That's the voice of our President Dr Bon Kalindo the DC,,, Tiyeni tiyeni tonse pamodzi tikapange Support Mayi Kaliati,, DPP,, AFORD,, UDF,, UTM plus other parties let's work together.
Mabishop Mulungu akugwiritseni ntchito kuombola amalawi. Munathaza kusintha one party system kubwera multiparty system ndinuyo. Musakhale chete, God is with you. God bless you ma Bishop athu.
Kom mavuto kwabas akuganiza bwanji chakwera alipamenepo chifukwa cha mai kaliyati wo leo kumawapanga chipongwe chotelo iye chakwerayo anapha a chilima bwanji?a police akewo osamanga, moses uja anapha watika bwanji osamanga chomangira zimayi ndi chani chani make make inu, anthu oyipa inu? we love you Bon Kalindo❤
Manganya achotsedwe ku UTM chifukwa ndi kazitape munthu oipa kwambili ndipo ndi mfiti. Kamunthu kaja kangofupika koma ndi oipa kwambili. ndikupempheni a Malawi 🇲🇼 ma demonstration aja ayambike lero. osadikilanso ndipo ineyo ndikanakhala mfiti ndikanamulodza Manganya ndi Chakwela. Koma osadandaula anthu amenewa atsala ndi nthawi yochepa kuti afe. Ndipo anthu amenewa adzafa ngati nkhuku za chitopa. let's wait and see and God he watching everything. God is God. and God is not Chakwela and Manganya. and let's pray all Malawians for madam Patricia Kaliyati.
A police ali ndi umboni ogwilika, Patricia Kaliati ndi anzake anakonza chiwembu choti aphe president wa dziko, ndipo pali VN imene Patricia akulankhulamo zoophya. Azinzake a Patricia atamva kuti wamangidwa iwo athawa. Nkhani ili lero tisathe mau tiyeni timve zomwe Kaliati wamangidwila
You can't even guess to say who is behind this. A father her daughter is involved in a road accident and is in hospital, who can be the first person to run to the hospital to see her? Imwee, manganya alikuti?
PALIBE ZA ONE PARTY STATE. MALANKHULIDWE ATHU OGOLANKHULAPO NANGA WOSABADWA KWA MUNTHU WA MZIMU... TISIYE. PALIBE KUMANGIDWA MUNTHU WOSACHIMWA . UCHIMWA KWA INEYO , INUYO SIMUNGANDILANDITSE . OSAPANGA MIRANDU POPANDA MIRANDU. NGATI SITIKUDZIWA IFEYO TISAVUTIKE NDI ZINTHU A MZIPANI IZOZO. ZONYOZANANZI NDICHO VHIFUKWA CHAKE TIMAGONYOZANA MOSANGANIZIRA IZO TIKULANKHULAZI. KUGULITSIDWA KWA MALAWI WINA YEKHA SANGALIGULITSE. KULIMBIKIRA POPANDA MTUNDA .. UMADZINYUMWA... AZAKO ATAKUSIYA MMALELE. TIYENI TIBVETSERE MWA CHIDWI IZO ACHIMWA A MAI ..KWENI KALIYATI. INUNSO MUNGAGWE MOMO.. Ati vhifukwa cha Democrancy... Ai Ai ... Need to be responsible citizens of Malawi Nation 🇲🇼💺🎓
Mavuto amenewa tikakhale bzy ku police chosecho azathuwo loko Ali police za kudya ndi mbweeee pomwe ife loko tili kunja koma kuchita kusowa ya bonya za ziiii
Ndimangoti mwagonatu guys 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
M'makwana inuyo ndi nambala wani😂
Kugona kulibe
@@MalawianCamera Tilipo ndithu,, tulo sitikubwera malingana ndi zomwe akuchita Mr Chikangawa.
@@MonalisaMwale-c5k 👌🎉
@@patrickmacheso5062 Eeeee zoonadi man zaukape
Olo kugonako mkumayambila Pati bro? 😂
That's the voice of our President Dr Bon Kalindo the DC,,, Tiyeni tiyeni tonse pamodzi tikapange Support Mayi Kaliati,, DPP,, AFORD,, UDF,, UTM plus other parties let's work together.
UDF,AFORD ili mu mcp, ngozi
@@OdettaLowrence Never,, never and never again MCP.
Mabishop Mulungu akugwiritseni ntchito kuombola amalawi. Munathaza kusintha one party system kubwera multiparty system ndinuyo. Musakhale chete, God is with you.
God bless you ma Bishop athu.
The RC Priests, pliz take action, MW needs your quick action to force the govt to stop immediately from leading us
Nthawi yakwana,yoti mcp iziwe mu ulamulilo wa democracy sikotsewelela,si one panty system.anthu, kofunika atuluke,mwela yonse go koko
Manganya akufuna Abe chipani apte nacho ku MCP
Koma mcp yafikapotu Mpakana kumanga mzimayiii 😢😢 but let GOD to be GOD Eksodo 14vs14 powerful vs Amen😢😢😢
Mvoto Bakili tv ikutichedwetsa ku Turkey zimai anatenga gun ndi ndikukapha anthu
Ndipo Anthu tulukani ndithu zisanafike ❤️❤️❤️❤️❤️❤️
Akweni don't worry about it, God is great, tili nanu mama 💪💪💪💪
Kom mavuto kwabas akuganiza bwanji chakwera alipamenepo chifukwa cha mai kaliyati wo leo kumawapanga chipongwe chotelo iye chakwerayo anapha a chilima bwanji?a police akewo osamanga, moses uja anapha watika bwanji osamanga chomangira zimayi ndi chani chani make make inu, anthu oyipa inu? we love you Bon Kalindo❤
Born Kalindo the DC mawa ndodo ituluke nthawi yakwana yokha💪💪
The only last man to stand we have the DC u are the best keep it up
Catholic Bishops & churches clerges yesetsani kut khalidwe loti tibwerere ku one party state tisabwerere. Yetsetsani posalola kut tisabwerere ku Egypt Kuja kut tizikaphula njerwa zamoto
Manganya mbolo yako, umve👊👊👊👊 Mr Kalindo more fireeeeee DC
Chikangawa chakwera ndi manganya mayikolo usiiii akufuna ataphedwa agalu amenewa
Ndiye Patricia kaliyatiyo ndindani iyeyo lamulo silimaona khope Andale akuzolowera kwambiri amaona ngati dziko ili ndilamawo.komaso Mary chilima musamupangise Kuti asauke osamukakamiza zandale zanuzo zanuzo
Bwana ulemu wanu mwandilakhulira chilungamo ngakhale chilungamo ndi mwano ❤
Mayi Kaliati ndi munthu olimba mtima we will vote for her
Koma akufuna nkhondo chakwela nd usi please please please tulukani mawa kumenya ndithu osawopa zangolakwika enafe tilikutali zandinyasa kwambiy😢
Amalawi simunati ! Tough time is lying ahead .
Akalindo Pena chilungamo ndikuona ngati chikusowa Pena ndindale izi muphana zinazi zotumidwa izi politic iyiiii
Trust is a luxury you cant aford betrayal is something you cant ignore
Akuyambitsa zonsezi ndi manganya
Malawi kuyambika mademo from no where
Manganya achotsedwe ku UTM chifukwa ndi kazitape munthu oipa kwambili ndipo ndi mfiti. Kamunthu kaja kangofupika koma ndi oipa kwambili. ndikupempheni a Malawi 🇲🇼 ma demonstration aja ayambike lero. osadikilanso ndipo ineyo ndikanakhala mfiti ndikanamulodza Manganya ndi Chakwela. Koma osadandaula anthu amenewa atsala ndi nthawi yochepa kuti afe. Ndipo anthu amenewa adzafa ngati nkhuku za chitopa. let's wait and see and God he watching everything. God is God. and God is not Chakwela and Manganya. and let's pray all Malawians for madam Patricia Kaliyati.
Aaaaaaaa Bon aaaaa ndi 1 amaona patari yooooh mumakwana mumatiimilira ndithu ulemu wanu 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Respect the DC
Kodi anyapapi inu mukumukakamiza mayi Chilima kundale chifukwa chiyani mukufuna mudzamubele`compasation yake eti. Zipani zakumabanjazi zikukakamiza mayi Chilima kuzolowera kusiyirana ma udindo achimwene apapansotu akukonzekera kusiyira ana awo chipanichi akukakamira akudikira kuti ana akwane zaka 35.
Tikanena za Kaliati ngati pali umboni okwanira kuti waphwanya malamulo adziko amangidwe chifukwa munthu ukakhala wandale sindiye kuti ali pamwamba pa lamulo ayi.
Anthu atuluka!!!! Ganyu wa lero ali pa lingazi😂😂😂😂😂😂
Tulo silingabwere kweni Ali pa cement. Mpakana kuche. Akweni must be free
Mmmmmm zosakhala bwino
A police ali ndi umboni ogwilika, Patricia Kaliati ndi anzake anakonza chiwembu choti aphe president wa dziko, ndipo pali VN imene Patricia akulankhulamo zoophya. Azinzake a Patricia atamva kuti wamangidwa iwo athawa. Nkhani ili lero tisathe mau tiyeni timve zomwe Kaliati wamangidwila
Mulungu alipo ndipo salora
Choka iwe this is propaganda
Osaperekera umboni zaathu anafa kuchikangaw 9 osalakwa aja bwanj? Imfa ya pilot ija imandipweteka kwambiri,lero ukupangira umboni zoputsa?
Bwanji osatulutsa VN yo kt aMalawi akhulupilire kt amafunad kupha chikangawa...
@@CharityMhone-uk9ym pompano mumva, sizobisatu izi
Ambuye mulowelele mu nyengo imenei kt patricia atuluke ndife olira azimai anzake chachtika ndi chian?
You can't even guess to say who is behind this. A father her daughter is involved in a road accident and is in hospital, who can be the first person to run to the hospital to see her? Imwee, manganya alikuti?
Ndpo
Michael usi ndiwakupha ,ndiyemwe anapeleke chilima kut aphedwe leromso ndi izi afuna out aphe kaliat kmano sizitheka ndthuuu
Koma iwe chakwela uliko hmmmm manganya iwe usi ai zikomo MULUNGU AKUWONA ZOSEZI M'MALAWI.......
Lero sitigona pokhapokha atimasulire ndipo iwe manganya panyero pako sungawine
Please tingwilane manja tonse a Malawi ndi ena onse tiyeni tiyeni
Ulemu wanu Mr bon kalindo the DC
PALIBE ZA ONE PARTY STATE. MALANKHULIDWE ATHU OGOLANKHULAPO NANGA WOSABADWA KWA MUNTHU WA MZIMU... TISIYE. PALIBE KUMANGIDWA MUNTHU WOSACHIMWA . UCHIMWA KWA INEYO , INUYO SIMUNGANDILANDITSE . OSAPANGA MIRANDU POPANDA MIRANDU. NGATI SITIKUDZIWA IFEYO TISAVUTIKE NDI ZINTHU A MZIPANI IZOZO. ZONYOZANANZI NDICHO VHIFUKWA CHAKE TIMAGONYOZANA MOSANGANIZIRA IZO TIKULANKHULAZI. KUGULITSIDWA KWA MALAWI WINA YEKHA SANGALIGULITSE. KULIMBIKIRA POPANDA MTUNDA .. UMADZINYUMWA... AZAKO ATAKUSIYA MMALELE. TIYENI TIBVETSERE MWA CHIDWI IZO ACHIMWA A MAI ..KWENI KALIYATI. INUNSO MUNGAGWE MOMO.. Ati vhifukwa cha Democrancy... Ai Ai ... Need to be responsible citizens of Malawi Nation 🇲🇼💺🎓
Manganya wapereka kaliati, machende aku usi
Wasangalala tsopano iweyo Michael usi chitsiru cha munthu garu iweyo Michael usi munthu wakupha iweyo
Ndipo chakwera iwe ulibe zelu mpaka kufika pompo ndi manganha
Iweyo kalindo ndiwe ndani kape weniweni iwe amalawi sitikuona cholakwika Ife sitituluka
Your brain something wrong
Let love lead Lord have mercy
😂😂😂Koma akalindo ine paka ndukanika kugona kimangotseka paka apule chisapato chachithali ngati mulamba ine ndilimbuyo mwanumo vote ya ine dpp batsi ndimava kukoma mukamawuza chilungamo agalu amenewa ndipo ndiye afika ponyatsa kwambili
The DC anakoza ndipo live wokupanga chipogwe ndinasi wako or wodya naye Mbale imodzi km MULUNGU simwana
Born kalindo umanena ngakhale chilima mumamuudza inu amanganya nyini yamanu plus yr boss
Akalindo ndmamva kukoma mzoyankhula zanu koma zomkakamiza mary chilima kt ayendetse chipani izo ayi munthu analuza mwamuna wake chifukwa cha ndale nde mphamvu yopitiliza kupanga ndalezo azitenga kt...izo ayi zitsiyen
Kodi andale akaswa lamulo asamamangidwe?
Kodi Mary Chilima Ali kuti?anthu ayambila kumuuza kuti abwere atenge chipani kapena akulangizidwa ndi anthu ogulidwa?musafike pokuganizilaniso zosayenela amai,zukani.
MCP manyazi mulibe .mwapha chilima panoso mukufunaso kupha kaliati?
Kongolesi yayaka moto....ngati mmene inayakira 1991/92 kumalipilitsa card azimai amimba..... nthawi yatha pakilani!
Ino ndi thawi amalawi tidzuke tsopano
Koma 2025 tikuwachotsa mavoti Ali Mwa anthu akulu amenewa atikwana kwambili
Kamanganya chaka chino ndekakutizunguza mitu anthufe wapha chilima pompano..anthu akadali ndi mafutso osayanhidwa lero akupereka kaliati mmmma ka satana aka😮😮😮
Sitikufuna mau anu koma chimene a police anene chimene a mmangira. Tidziwe choonadi chifukwa palibe Ali pa mwambapa pa lamulo.
Za ziii mmalo mokafuna chakudya cha ana
Anu bizy kukapanga sungar wa wina aaa za ukape
Inu kupanda umuthu kukulakhulitsani kumeneko
Mapwala Akonso pati
Manganya machede ake mbudzi yamuthu sangakhale president wa utm galu wachabe iwe
Iwe amene akunyoza mr DC kanyere
Ubwinoo wake munkatiuza tivotere MCP, ndipo tinaivotera ndipo tiivoteranso.
Mcp ndichipani choyipa kwambiri zowona mukumanga akweni amene anakumenyerani kampeni kuti milomo yanuyo iziwoneka ngati aswiswiri anthu inu mutimpha tose mumalawi muno
ukati tiyeni ku 18 tikatani mbuli yachabe chabe lwe unali muselo ndani adamema anthu kuti tiyeni tiyambe kutukwana ngat mwana
Enemy within ndi ka Manganya nkhavumbwa ukongwa
MCP ndi ufiti weniweni. Cholinga cha MCP ndikufufuta UTM chifukwa UTM ili my genZ koma MCP ili mu gen D=death.
UMAKWANA KALINDO MWANA OOSYA KWAMBILI
Mai chilima pls tamvan muliko
Phuma lo. Vote at tufuna change ndimeneyo osalila tikhaula sitinati
The DC mwana oopysa kwambiri kkkkk makwana
Manganya tsanachenjere bwino
Tigonabwanji atimangira mayathu?😂😂
Odya chitedze pitani ku lingadzi ife tupita kokasaka ufa
Boma ili eeeee latikwana mawa tili komweko MCP muva manyi agalu inu
Uyuyu sakufunikira ku UTM achoke Michael usi sitikumufuna ku UTM
Kodi bas Tabwereradi Ku one party???
Kkkk mulungu wake uti a DC adakuuzaniyo kkkk
Nthawi ndi kachitsilu lets wait
Komaso iye nayeso mayi chilima osamva mose muja sangazukeko zona
DC ndodo ija ikufunika sopano musachedwe
Zuwonesa kuti Maganya is an enemy from within.
Boma ilili nde ndi paMtumbo pa bomatu
Sitinagone kaliati amatiyimilira ku UTM
UDF Ndi Manganya asapite kumeneko
Manganya NDI MCP zatikwana
Tikapuma kumanda ngati kuli kopuma
Manganya simunthu
Mavuto amenewa tikakhale bzy ku police chosecho azathuwo loko Ali police za kudya ndi mbweeee pomwe ife loko tili kunja koma kuchita kusowa ya bonya za ziiii
Tauzeni akafune mafuta uko ndi za imfa ya chilima ilipati
Mr, DC ❤❤❤❤❤❤❤❤🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉
Go to any country anthu akapalamula amazengedwa mlandu basi. Kkkkkk amene atuluke kupita Ku police alibe zochita
Inunso nyopanu palibe chomwe mukudziwa tadzingotuwani kwanuko mboli yanu
Umangoziwilatu kut ndi chikangawa uyu
Ukudyatu iweyo ife tipita ,Tampa ndi mcp
Enemy from within ithyoke ithyoke pano ndipa home
Komatu mcp yalakwisa apa
Manganya ndi yudasi
I respect u the dc
Mr, usi Simunthu🚨🚨🚨🚨🚨
Kuli ziiii manganya or kuonekela
Tonse tili maso tifike pano timvele limodzi za DC
The DC munanenadi ndakumbukila
Vuto ndife a Malawi serious
Bon Kalindo bodza sutopa nalo mmmmm
Kma anthu DC timakonda
Chikangawa ituluka, sinathe
Apanga upo ndi manganya osati wina ayi
Tikumana mawa Koko mcp mwaonjeza