Amachita Bwino ryiton chifukwa akalowera kwachabe amabwerela mwachangu amadziwa Kuti amalawi amasiku ano anasukusula ..u are Wellcome Mr Mangochi.. Koma abilimankhwe awiri longwe NDI Munro.. ndalama Za magazi zi zikawathera asazabwere apa NDI manyaka siizaveka
Choka iwe wasowa zonena palibe wabwino kulibe ena amene angalamulile malawi? Kupusa Peter ndindaninso Peter,,And chakwela zao ndizimodzi Bola kusakha ena osati amenewa Zitchito zawo tauwona Ndiwe opusa ukulakhulawe
Komw iyiyi ndimbuzi yamunthu wawona kuti anzako anakuwukira aku mangochi galu iwe wayamba kusintha pitawuko satana wamunthu iwe koma ukunama chitsilu iwe
A Lyton Mangochi mwayankhula za nzeru kwambiri, Chakwera amangodziwa ma ves basi, mu mutu wake muli mamina wokha wokha. APM abwerere basi.
😊😊😅😊😊
Ma ARV a muzunguxa mutu uyu
A lyton pano ndi the DC Akugwila mtchito limoz
Pitan bas ku the peoples first baba mukalowe gulu
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤you right sir iwe Ng,alula
Mr Mangochi amayankhula chilungamo koma samaziwika kuti ali mbali iti ndi mbewa kapena Mleme 😂😂😂😂
Peter ndiyeso ayi malawi apite kwa axhinyamata
Malawi muli anthu nzeru tiyesepo ena achinyamata
Exactly man mutambo ananena kale kuti mcp ndi mfiti
، achoke achoke Chakwera achoke
Apapatu Mr Lyton Mangochi mwakwanisa Ulemu wanu apadi mwaima pachilungamo ulemu wanu
Amachita Bwino ryiton chifukwa akalowera kwachabe amabwerela mwachangu amadziwa Kuti amalawi amasiku ano anasukusula ..u are Wellcome Mr Mangochi.. Koma abilimankhwe awiri longwe NDI Munro.. ndalama Za magazi zi zikawathera asazabwere apa NDI manyaka siizaveka
Pa convention ya MCPigs
1) ma delegates 60 anakhapana.
2) ma delegates awiri anapezeka atafa ku room.
☝️Ndiye muziti "kwacha, kwacha" zakalekale.
Zosakhala bwino 😢
Bola zikhale zochokera pansi pamtima zomwe ukuyankhurazo
A very distinguished President, a few among many. Within four years Malawi has changed.
@ ur home yes not malawians
Mwayakhula zazeru bro
Mwabwela inuyo ❤❤❤❤mangochi
Achoke basi apm my vote
Aaaaaah wapengatu uyu
Lytton mangochi tiuzeni mbale imene muli 😂😂😂😂😂😂😂
Bola ukunena chilungamo
Pano tayambaso kukonda
Mcp ituluke M'boma basi
Choka iwe wasowa zonena palibe wabwino kulibe ena amene angalamulile malawi? Kupusa
Peter ndindaninso Peter,,And chakwela zao ndizimodzi
Bola kusakha ena osati amenewa
Zitchito zawo tauwona
Ndiwe opusa ukulakhulawe
😂 Vuto la uyu sachedwa kutembenuka😂😂😂😂 lyton ndimbuziso😅😅
Awa sanawalipire
Ndipo uyu vuto lake kusawuka kwambiri panopa akufuna Dpp koma chilugamo kuti Dpp ndiyomwe iliyabwino
Apa laitoni mangochi tagwilizana apa basi
Ndalama zatha zomwe anampasa
@@victorauwana7258 🤣🤣akatero akufunaso zina
Mutu sumayenda lyrtone
Mwapenga inu Malume
Chakwera ndi mbunzi kwabasi
Nanu bible lomwe amalidziwa chakwela ndiliti ?
Lausatana lomwelo , mumakweza nkhano muntengobwanji
Nthawi ija unatiuza kt mcp ikupanga chitukuko 😂😂😂😂😂 Chitumbuwa chamuthela sopano komabe ndazikonda wanena bho
Chakwela satana mbuzi sakuzi hata chimozi
Komw iyiyi ndimbuzi yamunthu wawona kuti anzako anakuwukira aku mangochi galu iwe wayamba kusintha pitawuko satana wamunthu iwe koma ukunama chitsilu iwe
Bola ngat sanatumidwe
Koma mkationese komwe mkuti Ali chilimako kuchikangawa tiziweko tikamuone
Banzi likakhala chimtuwitsa fanta amachepa. Koma fanta akachuluka banzi limachepa. Likachepa umayamba kunena zoona zokhazokha.
Zatha anampatsa zija?
@@Ahlubyt 🤣🤣😂
Kkkkkkk. khala ngat
Chamisala ichi😂😂
@@FosterChakanga 🤣🤣🤣
😂😂😂😂😂😂😂😂 Ulemu wanu
@@imraanJafal 😂😂🤣✌️🔥thanks
Zopusa chitsilu iweyo