LIMPOPO FM WITH COMRADE NTANYIWA 1 JULY 2024

แชร์
ฝัง

ความคิดเห็น • 267

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm วันที่ผ่านมา +2

    I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa God bless you all the time.

  • @user-wq9ex2sf3b
    @user-wq9ex2sf3b วันที่ผ่านมา +2

    From Zambia I love bro with bon kalindo my wife came from chitipa MCP yampa athu anzelu,

  • @MercyNyachi
    @MercyNyachi วันที่ผ่านมา +1

    Mulungu akulangeni achakwera mwadzuza amalawi ambiri ambuye ngati mukumva pemphelo lathu ife amalawi timenyeleni nkhondo ambuye amen

  • @FelixKada
    @FelixKada 11 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Big up mr ntanyiwa, ndipo pitilidzani kuigwira ntcito to.🤝🤝🤝🤝🤝🤝🇲🇼🇲🇼🇲🇼

  • @LYDIANYAKATU
    @LYDIANYAKATU วันที่ผ่านมา +1

    Ambuye azikutetezerani a ntanyiwa ,amene akulimbana ndi Inu akulimbana ndi Mulungu kumene amene akulimbana ndi a rwara akulimbana ndi Mulungu kumene anthu a Mcp opanda nzeru mmalo mopangira chitukuko ndarama akupangira kuti achotse mutiti ya anthu heeedee tawaonani eti anthu opanda manyazi ngati awo timakhnyadirani a ntanyiwa may God bless you all the time

  • @NastonVickta
    @NastonVickta วันที่ผ่านมา +1

    Tili ngaaaaaa pa Limpopo fm, mpaka agaru oyamwitsa Inu mawere auma

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 วันที่ผ่านมา +1

    Mumakwana ma Freedom fighters athu athu akumalawi, timakukondani guys❤, MULUNGU azikutetezani ndikukupasani zosowa za pa umoyo wanu, inudi ndima HEROES adziko lamalawi ❤❤❤😢

  • @user-ul1fb4yn5o
    @user-ul1fb4yn5o วันที่ผ่านมา +2

    I love limpopo fm with Comrade ntanyiwa

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj วันที่ผ่านมา

    Lipopo tiutseni soona shonde lipopo is my favorite shoiss ever from 6pm to 12am osawopha osavowonka ndive amalawi mtanyiwwa osawopha bakili muluzi TV osawopha mulungu adalise inuyyo nosse nkumene mulinko my must brress you orrowyess 💪💪💪💪👀

  • @jamesmulangalimatemba5351
    @jamesmulangalimatemba5351 วันที่ผ่านมา +1

    May God protect you my brother tikufuna anthu olimba mtima ngati inu

  • @meganabigail-ye7fw
    @meganabigail-ye7fw วันที่ผ่านมา +1

    We Love you our junior pangolin no matter what they can't find you chifukwa inuyo Muli mumapapiko a mwini moyo wanu Chauta, Namalenga chisumphi. Ndeno angotaya nthawi azingodya basi

  • @BlessigsChabzola
    @BlessigsChabzola วันที่ผ่านมา +2

    Nanga Iwo a Mcp sakulira nawo nanga bwanji 21days isanathe Iwo akupanga program ya convention. Ndizona zimezi,

  • @Blessings-td4cr
    @Blessings-td4cr วันที่ผ่านมา +2

    Andale ndi athu oipa ndizoona ,,koma ndale za tonse alliance ulendo una akutionjeza,,,zinazi this current government akuyenera afufuze nkhope yamulungu,,,azidziwatu pena kuti izi ndizachabechabe Iwo eni adzafasotu!!!

  • @clairelewis5309
    @clairelewis5309 วันที่ผ่านมา

    Mwadzuka bwa Comrade Ntanyiwa from Nottingham.ndakunvani ,very clear

  • @harrisonkalimbakatha5339
    @harrisonkalimbakatha5339 วันที่ผ่านมา +3

    Comrade ntanyiwa umatiyimirira MCP ndi chipani chakupha ndipo sichizasintha mpaka kalekale ndipo atikwana anthu amenewa tikuona kuchedwa 2025

  • @MadalitsoTamayenda-ez5pj
    @MadalitsoTamayenda-ez5pj วันที่ผ่านมา +1

    Stay safe doctor ntayiwa ,, God protect yu whereever yu go kept up💯🔥💥

  • @YohaneChibweya
    @YohaneChibweya วันที่ผ่านมา +1

    Mwadzuka bwanji Ntanyiwa musaope mulungu amapanga njira popanda njira masalimo 35 komanso masalimo 91 Pali mmawu a chilimbikitso

  • @MphatsoMhoney-xn2ft
    @MphatsoMhoney-xn2ft วันที่ผ่านมา +2

    MCP yonse ikupenga pano ?? Keep Resting well Klaus Chilima

  • @user-dq9oe8sp8k
    @user-dq9oe8sp8k วันที่ผ่านมา +2

    Long live bwana Ntanyiwa

  • @MerryWayson
    @MerryWayson วันที่ผ่านมา +1

    Mr Mtanyiwa End Mr Kalindo , mulungu sakutayani tikukuikizani m,mmanja mwa mulungu azikutetezani nthawi ndinthawi mukutiimilira ambuye akusungeni maka kukutetezani Kwa adani a MSP

  • @VirginiaPaulino-xc8ph
    @VirginiaPaulino-xc8ph วันที่ผ่านมา +1

    What either like or not ife nganganga pa Limpopo aziona agalu amenewa

  • @RuiJemusse-om7po
    @RuiJemusse-om7po 21 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Mulungu akhale Nanu amina Inu, wina asakutsekeni pakamaa, Mr Ntanyiwa and Mr Kalido go ahead

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 วันที่ผ่านมา +1

    Mungoti pheeee muone !!!! 🎉🎉

  • @mariamahamadu8402
    @mariamahamadu8402 วันที่ผ่านมา +2

    Nawoso amanganya ali kwangwalala njekate kuno olo ndimantha omwe alibe adzikale ng'oma mudzazafe mukale amuyaya ku MCP pamosi ndichimimba chanucho pamosi ndi chakwela chigawenga chakumpa chilombo chigawenga chakumpa

  • @SymonZemben-gd3ne
    @SymonZemben-gd3ne วันที่ผ่านมา

    Much love to you Limpopo FM with your team,Mr Born kalindo and Bakili TV we love you all keep it up leave long with 🐐🐐🐐

  • @frankdiyele7467
    @frankdiyele7467 วันที่ผ่านมา +1

    Truth shall prevail we have suffered enough abale

  • @user-ky4ce9gb6j
    @user-ky4ce9gb6j วันที่ผ่านมา +1

    Ndipo tikuziwa zinthu ndi BAKILI MULUZI TV bg up brothers

  • @Sabina-hw4js
    @Sabina-hw4js วันที่ผ่านมา

    People are sleeping literally without food yet they can spend all this huge amounts of monies just to protect themselves.May God honestly judge them.God bless you in and may he always protect you

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu วันที่ผ่านมา +1

    Manganya fiti yudasi chakwera pilato mwampha chilima wanthu tsogoro lathu tikulira lfe chakwera please usogoreri amatero manganya galu wanthu

  • @LunnahMtambo
    @LunnahMtambo วันที่ผ่านมา

    Comred munthanyiwa ndipo tili limodzi ,ndipo timakunyadirani chilungamo tichiziwa kudzera ku lompopo fm ndipo angero amulungu akutetezere

  • @user-ve4zn2ne1k
    @user-ve4zn2ne1k วันที่ผ่านมา +2

    😂😂😂morning Mr Ntaaaaaaaaanyiwaaaaaaaa we love you

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 วันที่ผ่านมา +2

    Mchewa watichitisa manyazi kwambiri zaonesa ngati achewa tonse ndi mbuli. Zandinyasa zedi.

  • @user-zr7wk4oq2x
    @user-zr7wk4oq2x วันที่ผ่านมา

    Buddy Ntanyiwa 🖤💣
    Keep doing the needful ♥️🙏

  • @HaliJana
    @HaliJana 7 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Zakhali n'goma panyopako wava ukuwasakilanji azako galu iwe osongomadya ndalamazo bwanji mimbayo ngati nyini yamako zakhali n'goma

  • @user-xk9vs9qc2s
    @user-xk9vs9qc2s วันที่ผ่านมา

    Fighting for the nation god never leave you like that freedom fighter mtanyiwa God protect you

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 วันที่ผ่านมา +1

    Mumuwuze Cilil Ramaphosa President wa South Africa kuti chakwela and his useless government ndi zigawenga

  • @memoryedwin
    @memoryedwin 20 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Mulungi azikudalitsani mr mtanyiwa

  • @user-xf8xb2iq9i
    @user-xf8xb2iq9i วันที่ผ่านมา +1

    Usi ndamuda bas tilire bwanji ifa ya chilima😢😢😢😢

  • @EdwardMathuwa
    @EdwardMathuwa วันที่ผ่านมา +2

    Kodi a zikhale ng'ona mvuto lawo ndi chani?

  • @LeonardMhone-cg1tk
    @LeonardMhone-cg1tk วันที่ผ่านมา

    May God protect you 2 Bakili tv and MR Ntanyiwa 🙏🙏

  • @aligrayjeo1071
    @aligrayjeo1071 วันที่ผ่านมา +1

    Kodi nzotheka kuti tikhale ndi silent special forces Ku Malawi kuno tingopanga za MCP iyi basi chifukwa campaign nde sapangatu akapangila ground yake iti yoti akhale ndi chikhulupiliro kuti a Malawi akawamvetsera nyasi zawo mapeto Ake akachoka ataphwanyidwa ndi miyala ngati sakudziwa savage people

  • @TwalikiWisiki
    @TwalikiWisiki วันที่ผ่านมา +1

    M'busa wa ntundu wanji opanda chifundo,opanda chisoni,, kukanika ku khululukila Chilima ngati adawalakwira

  • @jafalimussa5146
    @jafalimussa5146 วันที่ผ่านมา +1

    Wawa ma boss muwuze avesese azazolowela

  • @shadreckphiri1799
    @shadreckphiri1799 วันที่ผ่านมา +2

    Malawi army and police will side with the civilians on 10th July. You will see.

  • @patrickndojime1632
    @patrickndojime1632 วันที่ผ่านมา +1

    Sizayiwalika ifa ya Chilima mpakana kale kale tizakhala tikukumbukira misozi yosantha

  • @leviouslongwe2950
    @leviouslongwe2950 วันที่ผ่านมา

    Angoni akulira zoona a Malawi, averwni zadutsa malire.
    Kunaphedwa ANTHU odziwika ndiponso amene amafunira Boma lathu zoyenerara.
    Kuphedwa Kwa:
    Mr.Albert Muwalo
    Mr. Focus Gwede
    Mr. Dick Matenje
    Mr. Sam Mpasu
    Mr..Saulosi Chilima
    ANTHU asanuwa anafa imfa zowawa a Malawi muli apa.
    Zowawa kwambiri.

  • @hudycorex1893
    @hudycorex1893 วันที่ผ่านมา +1

    More moto Ntanyiwa!!!

  • @Yungjoe786
    @Yungjoe786 วันที่ผ่านมา +1

    142 million for what?they're very stupidity instead of helping the needy with that cash.....mitu ngati zidebe

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu วันที่ผ่านมา +1

    Apa palibe kusunga chilungamo chakwela wapha chilima ndiathu 8 opanga cholakwa dyela

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg 2 วันที่ผ่านมา +2

    Limpopo ndiyakatundu

  • @user-pl2lj6mh1z
    @user-pl2lj6mh1z วันที่ผ่านมา

    Tiyen tiyen ntanyiwa umandisangalatsa kwambili❤❤❤❤❤❤❤

  • @africahasani-gl2nq
    @africahasani-gl2nq วันที่ผ่านมา +3

    Manganya kumupeleka chilima kwa pilato mmmmm wandikumudwitsa kwambili manganya

    • @ZionekaMember
      @ZionekaMember วันที่ผ่านมา

      @@africahasani-gl2nq kamba ka udindo

    • @user-rl8xs2kf1o
      @user-rl8xs2kf1o วันที่ผ่านมา

      Ndamuda manganya

  • @MisheckBandah
    @MisheckBandah วันที่ผ่านมา +2

    I love and I'll ❤ chilima for ever

  • @SangwaniKawawa
    @SangwaniKawawa วันที่ผ่านมา

    Keep us posted boss💯

  • @GeorgeChakuamba
    @GeorgeChakuamba วันที่ผ่านมา +2

    kkkkkkk😂😂😂😂Ntanyiwa yemweyo auzeni aMalawi chilungamo

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 วันที่ผ่านมา +1

    Iwe Zikhale ng'oma udzathera mmanja tsiku lina😂😂😂😂😅😅😅😅mimba yako

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 วันที่ผ่านมา

    Ndipo ndewalasa mtantiwa, fans yonse yokonda limpopo FM and bakili muluzi tv alongside Bon Kalindo, sitimagona and daily timakhala tikusakasaka ma audio anu and popanda kutulusa ma audio anu, amalawi sitimamva bwino mmitima mwathu .
    Tinasiya kumvera times , zodiac , mbc, mtv, luntha, nzeru, too many to mention

  • @StiveKantiki
    @StiveKantiki วันที่ผ่านมา

    Timakunyadilani bigy🎉🎉 km ndipemphe Nyimbo mwaika kumapetoyi yemwe anaimba tikuifuna ikuti matembelelo agwele pamutu pako kkk

  • @sarahlukongolo4901
    @sarahlukongolo4901 วันที่ผ่านมา +2

    Tinaona kale ife a usi kuti aliku mcp mmene amkayankhira pa Times nawo akolola akuona ngati chilima anali opusa eti

    • @AlexManuelMisomali-sv1vn
      @AlexManuelMisomali-sv1vn วันที่ผ่านมา

      Zoonadi penapake Chilima anali osamva komanso osakhwima pa ndale chifukwa Michael Usi ankaonekeratu kuti ndiwa MCP and why Chilima bravery told Usi kuti akufuna kuthetsa m'gwilidzano, that's why he's died

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg วันที่ผ่านมา

    Nkhan nd pa 10 July tikalile malilo achilima ku Lilongwe 🥺🥺

  • @chimwemwenkute3839
    @chimwemwenkute3839 วันที่ผ่านมา

    May God bless and protect you wherever you are comred

  • @cynthiataulo5211
    @cynthiataulo5211 วันที่ผ่านมา +1

    Usi amaoneka maso mwa mwa mwa kuchenjelesa. Ka snake kenikeni. Blood in their hands, angobwelesa matemberero to their generations to come. Anawo zizukulu zawo mapemphero awo azakhala abomination before God. Peace will be their enemy.

  • @lottiempata2487
    @lottiempata2487 วันที่ผ่านมา +1

    Don't be afraid 😨 for anyone else

  • @dedzafranchise
    @dedzafranchise วันที่ผ่านมา

    much love to you comrade musadzamwalire

  • @ElasonAimon
    @ElasonAimon วันที่ผ่านมา

    Mukuti imilira a Limpopo mulungu azikusamalirani nthawi zose

  • @Sammy-vb1ed
    @Sammy-vb1ed วันที่ผ่านมา +1

    Mmmmm ay koma mcp yaonjeza nkhanza ndipo sitikuifuna.

  • @NgongireMwakasungula
    @NgongireMwakasungula วันที่ผ่านมา

    Ine ntanyiwa tikungodikila 10 July kuti zalire bwino marilo achilima from kalonga

  • @user-wq9ex2sf3b
    @user-wq9ex2sf3b วันที่ผ่านมา +1

    God bless you

  • @Jamesmwale-iz4ri
    @Jamesmwale-iz4ri วันที่ผ่านมา

    Ntanyiwa mukumatimvetsa kukoma za IFA chilima

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b วันที่ผ่านมา +1

    Mmmmmm koma ndalamazi zimenrzi zokumachokera kuti?
    Chifukwa nde zikumadabwitsatu

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx วันที่ผ่านมา +1

    Amenewo tikumana pa 10 pano

  • @ImanRashidi-so4oo
    @ImanRashidi-so4oo วันที่ผ่านมา +1

    Dziko lanthu la Malawi likamati lizilakhula chilungamo ngat Limpopo FM tikadalemela kwambiri koma eeeeeh

    • @cynthiakananji1608
      @cynthiakananji1608 วันที่ผ่านมา

      Dziko lija azaza ndi afiti adyera, magazi mmanja

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i วันที่ผ่านมา +1

    Oyimba anayimba kuti amene udyanaye ndiamene azakupeleke. Manganya unapangilanji zimezi ndalama sizitha koma moyo wamuthu ukatayika kulibe kwina kokautenga muzivele chisoni ambuye achitenanu ndiye tikuwonelali 2025 ngati muzapitilize nawo azanuwo kuyendesa boma kupepela kwake kwantunduwanji munampeleka zanu chifukwa cha udindo kapena kungongola kwake poti anabadwa ndizose zomuyenela zelu chifundo kukongola komaso kuzichepesa nfikusasakha ntundu mulungu simuthu amatulusa zobisika lino ndiziko

  • @MercyNyachi
    @MercyNyachi วันที่ผ่านมา

    Kodi ziko Lathuli lilindindala eti ife amalawi koma nkumwamwa tea sugar wake wa baks juice zoona achakwera inu😢

  • @FunnyKalimwayi
    @FunnyKalimwayi วันที่ผ่านมา +1

    comrad mungulu akuonjezele moyo

  • @mathewssiliya574
    @mathewssiliya574 วันที่ผ่านมา

    nkhani yofuta kuvesa kulingalila ndimalila 2024 zindizaiwala

  • @hassammaulana4529
    @hassammaulana4529 วันที่ผ่านมา

    Nsiku lina mlungu azakwiya nanu ndipo muzayaluka masana sanaa

  • @Nelliekaiya
    @Nelliekaiya วันที่ผ่านมา +1

    Ingoing'alulani azidzakugwilani atayaluka kale

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg วันที่ผ่านมา

    ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤ mtanyiwa iweyo usazafeyi😂😂😂😂 kusiteti hausiko wina akungonyeratu magazi uku 😂😂 mwazi wanthu amene aja ena akungosanza gamazi kkk

  • @Sabina-hw4js
    @Sabina-hw4js วันที่ผ่านมา +1

    God fights the battles

  • @TwalikiWisiki
    @TwalikiWisiki วันที่ผ่านมา

    Mayi Yolamu Mulungu akudalitseni,akuyang'anileni,,akusunge moyo wanu,, chonnde chonde musavomele kuti a MCP akupakeni magazi a chilima chonde mayi, a MCP panopa ali so desperate thay can do anything as long as it can keep them from being exposed,, may yolamu a MCP akufuna opita naye,,akufuna akupakeni manyi,,,zikomo mayi inu ndi nakubaladi osati joyce Banda

  • @EllahEllah-hu7hi
    @EllahEllah-hu7hi วันที่ผ่านมา +1

    God have mercy

  • @SteveMamani-nv3mo
    @SteveMamani-nv3mo 20 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Nice work brother

  • @AlinafeChimoto-pp7wp
    @AlinafeChimoto-pp7wp วันที่ผ่านมา +1

    Power message

  • @Uncle_B265
    @Uncle_B265 วันที่ผ่านมา +1

    Ndalama mmalao mothandiza a malawi Ali buzy kupanga hayala kuti azipha anthu osalakwa why koma

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f วันที่ผ่านมา

    Morning Mr Ntanyiwa

  • @OweniMalokooweni-es9qx
    @OweniMalokooweni-es9qx 2 วันที่ผ่านมา +1

    Kwacha bwenji if kuno ku khonjeni kwa bhobho 🎉🎉🎉🎉

  • @StanzioDymon
    @StanzioDymon วันที่ผ่านมา

    Alekeni ana a agaluwa

  • @AbdulsartalSartal
    @AbdulsartalSartal วันที่ผ่านมา

    Khani imeneyo mumuuzenso Leyton mangochi chifukwa ndi kangaude amagothengeka ndindalama

  • @DevisonHala
    @DevisonHala วันที่ผ่านมา

    Mumajambula bwanji mtima umawawa nimafunitsitsa kukambako bos

  • @HaliJana
    @HaliJana 7 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    A MCP NDIKUUZENI SIMUNGAWAGWILI ANTHU AWA KUFIKILA MUTACHOKA MBOMA ,

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn วันที่ผ่านมา

    Keep it up bro, ineso mkuona kut aUtm ayambe aziyimire paokha asakakamire kugwilizanoku ,mukakamira kumeneko ambiri akusikani

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y วันที่ผ่านมา

    Good Messnge Lipopo FM number one good

  • @BeatrizUlanda-ht2th
    @BeatrizUlanda-ht2th วันที่ผ่านมา +1

    Asirikari aja ayamba kuurura kuti anapasidwa ndarama zokwana 14mirioni

  • @wittinessnkhokwe
    @wittinessnkhokwe วันที่ผ่านมา +2

    Iwe Monica chakwela usatitukwanise ,mpaka tikutchule phunzo?khope yonyatsayo

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus วันที่ผ่านมา

      Km anthu kusankha akazi kunawadutsa kumanzere ...nkhope yopyelera.

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn
    @AlexManuelMisomali-sv1vn วันที่ผ่านมา

    Michael Usi wanted that position of vice president of Malawi than Chilima who helped MCP to come back to power after a lot of years

  • @vengesoko
    @vengesoko วันที่ผ่านมา

    Manganya ndi mthira kuwiri iiiih ,ndiye tawonani waphetsa mzake iiiihh😢

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 วันที่ผ่านมา

    Ndipo imfa ya chilima yizakhara history mupaka kalekale ndipo ndi ana womwe sanabadwe azayiziwa history imeneyi

  • @joyahmedjoma4615
    @joyahmedjoma4615 วันที่ผ่านมา +1

    Basi nkhani ndi pa 10 sitikuopa police tikaponda zimenezo pa 10 sikale tasala ndi 8 days so soon

  • @MadaloZelela-m4n
    @MadaloZelela-m4n วันที่ผ่านมา +1

    Musadandaule mulungu ali painu