Aaaaaaa this is out of hand now ngati zinthu zikutere tsopano ndiye Kuti apolice kapena Kuti achitetedzo sakugwira ntchito yawo, Koma zikomo kwambiri Inu anyamata a balaco semanao mukugwira ntchito yotamandika
This is very bad izi ndi nkhani zopanda umboni kodi munthu wakufa amalakhula?apa mwapha anthu osalakwa kunali bwanji kuwatengera ku police kusiyana ndikuwapanga khaza ngati zimenezi,boma likuyenera kuchitapo kanthu
Am watching you from Lusaka Zambia 🇿🇲😢😢😢😢😢😢
Zinazi pena umazaona ngati ukulotatu....tisamatengere malamuro mmanja mwathu chonde government must wake up and shield her innocent souls.
Zoona.
Exactly
Zooona
Ambuye atithandize
Heee angonia é outro nível 😢😢
Keep up bansosamana👏👍
Nkhani yoziziritsa nkhongono. Zambirizi zikuchitika chifukwa cha mangawa,umbuli ndinso kaduka. Izi zipangitsa kuti anthu adzingophana ngati nkhuku chifukwa cha nkhani ngati zimenezi.
Very sad watching live from Kuwait
Koma zosayenda
Umbuli akapolo umphawi Majerouse
Sukulu ndiyofunika. Kupha anthu ngat nkhuku akapolo otembereredwa...
Boma linayenera kutengapo gawo sizoona amalawi umunthu tinausiya kuti Nkhani zogopeka plus maudani aaaaaa amalawi pliz tiyeni tikondane ndithu komaso pena zimaonesa umbuli nanga mene awaphamo chisithe chani mudzimo maliro asiya kumwalira ana awo a malemu mwapasa picture yotani nakakonda atamagidwa anthu amenewa aaaaa munthu kumumpha ngati galu
Balanço Semanal está melhorando cada vez muito mais obrigado pela informação. E muito triste.
Kodi ku Mozambique malamulo a ufiti amati bwanji ?
Proud of you barancol
A balaco mwasowatu bwanji mwasiya kutipasira nkhani?
🤔🤔Mozambique nkhani izi zikuchulukiratu
😭😭😭😭😭komatu sibwino abale tapempherani iiii
Mmmmmm tili mmatsiku otsiliza zedi😭
Chilungamo ndichakuti anthu aku Mozambique sagawa kamba ndi ankhadza nkhondo yinawalowa mmitima
Kkkk mpaka pamenepo?
Ndipo ndizoonadi
Anthuwo akanadikira ndipo choonadi chilamaululika ... ndiye iwowo apha ndiye wakufa winayo apezeka bwanji
Za ufiti ziripo koma sibwino kutengela malamulo manja mwako boma lirowelerepo zikomo Agova
Umbuli wachuluka...Mukatero muyambe kumenyana,nkhondo sinakukwaneni eti?
Pitilizani kumatipatsa actualizações ❤
Zosayenda ayi anakangowamenya mkuwasiya mwina osati kumphelatu ayi mwina akanasiya ufitiwo
Apolisi sakugwila ntchito yawo anthu apha anthuwa aphedwenso
Afela zawo amenewo kumoto Basi
Ndikuti uku mwati
Oooo pepani kwambili
This is completely out of ignorance , civic education is greatly needed in these areas . Innocent souls are being killed.
Anakumana ndi zukwa
Sopano ngat mukut ufit kulibe mfiti zina zimafika poulura kunena zokha kut zimatamba ndikupha anthu muufiti..zimakhala kut ndichan
Aaaaaaa this is out of hand now ngati zinthu zikutere tsopano ndiye Kuti apolice kapena Kuti achitetedzo sakugwira ntchito yawo, Koma zikomo kwambiri Inu anyamata a balaco semanao mukugwira ntchito yotamandika
Inyo dine kalekale Kodi zimenezi zimakhala zoonadi timazionadi pa balaso semenalo
Koma kumeneko mkuti
Mmmmm koma abare inu sambi
Nsanje and kaduka
Mumakwana
Komano afiti awonjeza serious anthu amafika potopa abale osati anthuwa olakwa chifukwa even ukapita ku police uva zilibe umboni ndiye anthu atani kutopa ngati amfumu akuyankhula chocho afiti polani moto chifukwa anthu atopa
enanu mukut zalakwika km muzazindikila ufitiwo mukazakumana nawo.....ufiti ulipo guys wake up.......ine ndalhulupilira nkhaniyi...
Please pitiliza ni kutipasila
Apolsi akulephera ntchito yawo
School anthu awa ikufunika kwambili
😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Danger in the Last days
Koma simukufunikira mudziranga anzanu choncho
Zovetsa chisoni kwambiri 🥲
This area is too much primitive ,these people they must go to school they are still living old fashion ways they believe in witchcraft
Komatu ndikanakonda ndikadakhala mudzi umenewu
This is very bad izi ndi nkhani zopanda umboni kodi munthu wakufa amalakhula?apa mwapha anthu osalakwa kunali bwanji kuwatengera ku police kusiyana ndikuwapanga khaza ngati zimenezi,boma likuyenera kuchitapo kanthu
Eeeee abale ndi chian kwenikwen...tili mmasiku omaliza
a police sanathandize sanapeleke mau oteteza banjali
Boma lichitepo kanthu anthu tikutha ,
This is very bad
Mmmmmmmm mavuto aakulu zedi zikomo balaçio
,,,,