ไม่สามารถเล่นวิดีโอนี้
ขออภัยในความไม่สะดวก

MZIBAMBO WAPHEDWA MWANKHANZA CHIFUKWA CHA CHIMANGA CHITATU

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 30 มี.ค. 2024
  • WAPHEDWA CHIFUKWA CHA CHIMANGA CHITATU

ความคิดเห็น • 143

  • @user-dn5sf3md5t
    @user-dn5sf3md5t 4 หลายเดือนก่อน +13

    NGATI YESU CHRIST ANATEMBERERA NKUYU CHIFUKWA CHOSABEREKA , INEYO NGATI MTUMIKI WAKE NDIKUTEMBERERANSO JERE KUYAMBIRA LERO NYENGOZAKO SIZIDZAKHALA MONGA KALE UDZAKHALA UKUZUNZIKA MOYOWAKO.ONSE ANA AKO APABANJA PAKO MDZINA LA YESU CHRIST AMENE ANAPACHIKIDWA PAMTANDA CHIFUKWA CHA TCHIMO LAKO,MDIKULENGEZA NDI MWAZI WAKE WA YESU USOWE MTENDERE , USOWEMTENDERE ,USOWEMTENDERE .

    • @user-xi6sr7kd7p
      @user-xi6sr7kd7p 4 หลายเดือนก่อน +1

      Pa dziko lapasi Pano akhoza Kukhala wandalama Koma mulungu ndi amene angaweruze pakuti tonse ulendo wake ndiwomwewu nayenso jereyo ulendo wake ndiwomweyo.

  • @user-rl5zq1qr4d
    @user-rl5zq1qr4d 4 หลายเดือนก่อน +10

    Bukhu lopatilika lamulo lachimvekere usanamizire mzako lamulo Lina usaphe truck driver sangabe chimanga chiwiri nzosatheka nkhanza panali udani pakati pa driver ndi driver mzakeyu

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete 4 หลายเดือนก่อน +6

    Kukhala waphedwayo ndim'balewanga chilungamo chake ndingachipange ndekha because our police is useless

  • @DorothyKaimfa-ns8su
    @DorothyKaimfa-ns8su 3 หลายเดือนก่อน

    The pain still fresh Mr Jere muliko zikuwawa zikuvuta kuiwala ambuye achite nanu munatiphera munthu ofunika kwathu nkusauka kwathu sitimadzadya kwanu ifeee linali thandizo kubanja kwathu ambuye akhale nanu akuoneni misozi iyi one day idzatembenuka ndikukhala pamutu panu ndithu 😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭 My brow anapita osalakwa or kwathu chikhalire sanabepo anali ofatsa mbale wanga osayankhula koma inuyo a Jere

  • @gesinasutherland9241
    @gesinasutherland9241 4 หลายเดือนก่อน +2

    Osadandaula Mulungu ali mbali yanu..Mulungu akutonthozeni..ndipo Mulungu akumenyeleni nkhondo chilungamo chiyende ngati madzi....mulungu ali mbali yanu..

  • @charleslimbani8590
    @charleslimbani8590 4 หลายเดือนก่อน +7

    Mr jere ngati simulapaa chuma chanu chiyamba kupita pansii koma simufa nsanga kufikira mutaona maxunzo oophyaa kwambiri

    • @GiftJulius-gx2kb
      @GiftJulius-gx2kb 4 หลายเดือนก่อน

      Ndipo asafe asazafenso azizangovutika mpaka kale

  • @EstherBair
    @EstherBair 8 วันที่ผ่านมา

    Mmmmm kulakwa ndipo ajele ambuye akuwoneni

  • @rashidsaid2232
    @rashidsaid2232 4 หลายเดือนก่อน +4

    Malawi it's no democracy democracy of it's only for rich people not for the poor people nkhani yomvetsa chisoni

  • @WilfredMathews-yl6ij
    @WilfredMathews-yl6ij 4 หลายเดือนก่อน +2

    Komatu apa apolisinu chilungamo chioneke pliz pliz pliz 😭😭😭😭 musadye ndalama zatemberero pamoyo wamunthu ngt momwe adachitiramo ngt akupha nkhuku

  • @NumbDee
    @NumbDee 4 หลายเดือนก่อน +2

    Ajemu ndi Louis
    Mzimu wamunthu ameneyu ukuzuzani koopsyani

  • @patrickkalivea6879
    @patrickkalivea6879 4 หลายเดือนก่อน +4

    Koma zovesa chisoni kwambiri Abele Malawi wasanduka Ngati mukango Mau amanena Kuti tinkhale anthu onkhulukilala Wina ndi muzache chifuwa Ngati ifeyo sitinkhululuka anthu ena ndiziwe Kuti pasiku lomaliza ambuye yesu sakatinkhulukila

    • @HannaBanda-pj8vr
      @HannaBanda-pj8vr 4 หลายเดือนก่อน

      Aaaaa Malawi able akupita Kuti ? Ndikulila ine mbaleyo au Se muntendele ,anthu achita izi mulungu asawakhululukile ayi ,akayakhe mulanduu Amen

    • @estherkambewa7791
      @estherkambewa7791 4 หลายเดือนก่อน

      Chimanga chitatu mpaka moyo wamunthu? Zomvetsa chisoni

  • @user-tt1kv3oh7c
    @user-tt1kv3oh7c 4 หลายเดือนก่อน +1

    So touched story eeish!!

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu 4 หลายเดือนก่อน

    Pakudutsa chinyengo apa,, ine kanakonda khuluyu ndimudziwe , ine nditha kuthana naye ndekha

  • @user-zy1br2fy6v
    @user-zy1br2fy6v 4 หลายเดือนก่อน

    Thanks to you Hanifa Tv for bringing us this story
    Ndimakutsatani kwambiri nkhani zanu
    Koma mufunika kukonza pa editing zuoneka kt zimakuvutani kupanga edit zinthunzi zanu pena timakhala ngati tikuonera beyond the scene ija 😂😂😂😂😂

  • @tianarose9380
    @tianarose9380 4 หลายเดือนก่อน

    Zovetsa chisoni kwambili osauka alimbe mawu 😭😭😭

  • @user-im4bs7fk9o
    @user-im4bs7fk9o 4 หลายเดือนก่อน +2

    Pepani kwa mbiri.mzimu wake use muntendere chimanga sizinthu zophera munthu ayi.amene anapanga izibadzakolola pangatalike Patani .

  • @JohnBanda-ux9fy
    @JohnBanda-ux9fy 4 หลายเดือนก่อน +1

    Chuma cha magaza muyaluka nacho ..kulora kuchosa Moyo wa munthu chifukwa Cha 3 pic of maize muli NDI tsoka ..poti muli NDI Chuma chambili mugure Moyo mubwezere Kwa mwini wake iwoso akubwezeren chimanga chanu ..Koma osaiwa nthawi ili mkudza yomwe mudzayankhe

  • @LoydKameza
    @LoydKameza 4 หลายเดือนก่อน

    😭😭😭😭😭abale kulakwa kupha Munthu osalakwa

  • @HajaSande
    @HajaSande 4 หลายเดือนก่อน +1

    Ayi kuno ku south Africa tingoyika zonse manja mwa chauta

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj 4 หลายเดือนก่อน +1

    Kumbali yanga ndikuona kuti anthu Adela imeneyo pamafunika kuthandizana chifukwa chilungamo chiziwike chifukwa boma iripoyi ndilopondereza koma patokha titha kuthananazo

  • @peterlowole7841
    @peterlowole7841 4 หลายเดือนก่อน

    No Mr jere 😭😭😭😭 kulira Kwa munthu asalakwa mulindi zambi bwanji osapempha anthu akulipireni chitatu chimanga kupha munthu ayiii inuyo mumafuna zizimba timaziwa olemelanu ,koma ziwani mulindi mlandu kumwambako

  • @user-zy1br2fy6v
    @user-zy1br2fy6v 4 หลายเดือนก่อน +1

    Mukapanda kupeza chilungamo kuchokera ku polisi, pezani njira zanu ndi abale anu mpaka mupeze chilungamo pa nokha
    A police wa sakuthandizani

  • @user-zr6te9uq7w
    @user-zr6te9uq7w 4 หลายเดือนก่อน

    Jele Mulungu akukathe, mu dzina La yesu khristu

  • @user-tj8tt3ns6l
    @user-tj8tt3ns6l 4 หลายเดือนก่อน

    Zonvuta kwambili allah amulandile muthu ameneyu ndichimwemwe

  • @user-dv6wy1sq8g
    @user-dv6wy1sq8g 4 หลายเดือนก่อน +2

    Anthu tikama otcha ma police ndemuzit Malawi osauka tikulakwa?

    • @AnnieBanda-rb2dk
      @AnnieBanda-rb2dk 4 หลายเดือนก่อน

      One day tizazika mpeni pakhosi police imozi ndikuusiya pakhosi popo kuti apolice onse azave okasolola mpeniwo pakhosi azakhale apolicewo ndi chipatala, kuti azaziwe kuti zimawawa bwanji, olo mwana wa police imozi azakumana nazo adilikire one day azaziwa kuti khobwe sinyemba anthu timasungira chipongwe kwambiri anthu amenewo amaona ngati ochenjera akamadya ndalama zowahonga munthu wakupha mzake but one azaona zimene zizapangike, wa mozi wake azakhala ineyo ndizausiya pakhosi popo mpeni kaya ndikamwana kawo apolice eya ndizausiya popono azapange bwino birthday

  • @davidkadyakapita8836
    @davidkadyakapita8836 4 หลายเดือนก่อน

    Koma zoona mkuchotsa moyo wa munthu chifukwa cha dowe mutatu? Ngati akudalira ndalama mulodzeni ameneyo. Wapha tsogoro la anthu ambiri.

  • @musadinalaanusa9931
    @musadinalaanusa9931 3 หลายเดือนก่อน

    Sanachite bwino anduo

  • @MulemeeDaza
    @MulemeeDaza 4 หลายเดือนก่อน +1

    Osauka alibe mau 😭😭😭😭😭😭

  • @user-nb7dp6pr9n
    @user-nb7dp6pr9n 4 หลายเดือนก่อน

    Munthu ameneyi muti A jere ozinvaa chuma, kunalinso nzawonso ku Mozambique pa Vila ulongwe dzina lomwe ankatchuka nalo linali Anzeru ndinu anali ndi chuma choti Jere mukumunenayo alibe ndalama, koma anaphanso munthu wakubanja lovutikanso ngati lomweri la a Mayi athuwo aku Machinjiriwo. Nkhani yake inali chonchi, M'bambo waku Mozambique ameneyo amawoda golide kunkansosole mu Mozambique monmo ndiye tsikulina anawoda golide wochuluka ndiye atalingalila anaganiza zomugulitsa uja Anzeru ndinu, anakumana kunyuma kwake ndiye ntengo anamuuza uja Anzeru ndinu anati mmmm sindingakwanitse wadula koma ndikupezera nsika kwa azizanga ena ku Beira kapena ku Maputo mwini golide uja ananyamuka ulendo kunyumba kwawo koma nayenso amakhala pa Vila pompo koma mzathu osaukayi amayenda pa njinja ya moto ya DT. Iye phee uku akudikilira Business ya golide, koma ndalama zomwe anamuuzazo Anzeru ndinu akanapeleka tikuti chinali chikhomo, koma plan yake ankafuna kuti angolanda two weeks inapita kumapeto kwa week yachitatu lachisano, Anzeru ndinu anamuimbila phone nkulu uja pastnine PM undipeze ku Bottle store kuno munthu uja ozagula Golide uja wayandikila uja anatsazika madam giya pa DT yake, anafika paja onse ukuakudikila ankamwamowa. Mwini golide anafunsa this's past ereven titan bwana? Anzeru ndinu uja anangoti nthawi ilipo, kenako mwini Golide uja anatengelana pambali ndi bg uja kenakonso pambali paja panafikanso anthu ena koma kwaiyeyo amaoneka anthu osokoneza ndiye mwini golide uja anaitulikila kuti anthuwa alilimodzi iye mwachangu anatenga Golide uja ndikumeza onse aja akuona, kenako madolo aja amamuonekera osokonekera kwaiyeyo anamugwira kupita naye malo ena manmawa kutacha anapezeka atang'ambidwa pamimba ndichotsamo Golide uja, koma zitachitika izi akuchikazi anaimbila akuchimuna kuwadziwitsa zaimfayo koma akuchimuna anawauza akuchikazi kuti musalore a Police kuchotsa thupi ife tisanafike, thupilinachotsedwa akuchimuna atafika koma kwawo ndi ku Chimoyo kumalile a Zimbabwe ndi Mozambique koma iwo ali mu Mozambique. Koma mawu omwe analankhula panthawiyo anangoti nonse mwatenga gawo pa imfa ya m'bale wathuyi tiona. Ndikukamba pano (Anzeru ndinu) kulibe magalimoto oyendera amasintha ngati zovala adafela pa chiongolero anangoti mutuwanga omwewo koma galimoto siinagwenso ayi pomwe amakafikanaye pa Dedza Hospital atafakale koma chifukwa chandalama achibanja samakhutila anapitanso ku Lilongwe Central Hospital anawauzanso chimodzimodzi. Iyeyo asanzinve ndalama ayi.

  • @Madalitso-sj6gg
    @Madalitso-sj6gg 4 หลายเดือนก่อน

    Very bad, koma this boy wafotokoza moveka bwino momwe zinakhalira, Eeee koma this is bad msaname, may his soul rest in peace

  • @tiwongehojaney5873
    @tiwongehojaney5873 หลายเดือนก่อน

    Tangomugululabi mpezi ameneyo

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn 4 หลายเดือนก่อน +1

    Zomvesa chisoni ndiwakwathu munthu anaphedwayo😢

  • @user-xg5pq5ku4l
    @user-xg5pq5ku4l 4 หลายเดือนก่อน

    Sazapeza mwayi mzibambo waphayu,ndipo a Malawi,,,ena,umunthu mulibe.Akanthidwe ndithu anthu aphawo

  • @SawaJaribu-op1jj
    @SawaJaribu-op1jj 4 หลายเดือนก่อน

    Kulakwa zed mzimu wao uuse mumtendere Mulungu yekha ndamene akaweruze dziko lapasi lili chabe😢😢

  • @MichaelChaso
    @MichaelChaso 4 หลายเดือนก่อน +1

    Koma Ajele munapha munthu osalakwa, ndipo pangatalike bwanji Ajele mudzaona masoka komaso mudzayankha mulandu.Mulungu sagona ndipo sangakondwele nanu chuma chanu mulungu achitembelele anthu oipa inu

    • @frankkassim1254
      @frankkassim1254 4 หลายเดือนก่อน

      Ajele naonso aphedwe osangowasiya ndimoyo

  • @enochnkhata9812
    @enochnkhata9812 4 หลายเดือนก่อน

    Chimanga chitatu bwanji sanapite pamalo pamene panathyoledwa Chimangacho asanayambe kumumenya, kuti akapeze umboni woona aaa.
    Panangolowa chidani apa. Boma likulekerera ang'ona nkumamanga abuluzi nzomvetsa chisoni amphawi tizifa chonchi nkumapita kumanda achuma nkumakodzera khoma mmmm.

  • @MatumeMkhondo
    @MatumeMkhondo หลายเดือนก่อน

    Mzimu wawo ukawuse mutendele

  • @user-yh3dw6qu7z
    @user-yh3dw6qu7z 4 หลายเดือนก่อน

    Ngati boma likumva ndikuonera video imeneyi lamulo ligwire ntchito.

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu 4 หลายเดือนก่อน

    Ndimulongosole khuluyu ulele chonde chonde

  • @HenryGulani-fq5js
    @HenryGulani-fq5js 3 หลายเดือนก่อน

    dzovetsa chitsoni ine ndili Joz muno ndikufuna number

  • @MasharPablo
    @MasharPablo 3 หลายเดือนก่อน

    Tangotipasani ganyu ife muwone. No money just give us foto

  • @MkaiFrancisBendera
    @MkaiFrancisBendera 4 หลายเดือนก่อน

    Ash zobvuta ndithu koma limbani mtima kunjaku kuli mlungu

  • @user-vl5on2lj8b
    @user-vl5on2lj8b 4 หลายเดือนก่อน

    Koma Inu mumazitcha andalama ndi ndalama zanuzo nkumasowesa anzanu ntendere chifukwa CHOTI ndiinu achuma mudziwe kuti mulibe nzeru zomposa mulungu kupha nzanu ndi nkhani yongopeka ? Minyama masoko zipite pathupi lanu

  • @patricksinyala1345
    @patricksinyala1345 4 หลายเดือนก่อน +1

    Mtolankhani anaiwala funso limodzi loti, Kodi anthuwo anakwanitsa Lupita kukafufuza mmundamo Kuti akachitile umboni oti chimangacho chinabedwadi mmundamo? Chimanga chitatu, mmundamo munayenela kuonekanso miphesi itatu yochotsedwa chimanga Mmhmmh chilungamo chioneke pankhaniyi.

    • @user-eh1mg3ww6d
      @user-eh1mg3ww6d 4 หลายเดือนก่อน

      Simunave kuti anakamucholela chimanga kuti aonjezele pa chitatucho kuti mulandu ukule ambuye azitikhululukila

    • @inessmsiyambiri8517
      @inessmsiyambiri8517 4 หลายเดือนก่อน +1

      Ndipo munthuyo komwe ankachokerako anali atanyamula chimanga kale mmm zinali zobvutatu mh

  • @joyedward45
    @joyedward45 4 หลายเดือนก่อน

    So sad Ambuye dziko lathu lija lasanduka phanga la a chifwamba ndipo mizimu ya anthu osalakwa yatsikila ndi ikutsikila kuli chete Ambuye tathedwa nzeru .Inu oweruza olungama muyimilire ndipo mugwire nthungo mumenye nkhondozi patokha sititha

  • @henryngandu2936
    @henryngandu2936 4 หลายเดือนก่อน

    Malawi has lost it this is sad development even if person steal from you have got no right to take way life

  • @giftblack7690
    @giftblack7690 4 หลายเดือนก่อน

    Anthu ngati awa sipafunikaso police kungopita kunyumbako kukawotcha chilichose komaso ine nditha kuthana nawo why amupha munthu osamufufuza bwino bwino bwanji eish

  • @user-vt4xw5px5h
    @user-vt4xw5px5h 4 หลายเดือนก่อน

    Anthu ndioyipa kwambiri maka apolice sianthu

  • @user-dn5sf3md5t
    @user-dn5sf3md5t 4 หลายเดือนก่อน

    NKHANI IYIYO SIZIMASOWEKANSO A POLICE KUNALI KUGWIRIZANA KUMUGWIRA NAYENSO KUMUPHA CHIFUKWA KUYENDERA A POLICE KU MALAWI PANO KULIBE POLICE

  • @augustMag
    @augustMag 4 หลายเดือนก่อน

    Kodi apolice aku Malawi akafika pa maso pa Mulungu? Ndikunena inuyo apolice mukugwira tchito yanji? Chifukwa chiani simukufuna kuonesa chilungamo nkhani ikachitika? Muli ndi soka anthu obisa chilungamo chifukwa cha ndalama mukungokonda ndalama kusiya chimene munalembedwera tchito yanu koma ziphupu zokhazokha Mulungu ali nanu tchito inu iwenso mwini wake munda chimanga chitatu mpaka kuchosa moyo wamuthu? Dziko uliva kuwawa ukhala onthawaw ngati abele bolanso abeleyo Chauta anamuyika chizindikiro kuti anthu asamuphe koma iweyo usafa ngati galu mtembo wako abale ako sazauna athu kuipa mtima ngati kumanda choncho akapolo aka amene amafuna kuti uwatameyo kuti akugwira tchito bwino mzimu wamunthu ameneyu alange koopsya aszaonekenso padziko pano

  • @user-mk8cn2no3o
    @user-mk8cn2no3o 4 หลายเดือนก่อน +1

    That's why aoolice Ali osauka

  • @jennygardemalm7559
    @jennygardemalm7559 4 หลายเดือนก่อน

    Ooo😢😢,Anthufe😢,pepani mamma mulungu aweluza mulandu umeneu.

  • @khatazachibambo8732
    @khatazachibambo8732 4 หลายเดือนก่อน

    Koma Volume yanu very poor

  • @GrecianWyson
    @GrecianWyson 4 หลายเดือนก่อน

    Mzimu wake uwuse mtendere.chimanga chitatu zoona mpaka kuchotsa Moyo wamuthu Inuyo amene munagwira tchito yakuphanu mukuva bwanji mutima mwanu.Chenjezo mulanduwu sunathe oweruza olungama akudikilaso kukaweluza chifukwa mzimu wake ukulila kwambili kwamulungu.mwina inu NDA muyaya

  • @mchipengule
    @mchipengule 4 หลายเดือนก่อน

    A Malawi Chikondi cha chibadwidwe chinatha zowona kupha munthu chifukwa cha chimanga chitatu? Ameneyu akaseweze ndende basi. A Police samalani ntchito yanu.

  • @PeterNkwita
    @PeterNkwita 4 หลายเดือนก่อน

    Koma anthu muli ndi sambi

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x 4 หลายเดือนก่อน

    Izi kukanakhala Kwa Bvumbwe okuphayi akanaphedwanso ndipo a police amene amakateteza Munthu okuphayi kunyumba kwake nawonso onse akanaphedwa Ndipo police ikanaotchedwa. Izi kwathu kwa Bvumbwe sitimalorayi komanso antchito atchulidwa omwe anamenya nawo abambowa kwathu tikapheratu onse

  • @NaduMbewe-zz6iw
    @NaduMbewe-zz6iw 4 หลายเดือนก่อน

    Luwis anali paudani ndi nzakeyo

  • @DanMhone-iw6xg
    @DanMhone-iw6xg 4 หลายเดือนก่อน

    Soka kwaiye amene agwesa kachisi wa mulungu pakuti azalandla chilang'o chosatha

  • @MuhammadYusufu-ri7lr
    @MuhammadYusufu-ri7lr 4 หลายเดือนก่อน

    😭😭😭😭😭 koma abare dzikori rikurowera kuti maka maka

  • @paulmakaula4937
    @paulmakaula4937 4 หลายเดือนก่อน

    Sad koma akuba chimanga akusowetsa mtendere ndiye anthu akupanga mob justice

  • @HAPPY-mf3gw
    @HAPPY-mf3gw 4 หลายเดือนก่อน

    Sad story mmmm

  • @patiencetebulo
    @patiencetebulo 4 หลายเดือนก่อน

    That is nonsense akuyenela kumangidwa koma zitukuko zomwe wasiya malemuyo amalizise komaso aseve jele zikakhala dollar ndizache

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw 4 หลายเดือนก่อน

    Amalawi khalani ndi mtima wachison bwanji mukayitanisa ndalama mmmm

  • @NumbDee
    @NumbDee 4 หลายเดือนก่อน

    Mr jere komwe muliko muvumbuluke moyo wanu uzakhala ozuzika mpaka kale

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 4 หลายเดือนก่อน

    Dziko ili likungoyenda malamula anasiya kutsatiridwa Palibe chilichonse chimene chikutsatidwa ,very sad

  • @user-mx1jv8qn4w
    @user-mx1jv8qn4w 4 หลายเดือนก่อน

    Choncho kuti abwezeleno nde adzamanga iwowo

  • @amoschilangiza
    @amoschilangiza 4 หลายเดือนก่อน

    Malawi akupita kuti? Mr Jere amangidwe

  • @user-lg2ws2ki3d
    @user-lg2ws2ki3d 4 หลายเดือนก่อน +1

    Very bad :(

  • @HashimMustafa-yj1or
    @HashimMustafa-yj1or 4 หลายเดือนก่อน

    Ndalama ikamayankhula chilungamo chimakhala chete Ambuye akuthandizireni mpaka chilungamo chioneke

  • @marynkhata9707
    @marynkhata9707 4 หลายเดือนก่อน

    Zomvetsa chisoni kwambiri munthu kuluza moyo chifukwa chachimanga chitatu pepani nonse kubanja la ofedwa

  • @rashidlamos3403
    @rashidlamos3403 4 หลายเดือนก่อน

    Pepani kwambili ofeledwa inu akulakwirani MULUNGU akuwona zonsezo

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 4 หลายเดือนก่อน

    Osawuka alibe mau zombvetsa chisoni kwambiri MHSRIP

  • @user-lj7lm6ly7z
    @user-lj7lm6ly7z 4 หลายเดือนก่อน

    Truck driver ndimunthu oti amazioezera zake sangbe chimanga chitatu

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w 4 หลายเดือนก่อน

    Jere ameneyu amangidwe basi, ndi a ntchito womwe akalongosole ku police.

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 4 หลายเดือนก่อน

    Sanamangidwe apolice anamuthawitsa

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i 4 หลายเดือนก่อน

    Zimuwake akawuse muntendele koma ajele mulape kumanga chipatala kapena police chisakhale chifukwa choti muthele mizimu ya azanu apolece nanu mumuziwe yesu mupemphele zolimba kuti mulungu azele kwa chakwela akukwezeleni malipuloanu akhale okwanila musiye chinyengo zomwe mukupangazo zothela paziko mukayakha milandu

  • @user-zo4ok7md5v
    @user-zo4ok7md5v 4 หลายเดือนก่อน

    God will punish them

  • @user-mo4tv5eu5y
    @user-mo4tv5eu5y 4 หลายเดือนก่อน

    Pachiyambi munaka nyanyala malilowo ku police then you could have get justice

  • @ritaoffen7912
    @ritaoffen7912 4 หลายเดือนก่อน

    So sad

  • @user-mx1jv8qn4w
    @user-mx1jv8qn4w 4 หลายเดือนก่อน

    Komatu kulakwa

  • @user-mk8cn2no3o
    @user-mk8cn2no3o 4 หลายเดือนก่อน

    Apolisi amangothandiza a ndalama nde kumalawi kumeneko

  • @EllenBanda-gj4zb
    @EllenBanda-gj4zb 4 หลายเดือนก่อน

    Mulungu akumenyereni nkhondo akubanja!

  • @ziyamikanmakowa5981
    @ziyamikanmakowa5981 4 หลายเดือนก่อน

    Munthuyo wandalama Ka kukapha munthu chifukwa cha chimanga chawisi ,fear God

  • @user-sb2bg3dd3k
    @user-sb2bg3dd3k 4 หลายเดือนก่อน

    Jemu ndi Louis tikukawatenga tipite nawo ku Police Akayankhe Mulandu.

    • @user-zy1br2fy6v
      @user-zy1br2fy6v 4 หลายเดือนก่อน

      Apolisi ndi ndalama za tsoka sungawalekanitse
      Anthu osamva chisoni ngati awa simnawaone mpake kuwasandutsa ma tumba amakala mxieeeeew

  • @user-lq4bc2dr2n
    @user-lq4bc2dr2n 4 หลายเดือนก่อน

    Nsambi kulakwa zandikhuza kwambiri 😢😢😢😢

  • @mariamwandwanga3035
    @mariamwandwanga3035 4 หลายเดือนก่อน

    Ambuye wakanthe a jere

  • @AliajoeAliajoe-vv1wo
    @AliajoeAliajoe-vv1wo 4 หลายเดือนก่อน

    Eish so sad guys sorry

  • @giftdulamkalenga7344
    @giftdulamkalenga7344 4 หลายเดือนก่อน

    Under namabatile chakwera wa Amonika leadership

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x 4 หลายเดือนก่อน

    Boma la Malawi sililibwino ataaah

  • @user-dg3dn5zq7w
    @user-dg3dn5zq7w 4 หลายเดือนก่อน

    Koma kulakwa mmmmmmm athu amenewa anamuphwa angwidwe basi

  • @user-wd9yd1bg9n
    @user-wd9yd1bg9n 4 หลายเดือนก่อน

    Ine mmene ndinabadwira pano ndili ndi zaka 36 koma ntchito ya a police sindikuiona mmalawi muno

  • @user-rg4du4vu9r
    @user-rg4du4vu9r 4 หลายเดือนก่อน

    Km zonvesa chisoni kwambiri moyo wamunthu sungafanane ntchimanga ayi ambuye awakanthe km

  • @patricgama4788
    @patricgama4788 4 หลายเดือนก่อน

    Dziko lathuli muli tsatama dzinayambila kwabutsa athu onama ndiye aliyetse akupangadzofuna dzake koma Mulungu alinafe

  • @gracechiumia7103
    @gracechiumia7103 4 หลายเดือนก่อน

    Palibe chobisika Mulungu awalange komwe sli

  • @AaAa-qy9id
    @AaAa-qy9id 4 หลายเดือนก่อน

    Apolsi athu ndi zitsiru za anthu chinyen go basi
    Anthuni mungomupha nanunso pitani pa sing'anga aphe wachumayo ndi apolosi onse achinyengowo analandira ndarama

  • @JamesMalango
    @JamesMalango 4 หลายเดือนก่อน

    Munthu wa ndalama kupha munthu chfkw cha chimanga chitatu bas, shame on

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 4 หลายเดือนก่อน

    Anthu akulimba mtima et eishiiii

  • @user-rh4hf3yo9t
    @user-rh4hf3yo9t 4 หลายเดือนก่อน

    Amwene nzanu akufotokoza pamene inu muyang'ana zina. Ntchito ikuvutanitu inu.

  • @user-nb7dp6pr9n
    @user-nb7dp6pr9n 4 หลายเดือนก่อน

    Very sad😡