ACHEWA AKU DOWA ASAMBWAZA EE!!🙌🙌

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 26 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 94

  • @HamiltonwaNamuwah
    @HamiltonwaNamuwah 2 หลายเดือนก่อน +9

    Mtsogoleri akuyenela kukhala munthu oleza mtima. Osabwenzera choipa . Komano a Chakwela ngati mbusa ayi ndithu, zawabvuta ndipo sitimayembekezera kuti ulamuliro wao ungakhale oyipa moteremu. Chifukwa iyeyu amadziwa bwino lomwe za umoyo wa uzimu. Lero wasanduka wakupha . Anapha Sidick Miya komanso Saulosi Chilima ndi anthu ena omwe anali mu Ndege muja. Ifeyo tikudziwa zonsezo ndipo ma umboni alipo. Chakwela galu ameneyi , owona mizimu yonseyi singamusiye siye ayi imumzunza ndipo azunzika koopsya pansi pompano Chilango chake cha Mulungu asanachilandire galu ameneyi.

    • @VincentManyenje
      @VincentManyenje 2 หลายเดือนก่อน

      @@HamiltonwaNamuwahkoma awinabe.

    • @CoshantAsante
      @CoshantAsante 2 หลายเดือนก่อน +1

      @@VincentManyenje ndipo nkhan zaifa za anthu aja zisiyeni coz umbon mulibe kut anaphedwa nd munthu wina aiii... Mulungu ndamene akuziwa... ku Malawi vuto ndlimenero Kukonda kulenga nkhan

  • @RachelNkhoma-vn2jo
    @RachelNkhoma-vn2jo 2 หลายเดือนก่อน +11

    ❤❤ochewa ozanga ozindikila Dpp oyeeeee 💥💥💯 ❤❤

    • @CoshantAsante
      @CoshantAsante 2 หลายเดือนก่อน

      Mbuz zimalakhur paja zja mpaka mun2 kumanyumwa nazo?... Evn kwao zngakope anthu😂😂😂😂😂

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 2 หลายเดือนก่อน +2

    More 🔥🔥 adadi tikudikirani 2025 mwina moyo wungasitha 💃💃💃

    • @GanizaniCmbewe
      @GanizaniCmbewe 2 หลายเดือนก่อน

      Ichi ndi chathu ichi

  • @LexKatandika
    @LexKatandika 2 หลายเดือนก่อน +1

    Dpp,UTM,UDF,afford,,tagwilanani manja tichose amalawife Ku iguputu komwe tikumphula njerwa za moto

  • @PeterJanga-wv9nz
    @PeterJanga-wv9nz 2 หลายเดือนก่อน +5

    Munthu wakulu Brian Band mmmmm guys munthuyi akapangako kunali ntcito

    • @MasterMwandira-d3k
      @MasterMwandira-d3k 2 หลายเดือนก่อน +1

      Anthu awa akalamba asiyile achinyamata

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 2 หลายเดือนก่อน +3

    Inenso ndi Mchewa koma palibe chomwe yapanga MCP. Panopa biziness ikukomera oremeretsetsa.

  • @StalloneButao
    @StalloneButao 2 หลายเดือนก่อน +4

    Wachikulire sakhala ndiphuma akukagona woyeee

  • @sirgiftedmagalasi22
    @sirgiftedmagalasi22 2 หลายเดือนก่อน +1

    Zizafika poti olo a pule azavotera APM....kkkkkk

  • @omarajibu860
    @omarajibu860 2 หลายเดือนก่อน +4

    Mwana wa pa Dowa kulankhula chilungamo

  • @ThumbikoNgulube
    @ThumbikoNgulube 2 หลายเดือนก่อน +1

    Dpp yomweyo

  • @JoshuaNyirongo
    @JoshuaNyirongo 2 หลายเดือนก่อน +1

    Vilombo vozindikila

  • @GumuleKandawala-g7k
    @GumuleKandawala-g7k 2 หลายเดือนก่อน +4

    DPP OUR LAST HOPE

  • @VincentBorrah
    @VincentBorrah 2 หลายเดือนก่อน

    Kkkkkkkk koma ochewa mukuithanulatu apa 😅😅😅

  • @MathewKalinkhu
    @MathewKalinkhu 2 หลายเดือนก่อน

    Brian wadzinvela wekha ndi a Malawi onse. Zinthu silibwino mu dziko.

  • @trickermussa472
    @trickermussa472 2 หลายเดือนก่อน +1

    Anaziwa adad kuti or achokepo ana awo sangamenyane

  • @WilliamkaipahKaipah
    @WilliamkaipahKaipah 2 หลายเดือนก่อน

    Powerful brothers

  • @VesterLuke
    @VesterLuke 2 หลายเดือนก่อน

    Tawina kaye...

  • @damianokachingwe3531
    @damianokachingwe3531 2 หลายเดือนก่อน

    Nayenso Chaponda wakalamba mpaka 81 kakaka

  • @MeliaMichael
    @MeliaMichael 2 หลายเดือนก่อน +1

    Achewa awa ayankhula zonveka kwambiri

  • @haroldmazombwe8081
    @haroldmazombwe8081 2 หลายเดือนก่อน

    Nganga bulawayo wakagona watopa, nkhalamba yachabechabe

  • @FrankMsiska-i9j
    @FrankMsiska-i9j 2 หลายเดือนก่อน

    Peter watopa koma tikanampumitsa 😢😢😢😢

  • @HendryChiwezo
    @HendryChiwezo 2 หลายเดือนก่อน

    Brian uwapusita achewa koma mchewa sangaone kuti akuwapusitsa kodi mafuso amenewa adawafusa choncho kufunsa anthu aku Tyolo

  • @DeniaKaunda
    @DeniaKaunda 2 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂 kma Brian ukhalike

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 2 หลายเดือนก่อน +2

    Onyamata odziwa kulankhula ndi ozitsata ❤❤❤

  • @FebbyPhiri-n7j
    @FebbyPhiri-n7j 2 หลายเดือนก่อน

    Eeeeee Koma Cathay ndi Brian kkkkkkk

  • @ChrisyMbewe
    @ChrisyMbewe 2 หลายเดือนก่อน +1

    APA ndiye.dzikundivekelabwino.Dpp.wooooyeeee

  • @JanetJamesMachila
    @JanetJamesMachila 2 หลายเดือนก่อน

    APM my vote ❤

  • @FrancisGama-qb7ze
    @FrancisGama-qb7ze 2 หลายเดือนก่อน +1

    Awa nde anthu ozindkira kwambri

  • @BillionChigwirionaires
    @BillionChigwirionaires 2 หลายเดือนก่อน +2

  • @JeffreyKalepa
    @JeffreyKalepa 2 หลายเดือนก่อน

    DPP THE ONLY TRUSTED PARTY WHOLE NYASALAND

  • @MeliaMichael
    @MeliaMichael 2 หลายเดือนก่อน

    Kungonva kuti chatuluka mdabwe changa😂😂😂😂

  • @KunyengaMoyo
    @KunyengaMoyo 2 หลายเดือนก่อน +1

    Km Brian 🤣🤣Aliunena zoona

  • @sallyphiri-qz7if
    @sallyphiri-qz7if หลายเดือนก่อน

    APM WOYEE

  • @PaulBexter-c4g
    @PaulBexter-c4g 2 หลายเดือนก่อน

    Zikhale chani kodi usiku umenewu

  • @FrankMsiska-i9j
    @FrankMsiska-i9j 2 หลายเดือนก่อน

    Koma chichewa chaku Dowa nchokoma

  • @GreyShadreck
    @GreyShadreck 2 หลายเดือนก่อน

    ❤❤

  • @AlfredMatthew-v4h
    @AlfredMatthew-v4h 2 หลายเดือนก่อน

    MWAYENDA BWANJI ? TAKWERA MAMINIBASI😁

  • @MACFARLANEMULENGA
    @MACFARLANEMULENGA 2 หลายเดือนก่อน +2

    🤣🤣😞😞 mchona wapita kukagona

    • @EvanceEdson-fz1vn
      @EvanceEdson-fz1vn 2 หลายเดือนก่อน

      Labourers work more than professionals, biggy amagona ndi kudzuka nthawi yabwino

  • @PiusFumulan
    @PiusFumulan 2 หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @mcdonaldchakwira3145
    @mcdonaldchakwira3145 2 หลายเดือนก่อน

    Tumidala tovuta utu situkufuna kusiyira anyamata

  • @benjulius6070
    @benjulius6070 2 หลายเดือนก่อน

    Akut tawina kale 😂😂😂

  • @TimaNyirongo-jt5vy
    @TimaNyirongo-jt5vy 2 หลายเดือนก่อน +2

    Koma Brian anakonza

  • @FoxmanPhiri
    @FoxmanPhiri 2 หลายเดือนก่อน

    Woyeee

  • @JoyceBanda-k8t
    @JoyceBanda-k8t 2 หลายเดือนก่อน +1

    Dpp woyeeeee

  • @RiteRoderick
    @RiteRoderick 2 หลายเดือนก่อน

    Mbambande DPP❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @AgnessMwafulirwa
    @AgnessMwafulirwa 2 หลายเดือนก่อน

    God bless Malawi

  • @kennethkaunda3636
    @kennethkaunda3636 2 หลายเดือนก่อน

    Ndipatse number ya Brian Banda guys please

  • @FatimaUmali-pc8sy
    @FatimaUmali-pc8sy 2 หลายเดือนก่อน

    Nice one 😂😂😂😂❤❤

  • @LeyvanSamuel-pe5tc
    @LeyvanSamuel-pe5tc 2 หลายเดือนก่อน

    Brian Banda umakwana 😂😂

  • @MACFARLANEMULENGA
    @MACFARLANEMULENGA 2 หลายเดือนก่อน

    Chatopa chapita

  • @RuthKaunda-tc5qd
    @RuthKaunda-tc5qd 2 หลายเดือนก่อน

    DPP wooooyeeee

  • @hourlyview4226
    @hourlyview4226 2 หลายเดือนก่อน

    Kulamudi dziko sikuyakhula bwino English

  • @SueWahna
    @SueWahna 2 หลายเดือนก่อน

    Ndipo thaw mkachitsirud 😅😅

  • @RiteRoderick
    @RiteRoderick 2 หลายเดือนก่อน

    APM❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @thomluckson4557
    @thomluckson4557 2 หลายเดือนก่อน

    at fateleza

  • @AgnessMatchado
    @AgnessMatchado 2 หลายเดือนก่อน

    Dr chikangawa alibe mawu

    • @VincentManyenje
      @VincentManyenje 2 หลายเดือนก่อน

      Dr albino sangawine .

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d 2 หลายเดือนก่อน

      @@VincentManyenjeiwe pamtumbo pako Chakwera sangawine mistek yopha chilima ija zinalakwika pamene paja chomwe ungadziwe dziko lapasi limalamulilidwa ndi Roman catholic wekha malizitsa

    • @VincentManyenje
      @VincentManyenje 2 หลายเดือนก่อน

      @@Musa1828-l5d usavutike ndikutukwana koma ziwa kuti MCP ikupitilira ku lamura .sunga mawu anga.

    • @CoshantAsante
      @CoshantAsante 2 หลายเดือนก่อน

      @@Musa1828-l5d mpaka kumutukwana nzanu nkhan yake iti😂😂😂😂😂

  • @HaliJana
    @HaliJana 2 หลายเดือนก่อน

    INE NDAVOTA KALE DPP 2025 BOMA

  • @MACFARLANEMULENGA
    @MACFARLANEMULENGA 2 หลายเดือนก่อน

    Bola ngati sanagwe pa mpando

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d 2 หลายเดือนก่อน

      Olo atagwa mkufa koma muthu ozindikila sangavotere munthu opha mzake pamtumbo pakoso iweyo ndi chakwera wakoyo panyini pamanu nose

    • @spargomw
      @spargomw 2 หลายเดือนก่อน

      😂😂😂😂😂😂muuzen chilungamo ameneyu😂​@@Musa1828-l5d

    • @CoshantAsante
      @CoshantAsante 2 หลายเดือนก่อน

      @@Musa1828-l5d inu abwino mpaka kumatukwana anzanu... Namkhumwa my Vote

  • @CoshantAsante
    @CoshantAsante 2 หลายเดือนก่อน +1

    Mmmmmm APM wathawa kuopa kugona

    • @ShamilahSaizi
      @ShamilahSaizi 2 หลายเดือนก่อน +1

      Nde asakagone chifukwaaaaa

    • @CoshantAsante
      @CoshantAsante 2 หลายเดือนก่อน

      MLC anachezeratu

    • @ibrahimjackson-cg6tc
      @ibrahimjackson-cg6tc 2 หลายเดือนก่อน

      Waiopeladi 😂😂😂😂 koma alibho

    • @CoshantAsante
      @CoshantAsante 2 หลายเดือนก่อน

      @@ibrahimjackson-cg6tc kkkkkkk pamenepo

    • @limbanitambala3939
      @limbanitambala3939 2 หลายเดือนก่อน

      @@CoshantAsante Ndiye kuchedzera kwa Chakwera kunapangitsa kuti sugar atsike mtengo??

  • @noelmunthali3516
    @noelmunthali3516 2 หลายเดือนก่อน

    Walira mwana wapedegu 😅

  • @MACDONADLITIA
    @MACDONADLITIA 2 หลายเดือนก่อน

    Koma Malawi tinapusa kwa basi

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 2 หลายเดือนก่อน +1

    DPP ndichipani chafiko, chosapha,

    • @macleanwazalanyirenda4994
      @macleanwazalanyirenda4994 2 หลายเดือนก่อน +1

      Ma albino ajaaa zinali zinyama? achinyamata azathu anawaombela Ku Mzuzu pa 20 july ajaaa ndi nyama??

    • @limbanitambala3939
      @limbanitambala3939 2 หลายเดือนก่อน

      @@macleanwazalanyirenda4994 Ma alubino ankhaphedwa Chakwera nanu ali ku opposition pofuna kuyipitsa mbiri ya APM anthu 20 aku Mzuzu aja anaphedwa ndi apolice chifukwa after ma demonstration anayamba kumakathyola ma shop a wanthu osalakwa.

  • @ellensambo6323
    @ellensambo6323 2 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂😂😂

  • @HopeMakoka
    @HopeMakoka 2 หลายเดือนก่อน

    DPP woyeeeeeeeeee

  • @DaveMukhova
    @DaveMukhova 2 หลายเดือนก่อน

    Apa palibwino

  • @SlindiryLoveness
    @SlindiryLoveness 2 หลายเดือนก่อน

    Koma kuthamawu sibwino ngati mukufuna kuvota kavoteni osati kuti muthemawu achonchi mawa tizakugunsani

    • @AlihIbrahim-s7v
      @AlihIbrahim-s7v 2 หลายเดือนก่อน

      Yawawatu poti amzanu alankhula😂😂😂m'mene mumanyozela inu muja bwanji mwayiwala😂😂😂