nde kupha sivuto

    • @AHAMADUJRAminie-c6q
      @AHAMADUJRAminie-c6q หลายเดือนก่อน +1

      Machende ako iweyo shame for yourself

    • @ReeqoVescan
      @ReeqoVescan หลายเดือนก่อน

      Munthu osazindikira uyu musiyeni

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole หลายเดือนก่อน +10

    Bravo namiwa ndi team yanu yonse tili kumbali yanu simulinokha ❤❤

  • @FebbieNjewa-g3k
    @FebbieNjewa-g3k หลายเดือนก่อน +5

    Cded group,,keep it up!God bless n protect yu in Jesus christ name

  • @RosinaPatel
    @RosinaPatel หลายเดือนก่อน +12

    Viva Comrade Namiwa..enough is enough

  • @aggogokina8992
    @aggogokina8992 หลายเดือนก่อน +2

    Akulu akulu Namiwa ndi chibinyira chokanika kusenza awa ndi akamunadi amene ayima pa cholungamo mopanda mantha. Power to that💪💪💪👍

  • @GraceShaibu-i9d
    @GraceShaibu-i9d หลายเดือนก่อน +2

    Viva comrade namiwa big up

  • @ThomasMaulana-u4p
    @ThomasMaulana-u4p หลายเดือนก่อน +7

    Nsaname ine Chakwerayi amandisowesa choyankhura eeeish☹.

  • @SuccessorMupangami
    @SuccessorMupangami หลายเดือนก่อน +8

    Landilan Maluwa anu Mr Namiwa,Amalawi ochuluka tili mbali yanu.

  • @thomasmember2485
    @thomasmember2485 หลายเดือนก่อน +5

    Big up Comrade Namiwa Osaopa Osafooka Osatopa.

  • @JanatuCarlos
    @JanatuCarlos หลายเดือนก่อน

    Mr namiwa and his team may good lord protect them and continue their job in the name of Jesus,,,,

  • @bridgetmajor3646
    @bridgetmajor3646 หลายเดือนก่อน +4

    Elder ....Nàmiwa ....Respect....❤🔥🔥🔥🔥

  • @MussaRafael-d4q
    @MussaRafael-d4q หลายเดือนก่อน +9

    never give up Namiwa

  • @NyanguPaul
    @NyanguPaul หลายเดือนก่อน +7

    Let's continue comrade never give up

  • @catherinec1861
    @catherinec1861 หลายเดือนก่อน +2

    Why fight over the lake when we are not making any profitable use of it? Africa should continue to look to unity not divisions.
    I agree 100% with the Israel/Palestinian issue. We are on the wrong side of history for as long as our government supports Israeli genocide.

  • @WellosMoyo
    @WellosMoyo 18 วันที่ผ่านมา

    Umatiimirila more fire Namiwa

  • @BornfaceMponda-ny9tw
    @BornfaceMponda-ny9tw หลายเดือนก่อน +5

    Go go go

  • @EmmanuelNgambi-y6h
    @EmmanuelNgambi-y6h หลายเดือนก่อน

    Very wise and intelligent Namiwa go on,,,, osaopa osafooka osatopa 🔥

  • @WitnessChimera-r4i
    @WitnessChimera-r4i หลายเดือนก่อน +9

    Apa tinaimbila mfiti m'manja tilibe mau a 🇲🇼 malawi

    • @VeronicaChirwa-ct4os
      @VeronicaChirwa-ct4os หลายเดือนก่อน +1

      Ndipo zoonadi tinayimbira mfiti m'manja ndi chani chomwe chinatilodza ife? Tinapusitsika ndi ubusa, anavala chigoba cha ubusa

    • @WitnessChimera-r4i
      @WitnessChimera-r4i หลายเดือนก่อน

      @VeronicaChirwa-ct4os ndipo kwambili

  • @miraclejohnphiri7687
    @miraclejohnphiri7687 หลายเดือนก่อน +4

    Question kodi abwana athuwa analidi aku church kapena amkagwila ntchitito basi zikudabwisa???

  • @MolesBrown
    @MolesBrown หลายเดือนก่อน +11

    Kodi asilikaliwa ncthito yayo ndichiyani Kodi iwowo siwoteteza dziko chaka ndi chaka kulemba asilikali akati ateteza dziko ndikumademo zoona ndalama zathu zikungopita ndizowona asilikali athu adzisiya kuteteza dzi dzikolawo adzikateteza mayikol akunja zoona kunsanke analanda kumachinga analanda kumwanza analanda sizoonayi anamiwa mwayitenga bwino koma musakhale mwasamila chipani musawonetse mbali nenani chalakwikacho mbalizose mukatelo amalawi ose adzikuvetselani Imani panokha chonde mupange zadziko lose

    • @VeronicaChirwa-ct4os
      @VeronicaChirwa-ct4os หลายเดือนก่อน +1

      Ndi opepera awa amangodziwa kupita ku DRC

    • @FRANKMKWAILA
      @FRANKMKWAILA หลายเดือนก่อน +1

      Asilikali amayendera ma orders, ngati atsogolero ali chete, asilikali sangangopakira mifuti ulendo ayi. Nyanja yapita basi. Alandira bwanji map achilendo nkukhala chete?

    • @BerthaWasi
      @BerthaWasi หลายเดือนก่อน +1

      Honestly asilikali akumalawi ndopepela maiko ena kukamachitika zopusa kuboma amatha kuchosa president ndkukonza dziko koma athuwa mmmmmmmm

    • @NurjChilawo
      @NurjChilawo หลายเดือนก่อน +1

      Asilikali athu pano ali ngati Tambala onyowa

    • @AchinaKellz
      @AchinaKellz หลายเดือนก่อน

      Ayi alowa ndale ngati police

  • @WestonMakiyi-s9l
    @WestonMakiyi-s9l หลายเดือนก่อน +3

    Great man

  • @ezekieljambo4255
    @ezekieljambo4255 หลายเดือนก่อน

    Comrade Phiri mu kunveka ngat Namadingonamadingo eeh😊
    Big up!

  • @DAGAMAaaaa
    @DAGAMAaaaa หลายเดือนก่อน +1

    Worm heart of Africa ija ikusapota nkhondo chifukwa cha chakwera

  • @felixnyirongo5265
    @felixnyirongo5265 หลายเดือนก่อน

    Please go ahead Mr Namiwa

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy หลายเดือนก่อน +1

    Powerful our saviour
    God bless you namiwa

  • @FreddieKanyerere-u2z
    @FreddieKanyerere-u2z หลายเดือนก่อน +1

    Comrade Namiwa big Up ana anthu adzavutika ndi ziganizo zopusa.

  • @Hildamanda-e2x
    @Hildamanda-e2x หลายเดือนก่อน

    God bless you guys ❤ mulungu azikutetezani kuti malawi amulumuke kunzela mwainu chiyembekezo cha amalawi chili pa inu ❤❤❤❤❤

  • @GrecianWyson
    @GrecianWyson หลายเดือนก่อน +1

    Namiwa uremu 🎉🎉🎉 mukutiyimiriradi my God bless you

  • @Edward-y3v
    @Edward-y3v หลายเดือนก่อน +1

    May God bless you Comrade

  • @AlbertNambwale-sm9qe
    @AlbertNambwale-sm9qe หลายเดือนก่อน +3

    Nice briefing

  • @JohnChikuni-cr1xy
    @JohnChikuni-cr1xy หลายเดือนก่อน +3

    Namiwa is a true Malawian

  • @georgeaiwa8661
    @georgeaiwa8661 หลายเดือนก่อน +5

    Mr. Namiwa mulisinthadi dzikoli

  • @AmosBandula-up4yb
    @AmosBandula-up4yb หลายเดือนก่อน

    Number 1

  • @AggieKwekwesa
    @AggieKwekwesa หลายเดือนก่อน +1

    God z with u comrades ❤

  • @Moses51
    @Moses51 หลายเดือนก่อน +8

    Chilungamo poyela together with Malawi

  • @FatimanickisJaffer
    @FatimanickisJaffer หลายเดือนก่อน +4

    Mutu wao sungwir ntchito pan aprezident anth ndip sakudziwa chomwe akuchit akufunik kumtemela srs

  • @LawrenceDickens-jk3zx
    @LawrenceDickens-jk3zx หลายเดือนก่อน +2

    Mr Namiwa big up bro

  • @LeyvanSamuel-pe5tc
    @LeyvanSamuel-pe5tc หลายเดือนก่อน +2

    Keep it up good work 😇 Namiwa no peace for the wicked chikangawa akapuma kumwamba 😅

  • @ThokoMsonkho-hy4uc
    @ThokoMsonkho-hy4uc หลายเดือนก่อน +6

    Namiwa anabadwa kudzapereka chiyembekezo kwa olema ndi othodwa. Ndimamumvetsetsa pazomwe amapanga,amafuna zabwino zizichitikira pa a Malawi

  • @MikeNguluwe
    @MikeNguluwe หลายเดือนก่อน

    Kwa ine Mike Nguluwe Anamiwa ndi amzanu ulemu wanu anthu Azeru wow ona patli a chikondi wosazikonda wonganizira za athu ena wosakonda ndalama tikuyamikilen tithanzeni kukoza zikoli tiili ndi ana tonse tikupita ku tsongolo ulemu

  • @DavienBanda
    @DavienBanda หลายเดือนก่อน +3

    Atola nkhani nawonso zuwakhuza that's why akusowa mafunso. We need God's presence on this..........

  • @FrancisMcJossam
    @FrancisMcJossam 18 วันที่ผ่านมา

    Namiwa he is my favourite person

  • @felixnzunda1961
    @felixnzunda1961 หลายเดือนก่อน +1

    The other problem we have in Malawi is that we employ soldiers who are our very young children who cannot withstand the pressure and fight.

  • @fysonmalola383
    @fysonmalola383 หลายเดือนก่อน

    We have had a lot of briefings......are we making progress??

  • @sparkdymon3429
    @sparkdymon3429 หลายเดือนก่อน +3

    I trust namiwa hiro

  • @PETROLJ-n1t
    @PETROLJ-n1t หลายเดือนก่อน

    Mr namiwa timakunyadilani pokhala nafe amalawi❤

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs หลายเดือนก่อน +2

    Zamphavu 🔥

  • @JosephyStain-ty9oo
    @JosephyStain-ty9oo หลายเดือนก่อน +1

    I like your voice namiwa you are one continue nyanja ndi yathu not Tanzania apo bii ikhalapo nkhondo M v T tiona kut zikutha bwanja amene angavomeleze zanyanja asowa on this year 😢

    • @FidelisKumwenda
      @FidelisKumwenda หลายเดือนก่อน

      Tanzanians are our relatives, and nobody from around the border with Tanzania will want any conflict with our relatives over a useless topic which only serves people who have no relatives from either side of the border.

  • @PromiseKhenzo
    @PromiseKhenzo หลายเดือนก่อน +1

    NAMIWA THE BIG MAN🎉😊

  • @CharlyChigwembele
    @CharlyChigwembele หลายเดือนก่อน +1

    Big up namiwa

  • @DannieChimenya
    @DannieChimenya หลายเดือนก่อน

    Baba Namiwa god bless ❤️

  • @AwetuAmidu-u2j
    @AwetuAmidu-u2j 27 วันที่ผ่านมา

    👊✊💪🏿💪🏿

  • @LimbikaniTambala-z1y
    @LimbikaniTambala-z1y หลายเดือนก่อน +1

    Mukhalira yomweyo Chakwera mukunenayo awinanso

    • @GraceShaibu-i9d
      @GraceShaibu-i9d หลายเดือนก่อน

      muza winila kubela osati za chilungamo mukunama man

  • @aishamakisudi3220
    @aishamakisudi3220 หลายเดือนก่อน +1

    Our hero Mr

  • @AubreyShaba-b5d
    @AubreyShaba-b5d หลายเดือนก่อน +3

    Hei, Malawi is just a grain of sand full in a wheelbarrow..we aren't even counted worldwide... Check, all presidents except Her Excellency Joyce Banda and Kamuzu Banda,have had fuel crisis shortages of fuel supply..We see no angels here apart from the exceptional two.... Was it not Bingu who said, *Kagoneni pa mseu ngati galimoto sizikupondani* Is this a lie? Or he sounded Eddie Murphy?... Lake Malawi issue: Tanzania Government cannot just change boundary.. Neither Malawi nor TZ can just wake up and draw new boundaries... Country boundaries were a colonial baby, not a single African country drew its boundaries...Go back to Archieves in Zomba and check boundaries as demarcated by colonialists... Northern Malawi border was an agreement for reasons discussed between the British and Germans...Mbeya was part of Nyasaland (Malawi) while North east of Lake Nyasa(Malawi)..belonged to Tanganyika(Tz) The British and Germans settled for a swap... The British released Mbeya to the Germans,(Tanganyika), likewise the Germans released North East of Lake Nyasa (Malawi)to the British... What you must know is that no single country can just wake up and make new boundary without international consultation... it's not an easy process...I see no reason why politicians and some NGOs are shaking knees for nothing.. Those who made such boundaries, the British and Germans governments must negotiate it on a round table..If Tz wants North East of Lake Malawi,then Tz must secede Mbeya City back to Malawi as was the agreement between the British and Germans... International Law on Common Waters was born after this agreement.. They give us back Mbeya City and be part of Common Waters..No such a thing will work until Tz gives back Mbeya City to Malawi... unedited text...

  • @NovahiwaInnocent
    @NovahiwaInnocent หลายเดือนก่อน

    Namiwa ndi deal, keep it up

  • @chimwemwenkute3839
    @chimwemwenkute3839 หลายเดือนก่อน +2

    Katundu waboma uyu he's a freedom fighter

  • @lewisdicksonmlozi130
    @lewisdicksonmlozi130 หลายเดือนก่อน

    God bless you guys ❤

  • @GiftSoko-w4h
    @GiftSoko-w4h หลายเดือนก่อน

    Big up Namiwa mumatiyimilila

  • @ShukuraniTonex
    @ShukuraniTonex หลายเดือนก่อน

    God bless you guys ✊️

  • @nthawigolowa5158
    @nthawigolowa5158 หลายเดือนก่อน +1

    I like the confidence from Mr. Phiri.. Good composure

    • @KumbukaiMtawaliWaMoffat
      @KumbukaiMtawaliWaMoffat หลายเดือนก่อน

      @@nthawigolowa5158 Why is Israel in Gaza?

    • @nthawigolowa5158
      @nthawigolowa5158 หลายเดือนก่อน

      @KumbukaiMtawaliWaMoffat why are u asking me that? Didn't u hear from the briefing

    • @InnocentMtafya-c6b
      @InnocentMtafya-c6b หลายเดือนก่อน

      ​@@nthawigolowa5158, Kodi awa ndi azibusa mumati Ojiya waja akusiyana bwanji?

  • @eunicesaiti
    @eunicesaiti หลายเดือนก่อน

    Much respect Mr Namiwa 🙏

  • @TokozaniBanda
    @TokozaniBanda หลายเดือนก่อน +2

    Kodi munthu ngati amakonda anthu ake angadane naye chakwera ndi galu kapena mbuzi iweso ukusapota chakwera ndiwe galu kwabasi munthu osaganiza komaso wosaganizila ziko kapena amalawi.namiwa continue tili pa mbuyo pano tichela ziko lanthu

  • @EUGINEMWADALA
    @EUGINEMWADALA หลายเดือนก่อน +1

    Ndipo mai olemekezeka dr Joyce Banda solved it very well ndipo muthawi yochepa. It may look simple kokano that boundary tizalira tizapanga regret malawi will still remain poor and land locked. We already have few resources and we are failing to manage then instead tikungobetsa kwa azungu ndi maiko oyandikana nao thats being unreasonable

  • @AlihIbrahim-s7v
    @AlihIbrahim-s7v หลายเดือนก่อน +7

    Akristu ena ndiwozitsata eeee 😂😂😂😂

    • @NdaonaMsowoya
      @NdaonaMsowoya หลายเดือนก่อน +4

      Kristy nsilam tosefe ndi amozi palibe kusiyana apa km chigawenga ichi mumati chakwela azafa ifa yowawa kwambili

    • @AlihIbrahim-s7v
      @AlihIbrahim-s7v หลายเดือนก่อน +2

      @NdaonaMsowoya 😂😂😂😂😂adzafa ngati chitete chofela pa tsekela

  • @LastbornEnd-r9c
    @LastbornEnd-r9c หลายเดือนก่อน +3

    Koma awawa ayankhura kachiwiriwo akufunika adziyankhura yankhura plz mr Namiwa

  • @macdonaldkainga
    @macdonaldkainga หลายเดือนก่อน +1

    Namiwa umatha

  • @abangaabanga4677
    @abangaabanga4677 หลายเดือนก่อน +1

    Mawu......Mawu.....!

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule หลายเดือนก่อน

    Namiwa Big man ❤

  • @AlexanderTraffick
    @AlexanderTraffick หลายเดือนก่อน +2

    Wachiwiri kurankhurawe mmmmm ndakupatsa ulemu .uli ndimfundo komaso umadziwa kutambasura nkhani.History it's a best teacher

  • @WellosMoyo
    @WellosMoyo 18 วันที่ผ่านมา

    Asilikali,nanuso mukuopa Tanzania?

  • @SheriffBakili
    @SheriffBakili หลายเดือนก่อน +1

    Anthu akufa kumeneko sasilamu okha ena ndi achi khilisitu

  • @mikechasowa5915
    @mikechasowa5915 หลายเดือนก่อน +3

    A Mtondo Namiwa

  • @JosephHill-fy1bb
    @JosephHill-fy1bb หลายเดือนก่อน +2

    Nyanja imeneyo lazaro adzabweza ndalamazo...

  • @ThandiswaMqakai-v4i
    @ThandiswaMqakai-v4i หลายเดือนก่อน

    Am second tired with Chakwera
    Go to Ntcheu Dzunje area
    No good roads
    No good infrastructure
    No clean water
    I am here now
    Where is Malawi government?
    This is the home of my father
    But authorities please give them good tarmac road
    Thank you

  • @LukeMapukusa
    @LukeMapukusa หลายเดือนก่อน +4

    Chakwera wamaliza dziko lathu zed Nyanja yapita bas

  • @elishabanda1332
    @elishabanda1332 หลายเดือนก่อน +1

    Alomwe awa they want muthalika mu longwe nzawo agalu

    • @Geraldmkwewu
      @Geraldmkwewu หลายเดือนก่อน

      galu ndiweyo nose ndi chakwera fiti lnu

  • @GiftPaulMaononga
    @GiftPaulMaononga หลายเดือนก่อน +1

    Bwerela zokhazokha, palibe cha nzeru chimwe ndatolapo

    • @hannah-gs2kh
      @hannah-gs2kh หลายเดือนก่อน

      Muchira simunati muzingomwa mwandondomeko

  • @BOSTONMALISAWO55
    @BOSTONMALISAWO55 หลายเดือนก่อน +1

    KOMA CHAKWERA AKUMANA NAZO LELO 2025 KOMA AFA INFA NTHAWI YA MASANKHO ASANAFIKE IZOOO .CHIKHUNI CHAKALE NDICHOMWE CHIMASUNGA MOTO .....DPP ITENGA BOMA MUFUNE MUSAFUNE AMEC ASAZAELEKEZE KUFUNA KUBELA AZABWELETSA NKHONDO OSATISO NKHONDO NGATI ILI KU MOZAMBIKI MALAWI WALERO NDI WACHAMBASOTU MUZAONA .

  • @DeavncKapesi
    @DeavncKapesi หลายเดือนก่อน +1

    So sad 😢😢

  • @Nelsonmatenda
    @Nelsonmatenda หลายเดือนก่อน

    Namiwa timakuyamikani kwambili..mcp ichoke pa 16 Sept 2024

  • @MlaziJames
    @MlaziJames หลายเดือนก่อน +1

    Atule pansi udindo mr chikangawa

  • @stevenmwamadi3035
    @stevenmwamadi3035 หลายเดือนก่อน +1

    Osaopa osatopa osafooka comrade namiwa uremu wanu basi chakwera angochoka basi

  • @AarongeoffreyKaluwa-eb7ot
    @AarongeoffreyKaluwa-eb7ot หลายเดือนก่อน

    MCP is a cased party. Any one who joins MCP, no matter how blessed he or she is but will be cased as well. You must pray and watch Which party to join.

  • @vivianmkwate8536
    @vivianmkwate8536 หลายเดือนก่อน

    Bravo CDEDI

  • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
    @ChikumbutsoJohn-rs4tt หลายเดือนก่อน +1

    This chakwera regime is not chifuniro cha Mulungu yes,

  • @GraceChenda-q2g
    @GraceChenda-q2g หลายเดือนก่อน

    Wawa Namiwa

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz หลายเดือนก่อน

    That's the point icc ukufunika ndithu

  • @MosesTangwe-q8o
    @MosesTangwe-q8o หลายเดือนก่อน

    Ngati anatseka admark zogulitsa nyanja tisakaikire tilindi gwape wa president oti mmutu mwake mulibemo kanthu

  • @GhamaJohnus-b7x
    @GhamaJohnus-b7x หลายเดือนก่อน

    Abiti mumakwana landlani maluwa anu (achakwela asatibwezelese m'mbuyo)

  • @LufingoMulungu-z7u
    @LufingoMulungu-z7u 29 วันที่ผ่านมา

    Anamwiwa mumatiyimilira popanda inu zikoli bwezi palibepo

  • @AlfredKamphonda
    @AlfredKamphonda หลายเดือนก่อน

    Atola nkhani mmakataniko?

  • @RickBanda-p3m
    @RickBanda-p3m หลายเดือนก่อน

    Ngati malire amavuta a Munda mzere umodzi mpaka zikwanje nde mukanene dziko we have defence force and their major responsibility is to defend the territory akuchedwa pati let them go their anyamata a mmadzi akateteze nyanja go

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete หลายเดือนก่อน

    Free Palestine chakwera anavotela Israel Kuti izipha ana Ku Palestine mapwala ake chakwera panyapakepo ndintu 😢😢

  • @Mirriumkamwendo
    @Mirriumkamwendo หลายเดือนก่อน +1

    Tili pambuyo panu a Namiwa

  • @mansonchinkhuzi
    @mansonchinkhuzi หลายเดือนก่อน +2

    Uyu atule pansi udindo wa HRDC sakukwana wangokhala odzazidwa ndiukali koma mulibe utsogoleri pasankhidwe wina basi

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 หลายเดือนก่อน

    Nuff respect!....chakwera can not sell the lake ndikuchindila ndalama zonse mahule ndi achina chimwendo kunkuyu ndi zikhale kamajekete...osaiwala hule nanse mbeto

  • @SovietMzungu
    @SovietMzungu หลายเดือนก่อน

    Politics

  • @FridayKabade-t7x
    @FridayKabade-t7x หลายเดือนก่อน +5

    I starnd namiwa God is good all the time never give up more fire atiuze tiyambise tikatengeko nyanjayo

  • @EUGINEMWADALA
    @EUGINEMWADALA หลายเดือนก่อน +2

    2025 CDEDI yoyeeeee yanyanjayi tikhalitsepo