BAMBO NDI MWANA APHEDWA NDI ANTHU POWAGINIZILA KUTI NDI FITI By gova

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 25 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 60

  • @EmmanuelZiba-qz6ug
    @EmmanuelZiba-qz6ug หลายเดือนก่อน +1

    Am watching you from Lusaka Zambia 🇿🇲😢😢😢😢😢😢

  • @Mpungwe123
    @Mpungwe123 2 ปีที่แล้ว +8

    Zinazi pena umazaona ngati ukulotatu....tisamatengere malamuro mmanja mwathu chonde government must wake up and shield her innocent souls.

  • @RuthMvula-kq2dd
    @RuthMvula-kq2dd ปีที่แล้ว +2

    Ambuye atithandize

  • @TiagoManuelBanhaBanha
    @TiagoManuelBanhaBanha 3 หลายเดือนก่อน +1

    Heee angonia é outro nível 😢😢

  • @osamabinraden9391
    @osamabinraden9391 2 ปีที่แล้ว +1

    Keep up bansosamana👏👍

  • @joegibsonzulu2599
    @joegibsonzulu2599 2 ปีที่แล้ว +5

    Nkhani yoziziritsa nkhongono. Zambirizi zikuchitika chifukwa cha mangawa,umbuli ndinso kaduka. Izi zipangitsa kuti anthu adzingophana ngati nkhuku chifukwa cha nkhani ngati zimenezi.

  • @josuahkachali1489
    @josuahkachali1489 2 ปีที่แล้ว +2

    Very sad watching live from Kuwait

  • @EdwardGeorgeKasabola
    @EdwardGeorgeKasabola หลายเดือนก่อน +1

    Koma zosayenda

  • @cynthiakananji1608
    @cynthiakananji1608 ปีที่แล้ว

    Umbuli akapolo umphawi Majerouse
    Sukulu ndiyofunika. Kupha anthu ngat nkhuku akapolo otembereredwa...

  • @rabeccagama4067
    @rabeccagama4067 ปีที่แล้ว +1

    Boma linayenera kutengapo gawo sizoona amalawi umunthu tinausiya kuti Nkhani zogopeka plus maudani aaaaaa amalawi pliz tiyeni tikondane ndithu komaso pena zimaonesa umbuli nanga mene awaphamo chisithe chani mudzimo maliro asiya kumwalira ana awo a malemu mwapasa picture yotani nakakonda atamagidwa anthu amenewa aaaaa munthu kumumpha ngati galu

  • @sergiopauloposse7610
    @sergiopauloposse7610 2 ปีที่แล้ว +1

    Balanço Semanal está melhorando cada vez muito mais obrigado pela informação. E muito triste.

  • @lazarusziyaya3997
    @lazarusziyaya3997 ปีที่แล้ว +1

    Kodi ku Mozambique malamulo a ufiti amati bwanji ?

  • @austinvincent773
    @austinvincent773 2 ปีที่แล้ว +2

    Proud of you barancol

  • @jazakalemani3127
    @jazakalemani3127 ปีที่แล้ว +1

    A balaco mwasowatu bwanji mwasiya kutipasira nkhani?

  • @aleksawilliams710
    @aleksawilliams710 2 ปีที่แล้ว +1

    🤔🤔Mozambique nkhani izi zikuchulukiratu

  • @jvpondan4332
    @jvpondan4332 2 ปีที่แล้ว +3

    😭😭😭😭😭komatu sibwino abale tapempherani iiii

  • @mavuschitseko7757
    @mavuschitseko7757 2 ปีที่แล้ว +3

    Mmmmmm tili mmatsiku otsiliza zedi😭

  • @halimahussein6571
    @halimahussein6571 2 ปีที่แล้ว +1

    Chilungamo ndichakuti anthu aku Mozambique sagawa kamba ndi ankhadza nkhondo yinawalowa mmitima

  • @promise3693
    @promise3693 2 ปีที่แล้ว +1

    Anthuwo akanadikira ndipo choonadi chilamaululika ... ndiye iwowo apha ndiye wakufa winayo apezeka bwanji

  • @pililanibuliyani7684
    @pililanibuliyani7684 2 ปีที่แล้ว +1

    Za ufiti ziripo koma sibwino kutengela malamulo manja mwako boma lirowelerepo zikomo Agova

  • @louiskk100
    @louiskk100 2 ปีที่แล้ว +2

    Umbuli wachuluka...Mukatero muyambe kumenyana,nkhondo sinakukwaneni eti?

  • @majendauzananilimitedi2049
    @majendauzananilimitedi2049 ปีที่แล้ว

    Pitilizani kumatipatsa actualizações ❤

  • @lucysimbani3971
    @lucysimbani3971 2 ปีที่แล้ว +1

    Zosayenda ayi anakangowamenya mkuwasiya mwina osati kumphelatu ayi mwina akanasiya ufitiwo

  • @ririvilla1423
    @ririvilla1423 2 ปีที่แล้ว +2

    Apolisi sakugwila ntchito yawo anthu apha anthuwa aphedwenso

  • @martaarauio1347
    @martaarauio1347 2 ปีที่แล้ว +2

    Afela zawo amenewo kumoto Basi

  • @promixphotography8056
    @promixphotography8056 ปีที่แล้ว

    Ndikuti uku mwati

  • @MarcelinoManquena-ws8nd
    @MarcelinoManquena-ws8nd ปีที่แล้ว +1

    Oooo pepani kwambili

  • @ancientnkhata1137
    @ancientnkhata1137 2 ปีที่แล้ว +3

    This is completely out of ignorance , civic education is greatly needed in these areas . Innocent souls are being killed.

  • @ClementWanja-f4k
    @ClementWanja-f4k ปีที่แล้ว

    Anakumana ndi zukwa

  • @chifunirogoliat4630
    @chifunirogoliat4630 ปีที่แล้ว

    Sopano ngat mukut ufit kulibe mfiti zina zimafika poulura kunena zokha kut zimatamba ndikupha anthu muufiti..zimakhala kut ndichan

  • @frankmaluwa5120
    @frankmaluwa5120 2 ปีที่แล้ว +1

    Aaaaaaa this is out of hand now ngati zinthu zikutere tsopano ndiye Kuti apolice kapena Kuti achitetedzo sakugwira ntchito yawo, Koma zikomo kwambiri Inu anyamata a balaco semanao mukugwira ntchito yotamandika

    • @MarcelinoManquena-ws8nd
      @MarcelinoManquena-ws8nd ปีที่แล้ว

      Inyo dine kalekale Kodi zimenezi zimakhala zoonadi timazionadi pa balaso semenalo

  • @fatimahluis6450
    @fatimahluis6450 ปีที่แล้ว +1

    Koma kumeneko mkuti

  • @aliciabanda3656
    @aliciabanda3656 2 ปีที่แล้ว +1

    Mmmmm koma abare inu sambi

  • @ancientnkhata1137
    @ancientnkhata1137 2 ปีที่แล้ว +2

    Nsanje and kaduka

  • @HarryUmarih
    @HarryUmarih ปีที่แล้ว +1

    Mumakwana

  • @ibrahimalfred6539
    @ibrahimalfred6539 2 ปีที่แล้ว +1

    Komano afiti awonjeza serious anthu amafika potopa abale osati anthuwa olakwa chifukwa even ukapita ku police uva zilibe umboni ndiye anthu atani kutopa ngati amfumu akuyankhula chocho afiti polani moto chifukwa anthu atopa

  • @iangama35
    @iangama35 2 ปีที่แล้ว +1

    enanu mukut zalakwika km muzazindikila ufitiwo mukazakumana nawo.....ufiti ulipo guys wake up.......ine ndalhulupilira nkhaniyi...

  • @JosephBanda-fl5ss
    @JosephBanda-fl5ss ปีที่แล้ว +1

    Please pitiliza ni kutipasila

  • @sulaimanabanda9605
    @sulaimanabanda9605 ปีที่แล้ว +1

    Apolsi akulephera ntchito yawo

  • @peterbanda7003
    @peterbanda7003 2 ปีที่แล้ว +2

    School anthu awa ikufunika kwambili

  • @MrnjiwaNjiwa
    @MrnjiwaNjiwa 9 หลายเดือนก่อน +1

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @lydiaamos4214
    @lydiaamos4214 2 ปีที่แล้ว +1

    Danger in the Last days

  • @jvpondan4332
    @jvpondan4332 2 ปีที่แล้ว +1

    Koma simukufunikira mudziranga anzanu choncho

  • @bonifaciosimao8620
    @bonifaciosimao8620 2 ปีที่แล้ว +1

    Zovetsa chisoni kwambiri 🥲

  • @marianyirenda
    @marianyirenda ปีที่แล้ว +1

    This area is too much primitive ,these people they must go to school they are still living old fashion ways they believe in witchcraft

  • @jvpondan4332
    @jvpondan4332 2 ปีที่แล้ว +1

    Komatu ndikanakonda ndikadakhala mudzi umenewu

  • @victorbanda7546
    @victorbanda7546 2 ปีที่แล้ว +1

    This is very bad izi ndi nkhani zopanda umboni kodi munthu wakufa amalakhula?apa mwapha anthu osalakwa kunali bwanji kuwatengera ku police kusiyana ndikuwapanga khaza ngati zimenezi,boma likuyenera kuchitapo kanthu

  • @mariamhalid9185
    @mariamhalid9185 2 ปีที่แล้ว +1

    Eeeee abale ndi chian kwenikwen...tili mmasiku omaliza

  • @miloslundu6366
    @miloslundu6366 2 ปีที่แล้ว +1

    a police sanathandize sanapeleke mau oteteza banjali

  • @zainabchikakuda6297
    @zainabchikakuda6297 2 ปีที่แล้ว +1

    Boma lichitepo kanthu anthu tikutha ,

  • @dakasaul3111
    @dakasaul3111 ปีที่แล้ว +1

    Mmmmmmmm mavuto aakulu zedi zikomo balaçio

  • @armandojohn7641
    @armandojohn7641 2 ปีที่แล้ว +1

    ,,,,