Boma Bola Libwelele Ku UDF kusiyana Ndi DPP - Mr Abdull
ฝัง
- เผยแพร่เมื่อ 24 ก.ย. 2024
- On Nyasa VoiceBox, Mr. Abdull states that if Malawians decide to change the government, it would be better for power to return to the United Democratic Front (UDF) rather than the Democratic Progressive Party (DPP). Tune in to find out why.
Ku Nyasa VoiceBox, a Abdull akuti ngati Amalawi angaganize zosintha boma, kuli bwino mphamvu zibwerere ku United Democratic Front (UDF) osati Democratic Progressive Party (DPP). Yang'anani kuti mudziwe chifukwa chake.
#malawi
Thank you brother Pamauomalizawa zokuza ku gaza chakwera anenebwino
Atupele muluzi my vote ❤❤
Tanenan zoti tive osatite osati tigawikane
Wa chamba iwe Abdul
If we hate Atupele muluzi we lost our direction
Chilungamo ngati madzi ine wa mcp ,
Wabazaiwe naweso walandila etiiiii
Walankhula zomveka koma kongophatikizana ndi mcp mudziwe kuti sitidzakondwa komanso musakhale chete tupere adzuke ngati nthawi ya bingu ija
Atupele mphamvu zachepa mwina akhale vice president wa Peter then azakhala president......2030
Atupele sangawine bwanji akuyitana mcp inu simungawine timaziwa kuti atupele ndi wa mcp amangopanga manyazi chifukwa cha bambo ake ndiye inu musatinyase mutu wanu
Kupusa chani khondo imeneyi mungaikwanise nokha? Mwakhuta eti
Inendi kuyakhapo udf ngati atupele amuzuza adpp ngati awufuna gwilozano addp alole kuti mtsogoleli
Dpp yazuza muluzi yagwilitsa ychito atupere kukhala wapambuyo wa piter panopa ngati akufuma mgwilizano atupele akhale mtsogoleri bas ngati suzitheka palibegwilizano
Kapangeni alayasi ndi mcp inu ndachisilu mukufuna kwapusisa amalawi udf singawine koma apa zawonekela kut inu muli ndi mcp mumuyitana mdani wanu bwanji mukufuna mulowe mboma mungamuyitane amene mukupikisana naye galu iwe usatenge amalawi ngati opusa wamva chitsilu cha munthu