Dan lu ati palibeso wina ife titi chan ndye chipani chantendele Ali wa DPP chala mwamba apa ziwawawe aliko☝☝☝👏👏ulum kwa Peter big man bingu muthalika nzimu wako ukuyendabe kuno phwako uja akukondedwa ndi anthu malo mwaiwe professor simunthu wamba banja LA kwa muthalika ndi akamuna amwene eehh lodala banja munayamwa apule munthu wankulu
Amene mukuyakhura zamwano apa mulibe nzelu osangokhala bwanji osakomenta ndinu munamupha chilima eti mbuzi za athu chalakwikapo ndichani pamenepapa agogo ndabambo ako ufune usafine peter alowanso ❤❤❤❤❤
Bro osavutik ndikuwayankha amenewo Peter kufuna osafuna akulowa bs we must know that
😂😂😂@@AngolanChinga
@@YankhoGuza Madzi akamaphwa amabwera pamodzi
Kodi chilima anachita kuphedwa kani
Nankhumwa ndi chimulirenji ali kuti kodi
Chikangawa party I think ilipompa kukomenta nao zinthu zanegative.Munyanane...Apm my vote❤❤❤
Ndiye convention inali ya chani yopanda opikitsana i only support federal system of government in Malawi.
Koma ndiponso inu chinsankho chake chosekesa chopanda munthu wina aaa
Macoment enawa ndiianthu agulu lachikangawa
Kkkkkkk
Mcp okupha
Umangodziwiltu
Ndipo inu moti zinthu mmene zilili kuno ku malawi anthu ena nkumati zikuyenda aaaa mulungu ndiwadongosolo atimenyera nkhondo
Mr chikangawa 5 years nothing as Malawians achieve from him ,
Congratulations DPP ,
Ine ndine wa UTM , koma 2025 vote pa APM ,kaboma aka kazipita please
Apm my vote
God bless muthalika ❤❤❤❤
Koma mikundinvesa kukoma abale😂😂❤❤❤❤
Mcp ndi bomadi izizi ndizabwana kobveshoni ndimaona ngati amapikisana
Ana sangilatu Mbali yiliyonse nfichifukwa Chaka zanapikisane komaso ndi anthu omwe ndi osiwika kale
My vote APM ❤❤❤
My vote apm 2025
Ngati angoti tivote mawatu APM my vote
Aaaa anthu onseo ichi ndiye chibwana mcp boma
Mutiuza
Tinthokoze nonse mwasankhidwa kut mupabe ubale unodzi mutiombele mumavutowa atikwana zinthu zadula kuposa chakwela❤️♥️♥️♥️♥️
Ukhaula iwe wakuchikangawa pita uko usamaike comment sizikukhuza kapolo iwe
APM my vote 2025 Boma
Dan lu ati palibeso wina ife titi chan ndye chipani chantendele Ali wa DPP chala mwamba apa ziwawawe aliko☝☝☝👏👏ulum kwa Peter big man bingu muthalika nzimu wako ukuyendabe kuno phwako uja akukondedwa ndi anthu malo mwaiwe professor simunthu wamba banja LA kwa muthalika ndi akamuna amwene eehh lodala banja munayamwa apule munthu wankulu
Ndye kwabwinotu ,kosapikisana kkkk kkkkkkk ay aaaa kaya mwina........my vote be basi nanga mkutaaa
Convention and democracy has a different meaning in the blue camp🤔🤔🤔 or akanagoti akulegeza zotsatira zakumkumano waku Page house
Dpp my vote
😂😂😂😂😂
Ine kwanga ndikuonerela gule opanda nyimboyi 😁😁😁😁
My vote apm basi
❤❤❤❤❤ Apm
Kwanuko kunachuluka dyera mpake opikisana mbweee😂
Amakosana mukubowa tisaname...upgrade plz
APM my vote
𝙸𝚝𝚜 𝚠𝚑𝚎𝚛𝚎 𝚖𝚢 𝚟𝚘𝚝𝚎 𝚌𝚊𝚗 𝚐𝚘.
Ka sound kamene mumayambilira kutipatsa uthenga ndikonyasa kwambiri
Chikangawa kunukha kukhwapa
Nkhalamba APM
Awa ndi aja timati masanje
Mma position akuluakulu azimai awamana
k
dpp chipani chachikulu nggati chimenechi anthu sangalemphele kupikisana wu
Chakwera paja anapikisana nd ndan ku convention?
Paja mcp amafuna kulesa ena mpaka ku court.
Komso nec yonse ya mcp...central region
Olo mumunyoze pita koma palibe chomwe mupindule ndiekhayi munthu amene anatipasa mulungu enanu ndi akupha masataniki inu fosek
Kkkkkkkkkk zilikomuzivoteranokha ma robot wooo
Kkkkkk kulibeko zopikisanatu kumeneko eti
Ma udindo apite zigawo zonse beta bc
Iyi ndi njira ya mtanda simasankho amenewa munyanane 2025 ine ndine mcp
APM woyeeeeee Japi Mhango woyeeeeee
Ndili ndichiyembekezo Kuti 2025 nyasi zomwe zilipozi zikuchoka zatiwonongera dziko lokoma lija latendere
DPP boma 💙💙
Iyi si convention koma kuzaitana mayina
APM Boma we are praying for Malawi my mother land 2025 Boms ilo osawopa In God we win
Ndimava mawu ambiri azibambo pansi pansi kusonyeza kuti chipanichi chilindimphavu kwambiri
Zopusa masankho amapanga choncho uchitsilu
Ndipo inu
Galu iwe ukuti chani ana achikangawa inu anyalugwe
Zamunyasa ayanike ufa pachingwe,
Ana okupha achikangawa Inu
Well organized
Nde convention wanji sanasithebe akanakhala awawa eti mbalame za wathu mzimu wa Dr Chilima uziusabe mumtendere mukananya nose mcp ndi dpp
Chipani Cha nkhalamba,a dad kukakamila mpando yet akukanika ileven kuzutsa dzanja,Malawian politicians they are too greed for power
Congratulations DPP.... Convection yayenda bwino.
Ana anjoka mukuona ngat mungaloweso m,boma kut muzizamenyaso anthu ma bar iwalani zimenezo zaana adad kwanukomko
Galu iwe pita uko
dpp Boma 2025
Masanje mipando yonseyo anthu sakuifuna?
Akumva pain apaseni panado!
Taona maboma ife koma nyasi izi za kaboma aka ka chikangawa sindinaone
Azimai Kulibe Ku dpp or gender kulibe
Tikufuna tichose nyasi izi za MCP, kulibe kuwima MCP kwawo kwatha ndipo chipani cha MCP chathhera popo ali ndi zeru akuwona sichingazalowenso boma mpaka mathero adziko lino.
Zokungola ❤❤
Pepani amcp musalowelere sizikukhuzani izi ndi za dpp full stop
Too much osapikitsana no democracy. Or rubber stamp democracy .
Chipani chamakape cha dpp kuyambira President mpa mipando ina yochuluka opanda opikisana nawo ku phangila basi makape awa
Imwani panado,musadagwe😂😂😂
Get well soon bro 😂😂
Yabaya chakupwekani ndichani
Muchira Koma mochedwa
Dpp tipulumutsen ku nkhaza ,!!!
Ma unopposed achulukatu kusowa anthu chani?
Magogozeni akonzeka kukaba mboma
ndi kutsekanso njanji ndikukayimitsa kumanga misewu munya agalu inu
Chipani Chama robot vote palibepo pamenepo
Ine olo nditamwa delunde siningadzavotere m'kwadzamba
Asiyeni anthu akuphawo ife zanthu ndizau Christu pamene inu zanu masiku onse ma plan anu ndiongoganiza zopha anthu basi..... Mukufunanso kuti mupitilize kulamaula kuti mutipherenso anthu ena basi inu anthu Achikangawanu
Zilibwino 🎉
Achikangawa ali mommuno zanu izoDpp woyeee
Amen
one kuva kukoma mutima mwe
Koma mwati ndikobveshoni nanga bwanji anthu sakupikisana tiziona
Za chibwana zimenezo agalu inu kkkkkk
Sizankasatu izi 😅😅😅😊
Aaaah kodi dpp bwanji kupondereza u president osawapatsa ena mwai bwanji?
Term ikubwerayi muona mnkhope za chilendo but for the time being tilolen tikunthe uyu kaye
😂😅😂😅😂 ndpo kukutha ngt pang'ono @@CharityChanzah
Anali atasankhana kale uku ndie kutha kwa chipani uku
Mmmmm manyaz bwanj
@@CharityChanzahspa ndiye corvetion mukatani olowa ndi miyendo athu 20 aaaaa mugotaya thawi
Iiiiiii kkkkk chikangawyo
@@kingsleyhopematchaya5184amakhala kut ndi abwino ndikale...no change...even enawo amadziwa kut sangawine olo atapikisana enawo
Wachikangawa iwe inja
This is nonsense. what's the meaning of having convention when there is no one to complete on the positions. Aaaaaaa eish what a drama.
DPP dzitsilu they worship a person instesd of party.
APM ndi DPP tengani bomali amalawi alandire ndalama zao za pension zomwe alipowa akulephera kupereka mpaka, zaka zitatu anthu akuvutiikabe
Chikangawa watani kumabwera ndima comments achabe apa wakhaulatu
kunena zoona apa dpp yatha sindikuona munthu oti angapange kampeni ai ine ndi wa dpp koma zomwe ndikuona mmmmmmm
Koma kuti chakwerako wapya mutima kwabasi
Wapenga ndichiya kape iwe
Wapenga ndichiya kape iwe
Wapenga ndichiya kape iwe
Wapenga ndichiya kape iwe
Wapenga ndichiya kape iwe
More bpp 2025 boma basi osati chikangawa😂😂😂
Aliyese akwera yake
Nkhalamba zokha zokha yooo
Kubwera zikufunika chocho 2025 boma basi tichokeko kuno ku South Africa tikapange zathu ziko LA mtendele
Tikulowanso boma 2025
Apa zilibwino Kwambiri.zosangalasa Mayina amene kumwamba Kwa vomereza .osati kumawagulila anthu zinjinga kugawa ma million kupita Kwa azising.anga Kuti muwine Inu nokha nokha kuphana ..izi sizamagazi zamtendere ..ana achikangawa munva madzi ..😂😂😂 APM Moto Kuti buuu❤❤❤❤
Ndiye chochitira masankho ndichani apatu ndichimozimozi kumapita kuchipatala mutaziw Kate Kuti munthuyo watuluka kare
Ndie vuto lako nchani galu
@@FatimaNakomazamanyazi mukanagokhala ku magochiko mesa munasakhana kale
Adadi omwewo
Kozani admarc 2025 bwana.
Tsamafuna za ndewu nchifukwa anasankhilathu
Suleman alikuti
Tanthauzo leni leni la dpp ndi lakuti
"DONA PAMTUMBO PAKO" (DPP)
Kutukwanatu sikupindula limbikila kusaka ndalama nzanga anthu andalewatu ndiamozi timangozivutisa anphawife kutukwana
@@JhdaLifi-vu9sd zooona
Koma manyazi mulibe, inu ngt muli amcp sibwino kumagwela za a zanu kumatukwana. Ulemu ndi ofunika
Pajatu Chikangawa Party ngodya zanu ndi zimenezi. Kutukwana, Kupha ndi Kuba. Sitili odabwa nanu.
Chikangawa utonyapo apa
Chipani cha nkhalamba
2025 kuchema
Boma ilo
💃💃💃
Zilibwino
Adad the great
Mukanangopatsana mapozishoni osati kupanga convesione,,iyi siconvesion awa ndimasanje ndi azigogowa.
Mwana wa nyau kagwere uko, ukuyetsa ndi chikangawa party iyi
Komanso kumuona munthu wakeo omvetsa chisoni_ sukugona kwanu ndi njala iwe
Iwe si nyau imeneo wamva mapwala ako agulewo
Awononga nzanu kodi?