MA BISHOP NDI OKHUMUDWA..FATHER ELIZEO NTHALIKA

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 28 ก.พ. 2024

ความคิดเห็น • 34

  • @ManifoldPhiri
    @ManifoldPhiri 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Koma uthenga umenewu wakutumani ndani?
    Chifukwa uwu siwochokera kwa mulungu!!

  • @user-qq1uj7ct6n
    @user-qq1uj7ct6n 4 หลายเดือนก่อน

    Amen father.
    Mulungu aike dzanja lake pa dziko lathu.

  • @martinsailesi1731
    @martinsailesi1731 3 วันที่ผ่านมา

    Kopepesa koyenera anthu kupita ndikukapepesa ndi kunsipe komanso kumabanja ena. There is no business kuti ma Episcope sakuyenera ndikulora komwe kupita ku state house. People should not get money through the death of chilima and other people.

  • @user-ct9dx7mw9o
    @user-ct9dx7mw9o วันที่ผ่านมา

    Amen father

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 5 วันที่ผ่านมา

    There is Lack of Philanthropy and Patriotism in political and even in religious gatherings.REASON? Leaders' cupidity.

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 3 วันที่ผ่านมา

    Amen father🙏

  • @user-db7yn2lk1u
    @user-db7yn2lk1u 4 หลายเดือนก่อน

    Amen 🙏🙏 father mthalika alapedi anthu amenewa aziwe chowonadi

  • @user-hq2io8nk7s
    @user-hq2io8nk7s 4 หลายเดือนก่อน

    Zikomo kwambiri mabishop chifukwa zinthu zikamasiya Kuyenda bwino mumaunikira ndipo pitilizani. Dzikoli ladzadza ndizosangalatsa Mulungu.Ziphuphu zachuluka.Anthu ambiri akungosaukirasaukira ndipo ochepa akudyelera chifukwa chammene dzikoli likuyendera.

  • @evelynmakhaya2756
    @evelynmakhaya2756 4 หลายเดือนก่อน

    Amen father, powerful msg

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 4 หลายเดือนก่อน

    Mulungu atikhululikile ndikutipulumutsa ndithu ❤❤ amen 🙏🙏💪

  • @GeraldDicada-ug1eu
    @GeraldDicada-ug1eu 4 หลายเดือนก่อน

    Amen 🙏 father God bless you all the time

  • @user-pl8kw3dc9d
    @user-pl8kw3dc9d 6 วันที่ผ่านมา

    Azibusa osavutika kumpempherera chakwera azakumangani

  • @LekelenFab
    @LekelenFab 4 วันที่ผ่านมา

    Amen❤

  • @KelvinKalambo-uz9ex
    @KelvinKalambo-uz9ex 4 หลายเดือนก่อน

    Amen father Tinasowa uthenga wanu

  • @paulbanda9638
    @paulbanda9638 6 วันที่ผ่านมา

    MCP yayambaso nkhondo ija ya 1992 ndi ma bishop,

  • @user-wx1jt5fd2j
    @user-wx1jt5fd2j 4 หลายเดือนก่อน

    Mawu mulungu sazapita pachabe ku aheberi amanena kuti mkoopsya kugwa mzanja la mulungu wa moyo aprezident segulani kutu la kuweluzika

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x 4 หลายเดือนก่อน

    Amen amen father🛐

  • @user-cd4df3vg4y
    @user-cd4df3vg4y 4 หลายเดือนก่อน

    Amen Father

  • @clintonhodda9830
    @clintonhodda9830 4 หลายเดือนก่อน

    Amen father Mtalika

  • @JohnChinangwa-r2g
    @JohnChinangwa-r2g 6 วันที่ผ่านมา

    amen farther

  • @user-hk9gq7fb3j
    @user-hk9gq7fb3j 8 วันที่ผ่านมา +1

    Amen

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 6 วันที่ผ่านมา

    Tangoyambisani chipani musatinyasepo

  • @AhmadumkomaTambala-lr9gp
    @AhmadumkomaTambala-lr9gp 4 หลายเดือนก่อน

    Emen emen

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r 4 หลายเดือนก่อน

    Komaso lalikilani uthenga wachipulumtso siuthenga umene anamutumani ayi phepani

  • @AmusedDimSum-hd5yp
    @AmusedDimSum-hd5yp 4 หลายเดือนก่อน

    Inu ndiosokoneza acatholic mukhumudwa zeni zeni osangoyambisa chipani chanu bwanji

  • @MosesChifuniro-or7os
    @MosesChifuniro-or7os 4 หลายเดือนก่อน

    🙏👋😭

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 6 วันที่ผ่านมา

    awa ndimlomwe asaname apa akuona ngati boma lidzabwelelaso Kwawo akunama zazii

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r 4 หลายเดือนก่อน

    Mwaiwala mayitanidwe anu mwalowa ndale mulungu akuyendelen mabishop simulungu mulungu amene ine ndikumziwa siinu ayi

  • @user-fv8ey8hx6w
    @user-fv8ey8hx6w 4 หลายเดือนก่อน

    Amen father

  • @user-xv3nr5kj2u
    @user-xv3nr5kj2u หลายเดือนก่อน

    Amen❤

  • @lucianojames7555
    @lucianojames7555 4 หลายเดือนก่อน

    Amen

  • @ChristopherJailos-gq2cu
    @ChristopherJailos-gq2cu 4 หลายเดือนก่อน

    Amen Father

  • @user-vu9rt8gj3o
    @user-vu9rt8gj3o 4 หลายเดือนก่อน

    Amen