Ndalama zikusowa mmabanki chifukwa cha Chakwera." Dr Dalitso Kabambe, Former Reserve Bank Governor

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 12 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 97

  • @JubulaniRICHARD
    @JubulaniRICHARD 5 หลายเดือนก่อน +2

    Moto kubuuuu Dr kabambe muliphule dziko lili pa moto god bls u

  • @mercynavaka8489
    @mercynavaka8489 2 ปีที่แล้ว +5

    Dr Kabambe, is the great man..may God bless him

  • @chippiephiri4505
    @chippiephiri4505 2 ปีที่แล้ว +9

    I like the way he analysis the issue

  • @dreetosh8502
    @dreetosh8502 2 ปีที่แล้ว +3

    Dr D, freedom fighter, we need best Malawi

  • @mishhillinvestment1672
    @mishhillinvestment1672 2 ปีที่แล้ว +4

    Nice explanation koma unali konko you did not think this wise..... killing Malawi for your fame, shame to our educated machines.

  • @wydonmsongole8697
    @wydonmsongole8697 ปีที่แล้ว +1

    This guy is intelligent...DPP got brilliant economist ❤

  • @marthansaliwa7732
    @marthansaliwa7732 2 ปีที่แล้ว +5

    Nonsenu mbava zokha zokha palibe wabwino. Musaononge mawu Chauta akuonongani nonse. Inu ngati mumayendetsa bwino Malawiyu bwenzi titaona zabwino zambiri. Enawa ndiye a alowa ndi njala kudzakokotamo zonse. Malawi akufunika mamasulidwe a uzimu wadzadza ndi ziwanda

    • @giftgannet6871
      @giftgannet6871 2 ปีที่แล้ว +2

      Sikut sangabe ai koma kabedwe kake mpaka anthu kuyenda maliseche panthunda esh mcp ndi mbatata zeni zeni

  • @felaxnambazo1058
    @felaxnambazo1058 2 ปีที่แล้ว +4

    Chakwela anazolowela kuvina nyau kwao kwa malembo pamene chilima Wakulila tchile kusaka nyama ku tcheu sangakwanitse kuyendetsa Boma

    • @tingo3155
      @tingo3155 2 ปีที่แล้ว

      We need a town monger to run a state

  • @chelseajackson3200
    @chelseajackson3200 2 ปีที่แล้ว +3

    I would vote this person into govt but not with DPP!

    • @tingo3155
      @tingo3155 2 ปีที่แล้ว

      This man has a vision 'cos of his education

  • @johnstonechipeta8277
    @johnstonechipeta8277 2 ปีที่แล้ว +3

    This guy is brilliant " l wish kuti anthu amupase mpata wolamula zikoli🙏

    • @ibrahimwaka3916
      @ibrahimwaka3916 3 หลายเดือนก่อน

      Zapakamwa.Kungo peza mpando zimayiwarika.Amangofuna podyerera

  • @akilainter10ment
    @akilainter10ment 2 ปีที่แล้ว +1

    Dr Kabambe, come and teach me economics plzzzzz

  • @hguytigfjujufigfj2069
    @hguytigfjujufigfj2069 2 ปีที่แล้ว +1

    Kubambe politician and economic moto kuti buuu chakwera kuti fwaaa

  • @nditumenichagunda4192
    @nditumenichagunda4192 ปีที่แล้ว

    U deserve my vote wakumulanjeyu akumachezaso ndi makapewa ndiye ndamutaya

  • @ibrahimwaka3916
    @ibrahimwaka3916 ปีที่แล้ว +1

    Problem with democracy is everyone wants to be leader.Everyone has solutions to the problems but you vote them in they are clueless. They start doing they own ways

    • @jazielbenford5881
      @jazielbenford5881 3 หลายเดือนก่อน

      😊😊😊😊❤😊😊😊😊😊

  • @kamwazabonomali825
    @kamwazabonomali825 2 ปีที่แล้ว +3

    Reminds me of Bingu. This guy knows his story.

  • @stephenmondlane7844
    @stephenmondlane7844 2 ปีที่แล้ว +1

    A chakwela walephela kuyendetsa bom. Steven from mozambique

  • @RaymondKaumba
    @RaymondKaumba 4 หลายเดือนก่อน

    Just like Monday coaches
    What did you do when you were in govt

  • @princekabvina1718
    @princekabvina1718 2 ปีที่แล้ว

    The wise man!!!respect...

  • @wisdomchilanga723
    @wisdomchilanga723 หลายเดือนก่อน

    No fear tell them truth how the dragon 🐲 swallow all the money

  • @bobkenneth2947
    @bobkenneth2947 2 ปีที่แล้ว +2

    Chakwera ndi Chilima please stop playing games please

  • @charlessulumba2521
    @charlessulumba2521 2 ปีที่แล้ว

    Great wisdom and speech, but trust ya aMalawi inathawa on politicians, becoz you change within seconds. Kukuvoteran basi ma adviser mbwee opanda nzeru, without economic backbone and expected services to poor Malawians. But anyway, may God intervene pa zochitika pa mpando umeneu.

  • @mulanjehydro6684
    @mulanjehydro6684 9 หลายเดือนก่อน

    Thats true mr Kabambe zinazi ndi mbudzi zawononga dziko lokoma lija

  • @roychirombo1081
    @roychirombo1081 2 ปีที่แล้ว

    Wise and great munthu oganiza boh amanenedwa uyuyu osati apuludzuwa

  • @HendersonGonnessph-px1rb
    @HendersonGonnessph-px1rb 3 หลายเดือนก่อน

    Am waiting your book about your experience and economics please

  • @leonardjika2100
    @leonardjika2100 2 ปีที่แล้ว

    A NEW VERSION WILL GOVERN OUR LAND DON'T TELL ME WHAT TO DO I KNOW MYSELF HOW TO GOVERN A MY PEOPLE I KNOW HOW A SUCCESSFUL NATION SHOULD BE AND I WILL BE SUCCESSFUL SO HELP ME GOD

  • @JuvenileDebwe-bv8ow
    @JuvenileDebwe-bv8ow หลายเดือนก่อน

    kuti mavuto athe amafunika yemwe akudziwa vutolo this man may be capable sure

  • @jbchidothi7166
    @jbchidothi7166 2 ปีที่แล้ว +3

    That's voice of the failures just accept

  • @amosnyirenda5712
    @amosnyirenda5712 2 ปีที่แล้ว

    for this reason my interest is to know you Dr kabambe

  • @ryankabambe3298
    @ryankabambe3298 2 ปีที่แล้ว +1

    👏🏽👏🏽👏🏽👏🏽

  • @EmanuelMwanza-ko7tm
    @EmanuelMwanza-ko7tm 2 หลายเดือนก่อน

    President wakhala wovina nyau angakhale ndi nzeru that's why boma likumuvuta

  • @ramseychozale9526
    @ramseychozale9526 10 หลายเดือนก่อน

    True economy can't develop

  • @aubreywallo1987
    @aubreywallo1987 2 ปีที่แล้ว +1

    Kodi momwe munali pa mpando ku Bank kuja zonse zimayenda bwino?

    • @GiftJulius-gx2kb
      @GiftJulius-gx2kb 9 หลายเดือนก่อน

      Understand akuti anali just gorvener of reserv bank.nayenso amayendela malamulo a presdent

  • @samuelsergio5343
    @samuelsergio5343 ปีที่แล้ว

    Mwalakhula zovekatu

  • @susantembo2076
    @susantembo2076 ปีที่แล้ว

    Inde limbikirani blaming the president for everything so you can win in 2025.

  • @CHARLESJUNIORMPHELANJIRU
    @CHARLESJUNIORMPHELANJIRU ปีที่แล้ว

    This is best

  • @MonicaThocco
    @MonicaThocco 9 หลายเดือนก่อน

    Akulu akulu musamvutike zomalira kuti ndalama zikuchotsedwa ku bank ,komanso ndalama yagwa,nkhani yake ndi yakuti pali chinsinsi ndi ichi, akufuna ibwere ndalama yomwe imanenedwa ija ,kuti we are going to use one money,ziyambira ku Malawiko, ndalama zomwe zikubwera ku chokera kuja zikupita kuti ? 1, 2 achotsa ndalama ku bank ,cholinga chawo ndi chiyani? Pali chinsinsi chowopsya pamenepo chomwe chikuchitika

  • @alexnyirenda123
    @alexnyirenda123 2 ปีที่แล้ว +4

    Just keep quiet my friend,,,

  • @user-zn5xh1ki5e
    @user-zn5xh1ki5e หลายเดือนก่อน

    Making sense

  • @AminAbbasi-xc4qk
    @AminAbbasi-xc4qk หลายเดือนก่อน

    🎉🎉🎉🎉🎉🎉✊✊✊

  • @lifnetmakoka2175
    @lifnetmakoka2175 ปีที่แล้ว

    nzeru izi mukalowa mboma zimapita kuti? politicians please please mumalamulira anthu osati nyama consider the welfare of poor malawians, muzikhalako ndi umuthu.

  • @abisalomchunga6695
    @abisalomchunga6695 2 ปีที่แล้ว

    I like u Mrs man

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 ปีที่แล้ว

    Mukango khuta madeya mukuganiiza kuyamba za ndale cholinga mukakhala pampando muziba mulemere Mapwara ambwiyanu agalu osauka inu,mitu ngati zitanga sala zosungiramo anamapingo ndikazango bwerera ku malawiko tisaza kumane pazalewa iyai wina ndiza Mu ponda

  • @henlyyassin1718
    @henlyyassin1718 2 ปีที่แล้ว +1

    Mukanika kupanga produce ma companies ndalama mugula ma expensive houses and cars for your own. Ndalama mukuba Malawi is wise now, useless

  • @meesailikeyougirlmoosa9801
    @meesailikeyougirlmoosa9801 ปีที่แล้ว

    Mmakwana boss posaeopa kutulutsa mau owonawa

  • @chiefmalindi4070
    @chiefmalindi4070 2 ปีที่แล้ว +2

    Zofunika okumwa ink izi osati chifukwa amalima bwino fodya kumunda kwanga

  • @maxwellchikwanjembaya4596
    @maxwellchikwanjembaya4596 2 ปีที่แล้ว

    Malawi 🇲🇼,,,,,,,,.....,,,,,,,,,

  • @Benty_Pro
    @Benty_Pro ปีที่แล้ว

    Dolo Kwambiri

  • @ibrahimjackson-cg6tc
    @ibrahimjackson-cg6tc 10 หลายเดือนก่อน

    Mumatha abwana

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 26 วันที่ผ่านมา

    Awa ndi amunawa kwambili

  • @anoldkapolo4493
    @anoldkapolo4493 ปีที่แล้ว

    AKabambe mudalikuti apamukunamiza anthu lero? Osangonena kt mwayamba kubwebweta popeza pam'phika adakusamutsaponi? Ife ndi Chakwera 2030 wooolh

  • @johanessphili-ano788
    @johanessphili-ano788 2 ปีที่แล้ว

    Mwazidziwa liti izi a Kabambe

  • @RabsonMatope
    @RabsonMatope 20 วันที่ผ่านมา

    Anthu anzeru alipo

  • @rabsterkamoto8953
    @rabsterkamoto8953 2 ปีที่แล้ว +2

    Yah ichi nde chilungamo

  • @jafarisani
    @jafarisani ปีที่แล้ว

    Zinthu zinali bwino bwino koma tinagomera ndale, umbuli plus kupupuluma lero ndizi

  • @abduljafari6577
    @abduljafari6577 2 ปีที่แล้ว +2

    Agalu amkaona ngati kuyendesa boma kobwheka

  • @xevierharrykamiza3577
    @xevierharrykamiza3577 ปีที่แล้ว

    Then why u didn't put this energy when u were within the system

  • @thondoyaenterprise3795
    @thondoyaenterprise3795 ปีที่แล้ว

    Naked truth

  • @user-ky4ce9gb6j
    @user-ky4ce9gb6j หลายเดือนก่อน

    Dolo kwambiri uyu

  • @harrisonmwanga9812
    @harrisonmwanga9812 2 ปีที่แล้ว

    Munthu ofunika koma ku DPP ndiye mbola bola angoyambisa chake chifukwa ngati ali wa DPP angofana ndi chilima kapena Peter ku dpp

  • @kondwamlungu8384
    @kondwamlungu8384 ปีที่แล้ว

    Chiuta akutumbike nasetamanya apo pafuma suzyo

  • @jameskadete2196
    @jameskadete2196 ปีที่แล้ว

    Dr ndi ma equasation awo

  • @BonfacePhiri
    @BonfacePhiri 8 หลายเดือนก่อน

    Mukunena zoona bwana

  • @abdulullahkhamiss1236
    @abdulullahkhamiss1236 2 ปีที่แล้ว

    Akuba awa

  • @paulvimbamvula9508
    @paulvimbamvula9508 2 ปีที่แล้ว

    Uyuso a Malawi tinakuziwa kale mbiri yako...iyaaaah

  • @dennischikunkhuzeni5805
    @dennischikunkhuzeni5805 2 ปีที่แล้ว +1

    Double speak....

  • @moseselia6582
    @moseselia6582 2 ปีที่แล้ว

    Iweyo unali koko thawi ya peter koma umalandila 20 billion ndiye apa ufuna unene chiyani

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 2 ปีที่แล้ว +1

    Fuso labwino kwambili kuti kodi ma doller wose anawapeza mu boma alikuti?

  • @osamabinraden9391
    @osamabinraden9391 2 ปีที่แล้ว

    👏👏👏👍

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 2 ปีที่แล้ว

    Gbu

  • @frstyhavoc6678
    @frstyhavoc6678 2 ปีที่แล้ว

    Umatha ntchito yako ayise udangobadwira banja lolakwika 😀😀😀😀😀😀

  • @kensonmbewe6692
    @kensonmbewe6692 2 ปีที่แล้ว

    MUMANAMIZA AZUNGU INU KUTI MULI NDI MAKOBIDI AMBIRI

  • @innocentmanyera1861
    @innocentmanyera1861 11 หลายเดือนก่อน

    Machende

  • @jkfodya9997
    @jkfodya9997 ปีที่แล้ว

    Tidaonga vote ndithu

  • @gilbertmategula5613
    @gilbertmategula5613 2 ปีที่แล้ว +1

    Chitsilu cha munthu

  • @moseselia6582
    @moseselia6582 2 ปีที่แล้ว

    Oyamba kuononga dziko ndi ddp ndiye musatisokosele tionana 2025 takudziwa

  • @PaulKwenda
    @PaulKwenda ปีที่แล้ว

    Wakuba iwe galu kwanasi

  • @susantembo2076
    @susantembo2076 ปีที่แล้ว

    Ratios nazo

  • @isilagmaulana9425
    @isilagmaulana9425 ปีที่แล้ว

    Tausani

  • @user-bs1bw7yz5u
    @user-bs1bw7yz5u ปีที่แล้ว

    Àw😢

  • @yaowking4609
    @yaowking4609 ปีที่แล้ว

    Boma.ili ndi laziiiiii

  • @peterkasema9948
    @peterkasema9948 ปีที่แล้ว

    Kodi satta alikuti

  • @frankkamunde4575
    @frankkamunde4575 2 ปีที่แล้ว

    mbava zikuluzikulu kunamizano mtundu wamalawi kufuna mavoti 2025 anthuwa zawo ndizimodzi tinatopa ndimodza ife

  • @isaacthomas4005
    @isaacthomas4005 2 ปีที่แล้ว

    Khala chete iwe Dalitso suja unatibela ndalama nthawi yako ija ku Reserve Bank pamene unkadzilandiritsa K30 000 000 pamwezi. Sitinaiwale. Komaso unachita manufacture accounting yako kuti upeze ngongole kuIMF kuchitira kuti iwe ndizitsiru zinzako zakuDPP mupezeko kangachepe. Iweyo uli part of Malawi's problems sungatipatse ansala

  • @gabrieljulius6151
    @gabrieljulius6151 2 ปีที่แล้ว

    Sono akafusidwa akuyankha
    Akut ayi umboni ndi uyu

  • @victorchikuse9837
    @victorchikuse9837 2 ปีที่แล้ว

    Useless voice you were there kmano nothing you did ndie apa mukuoneka ngati wanzeru poti uli kunja kwa office, mnthawi ya Peter muthalika kwacha inagwa kangati? Kod chi nyengo chimene zonnet sattar amapanga ndi boma anayamba liti?