munalephera ku wina kwanu kamba ka moyo ngati umenewu wa nsanje. anthu akwanu sanakusankhe kukhala Mp iwe, ukufuna u president koma ulibe mphatso ya utsogoleri iwe.
Kodi conversion amakonza ndi a court kapena achipani komanso crime imeneyi yosapangitsa conversion imatchedwa contempt of court? Why ma administration onse adutsa kumbuyoku asanakakamizidweko ndi court kupita ku conversion?
muuzimu wadziwa bwanji iweyo, ntchito ndi chipanu ndizosiyana Mr Ken I think mumango lankhula but you don't know what you mean, now I understand you are good in talking but you don't know what is politics zangochitika kuti muli ndi mwayi okhala nawo pafupi ndi anthu omwe akupanga ndale.
A NEW VERSION WILL GOVERN OUR LAND SO HELP ME GOD GIVE ME THE WAY TO SAVE MY PEOPLE DURING THIS DIFFICULT TIME WHEN MY PEOPLE ARE STRUGGLING THEIR LIFE IS DETERIORATING LIKE A LOCKET SO HELP ME GOD TO SAVE MY PEOPLE
M'dala iwe tamva idzi "
{ 1 } Ndiwe chitsilu kwabasi.
{ 2 } N'kulankhula kwako dzikusonyedzeratu kuti umphawi wakutikita ndiye ukuyesano kuwabakila a Chakwera ndicholinga choti upedzeko Paketi ya Sugar galu iwe..
{ 3 } Kumbali ya mavuto ngati Freddy / Covid ,Idzo nzowonadi kuti it's a natural problem ,.Ndiyeno ntchito ya boma n'kupedza mayankho panthawi yoti mavuto ngati awawa abwera mdziko.
Ndiyenso since Chakwera ADMINISTRATION yakanika kupedza njira dzothanirana ndimavutowa ", Ndiye kutino bomalo lalephera pamenepo .
Zoba ameneyu MCP yamugula
He is two fulish
This lady is truly brilliant!
Ndale sizamwanadi adja . Nsonda is genius
Mumazivutisa pomaitana mdala amenei amayamkhula zosemphana ndi ma fuso always
Dobadoba wa MCP uyu
Nsonda ndimbuzi yeni yeni, ndiwe galu kobasi
Chemwali mukungwila ntchito ndi mcp ndakutulukilani nthawi yapitayi machine interview chisale chifukwa anali wa bodyguard wa peter lero mukuchitaso interview nsonda ai akuonengela ntchito mukanvela anthu that's why anthu amakonda Mr brain Banda alibe mbari
Ndale ndimasewela olikhana, and uyuyu ndiwandaled.
I like sonda, straight talk.
Nsonda chitsiru kusaka pofera
Watching Msonda's interview is not a waste of time at all, anthu awa ndi amene akuyenera kukhala ma presidential advisor.
Yes this great man
Ken Nsonda is a leader and can be a good presidential advisor
@@ancientnkhata1137
Komabe ndi mbava zokha zokha, zipani zonse zandale kumalawi ndi za mbava zokha zokha.
Honestly this lady Leah Zodiak has a gold in their hands
Uyu ndosokoneza
Awa ndiachisilu
Amsonda ndi munthu wabwino
Kwambiri ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Nsonda is a genius
Kkkkkk mbava iyi inu
True servant of dpp
Reyaa mafuso aphavu kwambili keep it up ❤❤
Ok
Akulu akulu wopanda nzeru Ku Malawi
Leah andale akuMalawi ndi amphawi.amalephera kuthetsa umphawi wawo nthawi yomwe ali m'boma.azao akachoka m'boma apita ndikakamapanga ulimi mma farm ndikumatukula dziko.iwo koma kusintha zipani,kumakanirira ntown.agalu kulephera kutukula dziko.anayamba ndi Bakili mpaka pano ndale.
Mafupa Ken msonda ndiwe galu
Vuto Latsonda ndimomwe amachitila ndiosokoneza yemweyi adatsokoneza UDF, DPP , PP again DPP now MCP watch out this fella
Msonda ndi wa MCP ndakhulupilira sopano eti boma la MCP lakumana ndi minyama kkkkkkk
Kkkkkkkkk galu iwe ungakhale pusident machende ako
Iwe Ndiwa mcp
Komaso sindingakuvere iweyo uribe zeru chimene ukuziwa ndi kusokoneza ndiwe chisiru bwanji 😅😅😅😅
Kkkk koma musonda umandivetsa kukoma Peter akanakomokadi siukunama big
Nsonda akufuna awasiye anthu mmavuto...in advance rip nsonda
Nsonda mutu wake suyenda bwino
gogo uyu ndi chitsilu chotheratu mbudzi ya munthu
This man is pure MCP and just causing confusion in DPP
Machende ako iwe nsonda wachule anthuwo ndiwe galu
Ansonda odya zopepha
Riah nd black beauty tu koma Ken nsonda at sikuti muzipopetu 😂
Sister mpapaliseni mafunso galu ameneyo chitsilu chamunthu
Palibepo chazelu inuso azodiaki muzioona ochezanawo kkkkkk
Mbuzi ya munthu
Yes brian and leya dinu anthu amamene ife timawafuna kuti muzifunsa mafunso ovuta kwaanthu omwe amati ndioganiza boh ngati amenewa leya uyu ndiye sunamumwese madzi wakumananazo nsonda waziyalusa yekha amaona ngati acheza ndiachina jowabu omangomvela nkhani basi
Ken Nsonda answered all the questions accurately unless you chose to be deaf
Leah Leah Leah how many times did I call ur name tikakhala amfana oshota ifeyo Leah???????
Chonde nose mukutukwananu muziwekuti munthuyu Ali ndi ana and zizukulu chonde Polani Moto ndikutukwana
Nsonda mbudzi chopusa kwambili
Excellency Ken Nsonda 🙏😀
Lea, mukapangako acknowledge compliment yo
munalephera ku wina kwanu kamba ka moyo ngati umenewu wa nsanje. anthu akwanu sanakusankhe kukhala Mp iwe, ukufuna u president koma ulibe mphatso ya utsogoleri iwe.
Nsonda amachokera kuti?
Achikeni nsomba ndimaona ngati ali ndi nzeru koma aaaaaa mbutuma ndichifukwa chake sanakhalepo kansala,mp, even nduna ya mfumu ayi kkkkkkkkkk
Sangawine over my dead body 😂😂😂
mnsonda chilungamo chimawawa at hu akuwabera a muthalika ndizoona
Nsonda ndi wa pp sitingamumvere
Anachenjera mofoila uyu
Msonda zelu ulibe iwe ukuzikolakola wekha unena kt boma likuyenda bwino zoona galu iwe
Msonda ndiopanda boza andale ena sangamukonde cz andale amakhulupirila kunama big up msonda
Mr msonda, kumpoto kulibe munthu akukufunani inu mutsanamize anthu apa, anthu angafune munthu oduka mutu ngati inu, inu zeru mlibetu, komaso anthu akudziwa kuti munalowa mcp. Amalawi uyu musamvere ndimunthu osokoneza kwambiri madala opanda nzeru uyu.
Tikumufuna
awa ayambe chawo chipani namkumwa dausi ajefry ndi smsonda kapena back to mcpp
Dyera awa
Kukalamba yet alibezopanga
Akunama galuyu magazi ake azilemba Hiv postive
😂😂😂😂 Nsonda ndi Drama..usazafe aise
😂😂😂😂😂
Wamisala uyu, osamuvera akufuna kungosokoneza chipani,Galu wachiwewe.
Uyu wau galu
inu a Ken Nsonda mwakalamba ndipo mulibe nzeru, mwawonetselatu kuti mu chipani cha DPP mumasokoneza ndiinu ndi anankhumwa, anthu opanda nzeru ofuna kulemera kudzera mukuba mu chipani mukuchulukira. inu ansonda mumayipitsa chipani ndiinuyo. 63 years mukunamanso.
Fortune seeker,wadyera uyu
Kavuwevuwe uyu
One of gready politician in malawi we don't need him in dpp lero ali ku dpp mawa ku mcp he is useless
Munthu wamisala amakonda kuyenda yenda kwawo kwenikweni sikumaziwika amamuziwa ndiwokhawo kumene amachokera.
Ada awa zeru ndizochepa kwabasi palibe choonadi pa inu nenani amene amamudyera ndalama apm? Ngati ndi achilungamo. Andale bwanji mukubisala mumawu a Mulungu pa mene ndinu mkango yolusa mukulemphera kuyankha chilungamo.munthu wachilungamo akamufusa sazemba kuyankha.
Msonda oyeee
Uyu amangidweso ngati chisale kumapeto
Kaigon msonda kkkkkk
Masala musamazikayikile mutha kukhala pulezidenti staubi
Nsonda just move !!!lots of partys in country takajoineni chipani china wat best for u ,like wat dausi did
Awa nd achisilu akudwala uyu
Matenda ake ndi edzi tu😂
Wagwetsa kwacha ndani msonda machende amako
Kodi conversion amakonza ndi a court kapena achipani komanso crime imeneyi yosapangitsa conversion imatchedwa contempt of court? Why ma administration onse adutsa kumbuyoku asanakakamizidweko ndi court kupita ku conversion?
Ndimaonera mwachidwi ndipo nsonda amayankha bwino mafuso koma kumapetoko ndipomwe ndaziwa kuti akutumidwa ndi mcp muvetsetse ku mapetoko
muuzimu wadziwa bwanji iweyo, ntchito ndi chipanu ndizosiyana Mr Ken I think mumango lankhula but you don't know what you mean, now I understand you are good in talking but you don't know what is politics zangochitika kuti muli ndi mwayi okhala nawo pafupi ndi anthu omwe akupanga ndale.
Kodi azodick mumachita interview ndi skeleton
Kodi madam alipo akumakutumani?
Hahaha sangawine skeleton uyu kkkk
😮😮
Usasowa pogwira nyapapi ngati iweyo
63 yopanda zeru 5 years atha kukhala ndi zeru 😂😂😂😂 adawa wosokoneza Ali ngati mayi woyendayenda ameyo Leah ongotaya naye nthawe
Alibechochita, amadyera mommo but ndalezinasintha azatamasoka one day nkuluyu
Ai msonda, kuchepa thupi kwako siuli ngati Lea please Msonda you're too much ghost
Malawian politicians are funny Koma
Tandikonzeni kugwa kwa kwacha ndi natural disaster
Nsonda kkkkkk! Dausi weniweni
KADHALA AKAKA SIKAKULA BWINO😂😂😂😂
This politician speaks truth
Mbali wanga mwa Ambuye Yesu Christu Keep fighting for the truth
A NEW VERSION WILL GOVERN OUR LAND SO HELP ME GOD GIVE ME THE WAY TO SAVE MY PEOPLE DURING THIS DIFFICULT TIME WHEN MY PEOPLE ARE STRUGGLING THEIR LIFE IS DETERIORATING LIKE A LOCKET SO HELP ME GOD TO SAVE MY PEOPLE
Best journalism❤❤😂
Ozayamba chipani chanu bwanji mukutinyasa kwambili
Dunderhead, nincompoop,I don't have any kind word for you
Kkkkkkk ine ansonda mulungu akudalitseni
Msonda ndiwe mbuzi ulibe mfundo Koma ife tili pamboyo pa APM
Leah ndimakufuna
Boza
Leah amakhala interested ndi mayankho abodza
Uyundicnisilu akukulakukamwa yet alive ndalama convertion ndalama za apm? Ntumbo wamako nsonda
Azibambo adyera awa
Komaso inuyo atora ngani mukamafuna kuyangura ndi andu osamafusa mafuso ndi amisara omwe nsonda ndi wamisara
🎉
Kodi sakuziona kuti watha anayenera kukapuma mphamvu zatha and nzeru zathanso palibe cha nzeru angokhala chete basi