Chitsiru chili ndi mwini Born Kalindo ali ndi anthu omwe amamuyamikila pa zomwe amachita kotelo ngati Chakwera ndi anthu ake angapange mistake yomuponya mundende Kalindo kwa ka nthawi, Malawi anunkha utsi komanso magazi. Ma galimoto ena tiziwawotchela mma parking mwawo pomwe nyumba zina ziziphya kuzela mu mphanvu yocholuka ya magesi a masenga omwe tizikonza tokha. Ndipo yemwe ayesele ku pitilira ndi plan ofuna kupha Born Kalindo, timukonzera ngozi ya mmadzi chingakhalenso ya panseu kudzera mu pemphero lathu la 00:00 monga ife achi slamu.
Apolicewa bwanji tizingoponda tokha guys kumalawi kulibe police kuli mcp security machende abambo wao chakwera
100%
Aaa alibe zochita apolice awa zaziii, kalindo ndi dolo ndipo GOD is always with you be strong brother
Ine ndifunseko Inu abon kalindo chimene mukupondulapa nichani pamenepa, komaso ma audio Anu amene mumatulutsa aMalawi amapindulapo chani akamawavera, Kodi simungayambe kutumikira mulungu monga amachitira mtumiki twaibu yemwe anali mkunja kwazaka zambiri ,koma pano akupulumutsa miyoyo yaanthu kupereka chiyembekezo kuwanthu , mumudziwe yesu lero ,yambani kutumikira mulungu noti kulimbana ndizadziko nzachabechabe kulibe chimene muzapindulapo.
Ulibe nkhani zoba iweeee
Utumiki sufana
Nkhani zabodza, mawu ngatiwathimbidwa ndi mbatata pakhosi. Za ziiii
Mbuzi zawanthu a police akumalawi
Ku Malawi mmmmmmm mm tiyeni nazoni tionenso mu Holy Bible. THE MOST IMPORTANT COMMANDMENT
apolisi zigwilani ntchito yabwino osati kumamvera BOMA pa nkhani ya abon kalindo chifukwa chimene mungadziwe ndi chakuti bon kalindo sakulakwitsa ayi komanso sanaphe munthu ayi ndi ufulu wake kuyankhulira amalawi ndiye BOMA LA mcp musalimbane ndi kalindo ,mulimbana ndi anthu omwe akuba ndalama zaboma bwanji simukuwamanga ,
M"malo molimbana ndi mavuto a njala, ma passport, driving licence, katangale muli busy kulimbana ndi Kalindo MCP imeneyo
Tapitani mukayambitse church mulungu akulankhuleni mwapadera isanafike poipa misala
Aboma ndizisuru makhoti anawo akwendera Chakwera mwina titi anagulidwa ndi Chakwera
Chitsiru chili ndi mwini
Born Kalindo ali ndi anthu omwe amamuyamikila pa zomwe amachita kotelo ngati Chakwera ndi anthu ake angapange mistake yomuponya mundende Kalindo kwa ka nthawi, Malawi anunkha utsi komanso magazi.
Ma galimoto ena tiziwawotchela mma parking mwawo pomwe nyumba zina ziziphya kuzela mu mphanvu yocholuka ya magesi a masenga omwe tizikonza tokha. Ndipo yemwe ayesele ku pitilira ndi plan ofuna kupha Born Kalindo, timukonzera ngozi ya mmadzi chingakhalenso ya panseu kudzera mu pemphero lathu la 00:00 monga ife achi slamu.
aaaah zopusa et
Palibe chomumangila born kalindo.nkhanza timangomva kut mcp inali nazo tisanabadwe.koma pano tikuziwona nafenso ndimaso athu.kodi ma audio akut chani?akungoti audio koma osanena audio yakeyo ndali zanji izi?
Ponena bon kalindo aziti ndimamenyera ufulu Amalawi ena, not kungonena kt Amalawi chifukwa enafe sitiona chanzeru mwa iye
Achisulu inu
Nkhan ya mfut yo ndyaboza coz yatenga thaw yaytalikomaso munga ngat alind mfut opanda chilolezo bwanj samawamanga
Khani yaboza ya mfuti yo iyaaa
Iwe sumandiwelengela bwino nkhani msaname!, aaaaaa.
😂😂😂komaaa
Mcp nkhaza
Chekwala ndiwaphwala
Chakwera mabatile ake ndithu
Ndale bc tidzigomenya apolice bc asamatipatse busy
tingo mupemphelela atuluke basi mcp siboma koma satanic bas
mcp ndiapolice zisilu