Akuluakulu agreed with him,i traveled different places especially in the villages kumene olemera zangatsafike moyo wake onse,athudi akuvutika kuti mukawone madzi omwe akumwa apa chitsime guys you wont believe it,i agreed with u too.ine Wales munundo,from ndauza village,TA Changata.God bless you guys keep on.
Kodi bwanji sipakukambidwa zoti tisanavote tiwunikeso malamuro a kayendetsedwe ka dziko la Malawi?Chifukwa kunena zoona a Malawi tikupwetekedwa ndi malamuro adziko lathu lomwe,tili mu democracy koma malamuro ndi omwe aja a chitsamunda ndi Kamuzu Kodi pamenepo ziku balancer?
Akatolika samapanga za mpingo koma ndale ndi usatanic basi.anthu ama thanyula awa opembedza mafano,ena oyika mkhosi ena mkachisi. Ine ndi mkatolika koma my vote is for Chakwera basi
I love this message!
Katolika imadana ndi anthu oputsa Chakwera udziwanso, APM my vote ❤❤❤❤❤❤
Mawu omveka bwino kwambiri 🙏
Akuluakulu agreed with him,i traveled different places especially in the villages kumene olemera zangatsafike moyo wake onse,athudi akuvutika kuti mukawone madzi omwe akumwa apa chitsime guys you wont believe it,i agreed with u too.ine Wales munundo,from ndauza village,TA Changata.God bless you guys keep on.
INUYO MA BISHOP MUKUTIIMIRIRA OSATI AZIBUSA ENAWA ADYERA KUIWALA ZA CHIMENE MULUNGU ANAWATUMA , KEEP IT UP,
Musanyoze atumiki Amulungu anati musakhudze odzodzedwa ake akunena zowona iyi ndi imodzi mwa ntchito akuyenela kugwila padziko Ambuye akudalitseni ma Bishop
MAY GOD BLESS PAX ROMANA IN MALAWI
Power to that 🙏
Apm my vote
Chakwera anawaputa akatolika ndipo akhaula zedi❤❤❤❤❤😂😂😂
Amen
Salute
Tell them man of God
Mulungu akulankhuleni mwapadera mutha kukhala amodzi mwaathu osokeretsa anthu
Zamphavu mmatiyimilila ma Bishop
Awuzeni father sakuziwa anyapipewo
🔥🔥🔥
Zona malume mutalika
Kunena mosanyengerera zofooka za awa zapambana eg kugwa kwa kwacha kusowa kwa cha kudya kukwera kwa zinthu ndi usogoleri otembereredwa
Mbambande kulamkhula mogwira mtima pitilizani
Ndiye muwaziwa alonwewo pano kuti ndinjuchi komaso olo nchewa oganiza fetereza mene wadulilamu chilichonse chakwera pano nkumavutikaso ndinthu kuvotera mcp guys olo muja asanaonjezere mavutowa pano ndiye nyanyi akanamgomusiya chilima akapikisane paground koma amamuopa koma mulungu apanga njila
Pakufunika changu kuchitapo kanthu tisanathe a Malawi
Mawu mawu achilungamo awa
Mpakana amipingo kuku ndaura chakwera uribe peace bas
Kodi bwanji sipakukambidwa zoti tisanavote tiwunikeso malamuro a kayendetsedwe ka dziko la Malawi?Chifukwa kunena zoona a Malawi tikupwetekedwa ndi malamuro adziko lathu lomwe,tili mu democracy koma malamuro ndi omwe aja a chitsamunda ndi Kamuzu Kodi pamenepo ziku balancer?
Koma zoti anapochera tuma envelope ndi zoona kapena ayi
Aaaaa malo moti azikakwatirana amuna or akaz okhaokha😂😂😂😂
MCP dzitsiru dza anthu ndithu inu kupha Chilima munthu oti anakuthandiza kuti mulowe m boma
Akatolika samapanga za mpingo koma ndale ndi usatanic basi.anthu ama thanyula awa opembedza mafano,ena oyika mkhosi ena mkachisi.
Ine ndi mkatolika koma my vote is for Chakwera basi
Iwe ndiwanyau, osati mkatolika
@@EmmanuelGasiten-fo5dryes uyuyu simkatolika
galu wachabechabe nkhope ngati yovala
Vuto ambiriwa ndi alomwe omwe mkale lose sanavoteleko MCP ndipo sitisowa vote yawo
Munya
Iyi ndi nthawi yothana nawe wa satanic tikufuna chilima wathu😢😢
Zoonadi tilidi kubagamoyo tinalakwitsa poasakha boma la MCP boma lopandamzeru
Chisilu china chake chikuti akatolika za ndale ndipo amapanga mathanyula ......iwe ndiwe munthu wopusa kwambili ....mmene chawera mmene waonongela zikoli ungamalembe zopusa zakozo .....iweyo ndi mbuzi kaya ukudya nawo ndalama zokubazi tazingodyani muzaona polekela ....galu iwe
Koma akunkuyu nkhaniyi Adaimva?akuyenera kuwauza a bwana awo kuti mwina asinthe
@@ChimmsRichardOrdenyou mean he doesn't know what is on ground? He knows
Ndipo wa satanic ndi iweyo ukudya ndalama zokuba zachakwera ndipo chakwera ndiye wa satanic weniweni galu iwe