'AMANDIYAMWISA MALISECHE DAILY '- MMWENYE AWUZA WA NTCHITO ADZIMUYAMWA MALISECHE

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 10 ก.ย. 2024
  • MMWENYE AWUMIRIZA WA NTCHITO KUTI AZIMUSEWERETSA MALISECHE
    Kupeza ntchito ndi chinthu chokoma kwambiri kwa munthu aliyense makamaka uyo amene wakhala nthawi yayitali akuyisakasaka ndipo ali ndi anthu amene amadalira iyeyo monga makolo, ana komanso mkazi. Pamene munthu wapeza ntchito ndiye kuti amakhala ali ndi chiyembekezo chachikulu kuti zinthu zake zisintha ndipo amene amamudalirawa ayamba nawo kukondwa. Komatu zimenezi sizili motero kwa mkulu wina wochokera mu mzinda wa Lilongwe. Mkuluyu amene dzina lake sitilitchula anapeza ntchito yophika kwa mmwenye wina a Jayesh Kumar Dalwad amene anali wothandizira ntchito za mkulu wa kampani ya Shayona Cement Corporation ku Kanengo analibe malingaliro akuti chimwemwe chake chakuti wapeza ntchito chitha posachedwa ndikuyamba kukhala moyo wa mavuto.
    Atakhala kwa nthawi yayitali asanapeze ntchito, mkuluyu amene amakhala kwa Mtsiriza mu mzindawu anali akukanika kusamalira ana ake atatu, koma mu mwezi wa January 2023, iye anapeza ntchito ngati wophika ku nyumba ya bwanayu imene ili ku malo amene kuli ma office a kampani ya Shayona yi ku Kanengo. Atangogwira ntchitoyo kwa mwezi umodzi, mwezi wotsatira wake umene ndi wa February zinthu zinayamba kusintha ndipo akuti abwana ake aja anayamba kumamawuza kuti adziwasisita bondo lawo.

ความคิดเห็น • 54

  • @user-ey6in8is5h
    @user-ey6in8is5h 3 หลายเดือนก่อน +7

    Mumabweretsa nkhani zofunikira koma musinthe speed yamalankhulidwee

    • @sharodynicier001
      @sharodynicier001 3 หลายเดือนก่อน

      Ndipodi ife kuti tinve bwino bwino palitu ntchito 😂😂😂🤣🤗🤗

    • @AleksaWilliams-qc6cn
      @AleksaWilliams-qc6cn 3 หลายเดือนก่อน

      Mwina ndi manyado,ineso sizimandiwaza

    • @PiscaDicksoni
      @PiscaDicksoni 2 หลายเดือนก่อน

      Ndipo ndie zimanyasa

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj 3 หลายเดือนก่อน +5

    Umphawiwo wakula bwanji mpaka kuvomeleza zimenezo bwanji osawulura kapena kusiyana ntchitoyo kuyamba zochita zina

  • @MelissaMondey
    @MelissaMondey 3 หลายเดือนก่อน +2

    It's bad!!!😢😢😢 plz amalawi munthu ameneyo amangidwe

  • @ChifundoNinje
    @ChifundoNinje 3 หลายเดือนก่อน +3

    Muthu kwanu ndimulolela kupanga zimenezo zaziii zauchisili ngati zimenezo

  • @IsaacMwale-hu9kg
    @IsaacMwale-hu9kg 2 หลายเดือนก่อน +1

    God have mercy on us

  • @mercynamangale98
    @mercynamangale98 2 หลายเดือนก่อน +1

    Aaaaaa zauchitsiru basi,amangidwe ameneyo basi

  • @IdiWilliam-uo8tw
    @IdiWilliam-uo8tw 3 หลายเดือนก่อน +4

    Koma ndikhani iyiyi boma lamalawi limayenera kumuitanitsa mwenye ameneyu kuonetsa kukwiya nazo

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x 3 หลายเดือนก่อน

      Boma lake litiro brother???😂😂😂😂😂

  • @e.r.mchanel1460
    @e.r.mchanel1460 3 หลายเดือนก่อน +2

    Eishhhhhh zosayenda bwanji

  • @user-lf6qf2tw5o
    @user-lf6qf2tw5o 3 หลายเดือนก่อน +3

    Km guys kwathu komwe tizilandila nkhanza zoterez amalawi ena kumavomeleza km mmm 😢

  • @user-xe3xo5mu9k
    @user-xe3xo5mu9k 3 หลายเดือนก่อน +1

    Aaaa zanchamba bass
    Iyeyoso anagwirizana nazo bwanjibosangosiya nchitoyo bwanji nonse machende anu 😂😂😂😂😂😂😂

  • @HellenGondwe-d1g
    @HellenGondwe-d1g 2 หลายเดือนก่อน +1

    Mpaka Chaka kumalorera zimenezo mavuto ake amtundu wanji

  • @giftblack7690
    @giftblack7690 3 หลายเดือนก่อน +2

    Hahahaha ine olo zitavuta maka sindingapange zauve ngati zimenezo

  • @CollinSepamatla-xk2lw
    @CollinSepamatla-xk2lw 2 หลายเดือนก่อน +1

    Mchitsilunso bwanji ameneyo

  • @AndyGama-m3u
    @AndyGama-m3u 2 หลายเดือนก่อน

    Ayi wachitola chikwama
    Nanga ma million onsewo pajatu ndalama zilimunyasi

  • @ElediaChingoma
    @ElediaChingoma 2 หลายเดือนก่อน +1

    Eshiiii

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 2 หลายเดือนก่อน

    ,,,😂😂mzimaiyo akunama amafunanso nae amagwilidzana naeso akufuna chipepetso eti 😂😂😂😂🤸🤸🤸🤸🤸

  • @EmmanuelMoyo-hy5ni
    @EmmanuelMoyo-hy5ni 3 หลายเดือนก่อน +3

    Umphawi ndi mavuto

  • @user-ln3zx6wo4w
    @user-ln3zx6wo4w 3 หลายเดือนก่อน

    Amangidwe mwenyeyu

  • @bdbigdream9015
    @bdbigdream9015 หลายเดือนก่อน

    Amalawi akaona nkhungu lofiira eish

  • @AlfredNazombe-me2ly
    @AlfredNazombe-me2ly 3 หลายเดือนก่อน +1

    Osamuluma nchilawakewo bwanji kkkkk ndikuluma maphwala akewo bs yesyes kkkk

  • @twavysibale4751
    @twavysibale4751 3 หลายเดือนก่อน

    We shouldn't Allow this in Malawi, that's not acceptable here,..

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x 3 หลายเดือนก่อน

    Osaiwala kuti Chakwera ndi chilima nawonso ndiodanatu ndi chilungamo ndie izi zangoyenera kumachitika basi

  • @StellahChikupira
    @StellahChikupira 2 หลายเดือนก่อน

    Kulakwa 😢

  • @PetroJack
    @PetroJack 3 หลายเดือนก่อน

    Sad

  • @mercybwanali-qe3dv
    @mercybwanali-qe3dv 3 หลายเดือนก่อน

    Nseu wamangochi wu zikukhala bwanji?

  • @FloridaOssy19
    @FloridaOssy19 3 หลายเดือนก่อน

    Mmmmmm 😢😢😢😢

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x 3 หลายเดือนก่อน

    Boma la Tonse Alliance ndilodana ndi chilungamo nalo ndie atha kukamumanganso bambo olakwilidwayi poti

  • @UmariBakari
    @UmariBakari 3 หลายเดือนก่อน

    Channel ichi ndichonama

  • @RobertKwazizira
    @RobertKwazizira 3 หลายเดือนก่อน

    Umfiti amabungwe loweleranipo chilungamo chichidwe basi

  • @WillmotChiuimia-vr6ou
    @WillmotChiuimia-vr6ou หลายเดือนก่อน

    Zopusa

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 3 หลายเดือนก่อน

    Umphawi szinthu

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 3 หลายเดือนก่อน

    Mmmmmm koma abale zina ukambva yohhh kukhwima kapena?

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 2 หลายเดือนก่อน

    Kupusa bwanji samakadandaula ku ma bungwe ndi opepera

  • @charityamos2183
    @charityamos2183 3 หลายเดือนก่อน

    Uchisiru bas

  • @user-xx4jb9se3z
    @user-xx4jb9se3z 3 หลายเดือนก่อน

    Munthu ukuvutika kut ukufuna ntchito umapanga chitheka so I don't blame him ndipo iyeyo amkafuna kusamala ntchito komanso amkakukumbikila mavuto akwao koma munthuyi adangokhala oipa basi

  • @lonnythom
    @lonnythom 3 หลายเดือนก่อน

    Koma amwenye sazatheka 😢

  • @MilacleSankhani
    @MilacleSankhani 3 หลายเดือนก่อน

    Km ndye bola andicose ntcito

  • @ErnestAllex
    @ErnestAllex 2 หลายเดือนก่อน

    Chitsiru ndiiyeyo vuto longochoka koweta ng'ombe 😒😒

  • @mercybwanali-qe3dv
    @mercybwanali-qe3dv 3 หลายเดือนก่อน

    Chanma lindimo umo😂

  • @augustMag
    @augustMag 3 หลายเดือนก่อน

    Bad news 🤔🤔🤔🤔

  • @FrankMkwala
    @FrankMkwala 3 หลายเดือนก่อน

    Why Malawian we allow such pple

  • @FatimaRehemah-gi4mp
    @FatimaRehemah-gi4mp 2 หลายเดือนก่อน

    ma gay achimwenye🤨🤨🤨

  • @juniortsegula3847
    @juniortsegula3847 3 หลายเดือนก่อน

    Asaaaa 😂😂

  • @janemsiska3345
    @janemsiska3345 3 หลายเดือนก่อน

    Zovuta aaa

  • @GidionJonas-sr4zr
    @GidionJonas-sr4zr 3 หลายเดือนก่อน

    Iiiiii shaaaaa!!!

  • @alickkachepa3801
    @alickkachepa3801 2 หลายเดือนก่อน

    Mmmmmmm zotsayenda

  • @clementMuyafula
    @clementMuyafula 2 หลายเดือนก่อน

    Amabungwe kuno changu