Zomwe ayankhura Mai Joyce Banda zokhunza Tonse Alliance kucha kwa Lero

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 13 ก.ค. 2024

ความคิดเห็น • 52

  • @PreciousKaliati-l6u
    @PreciousKaliati-l6u หลายเดือนก่อน +3

    Your excellency,Dr banda, your charitable initiatives are reflection of your remarkable character and dedication to the betterment of society. Keep shining mama , kudana ndi inu ndi thembelero chabe.God bless you

  • @MphatsoMhoney-xn2ft
    @MphatsoMhoney-xn2ft หลายเดือนก่อน +2

    Malawi leaders are always talk wisely when they are out of gavervent,give them charnceand see there performance

    • @mwale86
      @mwale86 หลายเดือนก่อน

      This one performed kungoti amalawi mpandila u can't appreciate because she is a woman,when she came in kunalube fuel kunalibe Forex anthu kuchipatala kumwalila because of magetsi after generator zinalibe fuel magetsi akuzima mwanyasi but she did it in just 100 days I feel that's something we need to acknowledge that she did good.

    • @chelseajackson3200
      @chelseajackson3200 หลายเดือนก่อน +1

      Performed where?? She is full of family politics. Look at her age kukakamila leadership in PP. I bet she was one of those voices calling for Chilima to join MCP! Fully knowing that she will get in through the backoffice.

    • @Lee-lee-w1r
      @Lee-lee-w1r หลายเดือนก่อน

      @@mwale86why do you want to make women to look like they are the most hated beings for no reason?? Pali zinthu zina zake adachitadi bwino koma anapoilabe ndithu.

  • @chelseajackson3200
    @chelseajackson3200 หลายเดือนก่อน +2

    Alipo women & girls oti anapindula ndi izi akamba awa?? Atchuleni. She could've mentored a girl or girls for presidency if she was sincere😢😢

  • @SanidaChirwa
    @SanidaChirwa หลายเดือนก่อน +4

    Our excellent ngat mfuna mbiri yanu izakhale yabwino mkamwalira ,tulukani mu Tonse Alliance,mpakidwa magazi oyipa kwabas

  • @user-uv5rf4zt5q
    @user-uv5rf4zt5q หลายเดือนก่อน

    The best leader

  • @GilbetaMasamba-te8kp
    @GilbetaMasamba-te8kp หลายเดือนก่อน +1

    God continue bless you your excellency ma, your such a blessing to malawi

  • @NatashaMakay-k5e
    @NatashaMakay-k5e หลายเดือนก่อน +1

    Anthu omwe munapanga ngwilizano, mumafunika kutuluka kalekale. Mwaona zisankho zayandikila muzioneka ngati okonda anthu..antku munawatengela kumavuto.

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 หลายเดือนก่อน +5

    Aaaa awa amayi adyela adzuzitsa malawi kutipatsa MCP yokupha komatsa yankhaza iiiiii tsitidzayiwala mayi banda anatipanga nkhadza dzedi chifukwa chofuna moyo wawo kukhale pabwino otsati amalawi akhala pabwini ayiiiiiiiiiiiiiiiiiiiii mulape mulungu akhululukileni mwanatiyika pa dzuwa

    • @mkajikosya-uq5hs
      @mkajikosya-uq5hs หลายเดือนก่อน

      Nanga malemu SKC apepesenso?

    • @FosterChakanga
      @FosterChakanga หลายเดือนก่อน

      ​@@mkajikosya-uq5hskumakhala ndi umunthu sometimes

  • @chikondichanza9772
    @chikondichanza9772 หลายเดือนก่อน +1

    Mayiwa is one of the creams ku Malawi Kuno. Awawa ndi machine enieni. Kudana ndi mayi awa ndikudana ndi chitukuko. aMalawi amzanga alot of known countries are recognizing her as very important trustworthy and helpful woman , why not us . Lord should have mercy on us , so that we can how potential this woman is. aMalawi tinazolowera kutamikira munthu akamwalira.what a shame

    • @juntoiman
      @juntoiman หลายเดือนก่อน

      Mmmmm Iwe wachibwana Eti Ameney Mesa ndimunthu Modzi adapusisa malawi

  • @user-ry9ql9jv3y
    @user-ry9ql9jv3y หลายเดือนก่อน +1

    This woman is our Gem. Very good and we love you

  • @MaryMlomba
    @MaryMlomba หลายเดือนก่อน +1

    Repent before it is late

  • @RuthChilobwe
    @RuthChilobwe หลายเดือนก่อน +2

    Kkkk Ndàlqma za cash gate zao sadzatenga kumanda.ayi..kumwamba sikufuna cuma..nkhale awawa a mr Sattargate wa a mcp wa ndi zinduna zaozi.kwa Yehovah kuchiweruzo sadzatenga Sattargate chuma chaocho amenYoù honoüable Robbers of our nation just be awaiting to be thrown in ĥll fire by Jesus Cĥrist.for crime of Stealing or Robbing malawi nation.all the same .be blessed as you walk towards jesus christ to be judged

  • @mkajikosya-uq5hs
    @mkajikosya-uq5hs หลายเดือนก่อน

    God bless her excellence Dr Joyce Banda

  • @dianachabs
    @dianachabs หลายเดือนก่อน +2

    Ambuye adzikudalitsani masten ntchito zachifundo ndiye mukuzichita

  • @AlexBand-f4p
    @AlexBand-f4p หลายเดือนก่อน +1

    Mwaganiza bwino kwambirimbiri tulukakoni kumeneko mwaganiza bwino kwambiri mayi zikomo zikomo

  • @vitujames53
    @vitujames53 หลายเดือนก่อน +1

    Chipanda Dr Joyce Banda sitikanadziwa kuti mu Boma mukunedwa ndalama

    • @mwale86
      @mwale86 หลายเดือนก่อน

      Ndipo zowona no president has allowed an audit while in office it's only HE Dr Joyce Banda mayi awawa ndikatundu

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 หลายเดือนก่อน

    Unakasiya Chilima mkamwa mwa Ng'ona.

  • @BenardPhili-wp5jt
    @BenardPhili-wp5jt หลายเดือนก่อน +1

    Amayi anthu timakukondani komanso Inu Mai mumatikonda amalawi munawamangira yumba anthu osauka ambirimbiri kuno kunkhamenya, anthu atavutika ndi ngozi za madzi munawathandiza powamangiranso nyumba kumwera

  • @FosterChakanga
    @FosterChakanga หลายเดือนก่อน +1

    Tulukakoni masten,,asakupakeni nawo manyiwa pliz.Inu ndi mbambande

  • @gladysbonongwe1038
    @gladysbonongwe1038 หลายเดือนก่อน +6

    Makhuluku akumalawi

    • @vitujames53
      @vitujames53 หลายเดือนก่อน

      Ukhuluku wakuti anasintha dzikoli with 100 days ukhuluku anapangila kuti

  • @PreciousJames-fh1xs
    @PreciousJames-fh1xs หลายเดือนก่อน +1

    Amai mumakwanila palipose zitukuko muno mudziko lamalawi mwapanga m, boma ririrose
    Tikanena zothandiza osowa nde ndikudya kwanu ndipo simuona khope kana mtundu
    Amai Banda Mulungu azikudaritsan thawi zonseeee eee

  • @DevisonHala
    @DevisonHala หลายเดือนก่อน

    Inu mayi chilima mumanena kuti ndi mwana wanu ndiye munachilandila bwanji chipongwe chimenechi

  • @vitujames53
    @vitujames53 หลายเดือนก่อน

    Anamanga nyumba Kameme , Chisenga in Chitipa District..
    Chilumba and Khwawa in Karonga
    Chintheche, Bandawe, Vizara, Chisala in Nkhata Bay
    Mzimba Boma, Njuyu, Thunduwike, Nkhamenya in Mzimba
    Lula and Ng'onga in Rumphi list endless under Mudzi Transformation

  • @BlessingsBanda-nh7ur
    @BlessingsBanda-nh7ur หลายเดือนก่อน

    Zilibwino koma zomayika background music instrumental ndizopoyila pama serious massages

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani5697 หลายเดือนก่อน

    Lankhurani chabe chichewa

  • @vitujames53
    @vitujames53 หลายเดือนก่อน

    Anthu amalandila nkhuku kumaweta mabanja kumapeza ndalama ndikumadya bwino panyumba pawo..
    Mbuzi, N'gombe

  • @SaeedHurzrut
    @SaeedHurzrut หลายเดือนก่อน +1

    hule wachabe chabe

  • @vitujames53
    @vitujames53 หลายเดือนก่อน

    Nthawi yawo mankhwala mzipatala samasowa..kunalibe basi kaguleni ku pharmacy

    • @mwale86
      @mwale86 หลายเดือนก่อน

      Ndipo zowona

  • @Shelifibraheem
    @Shelifibraheem หลายเดือนก่อน

    Mmmmmm m'mai otapa tapa uyu uliboh mudzapita ndindalama amzathu

  • @vitujames53
    @vitujames53 หลายเดือนก่อน

    Nzeru zawo ndizopititsa patsogolo dziko maka maka anthu ovutika ammamidzi

  • @vitujames53
    @vitujames53 หลายเดือนก่อน

    Ambuye azikudalitsani ndikukupatsani moyo wautali

  • @rightlombe380
    @rightlombe380 หลายเดือนก่อน +2

    Which youths do you assist?

    • @mwale86
      @mwale86 หลายเดือนก่อน

      Ambilimbili through her community Development initiative project people mainly youths benefitted kupeza chakudya in kasungu isn't that helping youths??

    • @mkajikosya-uq5hs
      @mkajikosya-uq5hs หลายเดือนก่อน +1

      Ambiri anapindula anagawa njinga zamoto pano akulipilira ana ma school fees through Joyce Banda foundation

    • @mwale86
      @mwale86 หลายเดือนก่อน

      Ndipo zowona zake even she feeds over 15,000 children through her Joyce Banda foundation pajatu Amati mmela poyamba hence ana akakula bwino azakhala ma youth othandiza dziko lawo​@@mkajikosya-uq5hs

    • @vitujames53
      @vitujames53 หลายเดือนก่อน

      Kodi kabaza ku Malawi kuno anabwera ndindani

    • @vitujames53
      @vitujames53 หลายเดือนก่อน

      Tapitani ku ma secondary a Boma mdziko muno atsikana akupelekedwa ma fees..

  • @vitujames53
    @vitujames53 หลายเดือนก่อน

    Mzimayi wachikondi uyu

  • @JusticeMpondaphili
    @JusticeMpondaphili หลายเดือนก่อน +1

    Awa ndi mai amzelu sangakakamile ku mcp acokako

    • @user-px6kt8rx2p
      @user-px6kt8rx2p หลายเดือนก่อน

      Nzeru sabwelekana inuyo muganiza zanu

    • @user-px6kt8rx2p
      @user-px6kt8rx2p หลายเดือนก่อน

      Inuyo mukati achokako ku mcp inu mudakhalapo wa mcp?

    • @user-px6kt8rx2p
      @user-px6kt8rx2p หลายเดือนก่อน

      Sitikufunaso makadeti muno mmmalawi