It always pains me when we Chewa tribe are taken like fools or all mcp funs. Some Chewaz are exceptional. TTV big up!! Osagawa ma sweet no!! We need leaders who love our Malawi through right decisions and good governance.
I can say bravo to the directors of security for both parties of MCP and DPP of what happened in Mzuzu, that was true exercise of a good Democracy. Let peace reigns this is nice. Zikhale choncho Ku madistrict onse especially South and Central regions Ma campaign akhale aufulu. Political tolerance a way to go.👏👏
Ku Mzuzu kuli anthu ozindikira zimenezi ku Lilongwe sizingatheke and always pamakhala special team ya ziwawa so amadutsanawa zaziwawa sizimawakhudzudza.Alipo ma baunsa amene amayenda ndi zikwanje aja
Ma top positions should not be appointed by the president but should be appointed through parliament like mec chairs, inspector genal , nrb chairs not by the president because president belongs to a certain political party.
Tipex yili ndi zolinga ziwili. Kwa oipa kubera. Kwa olungama kukhozera pomwe paonongeka. Koma cholinga chenicheni ndi kukhodzera pomwe pa wonongeka. Pa nthawi yija anali kukodza momwe m'naonongeka
Kmanso mmene mwayamikila ma supporters a MCP ndi DPP apangira liwudzeninso bola la MCP kuti kalembedwa ka ma ID zikhalenso chimodzmodzi ma boma onse mMalawi muno
Kosdi zoti ndege idafika ku mzuzu amamvana ndichani kuti ndege izathele? Nanaga mawu amenewo ku control alipo ngati Mundege mudalibe box ,,,yaku control ilikuti sound
Kodi imu mesa a ndevu zamwayi milati simutenga information ya social media mde za kumangidwa kwa mtambo munazitenga kuti? Inuyo mukudziwa kuti imali plan ya mvp yomwe imafuna kuipitsa mbiri ya dpp bwanji simukunena?
If the government wanted a fair and transparent election they could have reappointed Mr Chifundo Kachali because he did the last election religiously. But because the current government is aware that they can not win without kubela that's a Ntalimanja was appointed.
Tisayiwale koma kuti Chakwera was attacked in Mzuzu pa Katoto pompo when MCP was an opposition party. Ku Karonga was almost a no go zone area mpaka was nicknamed Bengazi for its terror nthawi ya DPP. Ndiye Northern Region is not as a holy region as is being speculated.
Well speaking men, chikangawa mwamuyankhula koma samamva za wanthu
Well done guys mumalankhula chilungamo keep it up
Bravo Times TV continue kuyima pachilungamo
It always pains me when we Chewa tribe are taken like fools or all mcp funs. Some Chewaz are exceptional. TTV big up!! Osagawa ma sweet no!! We need leaders who love our Malawi through right decisions and good governance.
This was very much impressed n it may b well tanen as to concerned parties
I can say bravo to the directors of security for both parties of MCP and DPP of what happened in Mzuzu, that was true exercise of a good Democracy. Let peace reigns this is nice. Zikhale choncho Ku madistrict onse especially South and Central regions Ma campaign akhale aufulu. Political tolerance a way to go.👏👏
In that commission of enquiry you should also include some of Chikangawa villagers please anthu akumeneku Aliso ndimau komaso umboni wabwino
Ku mzuzu ose ndi a DPP awo mukuona ndi amodzi ena angopita ku mcp kufuna ndalama koma vote yawo ndiya Dpp
Hmmmm ili nde bodza ili
𝐞𝐲𝐚 𝐱𝐨𝐨𝐧𝐚 𝐚𝐥𝐨𝐧𝐝𝐚𝐤𝐨 𝐧𝐝𝐚𝐥𝐚𝐦𝐚
Bola MCP DPP ayi tu kumpoto kuno
Good idea times yendani mudziwe zoona ndazikonda❤
Ku Mzuzu kuli anthu ozindikira zimenezi ku Lilongwe sizingatheke and always pamakhala special team ya ziwawa so amadutsanawa zaziwawa sizimawakhudzudza.Alipo ma baunsa amene amayenda ndi zikwanje aja
Kungong'alura zilungamo pwiiiiiiiiiii!
guys yehova akusungeni pobisika mwaima pa chilungamo mokonda dziko lanu mosatengela mbali pitilizani
North is special
Congratulations 🎉 Northern region this is what we call democracy
Nice speech with very good logic
I could be much impressed if all sensitive positions in the country were approved by a parliamentary commission where all parties are involved .
Exactly Malawi can change
Kuyankhula kofunira zabwino dziko lanu, zikomo.
Amadanitsa anthu ndi ma politicians. Zinachitika ku mzuzu ndizabwino
Powerful massage
Waiting for them in southwest and 😊😊
Kachali is a gentleman ❤
Pasakhale ndipo pasapezeke ntundu wa anthu ndi umodzi omwe odziona kuti ndiye oyenera kutsogolera dziko la Malawi .
Pa ifa ya Saulos Chilima Ndi Anthu 8 kuchikangawa akuluakulu Inu mwandiuankhulira bwino kwambiri 🙏🙏🙏🙏
Makosanawa Ali ndi mulungu asawope mulungu alipo awamenyela nkondo ine ndili nawo limodzi awawa❤
Good job times Redio❤❤
Nice speech ❤❤❤
Ma top positions should not be appointed by the president but should be appointed through parliament like mec chairs, inspector genal , nrb chairs not by the president because president belongs to a certain political party.
💓💓♥️♥️💪
Gentlemen,khalani serious munkhanizi.Mwina chifukwa mulibe Brain.
Mukuonjeza kutseka kwambiri.
Tipex yili ndi zolinga ziwili.
Kwa oipa kubera.
Kwa olungama kukhozera pomwe paonongeka.
Koma cholinga chenicheni ndi kukhodzera pomwe pa wonongeka.
Pa nthawi yija anali kukodza momwe m'naonongeka
ine ndi chewa koma mawu oti dziko ndilachewa nde mmm musasalalkhule wangokhala kuti mtsogoleli uyu ndi onyasa mtima ndipo sakukhalaso pampando
We can say mzuzu is the most civilized city.
Those people who look like mcp supporters are not mcp supporters. Mcp buys people to go to their rallies
This men they are telling the truth
Very good
It was nice indeed yoooh..😊😊
Ayitanise ndithu aaa asazembe
Congratulations 🎉 wana wakukaya
Atseke Kaye MBC imanenaso zopepera, katsakulaso akunena mwano kumeneko
Program ya lero ndi the best. Sikuona mbali
Kmanso mmene mwayamikila ma supporters a MCP ndi DPP apangira liwudzeninso bola la MCP kuti kalembedwa ka ma ID zikhalenso chimodzmodzi ma boma onse mMalawi muno
Amai aja ananena choncho chifukwa Mcp ndi imene imayambitsa za chiwembu ndinkona ananena kuti Mcp isadzapangitse ku phalombe
Kodi zikutheka kubela masankho? Ndizowina tipex 2019 MRs jean assah Tipex
Yah Kung,alula
Kosdi zoti ndege idafika ku mzuzu amamvana ndichani kuti ndege izathele? Nanaga mawu amenewo ku control alipo ngati Mundege mudalibe box ,,,yaku control ilikuti sound
👋👋 kuyakhula komatu uku
Mayi Yolamu akugwilitsidwa ntchito ndi Chakwera yemweyoi nothing can change as mcp they are commanding Malawi police to favour them
Koma nde kung'aluratu no mantra times kip it up
Chigawo chapakati sangapamge zimenedzi kwanyawu kumene kuja zitsilu za anthu
Ndipo sukunama,mbuli za anthu
Kkkk Koma anthu Inu pulizi 😂😂😂😂😂😂
Km kumalawi kuli ntchito eeeesh ai zikom
Kuleza mtima kumeneko kumapezekadi kumpoto kokha ,chifukwa choti Democracy inabwera ndi munthu kumpoto amene anali Chakufwa Chihana,kumwera ndi pa Central regional zikanathera magazi ,sakanatha kudutsana bwino bwino
Amadziwa kuti awa ndi anzathu a DPP uku tikudyako kaye ndalama zaphwekazo 😅
Dpp yokhayokha iyi agendana bwanji awo akungopita kukatengako ndalama basi
Ambuye chonde mukune muliko mupheni chakwera please Please ife ndakapolo anu please chakwera ntengeni chonde
Let's pray for the nation not to have blood she'd come 2025 elections
Achita manyazi aDpp nthawi zonse kuyipaka mbiri zoipa MCP anthu akuonetsanitu.
I think ikhale Dpp yomweyo zinazi ndizakupha, Kuba .chomwe tikudikira ife Peter akangolowa Ayesetse Anthu amenewa amangidwe basi
Apa tizavota chifukwa coz we are out of options koma MCP DPP zose ndi mbola
ndimkaona ngati times group ndi ya MCP komaa eeeeh! simmene kulili amwene
Nkhani izingokhala chikagawa ife tidzadya chingawa za ziii
Ndizoona zomwee mwalankula masapota atu pitilizani kalidweli Pali ena amawasokoneza masapotazi athu
Onsewa akuzavotera chipani chimodzi,alipo akudyeredwa apapa.akudziwana. sizingatheke kungodusana kumalawi kuno.kkkkkk ku mpoto kuli atambwari😂
Kwathukuno kummwela sitingalole Kuti MCP tidusane ndimagazi amenewo
Ndege yopanda battery kkkkkkk koma achakwera ai zikomo ambuye pomulenga chikangawayuu
Pamene akudusanapo ndi pa Ekwendeni po pamo pa nya Hara
Tafufuzanidi kuti zomwe anthu akunena za nrb nzoona chifukwa kukana kuvotela I'd atha kukhala ndi zolinga Zina ndipo awona kuti zilepheleka ndi nkhani ya id.
Mmmh mukudziwa zomwe akuchita kuseriku awa asakupusitseni ndithu 😂
Enafe tinapitila kukapeza 2 pin yandiwo koma ife tikavotela dpp
Ndikuona ngati malamulo adziko amakhwila tchito kumpoto kokha, chifukwa chake mmaboma Ena ake kumakhala chikulilano
😂😂😂😂😂 guys mwathira nchenga mumpunga wagulu
Apapa sungadyeke olo kumezanso ayi😂😂🎉
@@SolomonNjolomole 🤣🤣🤣🤣🤣
Sangaiseke times ife tikufuna zithu zisithe mcp ipakile tatopa nayo yatikwana ndi manyakala awa
Northern Region ndi anthu ozindikira sapanganawo zopepera
Anthu omwe akuoneka ngati ndi a mcp si a mcp. Mcp ikumachita kugula anthu opita kumisonkhano kwawo
Umu nde asambwazadi
Ndinu amanyi nosenu kuli pitala kunalibe nkhaza ? Ndinu zitsilu kwambili mcp singapange naw zaugogo ai
Hahaha 😅😅😅 yabayatu mwana wa njoka iwe ndye uphulika chfukwa simunat achikangawa party tikukhwekhwezani asatana inu
Chikangawa ichooo😅😅😅
Ine ndimawayamika anthu aku north amakondana
Zmukamanyoza mudziyamba kuon kut chatsitsa dzaye nchani kut njobvu ithyoke nyanga. Shhaaaaa abale
Week ya mawa abishop azakhaleposo
Chiripo akubisa anthu akuphawa anapha chilima ndi anzake
Kumpoto amantha
Naa ya gomboi nde iwamalzad abomawa
Ndazikonda kwambili zimenez
Kumpoto kuli anthu ozindikila kuti ndale zisawadanitse.
Dpp ndidye obera zisankho. Only dpp and their team b utm amakamba za chiavhine.
Kodi imu mesa a ndevu zamwayi milati simutenga information ya social media mde za kumangidwa kwa mtambo munazitenga kuti? Inuyo mukudziwa kuti imali plan ya mvp yomwe imafuna kuipitsa mbiri ya dpp bwanji simukunena?
Ae mcp mwawaphumzitsa chikhalidwe
Kod a bishop aja sadzabweraso ??ine amandsangalasa akamang'alula 😂
If the government wanted a fair and transparent election they could have reappointed Mr Chifundo Kachali because he did the last election religiously. But because the current government is aware that they can not win without kubela that's a Ntalimanja was appointed.
Ife si akumwera okonda ziwawa kapena a pakati
Kodi ukakwarila azimayi awili akadwala mozi kumawula ungapitise mzakeyo ?
Koma akumanyegererabetu kuwatengera ku china kodi tiwakhulupilire bwanji anyamata wa
Anyamatawa mpaka uniform ku ntchito
Kuyankhula kopusa achewa zikoli ndamene amaliwonga
Chomwe anthu angaziwe ndi chakuti anthu omwe amaoneka ngati a mcp si a mcp. MCP ikumachita kugula anthu opita kumisonkhano kwawo
This is northern region, it'll never happen in central and southern region
Tisayiwale koma kuti Chakwera was attacked in Mzuzu pa Katoto pompo when MCP was an opposition party. Ku Karonga was almost a no go zone area mpaka was nicknamed Bengazi for its terror nthawi ya DPP. Ndiye Northern Region is not as a holy region as is being speculated.
Mpaka ena ayedzedwe 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Boma sitikusintha mwayambakale kulira
Awa a dpp akudziwa kuti sangawine boma lidawakanika umbuli basi
Anthu a kumpoto ndiozindikira
Ku mpoto kuli anthu abwino okha okhatu
Kusekedwa ndi kutsekedwa ndi zinthu ziwiri zosiyana .