@@MarthaPhiri-q8m kkkkk km iwe waganiza bwanji ndani angataye nthawi imeneyo pa mdala amene uja,don't force matters please munthu sangalankhule for 2hrs choima ndibodza limenero vomerezan chilengedwe
Mistake yomwe amalawife achita maka aku opposion ndikuvomereza kuti ayese machine pamenepo ndi pomwe game yagonera mcp mphamvu zawo zili pamenepa cz monga kalindo ananena njirayo ndi imodzi yozabela next season
Ada awawa ndazelu chimene amandisangala ine akabwela khani satenga mbali enawa mmalo angoponya khani koma kuyikokomeza kuchita kunetsa kuti iwowo Ali mbali ya DPP
Akazangoyelekeza kubela anne mtalimanja wawoyo azaonongesa ziko azawona cnanga ana atenga mwana wa tembo kuti azabele zisakho akhawula awonaso sitizalola tikuziwa kuti chikangawa ndi woluza luza kale ameneyo or atamati ku votako mawa chikangawayo sangawine ka 😂😂😂😂
@@FrankChanza-l3g Anthunu nde simukumunvetsatu munthu yu ena akumunena kuti wa Mcp ena akuti wa Dpp😂 video yi mukuionera bwanji kodi sanaimire mbali iliyose tu uyu apa
Ukulota ase kuchokera 1984 Mcp sitingawine payokha ma bwana anuwo akutiimbila phone kuti apa zavuta nde inu mukuti chani apa ena ayamba kale kugula nyumba kuno kudzakhala ena atumiza kale family yawo sitingawine ase
Mwana wa John tembo ndiwa mcp kumene chakwera akufuna kubera mavote koma kuzamvuta simasewera
APM my vote
APM uja osazaphwekesa
*A Boni Kalindo akuphika zotibweletsela asowatu 🎉🎉🎉🎉*
Ndipo wasowadi apezeka mawa
Zisankho it will be just a formality....gule kwao already
Kkkkk pitala walephera even kupanga hold convention kudzalankhula komaliza chifukwa chokalamba ndie angayendetse dziko
@@damianokachingwe3531aaaaaa inu munali ndi cholinga chofuna kumuchera pobwerera mwagwa nayo achimwene amene uja si mwana anakuwerenga kare kuti kuli mbora nde mumafuna mumuchite mbora ng, ooo
@@MarthaPhiri-q8m kkkkk km iwe waganiza bwanji ndani angataye nthawi imeneyo pa mdala amene uja,don't force matters please munthu sangalankhule for 2hrs choima ndibodza limenero vomerezan chilengedwe
APA panunkha kkk tambala tamugwira pakhosi
😂😂
Ndipo kwambiri
MCP idaononga mbiri pa 10 june nde vuto.. and sakubweresa report mpaka pano
Exactly bro
Apm my vote
Ndimmene tikuvela kuwawa amalawi ambirfe singalore chakwera apitilize apapa nde bola tifele chilungamo
😂😂😂sakusamalaso zochosa moyo wamunthu
Dats true,aend a thief to catch a thief(ziliko)
Zoonadi brother simukunama apatu MCP singawine ngakhale atabera motani
Tipex Thief Jane Ansa. Mtalimanja ndi machine Jane Ansa tipex Ansa wachepa
Ukunama iwe chitsiru
Dpp ndiyowina kale
Taa, ng'ooo mudzakhumudwa
DPP is a system mwavomelazano😂😂
Chakwera adaziipitsira posamutsa ma office omwe amabweretsa mwayi wandalama kwa ochita malonda matauni a Zomba ndi Blantaya nkuwasamutsira ku Lilongwe. Komwe kuli kupha chigawo chakummwera. Choncho muchigawochi adzangopeza mavoti ambuli zo
Kuchokera pamene ndinamva kuti boma lamukhulukira Boni Kalindo milandu yache sakuonekanso,nkutheka pamwamba pa kukhululuka anapatsidwa ma millions ngati Chibanzi ,koma ndingadandaule bwanji chifukwa ndiyekhayo akuyankhulira amalawi tonse
Sanapasidwe kathu iye uja samapanga za nyerotu akuti amadwala mupange search watulusa odio lero wapepesaso kuti amadwara alipo ndithu
Mhmmm ukunama aise amene ndi The DC
Zitsankho zogwiritsa ntchito akazi kubera mavoti no use of voting.
Koma iweyo sindmapanga comment koma lero wandisangalatsatu keep it up bro ukuesetsa ntchito
Musaganize kuti mungadzachotse MCP ndi mademo ngati itawina! Zimenezo iwalani chimene muchite ndikupanga kampeni kuti mudzawine basi
👹🔨⛏️⚒️👹 Chikangawa Party 😂😂😂Devil at work
Mistake yomwe amalawife achita maka aku opposion ndikuvomereza kuti ayese machine pamenepo ndi pomwe game yagonera mcp mphamvu zawo zili pamenepa cz monga kalindo ananena njirayo ndi imodzi yozabela next season
Mulungu ndiwadongosolo mwina wapanga dala kuti ikhale 50.50
Apm my vote 🗳 ❤️
APM VOTE
Tizayenda kumene ASE MCP atayivotere ndan komaso inu khan imeneyo isiyeni zimenezo mumuphesa munthu
You are just imagining things tachoka iwe
Iweso ndiwa dpp mcp sinaluzepo amayibera ili fans
Adzawina ndi Dpp chifukwa iyenda ndi UDF,ndi Aford,UTM ndiye azaluza bwa
Mukapanda kusamala kukhala civil war Malawi be ready for any attack
Zamkutu, mumayidziwa inu nkhondo, agang'anthi
Big up brother man!!
❤❤❤❤
Kkkkkkkkk amwene koma mumaganiza apapa nde kunkhala drama sure and mwachiziwikire Jane asah azankhale monitor kkkk
😂😂😂 Azakhaledi monitor 😂😂
Adzakhar bwanj monitor ali phungu ? DPP inazolowela kubela kma MCP ndi 70+1
Kodi muli ndimaloto oti Mr chikangawa azawina ??
Pointless, straight wine for APM
APM My vote🎉🎉🎉🎉🎉🎉
Mwana wa John tembo asamale azaona nyenkhwe
Send a thief to catch a thief 😂😂😂😂
😂😂😂
Dpp 2025 woyeee
Ndiwe galu ufuna kupereka perception yofoila
Dpp ilowa awo kwao kwatha
Koma ine akulu awa nde amandisangalasa❤❤
🎉🎉❤Thanks 🙏
Ada awawa ndazelu chimene amandisangala ine akabwela khani satenga mbali enawa mmalo angoponya khani koma kuyikokomeza kuchita kunetsa kuti iwowo Ali mbali ya DPP
❤🎉 Thanks broh 👌
Ndipo kudzavuta 😢😢
Pamenepa yalakwa kkkkkk
Koma bro😂😂😂😂
😂😂😂😂
Kkkkk, ndipo live apa ndi game ya mbava zokhazokha
Ka Jane ansah nikandaniso kameneka kayidziwa MCP kuti sikugawa kamba idzawina iyeyo akuwona and adzavomekeza kt MCP wawina
Atiazvote ndiye ndiabamboako ndiamayiako kuphatikiza akazako anaako kumanso nkhukuzakwanu zonse olonso osazaiwala agalu ndiamphaka omwe kut ambwiyakoo azawine
U are intelligent man
❤🎉 Much love thanks 🎉
Akazangoyelekeza kubela anne mtalimanja wawoyo azaonongesa ziko azawona cnanga ana atenga mwana wa tembo kuti azabele zisakho akhawula awonaso sitizalola tikuziwa kuti chikangawa ndi woluza luza kale ameneyo or atamati ku votako mawa chikangawayo sangawine ka 😂😂😂😂
MCP PAYOKHA SINGATENGE BOMA MA DEMO AZAKHALA OCHEPA KOMA NKHONDO BASI
Kuzavuta
Heavy
Kutathauza kuti 2019 Jane adabela chisakho kuti pitala awine basi nowonso adzabela
Kungowina chakwera kudzachela tidzamatcha mpka kuchikangawa
Ndipo ndili pambuyo Pako mix watitopesa mmmmh 😊
Amayendana pansi palibe kubela zisankho kkkkkkkk chaka Cha mawa kuli zinthu za nyo
Ine sindingavotere munthu oti Mano mkamwa anatha nkhalamba ine ai 😂😂😂😂😂😂😂
@@daviechibwana3137 Boss mukuyankhula bwanji akumenyanitu anthu😂
Mcp sinawinepo zisankho
Ife chimanga tikuchisinja mutondo
MCP zinawavuta chifukwa cha anthu anafa ku Chikangawa. Anthu tilibe mayankho
This is true Mayankho mpaka pano sanabwere
ndipo kuzakhala kuomberana tizavotaso kawili
Kungobera kuzanunga linya
Eeeee kwambiri 😂
Bolani asamupheso Jeni Ansa yo a MCP
Athadi kumusowetsatu 😂😂 asamale kwambiri
😂😂😂
Kumpoto tili pheee kudya zammathumba mwathu
Tamugwila pa khosi tambala
Kuzavuta kumwela Koko
🙏🙏🙏🙏🙏🙏
Kodi DC anapita kut kwangoti zii
Pajatu ndi 50+1 musayiware
Kkkk a send thief to catch a thief😂😂😂
😂😂😂😂😂 Eeeeeetu azagwirana ufiti
Iweyo ndichitsiru kwambiri ase sukudziwqnso chimwe ukuyqnkhula
Aaaaa iweyo nde namache... Chikangawa
Azakhaula
DPP bomaaaaaaaa 😅😅😅😅
Kkkkkk umakwana iwe wabwera
😂😂Thanks broh
Mumakwana Pali mwambi amati mwana mbuu make mbuu
Aise zamademo usakaike mwinanso nkhondo
Akulu mukufuna mukambe chani sizikumvekatu
Ndipo 2025 kuvuta koopsa ..😂😂
Iwe tikamati ndiwe chisilu wawonatu kape wa mcp iwe galu
@@FrankChanza-l3g Anthunu nde simukumunvetsatu munthu yu ena akumunena kuti wa Mcp ena akuti wa Dpp😂 video yi mukuionera bwanji kodi sanaimire mbali iliyose tu uyu apa
Mn pangani nzero ina.imemeyo simunaganize bho inuyo
Ngati iyeyo akupanga nzeru? Mesa akuuzan za zomwe zizachitike kapena ndinu a Malawi Chikangress party 😂
Okay ndanva inusl mupeze comment ina ya nzeru iyiyi mulibemo zeru yayi😂
Kkkkkkkkkk nkhaniyo ndiyowona kuvutad
Kugwetsa boma sizamasewera
Uzikhala serious poyankhula
Paja winiko ananenatu kuti 2025 kuli zinthu 😂😂😂😂
😂😂😂 Atijigira madzi akuti mmidzimimu 2025
Jen asah wachani
50+1 m,bale
Kkkkk koma ndiye
😂😂Kuzachema
Kodi uli mbali ya mcp olo zita vuta ulendo basi
Ai baba 😂 nkhani ili apa ndiya Zisankho osati wa Mcp or not 😂
😂😂😂😂
Apapa agwirana umbavadi 😂😂😂😂😂😂
Ai Macson mbendela anabela zisankho, jane ansah anabelas ai palibe kusintha boma apa
Dr Lz 2025 boma kale
Ukulota ase kuchokera 1984 Mcp sitingawine payokha ma bwana anuwo akutiimbila phone kuti apa zavuta nde inu mukuti chani apa ena ayamba kale kugula nyumba kuno kudzakhala ena atumiza kale family yawo sitingawine ase
Chakwera sangawine zisankho 2025 pokhapokha adzabere.
Koma akadzangobera zidzaziwika bcoz ambiri samamufuna, tidzaonera zobwibwi
Maloto achumba😂😂😂😂😂
Day dreamer lwe!
@@ThokoMsonkho-hy4uc komaso kubelako zivuta Jane Ansah maso alipompo paja nayeso ndi dolo kkkkkkkuchematu
Thieves and evil.
😂😂😂😂😂
Apaaa MCP yagwidwa basi ma plan awo atha basi😂😂😂😂😂
😂Iwo anzao anawathothola ndi Mademo nao ayembekezere zomwezo 😂
@@MalawianCamera 🤣🤣🤣🤣Ndipo Adha apapa kulinkhondo koopsa Zedi azalira a MCP 🤣🤣🤣🤣🤣 wapanga dala Jane Ansah Kuti azizati lakutipo tionenso nanga apaaa bwanji?🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
APM my vote