tiyeni timuthamangitse bushiri ndi chifukwa chake peter wamunthalika amamukana kubwera ku Malawi komanso kuyambitsa church chake koma anthu amaona ngati angomuda komanso nonse amene munalandila zolandila zake za bushiri mudziwe kuti zomwe amanena boni kalindo kuti osamango susuka chifukwa choti tikuvuka zina mukulandilazi ndi za asatanic pano azathu aku South Africa anapumatu zangozi bushiri atamuthawitsa chakwela
Ngozi izi osati chifukwa Cha speed Ntanyiwa ayi satanic yakula akufuna mwazi Bushiri nda china Chakwela ndi gulu lawo pamodzi ndi ma Artist achinyamata satanic ndaame akupanga izi
Mulungu wakwiya ndizomwe anachita chakwela pothawa ntchito ya mulungu Sono mawu amati ndizapanga ana chifukwa chakholo ndiye ife tikulangika chifukwa Cha chakwela Malawi amzanga chonde tisavotele chakwela tikatelo mulungu atikhululukila azimulanga yekha ndikusamvera kwake
@@AlinaChauluka kwambiri
Awuzeni anyani aanthu enawa😢😢😢😢😢😢😢😢
Ndipo tikulangikanso chifukwa choti ndife anthu otengeka kwambili. We’re part of the problem and this is the time to make good decisions
@@AlinaChauluka kutengeka Ngati zing'ono aaaa
😭😭😭😭😭😭😭Abuye muyichitire chisoni mizimu ya anthu onse atisiya lero kuzera pa ngozi kuti ikause mutendere osatha🧎♂️🧎♂️Ame
Bushiri, Chakwera ndi nduna zake ndi afiti oopsa kwambiri ulosi wa Grace Chinga ananena kale
Chakwera chikangawa
Mizimu ya anthu aku Zomba iwuse mu mtendere kwathu ku Zomba 😢😢😢😢😢
Our Heavenly Father protect our beautiful Nation Malawi 🇲🇼 in Jesus Name. AMEN
Mmmmm koma ambuye.tichitilen chifundo ana anu tili pamasawuso akulu kwambili😭😭😭😭😭
Zoona ma driver mukumanyanya kuthamangitsa mukudziwa satana akumalowa njila zosiyana siyana
RIP grace chinga khondo ija tikuyiwonad ambuye tichitilen chifundo 😢😢😢😢
God have mercy upon our Nation 🙏🙏
Lord have mercy
So sad
Ambuye atithandize
Abale ngozi zimenezi ndi zamulungu kapena ndi Satana alowererapo ambuye lowereranipo dziko lathu zoona tizitha chocho 😭😭
Chakwela akuziwa bwino zimenezo
Inah lillah wah inah ilaih lajilunah Amen 🙏
Nda chakwera omwera amenewo Apereka sbe komatu eee ayi zikomo
Zoonadi Anthufe titha chifukwa chakwerayo magazi a bushiri sanamalize kupeleka ambuye mutimenyere nkhondoyi pa ife tokha sitingaikwanitsa
😭😭😭😭😭😭
Timufunse bwinobwino wapita ku Germany uja akudziwa po kathu ngozi zimenezi chifukwa chani tikudziwa kuti kunja kuno mulungu alipo koma . Izi zikudabeitsano
Timpephe Allah kuti zikuchitikazi kuti zisachitikeso
Tikupita Ku December N,sembe zipelekedwe ambuye akuendeleni ana anjokainu😢😢😢
MwaiwA kukasungu Abwana
Mmmmm zovuta nditha koma zonse akuziwa ndiambuye
God have mercy on us malawian
Chipani Cha nthukuta ndimwazi komwe wapitako ndikomwe akukanthira msembe wapita kopaga zimenezi chifukwa maulendo ake timadabwa kuti ndiwotani apa zikuwonetsano zomwe akukapanga akukatenga mphavu zakumidima
Koma ngati ndi munthu akupanga zimenezi akanakhululuka 😭😭
Koma abale 😭😭 this is too much
The main problem is poor roads in Malawi
Kwasala chakwera akamabwera kumene aliko naye ndege yake igwe naye afele pompo
Kkkkk anthu atopa alidi ndikhalidwe loyipa
Kkkkk it cannot happen
Chakwera atule pansi udindo anatenga ndalama kwa bushiri kut abweza mwazi
Tikufuna kuno bushiriyo abwelele kuno
@@wizzyamick1696nkaona peter ankadana naye
Chikangawa akupeleka nsembe ndalama zomwe anatengazo ndiye akubweza magazi zovuta sizochokera kwamulungu ayi komano sataniki yalowa mudziko lamalawi chifukwa chachakwera
Makamaka chikangawa akudziwapo kenakake maka kumene wapitako akupeleka msembe ku Italy 🇮🇹 kwa papa
I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa
Paja chakwera Ali kotenga mphavu ku Nice matter tiyembekezere zimenezo tipephere Kwambiri ndipo mosafooka
Eshiiii Koma abale zomvetsa chisoni 😭😭😭😭😭😭😭Ifeso kwathu Kukasungu TA santhe kwapangikaso Ngozi mmawa walero anthu 26 amwalira pompo onse😭😭😭😭
😢
Sorry kwambili
Pepa Rachel, Ambuye akukhuzeni ndi mizimu ya abale iwunse mu mtendere. 😢😢😢
Chamanga chimene mumalandi komaso dzikolo likulamulidwa ndi BOMA lamagazi
Zaonjeza mulungu alowelelepo
Satanic chakwela akufuna magazi,,president wachilowere miliri,,,frede,covid,njala,ngozi,,eee koma amalawi tiona zoopsa
Mulungu akhale ndi onse okhudzidwa. Mulungu achiritse dziko lathu. 😰😰😰
Tikulangidwa chifukwa chazitsogoleri even ana a Israel anakathidwa ndi nthenda tchifukwa cha utchimo wa Davide
pepani mizinu yazibale atuyiwuze mutendele
Mu dziko muno mwalowa mizimu yachabe
Malawi wakana eish tili pamasuzgo yakulu
Mmmmmmmm chimenechi ni chani Malawi walakwa chani tinalakwanji 😂😂😂
tiyeni timuthamangitse bushiri ndi chifukwa chake peter wamunthalika amamukana kubwera ku Malawi komanso kuyambitsa church chake koma anthu amaona ngati angomuda komanso nonse amene munalandila zolandila zake za bushiri mudziwe kuti zomwe amanena boni kalindo kuti osamango susuka chifukwa choti tikuvuka zina mukulandilazi ndi za asatanic pano azathu aku South Africa anapumatu zangozi bushiri atamuthawitsa chakwela
Eish Chikangawa is a big vampire 😠
Mcp ikufuna mamagazi akapereke kumidima
Eeeeeeeeee zosayenda
Mmmmm why malawi!!!! Ambuye tichitileni chifundo
Ngati ngoziyo yochokera kwa Mulungu basi tengani abwinoo mukhale nao tengani oipao avindikireni pansi kulisadabuza dzikoli lipangeni upset mukhale nao abwinoo
Ngozi izi osati chifukwa Cha speed Ntanyiwa ayi satanic yakula akufuna mwazi Bushiri nda china Chakwela ndi gulu lawo pamodzi ndi ma Artist achinyamata satanic ndaame akupanga izi
May the departed rest well in Jesus Christ name
Abwerere ku south Africa atitha
Ndipo ine ndayankhula kale Kuti zinalakwika amuthamangisa Ku Jonz kuja atimaliza 😢😢😢😢😢
Chifukwa timamukana bushiri ku malawi ngati simukudziwa mudziwe kuti bushiri ndiowopwa musatsekeke maso amalawi, olo chakwela akumaelekedwa simukudziwa kodi?? Zimenezo ndizasataniki bushiri wayamba zionetselo zakeno, atanyiwa muzidziwe Zimenezo
simbo yomwe wakagwila chakwera komwe wapita kuja ngat mwaonetsetsa tisamale
May their souls rest in peace, Jesus comfort the families please.
iwe waymba kunama et ku Zomba kuli 8mls???
Koma kumalawi zikukhala bwanji
Malawi tiyeni tisale kudya Mulungu ndiwazisomo
Ndikugwilizana nazo , prayers needed in Malawi 😢😢😢
Zowonadi ndithudi simukunama ndazikonda kwambili
Ndipo zoonadi tikuyenera kupemphera ambuye atichitile chifundo ndithu
😢😢😢zovuta kwabass sorry
Zomvesa chisoni dziko rathu zonsezi koma ndi chakwera amene akupangisa zonsezi
President asatulukeso kunja , nsembe
At wanjinga
Mwachuluka a satanic ku Malawi
Zomvesa chisoni
😢
Chakwera atitha ndithu
RlP 😭😭😭😭😭🙏🙏🙏🙏
Mmmm
Koma yaaaa
😭😭😭😭😭😭😭😭😭
😭😭😭😭😭
😭😭😭😭😭