Ambuye azikutetezerani a ntanyiwa ,amene akulimbana ndi Inu akulimbana ndi Mulungu kumene amene akulimbana ndi a rwara akulimbana ndi Mulungu kumene anthu a Mcp opanda nzeru mmalo mopangira chitukuko ndarama akupangira kuti achotse mutiti ya anthu heeedee tawaonani eti anthu opanda manyazi ngati awo timakhnyadirani a ntanyiwa may God bless you all the time
Lipopo tiutseni soona shonde lipopo is my favorite shoiss ever from 6pm to 12am osawopha osavowonka ndive amalawi mtanyiwwa osawopha bakili muluzi TV osawopha mulungu adalise inuyyo nosse nkumene mulinko my must brress you orrowyess 💪💪💪💪👀
We Love you our junior pangolin no matter what they can't find you chifukwa inuyo Muli mumapapiko a mwini moyo wanu Chauta, Namalenga chisumphi. Ndeno angotaya nthawi azingodya basi
Andale ndi athu oipa ndizoona ,,koma ndale za tonse alliance ulendo una akutionjeza,,,zinazi this current government akuyenera afufuze nkhope yamulungu,,,azidziwatu pena kuti izi ndizachabechabe Iwo eni adzafasotu!!!
Mr Mtanyiwa End Mr Kalindo , mulungu sakutayani tikukuikizani m,mmanja mwa mulungu azikutetezani nthawi ndinthawi mukutiimilira ambuye akusungeni maka kukutetezani Kwa adani a MSP
People are sleeping literally without food yet they can spend all this huge amounts of monies just to protect themselves.May God honestly judge them.God bless you in and may he always protect you
Kodi nzotheka kuti tikhale ndi silent special forces Ku Malawi kuno tingopanga za MCP iyi basi chifukwa campaign nde sapangatu akapangila ground yake iti yoti akhale ndi chikhulupiliro kuti a Malawi akawamvetsera nyasi zawo mapeto Ake akachoka ataphwanyidwa ndi miyala ngati sakudziwa savage people
Ndipo ndewalasa mtantiwa, fans yonse yokonda limpopo FM and bakili muluzi tv alongside Bon Kalindo, sitimagona and daily timakhala tikusakasaka ma audio anu and popanda kutulusa ma audio anu, amalawi sitimamva bwino mmitima mwathu . Tinasiya kumvera times , zodiac , mbc, mtv, luntha, nzeru, too many to mention
Usi amaoneka maso mwa mwa mwa kuchenjelesa. Ka snake kenikeni. Blood in their hands, angobwelesa matemberero to their generations to come. Anawo zizukulu zawo mapemphero awo azakhala abomination before God. Peace will be their enemy.
Mayi Yolamu Mulungu akudalitseni,akuyang'anileni,,akusunge moyo wanu,, chonnde chonde musavomele kuti a MCP akupakeni magazi a chilima chonde mayi, a MCP panopa ali so desperate thay can do anything as long as it can keep them from being exposed,, may yolamu a MCP akufuna opita naye,,akufuna akupakeni manyi,,,zikomo mayi inu ndi nakubaladi osati joyce Banda
I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa God bless you all the time.
From Zambia I love bro with bon kalindo my wife came from chitipa MCP yampa athu anzelu,
Mulungu akulangeni achakwera mwadzuza amalawi ambiri ambuye ngati mukumva pemphelo lathu ife amalawi timenyeleni nkhondo ambuye amen
Big up mr ntanyiwa, ndipo pitilidzani kuigwira ntcito to.🤝🤝🤝🤝🤝🤝🇲🇼🇲🇼🇲🇼
Ambuye azikutetezerani a ntanyiwa ,amene akulimbana ndi Inu akulimbana ndi Mulungu kumene amene akulimbana ndi a rwara akulimbana ndi Mulungu kumene anthu a Mcp opanda nzeru mmalo mopangira chitukuko ndarama akupangira kuti achotse mutiti ya anthu heeedee tawaonani eti anthu opanda manyazi ngati awo timakhnyadirani a ntanyiwa may God bless you all the time
Tili ngaaaaaa pa Limpopo fm, mpaka agaru oyamwitsa Inu mawere auma
Mumakwana ma Freedom fighters athu athu akumalawi, timakukondani guys❤, MULUNGU azikutetezani ndikukupasani zosowa za pa umoyo wanu, inudi ndima HEROES adziko lamalawi ❤❤❤😢
I love limpopo fm with Comrade ntanyiwa
Lipopo tiutseni soona shonde lipopo is my favorite shoiss ever from 6pm to 12am osawopha osavowonka ndive amalawi mtanyiwwa osawopha bakili muluzi TV osawopha mulungu adalise inuyyo nosse nkumene mulinko my must brress you orrowyess 💪💪💪💪👀
May God protect you my brother tikufuna anthu olimba mtima ngati inu
We Love you our junior pangolin no matter what they can't find you chifukwa inuyo Muli mumapapiko a mwini moyo wanu Chauta, Namalenga chisumphi. Ndeno angotaya nthawi azingodya basi
Nanga Iwo a Mcp sakulira nawo nanga bwanji 21days isanathe Iwo akupanga program ya convention. Ndizona zimezi,
Andale ndi athu oipa ndizoona ,,koma ndale za tonse alliance ulendo una akutionjeza,,,zinazi this current government akuyenera afufuze nkhope yamulungu,,,azidziwatu pena kuti izi ndizachabechabe Iwo eni adzafasotu!!!
Mwadzuka bwa Comrade Ntanyiwa from Nottingham.ndakunvani ,very clear
Comrade ntanyiwa umatiyimirira MCP ndi chipani chakupha ndipo sichizasintha mpaka kalekale ndipo atikwana anthu amenewa tikuona kuchedwa 2025
Ndipo kwambiri tu mmm
Stay safe doctor ntayiwa ,, God protect yu whereever yu go kept up💯🔥💥
Mwadzuka bwanji Ntanyiwa musaope mulungu amapanga njira popanda njira masalimo 35 komanso masalimo 91 Pali mmawu a chilimbikitso
MCP yonse ikupenga pano ?? Keep Resting well Klaus Chilima
Long live bwana Ntanyiwa
Mr Mtanyiwa End Mr Kalindo , mulungu sakutayani tikukuikizani m,mmanja mwa mulungu azikutetezani nthawi ndinthawi mukutiimilira ambuye akusungeni maka kukutetezani Kwa adani a MSP
What either like or not ife nganganga pa Limpopo aziona agalu amenewa
Mulungu akhale Nanu amina Inu, wina asakutsekeni pakamaa, Mr Ntanyiwa and Mr Kalido go ahead
Mungoti pheeee muone !!!! 🎉🎉
Nawoso amanganya ali kwangwalala njekate kuno olo ndimantha omwe alibe adzikale ng'oma mudzazafe mukale amuyaya ku MCP pamosi ndichimimba chanucho pamosi ndi chakwela chigawenga chakumpa chilombo chigawenga chakumpa
Much love to you Limpopo FM with your team,Mr Born kalindo and Bakili TV we love you all keep it up leave long with 🐐🐐🐐
Truth shall prevail we have suffered enough abale
Ndipo tikuziwa zinthu ndi BAKILI MULUZI TV bg up brothers
People are sleeping literally without food yet they can spend all this huge amounts of monies just to protect themselves.May God honestly judge them.God bless you in and may he always protect you
Manganya fiti yudasi chakwera pilato mwampha chilima wanthu tsogoro lathu tikulira lfe chakwera please usogoreri amatero manganya galu wanthu
Comred munthanyiwa ndipo tili limodzi ,ndipo timakunyadirani chilungamo tichiziwa kudzera ku lompopo fm ndipo angero amulungu akutetezere
😂😂😂morning Mr Ntaaaaaaaaanyiwaaaaaaaa we love you
Mchewa watichitisa manyazi kwambiri zaonesa ngati achewa tonse ndi mbuli. Zandinyasa zedi.
Buddy Ntanyiwa 🖤💣
Keep doing the needful ♥️🙏
Zakhali n'goma panyopako wava ukuwasakilanji azako galu iwe osongomadya ndalamazo bwanji mimbayo ngati nyini yamako zakhali n'goma
Fighting for the nation god never leave you like that freedom fighter mtanyiwa God protect you
Mumuwuze Cilil Ramaphosa President wa South Africa kuti chakwela and his useless government ndi zigawenga
Mulungi azikudalitsani mr mtanyiwa
Usi ndamuda bas tilire bwanji ifa ya chilima😢😢😢😢
Kodi a zikhale ng'ona mvuto lawo ndi chani?
May God protect you 2 Bakili tv and MR Ntanyiwa 🙏🙏
Kodi nzotheka kuti tikhale ndi silent special forces Ku Malawi kuno tingopanga za MCP iyi basi chifukwa campaign nde sapangatu akapangila ground yake iti yoti akhale ndi chikhulupiliro kuti a Malawi akawamvetsera nyasi zawo mapeto Ake akachoka ataphwanyidwa ndi miyala ngati sakudziwa savage people
M'busa wa ntundu wanji opanda chifundo,opanda chisoni,, kukanika ku khululukila Chilima ngati adawalakwira
Wawa ma boss muwuze avesese azazolowela
Malawi army and police will side with the civilians on 10th July. You will see.
Hopefully 🤞
Sizayiwalika ifa ya Chilima mpakana kale kale tizakhala tikukumbukira misozi yosantha
Angoni akulira zoona a Malawi, averwni zadutsa malire.
Kunaphedwa ANTHU odziwika ndiponso amene amafunira Boma lathu zoyenerara.
Kuphedwa Kwa:
Mr.Albert Muwalo
Mr. Focus Gwede
Mr. Dick Matenje
Mr. Sam Mpasu
Mr..Saulosi Chilima
ANTHU asanuwa anafa imfa zowawa a Malawi muli apa.
Zowawa kwambiri.
More moto Ntanyiwa!!!
142 million for what?they're very stupidity instead of helping the needy with that cash.....mitu ngati zidebe
Apa palibe kusunga chilungamo chakwela wapha chilima ndiathu 8 opanga cholakwa dyela
Limpopo ndiyakatundu
Tiyen tiyen ntanyiwa umandisangalatsa kwambili❤❤❤❤❤❤❤
Manganya kumupeleka chilima kwa pilato mmmmm wandikumudwitsa kwambili manganya
@@africahasani-gl2nq kamba ka udindo
Ndamuda manganya
I love and I'll ❤ chilima for ever
Keep us posted boss💯
kkkkkkk😂😂😂😂Ntanyiwa yemweyo auzeni aMalawi chilungamo
Iwe Zikhale ng'oma udzathera mmanja tsiku lina😂😂😂😂😅😅😅😅mimba yako
Ndipo ndewalasa mtantiwa, fans yonse yokonda limpopo FM and bakili muluzi tv alongside Bon Kalindo, sitimagona and daily timakhala tikusakasaka ma audio anu and popanda kutulusa ma audio anu, amalawi sitimamva bwino mmitima mwathu .
Tinasiya kumvera times , zodiac , mbc, mtv, luntha, nzeru, too many to mention
Timakunyadilani bigy🎉🎉 km ndipemphe Nyimbo mwaika kumapetoyi yemwe anaimba tikuifuna ikuti matembelelo agwele pamutu pako kkk
Tinaona kale ife a usi kuti aliku mcp mmene amkayankhira pa Times nawo akolola akuona ngati chilima anali opusa eti
Zoonadi penapake Chilima anali osamva komanso osakhwima pa ndale chifukwa Michael Usi ankaonekeratu kuti ndiwa MCP and why Chilima bravery told Usi kuti akufuna kuthetsa m'gwilidzano, that's why he's died
Nkhan nd pa 10 July tikalile malilo achilima ku Lilongwe 🥺🥺
May God bless and protect you wherever you are comred
Usi amaoneka maso mwa mwa mwa kuchenjelesa. Ka snake kenikeni. Blood in their hands, angobwelesa matemberero to their generations to come. Anawo zizukulu zawo mapemphero awo azakhala abomination before God. Peace will be their enemy.
Don't be afraid 😨 for anyone else
much love to you comrade musadzamwalire
Mukuti imilira a Limpopo mulungu azikusamalirani nthawi zose
Mmmmm ay koma mcp yaonjeza nkhanza ndipo sitikuifuna.
Ine ntanyiwa tikungodikila 10 July kuti zalire bwino marilo achilima from kalonga
God bless you
Ntanyiwa mukumatimvetsa kukoma za IFA chilima
Mmmmmm koma ndalamazi zimenrzi zokumachokera kuti?
Chifukwa nde zikumadabwitsatu
Amenewo tikumana pa 10 pano
Dziko lanthu la Malawi likamati lizilakhula chilungamo ngat Limpopo FM tikadalemela kwambiri koma eeeeeh
Dziko lija azaza ndi afiti adyera, magazi mmanja
Oyimba anayimba kuti amene udyanaye ndiamene azakupeleke. Manganya unapangilanji zimezi ndalama sizitha koma moyo wamuthu ukatayika kulibe kwina kokautenga muzivele chisoni ambuye achitenanu ndiye tikuwonelali 2025 ngati muzapitilize nawo azanuwo kuyendesa boma kupepela kwake kwantunduwanji munampeleka zanu chifukwa cha udindo kapena kungongola kwake poti anabadwa ndizose zomuyenela zelu chifundo kukongola komaso kuzichepesa nfikusasakha ntundu mulungu simuthu amatulusa zobisika lino ndiziko
,ooooooo
Kodi ziko Lathuli lilindindala eti ife amalawi koma nkumwamwa tea sugar wake wa baks juice zoona achakwera inu😢
comrad mungulu akuonjezele moyo
BV
nkhani yofuta kuvesa kulingalila ndimalila 2024 zindizaiwala
Nsiku lina mlungu azakwiya nanu ndipo muzayaluka masana sanaa
Ingoing'alulani azidzakugwilani atayaluka kale
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤ mtanyiwa iweyo usazafeyi😂😂😂😂 kusiteti hausiko wina akungonyeratu magazi uku 😂😂 mwazi wanthu amene aja ena akungosanza gamazi kkk
God fights the battles
Mayi Yolamu Mulungu akudalitseni,akuyang'anileni,,akusunge moyo wanu,, chonnde chonde musavomele kuti a MCP akupakeni magazi a chilima chonde mayi, a MCP panopa ali so desperate thay can do anything as long as it can keep them from being exposed,, may yolamu a MCP akufuna opita naye,,akufuna akupakeni manyi,,,zikomo mayi inu ndi nakubaladi osati joyce Banda
God have mercy
Nice work brother
Power message
Ndalama mmalao mothandiza a malawi Ali buzy kupanga hayala kuti azipha anthu osalakwa why koma
Morning Mr Ntanyiwa
Kwacha bwenji if kuno ku khonjeni kwa bhobho 🎉🎉🎉🎉
Alekeni ana a agaluwa
Khani imeneyo mumuuzenso Leyton mangochi chifukwa ndi kangaude amagothengeka ndindalama
Mumajambula bwanji mtima umawawa nimafunitsitsa kukambako bos
A MCP NDIKUUZENI SIMUNGAWAGWILI ANTHU AWA KUFIKILA MUTACHOKA MBOMA ,
Keep it up bro, ineso mkuona kut aUtm ayambe aziyimire paokha asakakamire kugwilizanoku ,mukakamira kumeneko ambiri akusikani
Good Messnge Lipopo FM number one good
Asirikari aja ayamba kuurura kuti anapasidwa ndarama zokwana 14mirioni
Iwe Monica chakwela usatitukwanise ,mpaka tikutchule phunzo?khope yonyatsayo
Km anthu kusankha akazi kunawadutsa kumanzere ...nkhope yopyelera.
Michael Usi wanted that position of vice president of Malawi than Chilima who helped MCP to come back to power after a lot of years
Manganya ndi mthira kuwiri iiiih ,ndiye tawonani waphetsa mzake iiiihh😢
Ndipo imfa ya chilima yizakhara history mupaka kalekale ndipo ndi ana womwe sanabadwe azayiziwa history imeneyi
Basi nkhani ndi pa 10 sitikuopa police tikaponda zimenezo pa 10 sikale tasala ndi 8 days so soon
Ndipo kwambiri tu
Musadandaule mulungu ali painu