KU MPOTO KWACHITIKA ZINTHU ZOKHUDZA PRESIDENT NDIPO PHALOMBE BOYS IKUZUKUTA MOZAMA

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 10 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 111

  • @user-ww4ei5fb7d
    @user-ww4ei5fb7d หลายเดือนก่อน +9

    Kulibe asirikari ndi nduna yachitetezo ku malawi. I wish minister wa chitetezo adakamakhala msirikari

    • @chippakaribafox2865
      @chippakaribafox2865 หลายเดือนก่อน +1

      Thats true....the minister not fit all for such position with no security skills at all

    • @wistonkamatenda
      @wistonkamatenda 22 วันที่ผ่านมา

      Zill good ndi malae❤❤❤❤❤❤

  • @MonicaBvumbwe
    @MonicaBvumbwe หลายเดือนก่อน +7

    Asilikali akumalawi amafasa kwambiri kuiwala kt. TChito yawo ndikuteteza ndikuyang'anila ziko lino kma amangoyang'anila zithu zikuwonongeka😢

    • @CatherineDesire
      @CatherineDesire หลายเดือนก่อน +2

      Sikufatsa Koma kumbwambwana komaso manthongo mu brain

    • @CatherineDesire
      @CatherineDesire หลายเดือนก่อน +1

      😒😔anangokomokeranji anakangopitilatu ka anakaferatu👹👿😈akanakamuona Chilima

  • @Dalitsombewe-f9l
    @Dalitsombewe-f9l หลายเดือนก่อน +3

    Pitiriza Phalombe boy.that's true and 100%

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire หลายเดือนก่อน +3

    Kulibe chimene MC P ikudziwa koma kupha kokha basi100 percent perfect palibeso owapotsa

  • @MonijaKataika
    @MonijaKataika หลายเดือนก่อน +2

    💯 mwana mulomwe mwamulapulamotu...😭 Uyu atenge u VP now till 2025. APM my vote.

  • @joyahmedjoma4615
    @joyahmedjoma4615 หลายเดือนก่อน +5

    Kma asilikali a Malawi anasaduka azilonda a chikangawa naga akuti chasika kapena chakwera aaaaaaaa ine guys ai

  • @user-di8hq3dl9o
    @user-di8hq3dl9o หลายเดือนก่อน +4

    Keep it up

  • @joyahmedjoma4615
    @joyahmedjoma4615 หลายเดือนก่อน +4

    Ben longwe machende ake tikamudzimitsa ife meneyo siyeni ndalama alandiradzo akadyera kumanda ndipo 2025 ku wina or wosa wina basi sitizalora kuti atiramule ife

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg หลายเดือนก่อน +4

    Ben longwe ochinda Mwana wake chimwendo Banda mphuno Ngati tomato

    • @SamKaposa-i5c
      @SamKaposa-i5c หลายเดือนก่อน +1

      😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023 หลายเดือนก่อน +6

    Pitilizani kutiuza alomwe azathue

  • @FrankKaufa
    @FrankKaufa หลายเดือนก่อน +3

    Amen m'bale

  • @EdwardZuze-r7w
    @EdwardZuze-r7w หลายเดือนก่อน +2

    Asilikali a MDF, sakulikonda dziko lawo, they are few solders amene ali ndi umunthu.
    A silikali, Ulemu wanu ndi mphamvu zanu zili kuti? musakomedwe ndi zosala kuleka kutetedza dziko la

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 หลายเดือนก่อน +2

    Asilikali anthu saziwa ntchito yawo chomwe amadziwa ndi kulondera ku state house basi. Ma guard bolanso a G4 amadziwa chochita koma MDF panja peni peni.

  • @MussaNgoma-r2k
    @MussaNgoma-r2k 22 วันที่ผ่านมา

    He was not foreverdeath😊 will be there for ever

  • @AshimayeGama
    @AshimayeGama หลายเดือนก่อน +2

    Chilima dzofuna bodza osati mcp ayi chilima chilima ndamene anabweletsa mavuto kuno kumalawo kuno ifetikutu dpp moto 2025boma

    • @user-uk3bz1hr5t
      @user-uk3bz1hr5t หลายเดือนก่อน +1

      Anachita kutitengerako yekha chilima ku MCP ndthu aaaa,,,popanda iye sitikanakhara pano tukamba za MCp konse mmm

  • @sthoramexjrsa902
    @sthoramexjrsa902 หลายเดือนก่อน +2

    Your big man 💪💪💪

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 หลายเดือนก่อน +3

    Aziwona achikangawa mizimu ya anthu 9 yiwasaka mupaka yiwakathe amenewo aziwona

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b หลายเดือนก่อน +2

    Asilikani nawonso akudya nawo ndlama za boma akuwopa kuchita po kanthu

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j หลายเดือนก่อน +3

    Koma zooona anthu ena ukalowa mmbalacks mpakana ukapha Anthu, aaaaa zooona asilikali mwatidabwitsadi .
    Asilikali alibe chipani koma apapa ndiye yai sipali bwino

    • @user-ww4ei5fb7d
      @user-ww4ei5fb7d หลายเดือนก่อน +1

      Asirikari onse ndi a MCP

    • @LovenessMagombo-t3c
      @LovenessMagombo-t3c 25 วันที่ผ่านมา

      Zoopsatu, ngati achiwembu akulowa kuzida komweko mpaka kupha munthu, mmmmm

  • @DevisonHala
    @DevisonHala หลายเดือนก่อน +2

    Asilikali amalawi adalowa ndale osati kuteteza dziko chilima amaphedwa iwo amawonera zikuchitika bwanji?

  • @joyahmedjoma4615
    @joyahmedjoma4615 หลายเดือนก่อน +2

    Apite ameneyo basi sitikumufuna chikangawa iwe watitopetsa ndipo ndikuona kuchedwa pa 8 tinthane nazo ife zimenezi isa

  • @Itemsworld
    @Itemsworld 28 วันที่ผ่านมา

    May God help Malawi, tears of the sun over Malawi

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y หลายเดือนก่อน +1

    Good man❤ Zoona

  • @Dinalamakanjira
    @Dinalamakanjira หลายเดือนก่อน +3

    Nzimu WA Achilima ndi Agadama

  • @SlindiryLoveness
    @SlindiryLoveness หลายเดือนก่อน +1

    Koma aromwe simugona turo ndiboma koma mukunamatu chakwera satuluka pampando boma la peter laromwe lokhalokha kodi malubino aja munalikupha anali mcp agalu inu zaziii utiwuza chani galu iwe

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole หลายเดือนก่อน +1

    Mwayankhula bwino braz zaonjeza kwambiri.

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i หลายเดือนก่อน +1

    No matter what chakwela ngwakumpha anampha amiya wamphaso SKC pamozi ndi abaleathu 8

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu หลายเดือนก่อน +1

    Kodi ife a malawi sitingathe kumupha chakwela yu, kodi ifeyo mene tilili mumalawi muno tikhulephela kumupha chilima yu, ine akundinyasatu chakwela koopysa , abale tiyeni tipange madhemo omupha chakwela asatizuze ife ayi , tatopa jonh longwe yo abwele tionetsane monga ine mwana wapa balaka longwe ndikufuna koopysa kwambili

  • @BeckhamDavid-v6c
    @BeckhamDavid-v6c หลายเดือนก่อน +1

    Jyce banda simunthu ameneuja wakhala akupha anthu maulamulilo wako uja pano aliwone ndi ndakwela okupha okha okha

  • @lyiemax
    @lyiemax หลายเดือนก่อน

    Powerful speech

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d หลายเดือนก่อน +1

    Musiyeni peter muthalika salimbana ndi chonde mudzatenga tsoka ndithu

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d หลายเดือนก่อน +1

    Mulungu atichitile chifundo dziko la Malawi

  • @GoodluckVithumbiko
    @GoodluckVithumbiko หลายเดือนก่อน +1

    yavuta ndindarama asondawo akuyendera ndarama amenewo chisiru chopusa

  • @ElizabethNkhonjera
    @ElizabethNkhonjera หลายเดือนก่อน +1

    #Malawi Difence Force

  • @SlindiryLoveness
    @SlindiryLoveness หลายเดือนก่อน +1

    Mbuzi yamunthu iwe saulos wamukonda kamba koti wamwalira ndiboza lako ukhaula udya ulomwe wako womwewo ukhaula ukuwonaso azipani zakozo akuthawaso akulowa mu mcp chifukwa chani ndiye 2025 uzafa ndi bp mulomwe wopanda khalidwe iwe azako aromwe panopa akuzindikira wanakomoka kutiko chakwera ndimaboza akowo mbuzi yamunthu iwe

    • @OdettaLowrence
      @OdettaLowrence 12 วันที่ผ่านมา

      Uli mbali iti iweo?

  • @GoodluckVithumbiko
    @GoodluckVithumbiko หลายเดือนก่อน +1

    iwowo akusangarara kuti anthu akurowa mcp akukafunako ndarama zo zabooka 😂😂

  • @GoodluckVithumbiko
    @GoodluckVithumbiko หลายเดือนก่อน +1

    zimastanic izizi zimangokharira magazi

  • @GoodluckVithumbiko
    @GoodluckVithumbiko หลายเดือนก่อน +1

    koma tigwirane m'manja ambuye atisogorere

  • @IssaLazack-ij1gf
    @IssaLazack-ij1gf หลายเดือนก่อน +1

    Koma chona chili mutima mwanumo mukuchiziwa chifukwa chimene mukwyila amenewa ndichani yiwenso ndiwe mfiti mumadya nyama yawanthu ndichikhangawa wanuyo wakhutha yee

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn
    @AlexManuelMisomali-sv1vn หลายเดือนก่อน +6

    2025 saafika ? 😂😂😂😂 Poti okupha ndi lupanga amati adzafanso ndi lupanga

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp หลายเดือนก่อน +1

    Ulemu wanu big boy umata man

  • @HassanTmasuku
    @HassanTmasuku หลายเดือนก่อน +1

    Asilikali opusa awa ntchito kumenya ma civilian asilikali analipo padzana achina chigawa ndi anzawo osati awa

  • @jameskachulu8141
    @jameskachulu8141 หลายเดือนก่อน +1

    Bola akadafa tigawane chuma a malawi

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q หลายเดือนก่อน +1

    😂😂😂😂😂😂 chakwera magazi kuribe kusi kwanyanja ukufunaso ena

  • @AlexKamowa-u7m
    @AlexKamowa-u7m หลายเดือนก่อน +1

    Kulankhula momveka bwino saowebas

  • @charlesmasauko4651
    @charlesmasauko4651 หลายเดือนก่อน +1

    Asilikali a Malawi ndi Ogona

  • @DevisonHala
    @DevisonHala หลายเดือนก่อน +1

    Asilikali amalawi akuphana wokhawokha chifukwa akulandila ndalama kwachakwera

  • @Randy-er2xo
    @Randy-er2xo หลายเดือนก่อน +1

    Pwiyapwiya mumaitha auzeni

  • @CharlesPhiri-ds1rk
    @CharlesPhiri-ds1rk หลายเดือนก่อน +1

    Ndye ife tizinva kutukwanako? Ngat mulibe fundo musileni kalindo bwanji?

  • @mbelengamavuto2517
    @mbelengamavuto2517 หลายเดือนก่อน +1

    Nkhani ndiyoona ndalama zabooka ndichifukwa anthu akukhamukilako

  • @MphatsoPemba
    @MphatsoPemba หลายเดือนก่อน +1

    Kwapula phalombe tsiku Lina tikanyele pakhomo pakwawo

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg หลายเดือนก่อน +1

    😂😂😂😂😂😂asilikari ake okonda sex

  • @OdettaLowrence
    @OdettaLowrence 12 วันที่ผ่านมา

    Usilikali pano walowa ndale , ndalama basi zisilu za asilikali za relo, ndipo ndie akundinyatsa bwino, Malo moti mademo akuchitikawa asilikali bwenzi Ali PA number one kma kuli zillll, Malo moti amuchose alamulire kwa salaku kma ayi, apa Nila manja mphechempheche zisilu

  • @Eric-gb9ms
    @Eric-gb9ms หลายเดือนก่อน +1

    Vuto nd wamkulu wa asilikali anadya chibanzi that's why mulibe chitetedzo mu dziko lanthu

  • @AjibuTwalibu
    @AjibuTwalibu หลายเดือนก่อน +1

    Mmm mpakana kukomoka

  • @wistonkamatenda
    @wistonkamatenda 22 วันที่ผ่านมา

    Ngoz ndi ngoz basss cilungam akudziwa ndi mulungu

  • @McfalenGola
    @McfalenGola หลายเดือนก่อน +1

    AFA nayenso chikangawa

  • @user-mi3ot6ms8x
    @user-mi3ot6ms8x หลายเดือนก่อน +7

    Asilikali tilibe ku malawi

    • @AlexManuelMisomali-sv1vn
      @AlexManuelMisomali-sv1vn หลายเดือนก่อน +2

      Ndizodabwitsa kwambiri kuti police ya Malawi, Army yaku Malawi, ati makhothi ndi mabungwe aja amati ndiomilira anthu aja onsewo angoti ziiii koma akulandira ndalama ndima allowance nthawi zonse, pamene anthu osalakwa omwe saadavotere Chakwera ndi anzake akuzunzika kwambiri, zomvetsa chisoni.

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire หลายเดือนก่อน +1

    Asilikali akomoka chifufu

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg หลายเดือนก่อน +2

    Inu mukunena Joyce Banda hule Amina ake mumawaona bwanji anagona kale achimwene😢😢

  • @GoodluckVithumbiko
    @GoodluckVithumbiko หลายเดือนก่อน +1

    mutu wataya

  • @LindaNkwazi
    @LindaNkwazi หลายเดือนก่อน

    Chikangawa muziona

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire หลายเดือนก่อน +1

    David anagonjetsa Golliat

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r หลายเดือนก่อน +1

    Apita musiyen

  • @ritchardchakuma5725
    @ritchardchakuma5725 หลายเดือนก่อน

    Wabwino zose ifekwathu kwatha😭😭😭

  • @wistonkamatenda
    @wistonkamatenda 22 วันที่ผ่านมา

    Ukusokosa boma koma mcp

  • @GetrudDube
    @GetrudDube หลายเดือนก่อน

    Palibe chinsinsi

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz หลายเดือนก่อน +2

    Sstana joyce banda even bushiri is involved

  • @IanAllstal
    @IanAllstal หลายเดือนก่อน +2

    Mlomwe kuliratu momveka apa Kodi Mukumva bwanji bwana Aliyese akukulozani Zala inu nchifukwa chani muzifuse bwana sure Enaso anazuzulidwa mokwana mapeto ake anapita ganizani bwino

  • @mustaf-q4j
    @mustaf-q4j หลายเดือนก่อน +3

    Asilikali apasidwa ndalama

  • @hagayichiluwe
    @hagayichiluwe หลายเดือนก่อน +1

    Kuteloko uganiza kuti alomwe mungalamule dziko chifukwa chambwelela zakozi? Zaziiiiii

    • @WorriedNdhlovu
      @WorriedNdhlovu หลายเดือนก่อน +2

      Kukula konseko madala koma nzelu mukibe

    • @user-hx6jl2jq9j
      @user-hx6jl2jq9j หลายเดือนก่อน +1

      Ndiye mwakula zinakukanikani kale .
      Ukubwera ndi iti madala

    • @SolomonNjolomole
      @SolomonNjolomole หลายเดือนก่อน +1

      Chokukhalani ndi ufiti basi a mcp kupanda chilima mwaphayu mukadalamulira ndani .

    • @user-eh1mg3ww6d
      @user-eh1mg3ww6d หลายเดือนก่อน +1

      Madala awa ndichocho amaikila kumbuyo MCP asiyeni ikubwela thawi oipa ose azatha phwiti

    • @SamKaposa-i5c
      @SamKaposa-i5c หลายเดือนก่อน +1

      Chikangawa team

  • @MsondaBanda
    @MsondaBanda หลายเดือนก่อน

    No point

  • @KenChitete-pg3ws
    @KenChitete-pg3ws หลายเดือนก่อน

    A MALAWI MBUZI ZOSE ZIKULONGOLOLA PA SOCIAL MEDIA NDI ZIMENE KU SUKULU SIZINAPITE,,,KHALAMBA YANU INAWONONGA ZIKO CHAKWELA ALI PA TCHITO CHACHIKULU KUKHOZA ZITHU ZIMENE KHALAMBA YANU INA ONONGA

    • @bisweckchimphamba8497
      @bisweckchimphamba8497 หลายเดือนก่อน +1

      Pakuti nawenso ndi m'mene walembera apapa zawonetsa kuti school mwa iweyonso mulibe,kulamulira si school Koma umunthu,a school ndi awa akungobawa

    • @SamKaposa-i5c
      @SamKaposa-i5c หลายเดือนก่อน

      Chikangawa team 😂😂

  • @KenChitete-pg3ws
    @KenChitete-pg3ws หลายเดือนก่อน

    PALIBE FUNDO YONVEKA MUTSAWAVUTITSE ATHU KUNVA DZOPANDA MUTU,,, JOYCE BANDA ATANI,,ANAKUUDZA KUTI NDI ASATANIKI NDI NDANI NDEKUTI NAWETSO NDIWE WATSATANIKI.

    • @IssaLazack-ij1gf
      @IssaLazack-ij1gf หลายเดือนก่อน +1

      Mpatumbo Pako Garu wamunthu osaumbaraooo

  • @KenChitete-pg3ws
    @KenChitete-pg3ws หลายเดือนก่อน

    IWE NDIWE MULOMWE CHICHEWA CHAKO SICHIKUNVEKA NGATI WATUMIDWA NDI PETER MUTHALIKA WAWUPONDA IFE SITIKUFUNA ALOMWE KUTI LAMULILA KAWILI IWALANI ZIMENEZO NGATI MUNAZOLOWELA KUDYA ZA MUCHIPANI MWAWUPONDA THAWI YAKWANA YOTI MUNYAMULE KHASU WAKUMUNDA MUZIKALIMA MADIMBA,,, PETER MUTHALIKA OLO AFUNE KAYA ASAFUNE MCP YILAMULILASO KAYA MUYAKHULE CHILIMA MUNGOONA KUTHA MAU ANU MCP NDI BOMMMMA KALE,,ALOMWE TENGANI MAKHASU PITANI KUMUNDA MUDZIKALIMA VUTO LANU SUKULU MUNAKANA NDENO TCHITO YOTI MUGWILE INUYO NDIYAKUMUNDA BASI.

    • @KenChitete-pg3ws
      @KenChitete-pg3ws หลายเดือนก่อน

      KODI PETER MUTHALIKA SANAMANGILE MADEMO AKOMA PATI PETER MUTHALIKA,,NGATI MUDZA VOTA NDINU NOKHA MWAINA MUDZAYITCHOTSA MCP KOMA NGATI ADZAVOTA NDI A MALAWI SANGANVELE FUNDO ZOOLAZO,,,,KODI IWE PETER MUTHALIKA AKUPASANI NDALAMA ZINGATI????MUTHU ALI NDI ZAKA 85 YEARS MUKUFUNAKO CHANI KWA KHALAMBA NGATI YIMENEYO

    • @Yahiya-wm8nd
      @Yahiya-wm8nd หลายเดือนก่อน +1

      iwe ukufuna ndani

    • @HappyAbyssinianCat-xt2bm
      @HappyAbyssinianCat-xt2bm หลายเดือนก่อน +1

      Naweso ndwe chisilu ine si mulomwe ndne nchewa km mcp sitikuifuna ife ngat iweyo umadya nao ndalama ndalama boma lakupha ili manja mwao mwazaza magazi chipan chakupha kuba agalu amenewo

    • @user-hx6jl2jq9j
      @user-hx6jl2jq9j หลายเดือนก่อน +1

      Zakuwawa basi zakuwawa ticosa cisoso kapena minga inalasa chilima

    • @Eric-gb9ms
      @Eric-gb9ms หลายเดือนก่อน +1

      Akulu ganizani before you think simumalikonda dziko lanu or muli mu gulu lasatana nanu

  • @JessicaManda-zm1ug
    @JessicaManda-zm1ug หลายเดือนก่อน +1

    Azikayenda ku midzi azikawona anthu mene akuvutikira agugawana onkhaonkha ndi ufiti wawo