ขนาดวิดีโอ: 1280 X 720853 X 480640 X 360
แสดงแผงควบคุมโปรแกรมเล่น
เล่นอัตโนมัติ
เล่นใหม่
Zikuchitsa mantha omwarira kumankharabe ndimoyo eee koma ufiti wake ndiweniwen
Koma kuli njara, Pali nkhani yodabwitsa chomcho koma azimai kudya osasiya😄😄
Kkkkk
😂😂eti osasiya kudya?
koma mdalayo kubelekera chikwamwa atavala jekete?
Mutidziwitsa mmene zithere mwake,,Keep it up Balanco selemanol
Eish koma zoopsa inna lillah waina illah llah rajuun
Azimai siyani kaye kudya inu mudziyankhula bwanji ndi nthongo kukamwa 🤔🤔
Ndipo inu Aaaaa akuona ngati zotsangalatsa inu Azimayi opanda manyazi awa😭😭😭
😆
Gova masowatu Mozambique mulibwanji?
Rádio yakula iyi Mwchidule ndi Tv. koma pa nkhani ya chitikayi ndiyomvetsa chisoni kwambiri nkhani ya ufiti ndiyovuta kwambiri mulimonse mmene zinthu zingakhalire imakhala yovuta basi.
Lamentável. zovetsa chisoni ndizlodabwitso, ndiye chachitika ndi chani Gova pambuyo posamba manja
Mukatelo munankhimila mulungu akukana pemphelani adzuka ameneyo
Apemphele kwakuya ambuye ndiwokhulupilika ifa nina sizikuchokela kwa mulungu
Zabodza izi ahh,sanadzuke. Wakufa ngwakufa
Man GOVA timakukondani mumatithandiza kudziwa zochitika mmudzi mwathu
A Gova mukuyesetsa kwambili
Koma kunjaku kuli zinthu, Lyford Vasco
Bwana mukuyesetsa kufukula khan
Malawi akadangomuononga athu ayiwala mulungu
koma azimaiwo nde akusema mbamu zachabe
Ashley mustafa
Abel zulanga wamibawa alondoloze nkhani imeneyi
Kmtu kumalawi
Koma zikoli silikuenda bwino
Tikutsatila mwachidwi mutiuza momwe zithele
Komabe tikanamdziwa Kaye yesu zamasiku otsiriza ndithudi tikupereka anthu amoyo kumanda
Zovuta kwambiri mutiziwitsa mmene zithere mumatiimirira
😭😭😭zoopsa
Timakunyadilani A Gova
Zodabwitsa ndipo
What happened next
Zochititsa Martha
Ngankhale chinachake chisachitike koma Bola agogo akewo asamba mmanja iwowo akanangovomeleza ndikusamba mmanja osati mpaka mphuma thikiti zomwezo ayi, chifukwa zikuoneka kut ndizamasenga zimenezo mensa azimayi amadya nsima aja avomeleza ndiye iwowo akukana chani?? Nkumat akunama muthuyo sakutuluka thukuta mmmmm madalawo a pole mot hetii
Kuma kumachitika zinthu zoopsa mmmmm
Hummmm koma!
Wina anangolota zimenezo zamabodza
Following
😭😭😭😭😭😭😭😢
Mmm zoopsya
Denza ndi ziko lina
Zikusowekera kupemphera zedi
Tidziwitseni ndithu
tikuthokoza kuti mukubweletsa zithu poyera
Ndipo kwambiri
Mmm z00pya
Zinatha bwanji tiuzeni
Onse anawasambitsa manja koma mwanayo sanadzuke. Mwambo wa malilo unachitika
Aaaaaaaa zinthu zake zovuta
Kulimbikitsa umbuli mMalawi
Ndipo aise, anthu tulo too much
Mocambique uku
Ndipo zoona zenizeni.komano mkumozambique
Muito triste
Koma azimai inu khalani serious nanga kudya kwabwanji uku tadikilni kale mudyabe
DRiemo
Tidziwiseni zosatil
Mwambo wamalilo unachitika
😭😭😭😭😭
But 3 ladies busy eating, while they are interview
😀
Kkkk
Not good
Koma mutiphunzitseko chilankhulocho chifukwa 1 day ndizapezeka kuti ndili komweko nde ndisazakhale mlendo
Zikuchitsa mantha omwarira kumankharabe ndimoyo eee koma ufiti wake ndiweniwen
Koma kuli njara, Pali nkhani yodabwitsa chomcho koma azimai kudya osasiya😄😄
Kkkkk
😂😂eti osasiya kudya?
koma mdalayo kubelekera chikwamwa atavala jekete?
Mutidziwitsa mmene zithere mwake,,Keep it up Balanco selemanol
Eish koma zoopsa inna lillah waina illah llah rajuun
Azimai siyani kaye kudya inu mudziyankhula bwanji ndi nthongo kukamwa 🤔🤔
Ndipo inu Aaaaa akuona ngati zotsangalatsa inu Azimayi opanda manyazi awa😭😭😭
😆
Gova masowatu Mozambique mulibwanji?
Rádio yakula iyi Mwchidule ndi Tv. koma pa nkhani ya chitikayi ndiyomvetsa chisoni kwambiri nkhani ya ufiti ndiyovuta kwambiri mulimonse mmene zinthu zingakhalire imakhala yovuta basi.
Lamentável. zovetsa chisoni ndizlodabwitso, ndiye chachitika ndi chani Gova pambuyo posamba manja
Mukatelo munankhimila mulungu akukana pemphelani adzuka ameneyo
Apemphele kwakuya ambuye ndiwokhulupilika ifa nina sizikuchokela kwa mulungu
Zabodza izi ahh,sanadzuke. Wakufa ngwakufa
Man GOVA timakukondani mumatithandiza kudziwa zochitika mmudzi mwathu
A Gova mukuyesetsa kwambili
Koma kunjaku kuli zinthu, Lyford Vasco
Bwana mukuyesetsa kufukula khan
Malawi akadangomuononga athu ayiwala mulungu
koma azimaiwo nde akusema mbamu zachabe
Ashley mustafa
Abel zulanga wamibawa alondoloze nkhani imeneyi
Kmtu kumalawi
Koma zikoli silikuenda bwino
Tikutsatila mwachidwi mutiuza momwe zithele
Komabe tikanamdziwa Kaye yesu zamasiku otsiriza ndithudi tikupereka anthu amoyo kumanda
Zovuta kwambiri mutiziwitsa mmene zithere mumatiimirira
😭😭😭zoopsa
Timakunyadilani A Gova
Zodabwitsa ndipo
What happened next
Zochititsa Martha
Ngankhale chinachake chisachitike koma Bola agogo akewo asamba mmanja iwowo akanangovomeleza ndikusamba mmanja osati mpaka mphuma thikiti zomwezo ayi, chifukwa zikuoneka kut ndizamasenga zimenezo mensa azimayi amadya nsima aja avomeleza ndiye iwowo akukana chani?? Nkumat akunama muthuyo sakutuluka thukuta mmmmm madalawo a pole mot hetii
Kuma kumachitika zinthu zoopsa mmmmm
Hummmm koma!
Wina anangolota zimenezo zamabodza
Following
😭😭😭😭😭😭😭😢
Mmm zoopsya
Denza ndi ziko lina
Zikusowekera kupemphera zedi
Tidziwitseni ndithu
tikuthokoza kuti mukubweletsa zithu poyera
Ndipo kwambiri
Mmm z00pya
Zinatha bwanji tiuzeni
Onse anawasambitsa manja koma mwanayo sanadzuke. Mwambo wa malilo unachitika
Aaaaaaaa zinthu zake zovuta
Kulimbikitsa umbuli mMalawi
Ndipo aise, anthu tulo too much
Mocambique uku
Ndipo zoona zenizeni.komano mkumozambique
Muito triste
Koma azimai inu khalani serious nanga kudya kwabwanji uku tadikilni kale mudyabe
DRiemo
Tidziwiseni zosatil
Mwambo wamalilo unachitika
😭😭😭😭😭
But 3 ladies busy eating, while they are interview
😀
Kkkk
Not good
Koma mutiphunzitseko chilankhulocho chifukwa 1 day ndizapezeka kuti ndili komweko nde ndisazakhale mlendo