ขนาดวิดีโอ: 1280 X 720853 X 480640 X 360
แสดงแผงควบคุมโปรแกรมเล่น
เล่นอัตโนมัติ
เล่นใหม่
Koma uthenga umenewu wakutumani ndani?Chifukwa uwu siwochokera kwa mulungu!!
Amen father.Mulungu aike dzanja lake pa dziko lathu.
Kopepesa koyenera anthu kupita ndikukapepesa ndi kunsipe komanso kumabanja ena. There is no business kuti ma Episcope sakuyenera ndikulora komwe kupita ku state house. People should not get money through the death of chilima and other people.
Amen father
There is Lack of Philanthropy and Patriotism in political and even in religious gatherings.REASON? Leaders' cupidity.
Amen father🙏
Amen 🙏🙏 father mthalika alapedi anthu amenewa aziwe chowonadi
Zikomo kwambiri mabishop chifukwa zinthu zikamasiya Kuyenda bwino mumaunikira ndipo pitilizani. Dzikoli ladzadza ndizosangalatsa Mulungu.Ziphuphu zachuluka.Anthu ambiri akungosaukirasaukira ndipo ochepa akudyelera chifukwa chammene dzikoli likuyendera.
Amen father, powerful msg
Mulungu atikhululikile ndikutipulumutsa ndithu ❤❤ amen 🙏🙏💪
Amen 🙏 father God bless you all the time
Azibusa osavutika kumpempherera chakwera azakumangani
Amen❤
Amen father Tinasowa uthenga wanu
MCP yayambaso nkhondo ija ya 1992 ndi ma bishop,
Mawu mulungu sazapita pachabe ku aheberi amanena kuti mkoopsya kugwa mzanja la mulungu wa moyo aprezident segulani kutu la kuweluzika
Amen amen father🛐
Amen Father
Amen father Mtalika
amen farther
Amen
Tangoyambisani chipani musatinyasepo
Emen emen
Komaso lalikilani uthenga wachipulumtso siuthenga umene anamutumani ayi phepani
Inu ndiosokoneza acatholic mukhumudwa zeni zeni osangoyambisa chipani chanu bwanji
🙏👋😭
awa ndimlomwe asaname apa akuona ngati boma lidzabwelelaso Kwawo akunama zazii
Zikungwiridzana bwanji ndi alomwe iziiiii????
Mwaiwala mayitanidwe anu mwalowa ndale mulungu akuyendelen mabishop simulungu mulungu amene ine ndikumziwa siinu ayi
Koma uthenga umenewu wakutumani ndani?
Chifukwa uwu siwochokera kwa mulungu!!
Amen father.
Mulungu aike dzanja lake pa dziko lathu.
Kopepesa koyenera anthu kupita ndikukapepesa ndi kunsipe komanso kumabanja ena. There is no business kuti ma Episcope sakuyenera ndikulora komwe kupita ku state house. People should not get money through the death of chilima and other people.
Amen father
There is Lack of Philanthropy and Patriotism in political and even in religious gatherings.REASON? Leaders' cupidity.
Amen father🙏
Amen 🙏🙏 father mthalika alapedi anthu amenewa aziwe chowonadi
Zikomo kwambiri mabishop chifukwa zinthu zikamasiya Kuyenda bwino mumaunikira ndipo pitilizani. Dzikoli ladzadza ndizosangalatsa Mulungu.Ziphuphu zachuluka.Anthu ambiri akungosaukirasaukira ndipo ochepa akudyelera chifukwa chammene dzikoli likuyendera.
Amen father, powerful msg
Mulungu atikhululikile ndikutipulumutsa ndithu ❤❤ amen 🙏🙏💪
Amen 🙏 father God bless you all the time
Azibusa osavutika kumpempherera chakwera azakumangani
Amen❤
Amen father Tinasowa uthenga wanu
MCP yayambaso nkhondo ija ya 1992 ndi ma bishop,
Mawu mulungu sazapita pachabe ku aheberi amanena kuti mkoopsya kugwa mzanja la mulungu wa moyo aprezident segulani kutu la kuweluzika
Amen amen father🛐
Amen Father
Amen father Mtalika
amen farther
Amen
Tangoyambisani chipani musatinyasepo
Emen emen
Komaso lalikilani uthenga wachipulumtso siuthenga umene anamutumani ayi phepani
Inu ndiosokoneza acatholic mukhumudwa zeni zeni osangoyambisa chipani chanu bwanji
🙏👋😭
awa ndimlomwe asaname apa akuona ngati boma lidzabwelelaso Kwawo akunama zazii
Zikungwiridzana bwanji ndi alomwe iziiiii????
Mwaiwala mayitanidwe anu mwalowa ndale mulungu akuyendelen mabishop simulungu mulungu amene ine ndikumziwa siinu ayi
Amen father
Amen❤
Amen
Amen Father
Amen