ขนาดวิดีโอ: 1280 X 720853 X 480640 X 360
แสดงแผงควบคุมโปรแกรมเล่น
เล่นอัตโนมัติ
เล่นใหม่
Mtsogoleri akuyenela kukhala munthu oleza mtima. Osabwenzera choipa . Komano a Chakwela ngati mbusa ayi ndithu, zawabvuta ndipo sitimayembekezera kuti ulamuliro wao ungakhale oyipa moteremu. Chifukwa iyeyu amadziwa bwino lomwe za umoyo wa uzimu. Lero wasanduka wakupha . Anapha Sidick Miya komanso Saulosi Chilima ndi anthu ena omwe anali mu Ndege muja. Ifeyo tikudziwa zonsezo ndipo ma umboni alipo. Chakwela galu ameneyi , owona mizimu yonseyi singamusiye siye ayi imumzunza ndipo azunzika koopsya pansi pompano Chilango chake cha Mulungu asanachilandire galu ameneyi.
@@HamiltonwaNamuwahkoma awinabe.
@@VincentManyenje ndipo nkhan zaifa za anthu aja zisiyeni coz umbon mulibe kut anaphedwa nd munthu wina aiii... Mulungu ndamene akuziwa... ku Malawi vuto ndlimenero Kukonda kulenga nkhan
❤❤ochewa ozanga ozindikila Dpp oyeeeee 💥💥💯 ❤❤
Mbuz zimalakhur paja zja mpaka mun2 kumanyumwa nazo?... Evn kwao zngakope anthu😂😂😂😂😂
More 🔥🔥 adadi tikudikirani 2025 mwina moyo wungasitha 💃💃💃
Ichi ndi chathu ichi
Dpp,UTM,UDF,afford,,tagwilanani manja tichose amalawife Ku iguputu komwe tikumphula njerwa za moto
Munthu wakulu Brian Band mmmmm guys munthuyi akapangako kunali ntcito
Anthu awa akalamba asiyile achinyamata
Inenso ndi Mchewa koma palibe chomwe yapanga MCP. Panopa biziness ikukomera oremeretsetsa.
Wachikulire sakhala ndiphuma akukagona woyeee
Zizafika poti olo a pule azavotera APM....kkkkkk
Mwana wa pa Dowa kulankhula chilungamo
Dpp yomweyo
Vilombo vozindikila
DPP OUR LAST HOPE
Kkkkkkkk koma ochewa mukuithanulatu apa 😅😅😅
Brian wadzinvela wekha ndi a Malawi onse. Zinthu silibwino mu dziko.
Anaziwa adad kuti or achokepo ana awo sangamenyane
Powerful brothers
Tawina kaye...
Nayenso Chaponda wakalamba mpaka 81 kakaka
Achewa awa ayankhula zonveka kwambiri
Nganga bulawayo wakagona watopa, nkhalamba yachabechabe
Peter watopa koma tikanampumitsa 😢😢😢😢
Brian uwapusita achewa koma mchewa sangaone kuti akuwapusitsa kodi mafuso amenewa adawafusa choncho kufunsa anthu aku Tyolo
😂😂😂😂 kma Brian ukhalike
Onyamata odziwa kulankhula ndi ozitsata ❤❤❤
Eeeeee Koma Cathay ndi Brian kkkkkkk
APA ndiye.dzikundivekelabwino.Dpp.wooooyeeee
APM my vote ❤
Awa nde anthu ozindkira kwambri
❤
DPP THE ONLY TRUSTED PARTY WHOLE NYASALAND
Kungonva kuti chatuluka mdabwe changa😂😂😂😂
Km Brian 🤣🤣Aliunena zoona
APM WOYEE
Zikhale chani kodi usiku umenewu
Koma chichewa chaku Dowa nchokoma
❤❤
MWAYENDA BWANJI ? TAKWERA MAMINIBASI😁
Kkkkkkkkkkk
🤣🤣😞😞 mchona wapita kukagona
Labourers work more than professionals, biggy amagona ndi kudzuka nthawi yabwino
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Tumidala tovuta utu situkufuna kusiyira anyamata
Akut tawina kale 😂😂😂
Koma Brian anakonza
Woyeee
Dpp woyeeeee
Mbambande DPP❤❤❤❤❤❤❤❤❤
God bless Malawi
Ndipatse number ya Brian Banda guys please
Nice one 😂😂😂😂❤❤
Brian Banda umakwana 😂😂
Chatopa chapita
Jerous people never winnnnnn!!!!!!
DPP wooooyeeee
Kulamudi dziko sikuyakhula bwino English
Ndipo thaw mkachitsirud 😅😅
Yakwani thawi
APM❤❤❤❤❤❤❤❤❤
at fateleza
Dr chikangawa alibe mawu
Dr albino sangawine .
@@VincentManyenjeiwe pamtumbo pako Chakwera sangawine mistek yopha chilima ija zinalakwika pamene paja chomwe ungadziwe dziko lapasi limalamulilidwa ndi Roman catholic wekha malizitsa
@@Musa1828-l5d usavutike ndikutukwana koma ziwa kuti MCP ikupitilira ku lamura .sunga mawu anga.
@@Musa1828-l5d mpaka kumutukwana nzanu nkhan yake iti😂😂😂😂😂
INE NDAVOTA KALE DPP 2025 BOMA
Bola ngati sanagwe pa mpando
Olo atagwa mkufa koma muthu ozindikila sangavotere munthu opha mzake pamtumbo pakoso iweyo ndi chakwera wakoyo panyini pamanu nose
😂😂😂😂😂😂muuzen chilungamo ameneyu😂@@Musa1828-l5d
@@Musa1828-l5d inu abwino mpaka kumatukwana anzanu... Namkhumwa my Vote
Mmmmmm APM wathawa kuopa kugona
Nde asakagone chifukwaaaaa
MLC anachezeratu
Waiopeladi 😂😂😂😂 koma alibho
@@ibrahimjackson-cg6tc kkkkkkk pamenepo
@@CoshantAsante Ndiye kuchedzera kwa Chakwera kunapangitsa kuti sugar atsike mtengo??
Walira mwana wapedegu 😅
Koma Malawi tinapusa kwa basi
Bwanjinso nanga
DPP ndichipani chafiko, chosapha,
Ma albino ajaaa zinali zinyama? achinyamata azathu anawaombela Ku Mzuzu pa 20 july ajaaa ndi nyama??
@@macleanwazalanyirenda4994 Ma alubino ankhaphedwa Chakwera nanu ali ku opposition pofuna kuyipitsa mbiri ya APM anthu 20 aku Mzuzu aja anaphedwa ndi apolice chifukwa after ma demonstration anayamba kumakathyola ma shop a wanthu osalakwa.
😂😂😂😂😂😂
DPP woyeeeeeeeeee
Apa palibwino
Koma kuthamawu sibwino ngati mukufuna kuvota kavoteni osati kuti muthemawu achonchi mawa tizakugunsani
Yawawatu poti amzanu alankhula😂😂😂m'mene mumanyozela inu muja bwanji mwayiwala😂😂😂
Mtsogoleri akuyenela kukhala munthu oleza mtima. Osabwenzera choipa . Komano a Chakwela ngati mbusa ayi ndithu, zawabvuta ndipo sitimayembekezera kuti ulamuliro wao ungakhale oyipa moteremu. Chifukwa iyeyu amadziwa bwino lomwe za umoyo wa uzimu. Lero wasanduka wakupha . Anapha Sidick Miya komanso Saulosi Chilima ndi anthu ena omwe anali mu Ndege muja. Ifeyo tikudziwa zonsezo ndipo ma umboni alipo. Chakwela galu ameneyi , owona mizimu yonseyi singamusiye siye ayi imumzunza ndipo azunzika koopsya pansi pompano Chilango chake cha Mulungu asanachilandire galu ameneyi.
@@HamiltonwaNamuwahkoma awinabe.
@@VincentManyenje ndipo nkhan zaifa za anthu aja zisiyeni coz umbon mulibe kut anaphedwa nd munthu wina aiii... Mulungu ndamene akuziwa... ku Malawi vuto ndlimenero Kukonda kulenga nkhan
❤❤ochewa ozanga ozindikila Dpp oyeeeee 💥💥💯 ❤❤
Mbuz zimalakhur paja zja mpaka mun2 kumanyumwa nazo?... Evn kwao zngakope anthu😂😂😂😂😂
More 🔥🔥 adadi tikudikirani 2025 mwina moyo wungasitha 💃💃💃
Ichi ndi chathu ichi
Dpp,UTM,UDF,afford,,tagwilanani manja tichose amalawife Ku iguputu komwe tikumphula njerwa za moto
Munthu wakulu Brian Band mmmmm guys munthuyi akapangako kunali ntcito
Anthu awa akalamba asiyile achinyamata
Inenso ndi Mchewa koma palibe chomwe yapanga MCP. Panopa biziness ikukomera oremeretsetsa.
Wachikulire sakhala ndiphuma akukagona woyeee
Zizafika poti olo a pule azavotera APM....kkkkkk
Mwana wa pa Dowa kulankhula chilungamo
Dpp yomweyo
Vilombo vozindikila
DPP OUR LAST HOPE
Kkkkkkkk koma ochewa mukuithanulatu apa 😅😅😅
Brian wadzinvela wekha ndi a Malawi onse. Zinthu silibwino mu dziko.
Anaziwa adad kuti or achokepo ana awo sangamenyane
Powerful brothers
Tawina kaye...
Nayenso Chaponda wakalamba mpaka 81 kakaka
Achewa awa ayankhula zonveka kwambiri
Nganga bulawayo wakagona watopa, nkhalamba yachabechabe
Peter watopa koma tikanampumitsa 😢😢😢😢
Brian uwapusita achewa koma mchewa sangaone kuti akuwapusitsa kodi mafuso amenewa adawafusa choncho kufunsa anthu aku Tyolo
😂😂😂😂 kma Brian ukhalike
Onyamata odziwa kulankhula ndi ozitsata ❤❤❤
Eeeeee Koma Cathay ndi Brian kkkkkkk
APA ndiye.dzikundivekelabwino.Dpp.wooooyeeee
APM my vote ❤
Awa nde anthu ozindkira kwambri
❤
DPP THE ONLY TRUSTED PARTY WHOLE NYASALAND
Kungonva kuti chatuluka mdabwe changa😂😂😂😂
Km Brian 🤣🤣Aliunena zoona
APM WOYEE
Zikhale chani kodi usiku umenewu
Koma chichewa chaku Dowa nchokoma
❤❤
MWAYENDA BWANJI ? TAKWERA MAMINIBASI😁
Kkkkkkkkkkk
🤣🤣😞😞 mchona wapita kukagona
Labourers work more than professionals, biggy amagona ndi kudzuka nthawi yabwino
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Tumidala tovuta utu situkufuna kusiyira anyamata
Akut tawina kale 😂😂😂
Koma Brian anakonza
Woyeee
Dpp woyeeeee
Mbambande DPP❤❤❤❤❤❤❤❤❤
God bless Malawi
Ndipatse number ya Brian Banda guys please
Nice one 😂😂😂😂❤❤
Brian Banda umakwana 😂😂
Chatopa chapita
Jerous people never winnnnnn!!!!!!
DPP wooooyeeee
Kulamudi dziko sikuyakhula bwino English
Ndipo thaw mkachitsirud 😅😅
Yakwani thawi
APM❤❤❤❤❤❤❤❤❤
at fateleza
Dr chikangawa alibe mawu
Dr albino sangawine .
@@VincentManyenjeiwe pamtumbo pako Chakwera sangawine mistek yopha chilima ija zinalakwika pamene paja chomwe ungadziwe dziko lapasi limalamulilidwa ndi Roman catholic wekha malizitsa
@@Musa1828-l5d usavutike ndikutukwana koma ziwa kuti MCP ikupitilira ku lamura .sunga mawu anga.
@@Musa1828-l5d mpaka kumutukwana nzanu nkhan yake iti😂😂😂😂😂
INE NDAVOTA KALE DPP 2025 BOMA
Bola ngati sanagwe pa mpando
Olo atagwa mkufa koma muthu ozindikila sangavotere munthu opha mzake pamtumbo pakoso iweyo ndi chakwera wakoyo panyini pamanu nose
😂😂😂😂😂😂muuzen chilungamo ameneyu😂@@Musa1828-l5d
@@Musa1828-l5d inu abwino mpaka kumatukwana anzanu... Namkhumwa my Vote
Mmmmmm APM wathawa kuopa kugona
Nde asakagone chifukwaaaaa
MLC anachezeratu
Waiopeladi 😂😂😂😂 koma alibho
@@ibrahimjackson-cg6tc kkkkkkk pamenepo
@@CoshantAsante Ndiye kuchedzera kwa Chakwera kunapangitsa kuti sugar atsike mtengo??
Walira mwana wapedegu 😅
Koma Malawi tinapusa kwa basi
Bwanjinso nanga
DPP ndichipani chafiko, chosapha,
Ma albino ajaaa zinali zinyama? achinyamata azathu anawaombela Ku Mzuzu pa 20 july ajaaa ndi nyama??
@@macleanwazalanyirenda4994 Ma alubino ankhaphedwa Chakwera nanu ali ku opposition pofuna kuyipitsa mbiri ya APM anthu 20 aku Mzuzu aja anaphedwa ndi apolice chifukwa after ma demonstration anayamba kumakathyola ma shop a wanthu osalakwa.
😂😂😂😂😂😂
DPP woyeeeeeeeeee
Apa palibwino
Koma kuthamawu sibwino ngati mukufuna kuvota kavoteni osati kuti muthemawu achonchi mawa tizakugunsani
Yawawatu poti amzanu alankhula😂😂😂m'mene mumanyozela inu muja bwanji mwayiwala😂😂😂