Rev. Alexander Kambiri kulalika pa Kapaza CCAP Church Mponera Dowa

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 10 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 83

  • @felixmadyandowe3184
    @felixmadyandowe3184 10 หลายเดือนก่อน +2

    POWERFUL MESSAGE MAY GOD CONTINUE BEING WITH YOU ALL THE TIME

  • @GracePhirisakala-ml9vt
    @GracePhirisakala-ml9vt 3 หลายเดือนก่อน +1

    Powerful message amen

  • @ethelsingano650
    @ethelsingano650 2 ปีที่แล้ว +2

    Thanks for the true word of God.. We nid more pastors like u.. Who can stand n preach the true gospel of our Lord JESUS Christ.. May almighty GOD continue to use n bless u.. Yu r a blessing to us🙏🙏

  • @petermsamariamapira8933
    @petermsamariamapira8933 2 ปีที่แล้ว +1

    AMEN powerful massage ali ndi khutu Amve chimene nzimu anena

  • @FlorenceMwamkonda
    @FlorenceMwamkonda หลายเดือนก่อน

    Amen mawu achilimbikiso

  • @rashidstamburi2705
    @rashidstamburi2705 2 ปีที่แล้ว +1

    Ndine Muslim koma akuluwa amandivetsa kukoma kwambiri ndimawu wawo👏🏻

  • @letitsiachisvisva
    @letitsiachisvisva ปีที่แล้ว

    Aleluya and Amen and Amen 🙏 Kuna Mwari kudenga

  • @fredrickamosi3930
    @fredrickamosi3930 ปีที่แล้ว

    Amen pastor and thanks,let God be God

  • @user-zi8vf4mz4g
    @user-zi8vf4mz4g หลายเดือนก่อน

    Amen and Amen

  • @HenryTruwa
    @HenryTruwa 10 หลายเดือนก่อน

    powerful sms thnx 🙏 from north west klerksdorp

  • @user-vp2lb7wz6w
    @user-vp2lb7wz6w 4 หลายเดือนก่อน

    Amenii abusa

  • @stellahmangani4880
    @stellahmangani4880 ปีที่แล้ว

    Amen

  • @user-ce2qd6zs4r
    @user-ce2qd6zs4r 7 หลายเดือนก่อน

    Inu amene uthenga wa abusa a kambri umakuipilani musataye nthawi kuverera ife tiziverera tilipo

  • @malawitunes97
    @malawitunes97 2 ปีที่แล้ว

    🚨🚨 PHILL J - ZAKOMA
    PRODUCED BY MAGULU
    DOWNLOAD NOW ⚡🔥: malawitunes.com/track/BtKYGgtLuqZJ2AB
    GET THE BEST OF URBAN MALAWIAN MUSIC ON www.malawitunes.com TODAY!

  • @HerbertMazengera-pz2jx
    @HerbertMazengera-pz2jx ปีที่แล้ว

    Ali ndi makutu akumva wamva. Osamva ndi osamva basi. Amen

  • @JohnGama-pj3mn
    @JohnGama-pj3mn 11 หลายเดือนก่อน

    Unthenga waveka bwino kwambiri, Amen pastor

  • @alfredandrea6039
    @alfredandrea6039 2 ปีที่แล้ว

    Powerful my pastor though ndamvera mochedwa 👏👏

  • @MildredMwanza-dw4zi
    @MildredMwanza-dw4zi 7 หลายเดือนก่อน

    Amen and amen point and powerful 🙏🙏🙏🔥🔥🔥

  • @user-er8pf1wo4q
    @user-er8pf1wo4q 6 หลายเดือนก่อน

  • @user-er8pf1wo4q
    @user-er8pf1wo4q 6 หลายเดือนก่อน

    Powerful massage

  • @noriachirwa3709
    @noriachirwa3709 2 ปีที่แล้ว

    Amen abusa olalika chilungamo ngati awa palibeso

  • @moisesmatoladjefule3412
    @moisesmatoladjefule3412 2 ปีที่แล้ว

    Mumandidalitsa pastor ambuye akudalitseni

  • @blacksonkoloneriyo7661
    @blacksonkoloneriyo7661 ปีที่แล้ว

    Very powerful message

  • @westerbolloma2241
    @westerbolloma2241 2 ปีที่แล้ว

    Amen PS Alexander
    Kambri, chifukwa cha mtima wa nsanje, powerful

  • @user-po2yk3hf1i
    @user-po2yk3hf1i ปีที่แล้ว

    Mumandisuntha kwambiri

  • @modesterkalinga7174
    @modesterkalinga7174 9 หลายเดือนก่อน

    Am blessed

  • @user-kb6mu3is3e
    @user-kb6mu3is3e ปีที่แล้ว

    Koma mumandimasula mu zambili abusa olalika chilungamo🙏🙏

  • @user-rg4du4vu9r
    @user-rg4du4vu9r 5 หลายเดือนก่อน

    That's true man of god lm bresd here in cape town

  • @lindabalakasi9921
    @lindabalakasi9921 2 ปีที่แล้ว

    Abusa awa palibesoi amalalika chilungamo 🙏🙏🙏

  • @user-qu5wp2wo7i
    @user-qu5wp2wo7i 6 หลายเดือนก่อน

    Uthenga wabwino kwambiri

  • @piliranikabango6563
    @piliranikabango6563 ปีที่แล้ว

    Powerful message

  • @user-ce2qd6zs4r
    @user-ce2qd6zs4r 7 หลายเดือนก่อน

    Chilungamo sashatila abusawa akutivetsa kukoma

  • @RomansKahiya
    @RomansKahiya 3 หลายเดือนก่อน

    Watching you live from here at jcc, RSA,
    One month ago here at website launch,,
    May God keep blessing you.

  • @user-mn6hu6vy9t
    @user-mn6hu6vy9t ปีที่แล้ว

    Powerful

  • @HawardChipula
    @HawardChipula ปีที่แล้ว

    Kumva kukoma pastor ndi ulaliki wanu

  • @sisiliangulube4132
    @sisiliangulube4132 2 ปีที่แล้ว

    Amen amen abusa

  • @isaacfesani2357
    @isaacfesani2357 2 ปีที่แล้ว

    Kkkk, this is my brother wow

  • @fenordmachaka1736
    @fenordmachaka1736 ปีที่แล้ว

    Zachabe chabe ndipo zonsezi nzachabe

  • @emmanuelmakwati6915
    @emmanuelmakwati6915 2 ปีที่แล้ว

    Amen 🙏

  • @gibsonzunda6512
    @gibsonzunda6512 2 ปีที่แล้ว

    Uthenga wabwino kwambiri. Kumalalikila zachilungamo Mulungu amasangalala. azitumiki ambiri ndiofuna kuziunjikila chuma sapembeza Mulungu mwini dziko lapansi ndikumwamba.

    • @jamsonmushani3324
      @jamsonmushani3324 ปีที่แล้ว

      Your preaching is touching me more in my heart

  • @vascosaidi729
    @vascosaidi729 2 ปีที่แล้ว

    Mqaphunzitsa moyo wanga, ndasiya nsanje ineeeè

  • @patrickbanda8047
    @patrickbanda8047 2 ปีที่แล้ว

    🙏

  • @mikemwamudu9438
    @mikemwamudu9438 2 ปีที่แล้ว

    AMEN

  • @bravechinkhuntha3850
    @bravechinkhuntha3850 ปีที่แล้ว

    Abusa mumakwana ndipo uthenga wanu umatiphunzitsa zambiri

  • @mtongacephas2661
    @mtongacephas2661 ปีที่แล้ว

    Gud news

  • @yusucukangwanda2715
    @yusucukangwanda2715 2 ปีที่แล้ว

    Mbambande

  • @johnmvula9544
    @johnmvula9544 2 ปีที่แล้ว

    Mlaka malilo

  • @kondwaniharawa7684
    @kondwaniharawa7684 2 ปีที่แล้ว

    Kungokhalira kuzuzula pena muziphunzisa osamakhalira kuzuzula.

    • @twinktv6350
      @twinktv6350  2 ปีที่แล้ว +4

      Nkutheka kuti mwina inuyo mumanvera ulalikiwu muli kale ndi mbali yomwe mudasankha, ndiye mumangonva koma osanvetsetsa, kudzudzulana zikamalakwika nkofunika ndithu.

    • @veramphande7856
      @veramphande7856 2 ปีที่แล้ว

      @@twinktv6350 anthu akudana ndichilungamo ame

  • @alexanderkaunda9554
    @alexanderkaunda9554 2 ปีที่แล้ว

    This is my brother 😂😂

  • @Alex-cy3dz
    @Alex-cy3dz 2 ปีที่แล้ว

    Praise lord

  • @kondwaniharawa7684
    @kondwaniharawa7684 2 ปีที่แล้ว

    Pena umazalalikila mumisonkhano ya ndare munthu wa mulungu ndi ndale zikukumana pati

    • @twinktv6350
      @twinktv6350  2 ปีที่แล้ว +2

      Poyamba mudziwe kuti ngati mukuti pa misonkhano ndekuti pamalopo pamasonkhana anthu nde mudziwenso kuti tikachotsapo ndalezo anthuwo ndi ake ndithu a Mulungu, pamenepo mpamene zimakumana, choncho ndale si cholepheletsa kuti anthu asalalikidwe. Nchifukwa chake olo pamaliro pamalalikidwa ndithu ngakhale wena akulira pomwepo kufuna kukumbutsana kuchita chifuniro cha Mulungu.

  • @kondwaniharawa7684
    @kondwaniharawa7684 2 ปีที่แล้ว

    Koma lilipo siku limene muzaphunzisapo anthu za Yehova kuti amuziwe? Kungokhalira kunyoza anthu ndikumapempherera anthu zoipa zokha zokha. Ndikukayika ngati mbusa iwe unapitako ku bible koleji. Zimene umalalikila sizikuveka olo pang'ono.

    • @rayyaancarriem1994
      @rayyaancarriem1994 2 ปีที่แล้ว +1

      Each and everyone has got his or her own calling ... Ngati iweyo calling yako ndiimeneyo yoona zofooka zaanthu amulungu ... Mulungu akukhulukileni ndikukubweletsalani anthu amulungu onga awa Oti akuzuzuleni

    • @twinktv6350
      @twinktv6350  2 ปีที่แล้ว

      Sitikhalira kunyoza anthu ayi, munthu ukakhala kuti sukunvetsetsa umaona ndi mmene iweyo ukuganizira, vuto limeneri inuyo mulinalo. Kupemphelera anthu zoipa zokha zokha nde kofunika zedi cholinga choti asiye zoipazo azichita zabwino. Nanga kodi tingamapemphelerane kuti tisiye kuchita zabwino?, ayi ndithu, pakufunika kuti muthandizidwe ndithu mwapaderadera, chifukwa ngati mukuti simukunva chilichonse kuyambira kuwelenga Bible mpaka kumaliza ulaliki ndekuti pali vuto.

    • @Kuwacha6075
      @Kuwacha6075 2 ปีที่แล้ว +1

      Uyu munthu mubusa wakuyooya makola chomene and wakuyooya nkhana makola chomene, wakuyooya kose kose, not only shouting, wakuyooya naumo wawelengela mutu wa bible, am very happy with him, Pitilizani abusa osasiya osavela za anthu , And uyu kubusa nimunthu muwemi coz iye wakulalikila kumuzi not ivi wakupanga ma busa yanyake yanchuka aya chaa waka ma million mphaa vabweka utesi wekha , kwe uyu wakuyooya nkhana exactly umo chalo chilili pasono, wakuyenela kupephela nthena indeed, iye walinavo nachito vakutauni yyso or kuyenda malo uku na uko pitilizani basi iyaa , happy for you 😄

    • @alltruth881
      @alltruth881 2 ปีที่แล้ว

      Kondwani Harawa I agree kwambiri. The reason why this world is finished is evident in such type of sermons. People prefer this preaching to tickle their ears. It’s mostly moralism and jokes. Sadly, most people think they are being fed spiritually. No wonder millions are headed for hell.
      The truth is supposed to pierce one’s heart not be anticipating laughter. The reason why this guy is trending is because he makes people laugh. Not that people are getting saved or knowing the truth.
      Ecclesiastes 7:4
      The heart of the wise is in the house of mourning, but the heart of the fools is in the house of mirth.

    • @veramphande7856
      @veramphande7856 2 ปีที่แล้ว

      @@Kuwacha6075 me too l'm happy to him

  • @MontfortChinga
    @MontfortChinga 10 หลายเดือนก่อน

    Amen

  • @YassinMackishon
    @YassinMackishon 8 หลายเดือนก่อน

    Amen powerful message

  • @georgechimaliro9908
    @georgechimaliro9908 2 ปีที่แล้ว

    Amen n amen

  • @williamsadunola3177
    @williamsadunola3177 ปีที่แล้ว

    Powerful

  • @chisomchiwoko2327
    @chisomchiwoko2327 2 ปีที่แล้ว

    Amen and Amen

  • @Patricknyirenda-gh2gc
    @Patricknyirenda-gh2gc 8 หลายเดือนก่อน

    Amen

  • @SimeonMtambo
    @SimeonMtambo 10 หลายเดือนก่อน

    Amen

  • @SalayekhaHewsi
    @SalayekhaHewsi 4 หลายเดือนก่อน

    Amen

  • @carinmartens2207
    @carinmartens2207 3 หลายเดือนก่อน

    Amen

  • @christopherchirombo
    @christopherchirombo ปีที่แล้ว

    Amen

  • @magretphiri7703
    @magretphiri7703 ปีที่แล้ว

    Amen

  • @samuelpedrorabissonerabiss9745
    @samuelpedrorabissonerabiss9745 ปีที่แล้ว

    Amen

  • @idrisphiri6114
    @idrisphiri6114 2 ปีที่แล้ว +1

    Amen and amen

  • @user-uo1xp7em8o
    @user-uo1xp7em8o ปีที่แล้ว

    Powerful

  • @elisalegman8406
    @elisalegman8406 2 ปีที่แล้ว

    Amen

  • @edithmughogho2011
    @edithmughogho2011 2 ปีที่แล้ว

    Amen