Interview ndi Norman Chisale

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 15 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 385

  • @mengokumwenda3832
    @mengokumwenda3832 11 หลายเดือนก่อน +23

    The lady was carefully selected to handle this interview am impressed with how she has handled this heavy interview. Professional indeed

  • @RuthNankumba-ux3sw
    @RuthNankumba-ux3sw 11 หลายเดือนก่อน +21

    Big up Norman Chisale ,I love your courage 🔥 Ambuye apitilize kukumenyeran nkhondo ,,,I'm one of your supporters

    • @NzeruDesign-ut1go
      @NzeruDesign-ut1go 7 หลายเดือนก่อน +1

      Ndpo nthawvyamayankho ikubwela big tipanga zobwezera ntoporao

  • @frankiechasokoneza5802
    @frankiechasokoneza5802 4 หลายเดือนก่อน +5

    Komano pa point ya human rights Peter Muthalika he really respects

  • @paulgodfrey3361
    @paulgodfrey3361 11 หลายเดือนก่อน +9

    Leah you the best journalist...well done to Me Chisale

  • @Catherinesmart-xk4zx
    @Catherinesmart-xk4zx 11 หลายเดือนก่อน +4

    Chisale ndimunthu wabwino kwambiri wamanga ma church wachita zambiri Ambuye akudalitsen achisale long live

  • @hectortambuli605
    @hectortambuli605 11 หลายเดือนก่อน +4

    Great man Norman Chisale. Oceans of luv to you and your family.

  • @mijerimasiye7310
    @mijerimasiye7310 8 หลายเดือนก่อน +5

    Azodiak tamakhalani ndi ma bottle amadzi mukamapanga interview ndi anthu please

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus 3 หลายเดือนก่อน

      Komadi man
      I support 😂😂😂good

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 11 หลายเดือนก่อน +12

    Chisale akumva zowawa chifukwa cha anthu ansanje but Chisale is the best Man in Malawi he spend his money to help the orphans and community, God bless you always and protect you Mr Chisale.

    • @AngellahKunsanama
      @AngellahKunsanama 11 หลายเดือนก่อน

      Zoonad ol evn Ines zimandiwaw, km Amalawi if nsanje😢

    • @Homeofpeace321
      @Homeofpeace321 11 หลายเดือนก่อน

      @@AngellahKunsanama amalawi amamukonda munthu akafa, that's why dzikoli lili lobwerera mbuyo,

    • @AubreyKennethchingamba-gq6et
      @AubreyKennethchingamba-gq6et 2 หลายเดือนก่อน

      Titakhala ndi anthu 20 nziko lino ngati Mr Chisale Malawi atha kusintha I proud of you Mr Chisale ndimakunyadilani chifukwa chakulimba ntima kwanu

  • @ChristinahNkwanda
    @ChristinahNkwanda 8 วันที่ผ่านมา

    Norman ooooye.Please Please please Mr N Chisale keep it up God will help help you, always pray, praise him Amen Amen Amen

  • @JamesKamanja
    @JamesKamanja 3 หลายเดือนก่อน +1

    God bless Mr chisale komano mokupemphani ndithu pepani uyu akufuna kut mumukhululukileyu imvani kulila kwake kut ukulu wayehova ukhalebe pa inuyo yesu anat muwakhululukile chifukwa sakuziwa chimene akuchita
    Musaiwale kut munthu payekha alibe vuto koma satana akamulowa amapangisa munthu kuchita zimene choipa chili mwa iyeyo chikufuna please ndikuziwa ndithu ululu ndi ochuluka kwambili koma khululukani ambuye apitilize kukupasani moyo wamphanvu madaliso avumbebe kut wamasiye apeze popumila

  • @LetsSeePlaces43
    @LetsSeePlaces43 11 หลายเดือนก่อน +11

    Interviewing a well trained professional soldier should be different with interviewing a well trained professional economist💪🏾💪🏾Bravo snipper Norman Paulosi Chisale🤣🎉🎉💥💥

  • @thomluciouss7360
    @thomluciouss7360 11 หลายเดือนก่อน +13

    The one who talk the truth doesn't fear and it's really true that the truth pains big up Mr Chisale

  • @matembanevermind-po3me
    @matembanevermind-po3me 10 หลายเดือนก่อน +1

    Gud interview love you questioner and Mr interviewer Norman

  • @CresentShaba-k3q
    @CresentShaba-k3q 7 หลายเดือนก่อน +2

    Mr Chisale isn't my relative but ndawamvesa he is a real soldier, BRAVO CHISALE. BULL Sheet kayun.

  • @DairesBaina
    @DairesBaina 11 หลายเดือนก่อน +4

    Chisale your number 1 well trained soldier

  • @chifunirosaka9077
    @chifunirosaka9077 11 หลายเดือนก่อน +12

    Soldier never die chisale more 🔥

  • @falayichitsotso5371
    @falayichitsotso5371 11 หลายเดือนก่อน

    Mr Chisale I hear ur story it's very bad and am very happy with u ustand with God dnt give up mukuyakhula kwako mulungu akumva ndipo mulungu amalora Kuti ana Ake andutse mmavuto ndicholinga Choti ukulu wake ukaonekere God will be with u mwaiwe muli usogoleri

  • @JohminMatick-c9h
    @JohminMatick-c9h 11 หลายเดือนก่อน +1

    Msilikari adzakhare msilikari mpaka kare. Big up bro N. Chisare❤❤

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn
    @AlexManuelMisomali-sv1vn 3 หลายเดือนก่อน

    Norman your statement is clear and comprehensive but what about Chthyola, Chimwendo Banda, Kunkuyu etc ??

  • @GodfreyMphaya
    @GodfreyMphaya 7 หลายเดือนก่อน +1

    Bravoooo big man chisale i salute you

  • @Edgar.RatheilKapalamula
    @Edgar.RatheilKapalamula 11 หลายเดือนก่อน +5

    Akuzuzika ngati yesu chisare ndi Good Samaritan athu abwino amazuzika

  • @kannockRichy
    @kannockRichy 11 หลายเดือนก่อน +4

    Mr chisale attitude in this interview shows kuti bambowa ndionama..😂

    • @magdalenachipeta2394
      @magdalenachipeta2394 11 หลายเดือนก่อน

      Ndipo sukunama uku ndiwabodza auze mtundu wa a Malawi kuti ma billions a chuma anawapaeza bwanji osamangobwebweta zopanda phindu, kufuna anthu akumvele chisoni.

    • @DouglasDazuKamwendo
      @DouglasDazuKamwendo 3 หลายเดือนก่อน

      Ndinu mabulutu guys

  • @mordecaikachale2497
    @mordecaikachale2497 11 หลายเดือนก่อน +10

    I like the energy tht u hv Mr chisale as a soldier...big up❤

  • @lyiemax
    @lyiemax 11 หลายเดือนก่อน +6

    Powerful talking and intelligent, proud of you @Norman Chisale

    • @henryhenry6632
      @henryhenry6632 11 หลายเดือนก่อน

      Intelligent ya ku machende amalawi mapanga support zingawenga bwanji, kupusa

    • @yamikanijames6915
      @yamikanijames6915 10 หลายเดือนก่อน

      Mukuyamikila chisale man? After all what he did now you're embracing his work.... don't you know people lost trust in DPP and one of the biggest reason ndi iyeyu

    • @LetsSeePlaces43
      @LetsSeePlaces43 10 หลายเดือนก่อน +2

      People never lost trust with DPP...anthu tinanamizidwa kuti tizaona zabwino...pano misozi yatha mmaso yayamba kutuluka ndi misozi ya magazi chifukwa Cha bodza la CHAKWERA ndi chilima.

  • @EmmanuelKamwagha-m5u
    @EmmanuelKamwagha-m5u 11 หลายเดือนก่อน +2

    Courage muli nayo...komano kusa kululukako kuchita kuoneseratu kuti muli ndi mtima wakupa

    • @happyzumatembo2174
      @happyzumatembo2174 8 หลายเดือนก่อน

      😢 or uli iweyo kut munthu akunamizele mulandu wa murder. Uthakumukhululukira?

    • @DouglasDazuKamwendo
      @DouglasDazuKamwendo 3 หลายเดือนก่อน

      Sukudziwa chomwe ukunena, sukuona kuti Chisale amuzuza popanda zifukwa?

  • @ThomasKawina-o5n
    @ThomasKawina-o5n 23 วันที่ผ่านมา

    Ana achepa ulemu wanu bwana chisale 👏👏👏👏👏👏

  • @LingstonManjolo
    @LingstonManjolo 23 วันที่ผ่านมา

    Amalekano zikomo chifukwa Cha machezedwe anu ndi achisale mkazi odziwa kufusa ngati iwe thanks

  • @blessedmichael5124
    @blessedmichael5124 11 หลายเดือนก่อน

    I like sir Norman Chisale he's been good in speech osamaopa pa chilungamo

  • @AcacioWilsonPhezula-t8l
    @AcacioWilsonPhezula-t8l 2 หลายเดือนก่อน

    Wn am the of them amene ndimamva kuwawa ndikamva kuti mwamangidwa,sinakumane nanu ,sitinayankhulako koma zimkandiwawa koopsa

  • @paulmakaula4937
    @paulmakaula4937 11 หลายเดือนก่อน +6

    Political prosecution has ever been in existence since our independence....please follow the rule of the law always! Clear conscious is the medicine...God is watching and will judge everyone right..

  • @GodfreyMphaya
    @GodfreyMphaya 7 หลายเดือนก่อน

    One thing i like this guy he talk straight

  • @TwalikiWisiki
    @TwalikiWisiki 4 หลายเดือนก่อน +1

    Mr Chisale i understand your pain please please firgive him isbus for your own good, you saud you are Christian our master jesus taught us to forgive those who do us wrong before we ask to be forgiven

  • @Johnybegood260
    @Johnybegood260 11 หลายเดือนก่อน +9

    This woman is brave

  • @williammaseko8542
    @williammaseko8542 11 หลายเดือนก่อน +3

    He is very emotional and trying to run away from facing justice. No one accepts to be guilty in public and whatever is doing here is normal for suspects. 42years doesn't match with the way he looks unless he tells us kuti amasamba Nyanga.

  • @LevisonSimssimbeye
    @LevisonSimssimbeye 11 หลายเดือนก่อน +1

    Watching from zambia

  • @NodiceChakwala-tz5gg
    @NodiceChakwala-tz5gg 11 หลายเดือนก่อน +1

    great mtolankhani , kip the fire burning girl

  • @magdalenachipeta2394
    @magdalenachipeta2394 11 หลายเดือนก่อน +1

    1986 he was already working as a soldier but he is saying is 42 years old eeeeeish!!! 😂😂😂komatu munthuyu akuoneka ndiokakala mtima mayankhulidwewa atha kupanga zoophsya. He is saying kuti ndiopemphela koma akuti sangakhululukile aSteven Kayuni 😭😭 chonsecho amayenda ndi bible , mawu a Mulungu mwamunthuyu mulibemo.

  • @shupikayintuwaluwa-5899
    @shupikayintuwaluwa-5899 11 หลายเดือนก่อน

    Kkkkkkk aaa zoona. Msilikali kiching, amba chilungamo n how he's feeling with de way they r treating him

  • @chawagondwe6404
    @chawagondwe6404 11 หลายเดือนก่อน +1

    Those who are saying bravo chisale you need special prayers..this guy stole our money tax payers money....he accumulated wealth within a short period of time....hotels cars houses etc he is backing himself apa he can't admit it.....and you are busy kumunyadira 😮Malawi ndife ogona too much.....he is lucky he is outside otherwise he belongs inside

  • @JohnThomola
    @JohnThomola 11 หลายเดือนก่อน

    Kmat adakufikisani pamenepo ndi bambo anga mudawathokozapo ndi chani ???

  • @alexjeremanuel2541
    @alexjeremanuel2541 10 หลายเดือนก่อน

    Haters will always blame you my brother just because all the enemies of APM can't be happy with your speech. Even the way this woman is interviewing you just shows that she is one of the haters because of this ( I feel bad and hate those ones who are blaming APM for useless things or political reasons and I handle him as my biological father) but no stress brother you're a real and very strong soldier and you're humble man otherwise stupid questions this woman was asking you if it was I, I would just fu....k off from that interview. Your character is a real good courage and discipline soldier and we love you and everything is going to be good

  • @ndalamaandrew
    @ndalamaandrew 11 หลายเดือนก่อน +2

    Koma Chisale uyuyu eeeeeeh 🙌🙌🔥🔥🔥

  • @peterbyson6269
    @peterbyson6269 6 หลายเดือนก่อน

    respect to you both you building Malawi in this interview ..

  • @JuliusSantos-l7h
    @JuliusSantos-l7h 11 หลายเดือนก่อน +4

    This guy is some how mad

  • @jumazabula2908
    @jumazabula2908 11 หลายเดือนก่อน +1

    Definition of having readership, fire 🔥 chisale

  • @richardskumwendah9072
    @richardskumwendah9072 11 หลายเดือนก่อน +8

    Once a soldier always a soldier 💪💪💪💪

  • @eliasMwamba-q5f
    @eliasMwamba-q5f 11 หลายเดือนก่อน +4

    Once a soldier always a soldier❤❤❤

  • @maonekedweDaniel
    @maonekedweDaniel 11 หลายเดือนก่อน +3

    Kma this interview must be repeated even pa wailesi , nice Leah keep on going more fire

  • @pempherokatakwala6451
    @pempherokatakwala6451 11 หลายเดือนก่อน

    Norman chisale iweyo ndi number 1 moto kuti buuuuu!!

  • @dumisanimoyo3152
    @dumisanimoyo3152 11 หลายเดือนก่อน +1

    Chisale usatiuze kuti akhale wo opa mulungu suyo chakwera wo opa mulungu akutizunza

  • @Chief-Phungwako
    @Chief-Phungwako 11 หลายเดือนก่อน +1

    This was nice chisale seems a good one though ndindale

  • @DouglasDazuKamwendo
    @DouglasDazuKamwendo 3 หลายเดือนก่อน

    Am watching this interview kachikenaso Norman Chisale yu ndi #1 kwa amene alipa chilungamo akudziwa kuti big wa ndi real man osangoti mwakati poti umadana naye.

  • @enipherphiri207
    @enipherphiri207 11 หลายเดือนก่อน +2

    Chisale oopsya eeeee. Bible mmanja koma Bullshit pakamwa mbweee ashiii

    • @DouglasDazuKamwendo
      @DouglasDazuKamwendo 3 หลายเดือนก่อน

      Iwe umati atani? Uzaziona ukadzapeza ndalama

  • @MikeGama-j6j
    @MikeGama-j6j 11 หลายเดือนก่อน +2

    Tikukuvesesani mr chisale.

  • @PetrosKachingwe
    @PetrosKachingwe 10 หลายเดือนก่อน +1

    Once a soldier always a soldier

    • @Cee-H-Cee
      @Cee-H-Cee 10 หลายเดือนก่อน

      Exactly

  • @MisheckChangata
    @MisheckChangata 3 หลายเดือนก่อน

    Great man ,i like u

  • @SheenahMwalabu-iz3pr
    @SheenahMwalabu-iz3pr 11 หลายเดือนก่อน +2

    Ndamva chisoni pokumva nkhani yanu bambo Chisale 😢 koma chilungamo chilipo ndipo momwe mwadutsa inumo enanso adutsamo ili ndidziko. Abale whyyy a police athu mmatero, olo ndiliineyo ndingaophwezetu ndipo ndikanamizilidwa ndimakwiya kuposanso achisalewo 😂😂

  • @paulgodfrey3361
    @paulgodfrey3361 11 หลายเดือนก่อน +1

    Your the best Leah

  • @frazerbstaffwell5083
    @frazerbstaffwell5083 11 หลายเดือนก่อน +3

    Wabodza iwe umakhala kukawale pa rent bingu akulamula unalibe kanthu unaba chuma bingu atamwalira ku state house

    • @CharityAlex-r3v
      @CharityAlex-r3v 3 หลายเดือนก่อน

      Eeeeeeeeee ai zikomo kwambili koma Mulungu arimbariyakhe

  • @MjombaMjuba
    @MjombaMjuba 11 หลายเดือนก่อน +1

    Akunama uyu, wakupha komanso wakuba, chitsiru chimangidwa chisiyeni, sakudziwa kuti apita kundende.

  • @Liam-ky5cu
    @Liam-ky5cu 11 หลายเดือนก่อน +1

    Bravo Bravo 👏 😁 Soldier...

  • @jamessmithnjirayafa5252
    @jamessmithnjirayafa5252 11 หลายเดือนก่อน

    Substandard journalism. Nkhani ya kuti ndalama anazitenga kuti sanayimalize. Amati kunali nkhani yina imene amayenera kugundako they didn't. Komanso kumusiya munthu using profanity language over and over on national osampatsa warning or even ending the program it's way below par.

  • @maskinmsungeni8763
    @maskinmsungeni8763 11 หลายเดือนก่อน

    Kkkkkkkkkk Norman Chisale !!!!! Ur a big Man. Wandiwaza kwambiri Msungeni all the way from Zambia.

  • @edwintshepang5108
    @edwintshepang5108 11 หลายเดือนก่อน +2

    Iwe interview sayamba choncho aaaaa introduction first

    • @Littlefair7
      @Littlefair7 11 หลายเดือนก่อน +2

      Interview ili yonse imakhala ndi mayambidwe osiyana, iyi si program ya tikudziweni, muziyamika kuti mwa atolankhani achizimayi, Leah is one of the best.

    • @alfredbanda1693
      @alfredbanda1693 11 หลายเดือนก่อน

      ​@@Littlefair7😂😂😂 koma ndi fact

    • @Littlefair7
      @Littlefair7 11 หลายเดือนก่อน

      @@alfredbanda1693
      Samala Alfred upalamula🤣🤣🤣

    • @alfredbanda1693
      @alfredbanda1693 11 หลายเดือนก่อน

      @@Littlefair7 ndaleka😂😂

    • @Littlefair7
      @Littlefair7 11 หลายเดือนก่อน

      @@alfredbanda1693
      🤣🤣🤣🤣

  • @LameckManuel-h7e
    @LameckManuel-h7e 11 หลายเดือนก่อน +2

    I love you Mr noman❤

  • @chimwemwenkosi-nl4zj
    @chimwemwenkosi-nl4zj 11 หลายเดือนก่อน

    True leadership timakunyadilani mr

  • @Bushiriderick811
    @Bushiriderick811 11 หลายเดือนก่อน +11

    Interview without introduction 😂😂😂😂😂😂Lea be professional plz

    • @Chiso2019
      @Chiso2019 11 หลายเดือนก่อน

      Ndipo ineso ndikudabwatu interview yanji yotero no introduction

    • @alfredbanda1693
      @alfredbanda1693 11 หลายเดือนก่อน

      Kkkkk I hope akuphunzira adzitolera

    • @chifunirokachingwe3700
      @chifunirokachingwe3700 11 หลายเดือนก่อน +1

      Pajatu anthu odziwika ngati amenewa introduction sikhala yofunikira kweni kweni, komabe as far as ma dos and don'ts are concerned apopo sizinayende kweni kweni😂

    • @kusalaphameya3421
      @kusalaphameya3421 11 หลายเดือนก่อน

      i was riding in your ship until i took some time to regurgitate
      and i learn kuti amacheza naye ngati bodyguard wa Peter, his professional, and not as him as a person
      brian banda akucheza ndin Bushiri, 27th may times exclusive, followed the same lane
      yomwe anacheza ndi a Kapito pa 7th october anatero
      even yomwe anacheza ndi Dr. Joyce Banda

    • @Taonga0ngieKalua-yc6ok
      @Taonga0ngieKalua-yc6ok 11 หลายเดือนก่อน

      Kkkkkkk ndipo etiiiiiii inuuuuuu iiiiii

  • @yamikanichakuluntha651
    @yamikanichakuluntha651 11 หลายเดือนก่อน +2

    Kulavula Moto munthu wamkulu, Lord have mercy on him

  • @patrickjoda2165
    @patrickjoda2165 11 หลายเดือนก่อน +2

    Mulungu akhale patsogolo basi Mr chisale Angoni

  • @GiftMeja
    @GiftMeja 11 หลายเดือนก่อน +1

    Komatu chisale ndye akumulakwla

  • @LawrentNyasulu
    @LawrentNyasulu 2 หลายเดือนก่อน

    Leah ndikadziotche apa adakamenyedwatu

  • @V_Diesel
    @V_Diesel 9 หลายเดือนก่อน

    42 years old? Did I hear that well? 🤔 Interesting.

  • @NkhumbuSichela
    @NkhumbuSichela 11 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂 so in love with his courage 🤦🥰

  • @ChifundoBeston
    @ChifundoBeston 11 หลายเดือนก่อน +3

    Achibale zimenezo ndizija mumkachita kwa anthu ena muli m'boma limodzi ndi DPP. Zimatelotu chisale, iweyo ndiye akupsote kumene galu iwe munthu oipa iwe

  • @YohaneGauti
    @YohaneGauti 2 หลายเดือนก่อน +1

    Bwana chisale ineyo ndikuti pepani kwambili pa zomwe munazunzidwa
    Ifenso timamvanso kuwawa

  • @Dango79394
    @Dango79394 11 หลายเดือนก่อน

    This lady, knows how to calm somebody. Mamuna wake anapata.

  • @ElizabethMnemba-c8j
    @ElizabethMnemba-c8j 11 หลายเดือนก่อน +2

    Aaaa😮zaka 42 ndeine ndili 15 years 😂😂awa ngabodza

  • @alfredbanda1693
    @alfredbanda1693 11 หลายเดือนก่อน +1

    Leah try to write questions to be asked and kungoti bwana chisalewo amachita kokuwongoleranso plz plz plz interview opanda introduction aaaaaaa 😂😂😂

    • @Dango79394
      @Dango79394 11 หลายเดือนก่อน

      munazolowera zoloweza, muziganiza.

  • @kingsleynaluso2358
    @kingsleynaluso2358 7 หลายเดือนก่อน

    Ndipo live akunenazo ndi zoonad km Malawi kusamva😂😂😂

  • @tisuhmakhwah7085
    @tisuhmakhwah7085 11 หลายเดือนก่อน +1

    Kkkkkk ayayaya malawi tingogulisa tigawane dollar zo

  • @NishaMakwiya-l1x
    @NishaMakwiya-l1x 11 หลายเดือนก่อน +1

    Koma poti APM ayimezo nde tasephana basi aaaa..mwachidure kumalawi ndare zithe

    • @DouglasDazuKamwendo
      @DouglasDazuKamwendo 3 หลายเดือนก่อน

      Iweso khala chete mapazi opotokawo ngati milomo yako ikuyankhula mopotokayo

  • @Gorilla-k8e
    @Gorilla-k8e 11 หลายเดือนก่อน +2

    😂😂😂😂😂😂😂moto kuti buuuuu L malekano umatimilila koma bwinotu akubandula mbakela bwana ameneyo 😂😂😂😂😂

  • @chrisscapper-zw5rk
    @chrisscapper-zw5rk 9 หลายเดือนก่อน

    Bravo Mr Chisale

  • @AlfredMponda-n3u
    @AlfredMponda-n3u 11 หลายเดือนก่อน +3

    MCP ikazachoka m'boma idzazunzika kwambiri

  • @hendrinagama5325
    @hendrinagama5325 11 หลายเดือนก่อน +1

    Uyu mafunika brain Banda osati ana awa

  • @wisdomluhanga
    @wisdomluhanga 11 หลายเดือนก่อน +2

    Munthu ukulempera to forgive while holding bible

    • @chesterphiri7523
      @chesterphiri7523 7 หลายเดือนก่อน

      Kkkkkkkk😂😂😂😂😂😂

  • @dumisanibanda6338
    @dumisanibanda6338 11 หลายเดือนก่อน

    They are asking this guy what challenges did you face.. akufotokoza ma situations.. he was expected to mention political challenges, kapena professional dilemmas. Ayi, zopepela

  • @InnocentMsiska-sr8pe
    @InnocentMsiska-sr8pe 7 หลายเดือนก่อน

    Norman is right,the fact that aperson is working in the government does not bar aperson from being rich . Malawians justify poverty as being honest and truth

  • @djmakedzana9917
    @djmakedzana9917 11 หลายเดือนก่อน +1

    chisale ndi chitsiru. nkhani ya chilima ikukhuzana pati ndi kuba kwakoko

  • @SydneyRajab
    @SydneyRajab 9 หลายเดือนก่อน

    Leah , bravo 💪

  • @quintonmutume82
    @quintonmutume82 9 หลายเดือนก่อน

    Dpp yangoyenera kubweler 💓💓🙌🙌

  • @blessedmichael5124
    @blessedmichael5124 11 หลายเดือนก่อน

    Akuti thats totally bullshit yes yes
    I like the confidence.

  • @sainetjackson6183
    @sainetjackson6183 11 หลายเดือนก่อน +2

    Chisale ndikatumdu🤗

  • @Discar_mw
    @Discar_mw 11 หลายเดือนก่อน +2

    This was a hot 🔥 one lol 😂

  • @stanleykaludzu-bm4pm
    @stanleykaludzu-bm4pm 11 หลายเดือนก่อน +2

    Brother chisale takumvani...Proud of you now.

  • @lonjiekaselera9651
    @lonjiekaselera9651 11 หลายเดือนก่อน

    The real legend khaaa wauuza ngamo

  • @samaxodala7587
    @samaxodala7587 11 หลายเดือนก่อน +1

    Chisale💪💪💪🇲🇼🇲🇼

  • @chawagondwe6404
    @chawagondwe6404 11 หลายเดือนก่อน +1

    Why even giving him a platform to say this nonsense.? He was very powerful, kusowa umboni doesn't mean you re innocent...you did 99percent of what you were accused of .....we know you can see even his tone kuti angaombele munthu awa

  • @LingstonManjolo
    @LingstonManjolo 23 วันที่ผ่านมา

    Achisale ndakutsatani pa u tube Mumapemphela zinazi msiireni Mulungu akhale Mulungu Ambuye yesu amamunamizila koma samayankha kanthu mpaka anaphedwa Eksodo 14v14 Chonde chonde

  • @lukainnocent5380
    @lukainnocent5380 11 หลายเดือนก่อน +1

    mbuzi chisale ukuona ngati bambowakowo sangawine ameneyo wapha albino wakwa na