Akuti ndikavote pa 20 pano. Meaning Nyimbo iyi Mbenjere anaimba dzaka zambuyozo. Chorus ndiya Mbenjere koma wina walowa ma verse`wo ndi kuika zomwe zachitika chaka chino cha 2024.
@@AlfRed-i6y musaiwale kuti kunali zogulitsa ndege ya air malawi ndi a jb that's y ndege ikutchulidwamo ndithu ineso nyimboyi yandisangalatsa kwambiri kmno anyamatawa akumapita kukayimba ku misonkhano ya mcp.
@@FalesichiutsiFalesi komaso imvani za tsiku lovota akuti pa 20 yet vote ya 2025 ndi pa 16 September km anthu sangazindikire chifukwa mind yathu ili ya za ndege ya ku chikangawa.
Ndale za kwathu kuno zandidziwitsa kuti anthu ambiri mmalawi muno brain nzobooka ,akangomva chinthu osachifufuzanso Basi Ena Ali pa nyimbo ,Ena m'ma social media, kulibe Boma lingadzathetse mavuto athu izo nde kulibe Kaya palowa wins nde worse alipowa sangakwanitsensoyi ,ulesi(n'sanje Ndi katangale) ndiimene utiphweteke
Wazindikila chilungamo ndiyemweyo 😂
Yaaaah bro ndimbenjere ameneyo I know this guy he has also another style of singing
anthutu chilungamo akuchidziwa mutha kuona & mbenjele ndi ozindikila😂😂
Kkkkk wazindikila cuz Ali kuchikangawa party? Ndipo Kodi akat kuzindikira nchani ngat sikuchikuta zinthu mwanzeru munthawi yoyenera? So ngat nkuzindikira KO kwagona pati pot posatengera ndale or chipan chosatira koma kuima pachilungamo zinthu sizili bwino pankhan ya umoyo kamba Ka usogoleri ulipo omwe anthu Ake akukhala ngati agontha komaso khungu moti sakuoan ndikunva mmene anthu Ake akuvutukira then kod Munthu ozindikira panthawi iyiyi yomwe anthu akuvutika ndipo akusowa anthu omwe angathe kuwayankhulira zammene uli Moyo angasapote zomwe zikuzunzitsa anthuzo?
Yaphedukadi for real, big up!!!love it
Ameneyu ndiye timati Legend Mbenjere💪 Not anyapapi omwe akumakayimba ku MCP music Show!
Zoona Chakwera you must go, watikwana
Mbenjele kubaya pa liwombo 😂
Mbenjele katundu wa amalawi uyu 😂😂😂
Inu zimenezo sinzikugwirizana ndi zomwe akumvena pamebepo mix inyimbo imeneyo ndiyakele oro Dr Laz asalowe m'boma
Komaso mmene ndikumverela mau enawo simbenjere ayi ndiwomwe anyamata olubwalubwa 😂😂😂😂
good composition Mbenjere amatha
Km boma ndilomweri stikusintha m'paka 2030 wooooo
Yemwe akufuna kusintha
boma angosintha mkanzi oro mwamuna pamenepo ndiyekuti zimunthekera
😂😂😂😂😂😂
Imbwaiwe
Mbuzi 😂ndi mbuzi olokuyingenda pompo imaona ngati dzuro
Nice song mbenjele tufuna izizi iyi ndiye sound yanzelu
He's the one 😂😂😂, galu wake yomwe wayamba kukuluma
M-malawi aliyense akudziwa nkhaza dzimene adapanga a mcp ku Chikangawa.
Akuti ndikavote pa 20 pano. Meaning Nyimbo iyi Mbenjere anaimba dzaka zambuyozo. Chorus ndiya Mbenjere koma wina walowa ma verse`wo ndi kuika zomwe zachitika chaka chino cha 2024.
Iwe wabodza nyimbo yaimbidwa Pompano usaname
Uzinva nyimboyo message yake, Kodi mesa zotenga ziphatso Kuti abere mavoti zikuchita pompanopa kumawanamiza anthu Kuti awapatsa chimanga apititse ma ID. Open your eyes big Amalawi ndiochenjera MCP Siingatipusitse
Chorus ndi beat ndi mbenjere koma zinaz ndi wina 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Anthu alowetsapo zawo apa mbenjere maimbidwe ake timawadziwa kkkkkkk izizi ndingati zomwe zinawachitikira mablacks kungowanamizira😂😂😂😂
Madobadoba amujudula mbenjere,
Nyimbo ndi ziwiri zosiyananso
Tikumva kuti wamangidwaso anyway Mchinji simagawa kamba😂😂😂
Ndiwe Galu heavy that is old music since 2014 I'm remember ase.
Koma anenamo za ndege umu it's like niku chikangawa 😅😅
Nde bwez akukambamo za ngozi ya ndege?
Yabaya kkkk
Mbenjere ulemu wanu big brother be strong 💪 🙏 that is true 👍 🙏 👏 🙌 😄 😆
Nyimbo waswa iyi eeeeh, mpaka Mr Chi........ atayimva Mmmmh
😂😂😂 Nyimbo nd iz zot ukamamvera uku ukunyekhula
Kkkkk
Ndalamazo idyani Koma Vote ili mu mtima Awa akomoka ndithu Komwe tikupitaku
Ine mbenjele ndimakhala naye kuno uyuyu simbenjela koma amene wayimba nyimboyi wangotengako ma part ena ambenjele anyimbo zakale
We are creating the Kamangilas more and more ❤
This song ndyakalekale and it's mbenjere himself who sung it
😂😂😂😂Kaya ndi iyeyo kaya si iyeyo nyimbo yi ilibwino😂😂😂
Ati kuli Adani luu akuyimba tidasungira wanthu wasundwe kkkkkkDPP boma
Big man Mbenjele nyamata wama suit otchena
Ndi mbenjere ameneyo 😂😂😂😂😂😂
Inu ndi mbenjere uyu weni weni
@@ShamilahSaizi 🤣🤣🤣😂😂
Ine Nyimboyi ndidayimvelako tikuyandikila zisankho za 2020 wina wake adapangila TikTok
Nyimbo yakale iyi, he was singing against APM.
I like mbenjere they song sound malawi ❤
Ndi yakalè kale ase nyimbo imeneyo
Ndimbenjela ndithu sangalephe Ku MCP alawoko posachedwapa chifukwa kumbuyoku anayimilako u mp koma ndi UDF
😂😂Ndamumva ndiyemweyo
Nyimboiyi amaimba kalekale thawi pp
Uyutu ndibwezi akumangopitiliza kuyimba chifukwa samaguga ngati mmene alili ambili a reggae a ku Jamaica
Ndiyemweyo
@@GoldenNamanguya-q9u 🤣🤣 afananaditu komaso Bit yo ndiya Mbenjere
Palibe amene savakuwawa mbenjele nayendi Muthu mwina achita manyazi
Nyimboyi adayimba ndi mbenjere ft symon mu nthawi ya pp kmno zangogwilizana kwa mbiri ndi nyengo ya chikangawa ino kmno pano akuyimba za mcp😂😂😂😂
I think you are right
But he did not feature Symon, it's someone else
Komano zandegezi bwanji
@@AlfRed-i6y musaiwale kuti kunali zogulitsa ndege ya air malawi ndi a jb that's y ndege ikutchulidwamo ndithu ineso nyimboyi yandisangalatsa kwambiri kmno anyamatawa akumapita kukayimba ku misonkhano ya mcp.
@@FalesichiutsiFalesi komaso imvani za tsiku lovota akuti pa 20 yet vote ya 2025 ndi pa 16 September km anthu sangazindikire chifukwa mind yathu ili ya za ndege ya ku chikangawa.
Oyimba amene akulowa muchipani cholamula bola nyani angakhale ndizeru pamene wafika Malawi munthu wazeru sangamene kuti boma ndilomweli okhawo womwe nali ndi mizimo yoipa andi amene akuti mboma ndilomweli chifukwa satana or munhamuphuzitse bwanji mawu a Mulungu sadzatembenuka.
Nyimbo ndiyakalekale iyi 😂 koma cadet ali pa job
Nanga za ndege nzaliti?
Koma nyimbo iyi ndiyapakanthawi siyatsopano ayi koma ndi yomweyo mbenjere
Ndikalekale nyimbo iyi kkkkkkk , inu mwaivera kumene.
Nyimbo ndya kalekale iyi 2019
Mbenjere ya kalekaleyi inuyo mwaimva lero koma kumalawi kkkkk
More 🔥 🔥🔥🔥🔥
Mbenjere ndi Mp koma wadatuluka Dpp pano ndi wa Mcp ndiye inuyo musamunamizire pa za nyimbozo
Mbenjere ndi Mp?????
@@MalawianCamera ineso kudabwa
@@MalawianCamerabro dont mind him samadziwa.chomwe amakamba nthawi znse awo
@@AmanaHambaliemukamva kuti ku MCP kuli zisru zokha.zokha musamadabwe nazo zimenez
Mp wo akuphirira paborder?
Kkkkk ndiyemweyo😊
MCP my vote
ipase moto mbenjele nyimbo koma imeneyi osati atuluka ukweche ndiye zichani
We need some more teachings!!
Yomweyo mbenjele 😂😂😂
Nyimboyi ndi ya nthawi ya Joyce Banda musapusitse anthu
Nyimbo yakale kwambiri nthawi ya Joyce Banda amanena zandege idagulisidwa
Title take chani nyimboyi?
Usanchimwitse
Kkkkkkkkk koma ayi mcp mwanyanayo basi sinchewa ameneyi ayi zikomo
Mulungu naye watopatu pano anthu azingo ng'alula basi
Nyimboyi ndi ya Mbenjere anayimba 2019 towards 20 May mmenemo DPP ikugawa Chimanga ndi ngongole ya madefu.
Ameneyi ndimbenjele emweyo komansotu paja anaimbakale yatinkat tambalawakuda komandimloza
Mbenjere at his best
Chimozichakwetekwete ndi mutu wanyimboyi ndiyakale ife amene timamvera nyimbo zake imeneyi tilinayo
Ndiya chinkangawa yoo😂😂😂😂
Ikhala bwanji yakale atatchulamo zandege ndiyapompa no
Mwakalipa amalume DPP BOMA kkkkk
Nyimboyo angoipanga Remix ndiyakale kale
Nsokhano wa Apm rikavinila yomwei
Anaimba nthawi ya Joyce Banda when she was a president and he was on wanted mpaka anathawa
Wow thanks for the information timadabwatu
@@MalawianCamera 😂😂😂😂I like that song ndilinayo since that time
@@Mpungwe123 koma anaimba bwino coz ikupangaso fit mu nyengo ino 😂😂
Uyu ndi Mbenjere weniweni
Umakwanaaaaaaaaaaaaa💪💪💪💪💪💪💪💪💪🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥💯💯💯💯💯💯💯💯🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
Sangagule oimba onse ....kuswa kuswa basi
ndi mbenjele komaso nyimbo iyo ndiyapakanthawi ndithu osati panopa
Ndi mbenjele of course
Akuziziwa ndimwiniwakeyo
Mbenjere Ali ndi mnzake ameneyu
Amenenu ndi mbenjere koma Ali mnzake
Auzeni a MCP adziwe okha Mbenjere
Kodi in mukumati Boma ndilomweli mumagula zinthu motchipa nde kuti
Nyimbo iyi ndiyakale kwambiri
Ndiyakale koma yimakhala ngati ndiyasopano inali yamunthawi ya joice Banda
Wawonatu mbenjele😅😅😅😅😅😅😅😅😅
Mbenjere yemweyo😂😂😂😂😂😂
Ndiyebweyo ndithu
Uyu waionela patali akuziwa kumene kukupita boma pa 16 sepitembala
Symon & Kendal uyu
Pali colab
Kkkk ndimbenjele ndianyamata ake
Ndale za kwathu kuno zandidziwitsa kuti anthu ambiri mmalawi muno brain nzobooka ,akangomva chinthu osachifufuzanso Basi Ena Ali pa nyimbo ,Ena m'ma social media, kulibe Boma lingadzathetse mavuto athu izo nde kulibe Kaya palowa wins nde worse alipowa sangakwanitsensoyi ,ulesi(n'sanje Ndi katangale) ndiimene utiphweteke
Nyimboyi ndi yakalekale anaimba munthawi ya joice banda
Kunaliso zandege kodi nthawi imeneija
Yemweyo
Ai simbenjere
Nyimbo ndi 2014.
Mbenjeleeeee❤
😂😂😂😂lpatse moto ❤❤
Nyimbo yakale iyi
Alright ndiyakedi?
Nyimbo yakalekale iyi nthawi ya Joyce banda muveleso salowa 50@@MalawianCamera
@@BrightonEnockEnock Thank you brother that's what we wanted to know 👍
Ndimbenjere tape yake ine ndilinayo😂😂
🤣🤣😂 Serious?
@@MalawianCamera eya ndiyakale ndithu tikupukusila tape sekela🤣🤣
@@paulpaseli6310 😂😂😂
Mbenjere yomweyo😅