Another God sender is this guy, ❤Mulungu atimenyera nkhondo tili chete ngati m'mene anachitira Israel. May the almighty God bless and protect you our brother clif chinyama
this thing when you come to a point where you realize you have nothing to lose all the fears go you starting behaving this way, we have alot of them benefiting from these guys hence their voice is taken shame, awawa amadya zawo thats kulimba mtimaku.
May God proetect u where u r broh always mdima umadana mkuunika koma mawa tisamve kuti china chake chachitika kwamchimwen uyu anthu ongoganiza zokupha inu malo motukula dziko mzaziiiiiiii
Kuphatikiza apo malawi siyaku Lilongwe kokha ayi, koma achakwera mwalivula dziko ngati nzimayi oyendayenda kapena kuti hule, malawi Ali PA map a manyazi chifukwa cha ubusa wanu otsogolera amalawi ku mimbulu osati ku nkhosa, malawi ayaluka mochitsa manyazi chifukwa cha a Busa inu and tikuwona Zambiri zowopsa zoti chibadwile sitinaziwone, anthu mpaka kudya chitedze koma olo kulankhula kapena kutenga po gawo ngati kholo, tate wa dziko ayi ndithu abusa???? 😢😢😢😢 Mwachitsa manyazi dzina la ubusa malawi Ali pamoto uyu and dziwani kuti anthu sakukufunani 2025 ndipo mukadakhala Ena kunali kongoimika manja kuti zakuvutani Bola....🤔🤔🤔🤔
Pakhale corabo ya the DC ntanyiwa bakili muluzi tv alexious kamangila and this guy. 🔥🔥🔥🔥
Hahaha koma ndipoooo
@@JulietLizziePhiri zafikapa malawi yufunika anthu olimba mtima ngat amenewawa
Strong words and takunyadilani mr.Chinyama, a MCP akutitola kwambiri ndi achina Chimwendo Banda.
Brave and bigup. I like his courageous!!! Let's work up guys & support these our fellow youths like the likes of Kamangira and others
Woke up achinyamata andale atiwonjeza tsopano zafikapa lets fight for our freedom ( Alunta continua 💪)
you do say wake up in your hiding hahahaha no bho
100% truth, anyamata a MCP ndi opusa kwambiri
Bravo CLIF CHINYAMA
long live u r more hero
😅😅😅😅 Brada well done, please tell them the liyaliya more 🔥🔥🔥 a chikangawa party aonjeza
Another God sender is this guy, ❤Mulungu atimenyera nkhondo tili chete ngati m'mene anachitira Israel. May the almighty God bless and protect you our brother clif chinyama
Let's support him guys this is enough
I think a chinyamata Les make new group to crean our Malawi
Mcp simbali yanga kuyambira kale kale,
Kkkkk ndimamva chisoni ndi apolice,akungomanga anthu kulephera kumanga nyumba zawo
Cliff chinyama real man❤
Zoonadi Brother Clif Chinyama, Chakwera ndi chitsiru cha chabe-chabe
this thing when you come to a point where you realize you have nothing to lose
all the fears go you starting behaving this way, we have alot of them benefiting from these guys hence their voice is taken
shame, awawa amadya zawo thats kulimba mtimaku.
Come clif my allah guide and protect you all the time allah akbar respect to big up my bro be strong
Ndipo ine singachose chikhulupilo PA anthu Inu, Clif, Ntanyiwa, Bon, bro sallo ndi Ena onse Bakili TV, tilipambuyo panu
Kd mukuti ndichani mukufuna chani mupha anthu angati inuyo mudzapita kt kd inuyo mukuopseza anthu cz mwachuluka phavu guys zimenezo ayi ingotengani mifuti mutiphe tonse mwava chipani chanji chokhara ndi zigawenga ala Inu zimenezo ayi kd inuyo simuzafa moti simudziwa kt kupha munthu ndichimo kd Inu boma muli nduna zingati kumangoti chimwendo kukuyu osadabwa ng,oma olola kwambiri sichedwa ku sweka musamare Mcp mwava
Mitunda yosaopa, thanks bro
Zoona big mumwa chani brother mwayakhula bwino kobas
May God proetect u where u r broh always mdima umadana mkuunika koma mawa tisamve kuti china chake chachitika kwamchimwen uyu anthu ongoganiza zokupha inu malo motukula dziko mzaziiiiiiii
Powerful brother Man ❤❤❤
Akamangila akutulukatu, wina amva 'bebe.
More fire brooh
koma m c p mwaonjeza kwambiri kod afiti ose adatha kumarawi kuno. bwanji osangorodza amenewa kuti tipumure lfe
Malawi need courageous young men like you,bravo
Guys kumalawi kuli anthu olimba ntima ndaimikamanja. Mr kumkuyu muliso ndifuso? Mumachuluka nzelu kwambili. Man awawa aposa Ntanyiwa, Bakili TV, Man awa ndichida
Amene amasapota mcp ndi mfiti ndithu
Pofikana achinyamata awawa kutuluka ndiye kuti pavuta.
Ali ndizochita zamphavu koma azisiya zimenezo kumalankhula za ziko. Akuluakulu ziko muno MCP tatopa nayo kwambiri zikuwawa koma zoona zikoli tizingomvera za MCP ndi MEC basi.
Ife tikati tipereke maganizo athu iwo ati zimenezo ayi, DPP chipani chachikulu ziko muno akanena akuimilira anthu 17,000,000, a MCP akayankhula akuimilira anthu osalawo
Akutetezeni Yehova man🎉🎉🎉
Ulemu wanu big mukunenedzo zoona
More fire morefire wachikulile tiyenawo anyapapi amenewa
Zikomo murungu akudariseni
Osaopa nchimwene wanga
Takunyadirani a clif mumatiimilira ife amalawi
AKANGOFAT UYU NDIBWEZERA NDINEYO WINA AZAPEZRKA ALIBE ZIWALO WANGOSALA MIMBA PATUNDA NDIY CHIMWENDO BANDA ,ASASOWE UYU ? MCP. MUTISAMALET AMALAWI
Kuphatikiza apo malawi siyaku Lilongwe kokha ayi, koma achakwera mwalivula dziko ngati nzimayi oyendayenda kapena kuti hule, malawi Ali PA map a manyazi chifukwa cha ubusa wanu otsogolera amalawi ku mimbulu osati ku nkhosa, malawi ayaluka mochitsa manyazi chifukwa cha a Busa inu and tikuwona Zambiri zowopsa zoti chibadwile sitinaziwone, anthu mpaka kudya chitedze koma olo kulankhula kapena kutenga po gawo ngati kholo, tate wa dziko ayi ndithu abusa???? 😢😢😢😢 Mwachitsa manyazi dzina la ubusa malawi Ali pamoto uyu and dziwani kuti anthu sakukufunani 2025 ndipo mukadakhala Ena kunali kongoimika manja kuti zakuvutani Bola....🤔🤔🤔🤔
Aulule before they try to attack you MCP ndi anthu opanda mzimu
Nuff respect comrade cliff
Eish koma zigandangazi
Kkkkkkk komatu phamvu sumaziziwa wekha
Athu ali ndi phamvutu kunjaku khope zake osakhalaso ngati zanuzo
Iwenso ndiye ulimbali ittiyo Bumbu laamako wamva
❤❤❤❤ comrade more fire
Auze Amvetsetse Chilungamo chimaba mumtima osawabisa asatana
Osamat opyeza musiyen ayankhule chilungamo
Ada awa akulankhula zanzeru, wandiwaza
Tayakhulani leroli baba ayaluke lero LA 40 likakwana yakwana tayakhuleni baba chimwendo wado wado wajaira
Koma Mulungu akutiyendeladi kuzela mwa anthu ngati awa'mwe
Auze bro anyapapiwa dzianthu zokupha
Tiyenawoni Makape amenewa atijaila
Kkkkkk koma kumalawi athu achilungamo ndiambili chilima anasegula maso achinyamata aaaaaa amalawi 💪💪💪💪💪💪
❤❤❤❤kuswa kuswa basi
Achinyamata tatiyen tidzuke mzathu wayamba kale uyu
Koma uyuyu ndikatundu payekha, Kamangila 2 baba
Mfumu iliyonse ikuyenela kudziwa figure ya anthu ammuzi mwake....everythung starts from the local government....where is the youth?
Faka Dadieeee 🔥🔥🔥🔥🔥
Tawauzeni anyapapi amenewo ,, la 40 lakwana basi
Ndiwantchito wathu namachende amaneyu nkumatiphaso mdi nzake moses....
The DC 2
Alex kamangila 2 wafika 🔥🔥🔥🔥
Kodi bwanji amalawi munthu akati ayankhule chilungamo akuti tithana naye chifukwa chiyani MCP maganizo akupha basi ayi mani MCP ndatopa nayo ine, nthawi zonse MCP basi
❤❤❤
Azipanizotsutsa akuzitenga pa n'gono akufuna kutisiya mavuta taonda nawowa, zisithe izizi
Uyuyu mkatundu eee💪💪💪💪💪😂😂😂❤❤❤
Ngati akulephera kupanga passport kuli bwanji kupanga ID ya dziko, padziko lonse ndi dziko lamalawi lochitisa manyazi kukanika kupanga passport. Chiyambire mbiri ya dziko lamalawi aka ndikoyamba anthu kubwezedwa pa border
Ndiwe dolo timafuna madolo ngati inuyo big
BIG MAN ULEMU WANU
Auze fada
Zoona.kweni.ipase.moto