A Chimwendo Banda Tengani Ndalama Mukonze Chipani Mosangalatsa A Malawi Osati Kuwapatsa Oyimba
ฝัง
- เผยแพร่เมื่อ 24 ก.ย. 2024
- On Nyasa VoiceBox, a concerned citizen asked Honourable Richard Chimwendo Banda, Secretary General of the Malawi Congress Party, to use the money to buy maize for hunger-stricken Malawians instead of distributing cash to celebrities and recycled politicians as a means to win votes.
Ku Nyasa VoiceBox, nzika yokhudzidwa idapempha Mlembi wamkulu wa chipani cha Malawi Congress a Richard Chimwendo Banda kuti agwiritse ntchito ndalamazi pogulira Amalawi omwe ali ndi njala chimanga m'malo mogawa ndalama kwa anthu otchuka komanso andale omwe amawagwiritsanso ntchito ngati njira yopezera mavoti.
#malawi
Well spoken ndalama zikuwonongedwa anthu tikuvutika,..
Chimwendo Banda will no going anywhere with his dirty politics.
Truth talk Mr apenga a mcp
Auzeni chilungamo malawi walero si wa 2019 anthu akuona patali
2025 no more Chikangawa party
Facts big man ❤❤
nzeru palibe
No tikufuna agule chimanga kwa anthu ovutika
MCP ikuononga ndalama oimba uyuyu mpaka kumupatsa mk1.8millins ndi yantchito yanji? MCP yanyanya.
Bwana chipani chathuchi chaonongeka ine kuchokela kale ndili mu mcp koma panopa chipani chathuchi chaola bwana, ndipo panopa ndili okhudwa kwambili ndi tsogoleli wathu chakwela, nzelu mulibe kunena choona,ndipo ifa ya chilima ndikaziyan'gana kuchokela pachiyambi kufika lelo mmmm chakwela anapha chilima ,apa palibeso kukhonza bwana athu ndokwiya,chilima amakondedwa, bola akanakambilana osati kuphaa
Truth to be told
Chifukwa ndi ndalama zamasiye zotembeleledwa sizimagwila ntchito azazindikila ali kunja kwa boma ndi zitsilu zokha zokha ku bomako kulibe owalangiza
Dan lu watha ngat makatani
Koma MCP mukumva nayo nyunyunyu
M'mene amavutikira a police kukhala 5 days panja ngati kubwera Chikangawa kupangitsa msonkhano kuwapatsa ma 2 thousand koma oyimba kuwapatsa ma million.
Koma boma kudelera a police
Vote yanga ndi DPP
Cadet
Wayankhula mukwAnila sangamukwaniseso malawi kkkkkkkkk
Ndipo awuzeni nkhale zitsili zikumamenya anthu chifukwa cha 5000 kuvina azimai zitsilu akatha nkuwapasa 2000 nkhale nyumba alibe akukhala mma rent zitsilu wina kubwela kuzangoimba akupasidwa 50 million wovina 2000 uchitsilu weni weni agalu..nymba mulibenso ..
Wapenga misala?
Dan analandila 50million taganinzani talama yotseyo ndipo munthu amene wamugulayo zangabwelenze anthu chipani tawonani yemweyo adayimba chimo yoti atule pansi udindo lero akulowa chipani chatu tingakhuluphilile amenye akufuna ndalama zangatandinze chipani dan alibe ntchito kuyimba ndindale ndizotsiyana kwabasi
Kwinaku mutukwana
NDALAMA SI VOTE TIONANA 2025 AKUONANGATI ADZAWINA CHIFUKWA CHOGULA OIMBA AONA NYEKWE
Very shame adzaziona thawi ikubwera
Ndipo mcp ikupeleka matama chipani cha dpp nanga tawonani dpp inapita kupoto mcp nayotso komweko malo moti asiyeni adpp apange zawo pomwe anthu adazindikila pano amata kuwona olakwitsa tiyeni ife amcp tilongosole chipani km zoti dpp ili kwakuti ifetso komwe ndikulakwa kumeneko mapeto ake dpp izinyawuda kwambiri tiyeni ife tilongotsele chipani nthawi ikadali amalawi akwiya kunjaku tiyeni tanyengelele
zoona munthu wakhulu malo moti mcp ikanalongosola chipani alibusy kugula anthu oyimba zopanda ntchito malo moti apange kapeni kukopa anthu kd Dan lufani wamugulayo angabweleze anthu mchipani kodi more over pali blunder yomalila chilima bwenzi akumakopa anthu mchipani alibusy kugula anthu
😂😂😂😂😂😂😂