mwaswela bwanji achimwene wanga pa program ya nkhanga zaona amutanyuwa ndi enanso amene amamvesela pa program ya nkhanga zaona pempo yanga asakwiye mulungu azamasula zonse. ezafika nthawi
Aaaaaaa iwe umakhala msika wake UTI? Msika wa Lilongwe unatamba kupsa ku gate yaku mtunda ku nsomba ndiwe iwe ukuti chani umakala kuti iwe usatpsenso myima pano
Comrade mtanyiwa sopanooo kkkkkkkk, ndigaileko ulbum ya nyimbo zomwe ukuponya pa limpopo fm' zi please, zimandidalisa kwambiri. Makamaka iyi yoti ACHAKWELA UFUMU WANU AKUBWERA AMEKI AZAUTENGE, just give de full ulbum please
Osatopa chonde . Mulungu akudaliseni nooooonse
Powerful words
Anisha moosa Pretoria ludiam 😂😂😂
Mwaswela bwanji abale anzanga apa pa nkhanga zaona ,Kodi nkhanga ziipo ?papita masiku sizikumveka ,kapena Zina gwidwa pakhosi kkkkkkk
mwaswela bwanji achimwene wanga pa program ya nkhanga zaona amutanyuwa ndi enanso amene amamvesela pa program ya nkhanga zaona pempo yanga asakwiye mulungu azamasula zonse. ezafika nthawi
Moni nooonse a human rights group
tikukala mofinyika tikukala munga ndife akaydi
Osatopa Comrade MTANYIWA will stand up until to the end.
Mcp apa ili pamatenda akulu ndipo akudziwa kuti there days are numbered
Ntanyiwa more fire
Anisha moosa Pretoria l west
Ise kwinthu kuno za uchisilu sitikufuna chakwera achoke basi ngati sakuchoka timuwombera
Apolice wakwathu kuzolowera kunyera matumba mwalo mongwira tchinto komwe munalembendwa..pano mukunkhalila kupepha yambonya. Akakupasani inu zongo paseu kundikira kti atulukira kti . AChina munulo .. ndy azawo ndy lelo mwaona ziiii mwasowa osetela Poona kti born kalindo palimbe mwankhaula mwamva mawa poteniso kulipiran mupedza ya tea ..mawatso mupite ikamati 30:08 kunkhala mutafika kti moyo watsiku ndi tsiku ukukomereni inuyo mwamva ndikukutumani ine tsopano boss lady zakupedzani komweko olo dzuwa libandule...imani popo zabwerese ya mkaka kunyumba mayi akalandire mawa banja kti liyende bwino ndakuuzani tsinanga tchinto yongwire kulimbe ine ndy ndakupatsani imeneyo .
Kuno ku Zambia nimakonda kumvela nkhanga zaona ndi nkhani zam maboma
Chilima ad Chakwel agul onseo tikundinkil atupele muluz ife come duz atupel
Anthu kumangophedwa kuberedwa koma chakwera kungoti ziiii tiziti akutuma ndindani kuti zizichitika zotere akutuma ndi chakwera
Nyimbozi nduzifuna ndingazipeze bwanji
MCP mbiri yake ndi yakupha basi nde zomwe mukunenazi ndizoona ndithu
Sondinamuonepo president Kuyenda pansewu osayimisidwa pansewu kuti apasidwe moni koma kuwowozedwa chisiru 😂😂😂😂😂
Nkhanga zaona
Nsika wapsawo nde UTI ine ndiwamunsika momwemo,I do follow u koma izi mwanamatu a ntanyiwa
Aaaaaaa iwe umakhala msika wake UTI?
Msika wa Lilongwe unatamba kupsa ku gate yaku mtunda ku nsomba ndiwe iwe ukuti chani umakala kuti iwe usatpsenso myima pano
Comrade mtanyiwa sopanooo kkkkkkkk, ndigaileko ulbum ya nyimbo zomwe ukuponya pa limpopo fm' zi please, zimandidalisa kwambiri.
Makamaka iyi yoti ACHAKWELA UFUMU WANU AKUBWERA AMEKI AZAUTENGE, just give de full ulbum please
Pitani ku you tube muipeza muipeza brother
Olo atapasidwa mfuti zokwana 10 malatayo, wapolice komanso wa army amaphedwa mfuti ilimmanja ena ilimuchiuno
Gule ndipa ground asogoleri muzanyowa
Achimwene mumani kwana
Koma hule ameneyu patricia eeeee wandichimwitsa ponganiza
🎉🎉🎉🎉🎉
Bwanji muzitiuzako zomwe muzatichitile mukazatengaboma?
This is the person full of lies. Mabodza too much pa limpopo fm.
Nkhanga zaona
Nkhanga zaona