DC kuno ku Kasungu tiyankhulireni , akufuna kupeleka ngongole koma chodabwitsa akufuna ma lD ,ndiye kuno anthu akupeleka ma ID maka ife ma MUSLIM, chonde bwana DC tiyankhuleni
@@WorriedNdhlovu akuluwa a kupanga target mcp bac chifukwa adakanikanika kupita Ku embassy mpaka kum@ngonyoza awa nde Kaya ingonenani kuti mufuna dpp osati kumazembera
Ndikadakonda bon kalindo utakhala president kwinako Malawi angasithe coz umphawi mumaudziwa bwana🎉🎉🎉
amaoneka olungama akakhala kunja
Kkkkk ndale pa Malawi
@@kishasbeatsproduction4944mumwa chan bwana pa bill yanga
Mumakwanira boss man ipasen moto🔥🔥🔥🔥
The DC, President wa a Malawi osawuka, Malawi First go deeper
Osaopa osafooka comrade tanyiwa ,karindo again via bakili muluzi tv
munthuyu mutu sugwira ndavetsetsa coz munthuyu akupanga target ma lndividuals😮😮😮
More 🔥 the Deeeeeceeee mwana oophya kwambiri 💪
my brother man for others woman u are number one
Ulemu wanu Mr DC timakunyadilani kwambili❤❤❤
He is making total sense.
Aluza ku convention atiphweteka awa.
Medison usi malawi akudataula kuti
Palibe amene akusapota
Akuipa bwino bwanji fanayu akutulusa
The dc mwana owophya kwambiliiiii❤❤❤❤❤❤
Tamangooyikani Audio straight basi. Osatinso kummaiyankhulira kaye, voice yanuyo ikumapweteka mkutu.
Ya zoonadi ine imandinyasa
We need to have 10 people in Malawi like Born kalindo
Mau koma awawa olo alipo five
Mmmmm wankali samadzing'amba yekha tsiku lidzakwana akalindo
Iwetu iwe unya ndi chakwera wakoyo
Pita ukakumane naye nde uzatiuze zomwe ukazione
Pamtumbo pako ndi Chakwera wakoyo munapha chilima inu fiti simuwina agulu onukha kuthako
Iweyo koma ndiye uny'a nayo
Chaka chake sichino
Ukanakhara wazelu ukanakhala chete ,😡mwadzi...
I like you so much Mr president watu
Aaaaaah inu zachapani zigwirizana bwanji ndi za dziko ndindani angalimbane ndi munthu openga
Koma ine nkhani ya njuchiyo mwinatu nduna zinazi sizikudziwa akusewelatu amenewa😊😊😊
The Dc...... Mwana wA line katola
Apambaze amenewo 🤣🤣🤣🤣🤣🙆🙆🙆🙌🏽🙌🏽🙌🏽💥💥💥💥💥
Awa koma apange resin chifukwa chachani mmmmm tapanga zako Bon
Pamtumbo pako galu ndi chakwera wakoyo munapha Chilima simuwina anthu onukha kuthako inu
Awa kwao kwatha let's see, time is coming amalawi atopa.
Sazanthekadi mmmmm katundu waboma kkkk🎉🎉😊
Ndipo ayidya momvutadi ameneyoooooo😊
Mwana wa line katole😊😊😊😊😊
The DC bon kalindo akunama iyeyo mr chikangawa aziwa chaka chino
Uyu ndi big man the DC chakwera chakwera ndimwana
the DC ❤akamuna muna
The DC mwana owoopsa kwambiri... Umakawana aise. Afiti a MCP sakupuma nawe bwino
Uyu eee ndi akatundu omanga ndi mawaya👐👐👐
The DC mwana ophya kwambili❤
akufunika uwaphe mkhwala kkkkk
Koma Born kalindo ndakakutundu 😂😂😂😂
GOD BE WITH YOU BON KALINDO
Love you Bon kalindo we silute you forever❤
Boni kalindo DC ukumuyiliradi Mmalawi osauka, pitilinzani kuwaunikira azipani zomwe zikufuna kupanga mgwilinzano 2025, kmso kumuunikira munthu wa kumudzi chifukwa munthu wa kumudzi amangovota moti zingomuchoka mosaonetsetsayi mosaonetsetsa
Km ichi amwene
DC kuno ku Kasungu tiyankhulireni , akufuna kupeleka ngongole koma chodabwitsa akufuna ma lD ,ndiye kuno anthu akupeleka ma ID maka ife ma MUSLIM, chonde bwana DC tiyankhuleni
Aaaa zaziii, ofuna kuzipha salengeza, panga zomwe umatha tiwone
Tiyeni nawo bon kalindo aña achepa ngt àli madolo tikakumane chikagawa
UTM koma musitisilizaaa koma mulumgu alowerelepooo
Mfana wammudzi sopano eeeee❤
ndimakunyadira bon karindo uremu wanu
The D.C umakwana and proud of you
The DC mumatiimilila asiyeni agaruwo chao palibe
Ndiwe Bon Mwana Owoopsya kwambiri muziko lonse la Malawi
No to Nyawu party
Waufiti samazitamandila....awa ndi mantha chabe
Mmm!! Zoonadi, ngathi munthu walephela, obviously it shows that, kwa yiye mphamvu Mulungu wazilanda.
Chilipo chikukusata Bon Kalindo
Simungamuthe Kalindo munama kwambri, munapha Chilima anthu oipa inu simuwina 2025 kumtumbo kwamako galu iwe
Koma kutchuka unakufunisisa 😂😂unayiwelenga boh uli kuti nditchuke ndizingotukwana MCP 😂😂ndiwe dolo
Wamisala anaona nkhondo
Ulemu wanu the DC timakunyadilanitu pachilungamo osaopa osafooka osatopa
Bon kalindo ndi mbuzi kwambiri. Every day kumankamba dzautsiru basi.
Kalindo my guy,thana nawi agalu amenewa athe onse ena atengerepo phunziro achule achabechabe
this is true i know this man
DC amatiyimirira ....ulemu wako....
No rest for the wicked,DC kachilungamo kalilmo
Ndipo anthu amenewa akuiputa nkhondo kwambiri
The DC ❤
A Kalindo langizani chipani chanu chikupita ku komvesyoni pa 18 August nanga munthu umalangiza zinthu zitachitika kale
The DC mnyamata oopya kwambiri, mufatu mkalimbana naye
Tamvanao 😮😮😮😮😮
Ichidi ndichamisaradiiii!!!!!! Wangokura mutu koma zelu aribe
Kkkk wanyama zing'onozing'ono wagwa mu mtengo wamkuyu
Ba Bon K nanga mbaa mwakanika bwanji kumuchosapo chakwex yu
Ba Bon K nanga mbaa mwakanika bwanji kumuchosapo chakwex yu galu oluma samakuwatu
aboni kqlindo akuoneka kuti zokamba zawathela
Kod apopo sanakambe or akunveka ngati akuimba nyimbo
@@WorriedNdhlovu akuluwa a kupanga target mcp bac chifukwa adakanikanika kupita Ku embassy mpaka kum@ngonyoza awa nde Kaya ingonenani kuti mufuna dpp osati kumazembera
@@WorriedNdhlovu😂😂😂anthu kufika potopa😂
We support you Kalindo
Kom A mcp musamale chifukwa tonsefetu ndife okwiya kwambri chakwela mbuzi yamunthu
Malawi kung'amba kkkkkk koma DC kkk
Munthu waufiti samazitama a bon iwe ndiwe saiz yanga osat ungalimbane ndi ziko
DC alozeni bas
The DC bon kalindo more fire 🔥🔥🔥🔥
Akhalitse Dc
the dc mwana oophya kwambili
Ati nkatikati mwanyamamo muli nchenga hehehe!!!😂
I think akalindo mukamayankhula izizi mumakhala kut mukupanga mantha n ndiwe munthu wamatha. Coz munthu amene saopa kathu sayankhula koma munthu amene akungokuwa amakhala kut akuopa, n inuyo akalindo ndiinu munthu wamatha that's it.
Amawopa kumangidwa 😂😂 chifukwa ndi anthu akuba
Mwana wa mulanje weniweni
DC salute kwanu
Koma dc atakhala kuti kumalawi alipo athu 20 ayi futi kumalawi zitalila kale chifukwa ndimuthu wolimba mtima kwambili
The DCCCCCCCCCCCCCCCCCCCCCC Mwana oopsa kwambiriiii!!!!
Mcp manyadzi bwa
Dziko ndi lathu tiziwopa ndani?
Mavoti simayesu tisakole amalawi Kuti tipange mavoti woyesera zayamba liti zimenezi asatipusise
Chisankho I chichi mulungu azakhle pa tsogolo
Ngati amangova mulanje mulanje ayiziwira pa the DC
Inu ndakatundu big
💪💪 Viva DC
Daily kunyodza MCP chakuntha ichi
Tangomuloza chikangawa man yo
Amwene inu ku MCP kulibe kugawikana iweyo uchedwa nazo
Ndinu agalu nokha nokha ndi anyani azakowo
Malume, pangani zanu, alekeni a mcp apange zawo...
Simukuvutika inu 😢
Chikangawa party
Koma nkhani umaziziwa bwanji 😂
My question too
Coz zimakhala zoonansotu nkhan zake😂
Ndy iiihm kaya tsono😂
Koma DC kuyankha mopanda mantha zoona 😅
Awa ndiye opusa kwambiri azawo zikuwayendela koma iwo😢😢😢
The voice of DC
Chimene amafuna kalindo sachidziwa oipa ndamene amabweletsa chisokonezo mdziko
Mwana wa line katole😂😂😂😂
Hiiiii chakwela ali male