Limpopo iiiih! ma demo ajatu kwabwela anthu akunja kudzaletsa atapangidwa hayala Ntanyiwa waulura

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 4 ก.ค. 2024

ความคิดเห็น • 98

  • @ShaolinThomas-ow8yn
    @ShaolinThomas-ow8yn 3 วันที่ผ่านมา +6

    Inuyo mulungu adzingokuonjexelani moyo wautali basi ,chifukwa mukutimvetsa kukoma

  • @JuuuKomba
    @JuuuKomba 2 วันที่ผ่านมา +3

    Koma iweyo pokhapa pot awagwila ndakuimikila manja mwamba athuo agwidwad

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du 2 วันที่ผ่านมา +2

    Akulu akulu mukulankhula koma sitikumva 😢

  • @user-mw3kj4qz7b
    @user-mw3kj4qz7b 3 วันที่ผ่านมา +13

    We won't fear anything even as Zambian s were coming in Malawi guys to fight that evil man chakwela

  • @mthawisakaunda
    @mthawisakaunda 2 วันที่ผ่านมา +2

    Akatula udindo chakwerayo, azibale ake onse azachotsedwe ntchto. Galu watitopetsa

  • @Hassankazembe-d3o
    @Hassankazembe-d3o 2 วันที่ผ่านมา +1

    May God bless you comrade Ntanyiwa

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 3 วันที่ผ่านมา +3

    I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa.

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du 2 วันที่ผ่านมา +2

    Koma chakwera wandikwana one day ndi kupedza people they call gringo

  • @UsenLashid
    @UsenLashid 2 วันที่ผ่านมา +2

    Komaso Mr ntanyiwa musalore Kuti anthu 8 amene agwidwawo asatuluke Ayi kufikila chakwela atule pansi udindo komaso dziko la South Africa asawapange rilizi Ayi kufikila lamampho atamuzenga mulandu chakwela

  • @mellipherjohn7158
    @mellipherjohn7158 วันที่ผ่านมา +1

    umakwana mtanyiwa tikuziwa zambili amalawi ambuye azikupasani moyo wautali 🎉🎉🎉🎉

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e 2 วันที่ผ่านมา +1

    Asilikali a ku Malawi ndi ogona tulo zitsilu zimalimbana ndi anthu wamba usayelekeze kuvala kabudula wa makaka ndiye amaonesa mphamvu zawo ati wavala unform yawo mbudzi

  • @WatsonNtchito
    @WatsonNtchito วันที่ผ่านมา +1

    Mademo akayambire kumamfumu hotel komweko tiyeni tonse tikasokhane popo pa mfumu hotel ku ma room achulidwawo osaopa

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du 2 วันที่ผ่านมา +2

    Asilikari anthu ntchito yao ndi kuchinda mahule mutchesi umu😂😂

  • @user-ht7vs3dp2u
    @user-ht7vs3dp2u 3 วันที่ผ่านมา +2

    Ntanyiwa iweyo ndi number one radio yako timainyadira kom athu athawa ziko lili rawo kom kumeneko moto kuti buuuuu mumtimamo angokhuta mphuma lokhalokha km mulimba Ntanyiwa woyeee

  • @JaneLikome
    @JaneLikome 2 วันที่ผ่านมา

    Nice mr ntanyiwa

  • @MathpeterLemon-ls1ns
    @MathpeterLemon-ls1ns 3 วันที่ผ่านมา +3

    Pano malawi ndi North Korea 😭😭😭

  • @CadTafa2
    @CadTafa2 3 วันที่ผ่านมา +3

    Apolici a malawi a kuzishipisa

  • @AjibuTwalibu
    @AjibuTwalibu 2 วันที่ผ่านมา

    Umakwana ya mtanyiwa tili nawenawe my brother

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi 2 วันที่ผ่านมา

    Apapa ndatanganidwa kuwerenga nkunvesera😂😂

  • @CathrineRamseyJafaal
    @CathrineRamseyJafaal 2 วันที่ผ่านมา +1

    Anthu nonse amene mukudana ndi nthanyiwa mitungati zoswera malambe inu zikukusangalasani mmene akuyendesela dzikoli gule wanuyi achoke alibe phindu

  • @DuntumaziyaDuntumaziya
    @DuntumaziyaDuntumaziya 2 วันที่ผ่านมา +1

    following you sir

  • @blacksonpeshes5057
    @blacksonpeshes5057 2 วันที่ผ่านมา

    kom mukutivetsa kukoma ndikapanda kuva uthenga kuchokela kwainu sindipuma bwino kod mudarikuti mosemunja

  • @BitonFred
    @BitonFred 6 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Anthu akumalawi umbuli, anachotsa peter, ati wabwino chakwera, pano akufuna peter yemwe uja, mmalawi wanzeru sakuyenera kupeleka vote ku president yemwe analephera kale, votelani atsopano osati apeter muthalika

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 2 วันที่ผ่านมา

    Ankolo ku malawi kulibe a silikali akanakhala kuti alipo zikuchita galu ameneyo mukumuti chokwerayu atamukhazika kale pansi, koma nawo asankha kugwirantchito ndi chipani ayiwala makamulo awo ndi mbuzi za silikali za manu pansi ndi mbuyao chakwerayo tionana chaka cha mawa onse amene akupha ndi chakwera tikhaulitsa boma ili lapita olo ataopseza motani zosatheka

  • @MikeMerecah
    @MikeMerecah 2 วันที่ผ่านมา

    Ma activists athu musakhare chete kunoko akumangidwa mwachisisi mudziwe zimenezi, anthu osatchuka panopa Ali ku area 30 guyz,

  • @misoMoyo
    @misoMoyo 2 วันที่ผ่านมา

    Limpopo FM ineyo ndimachedwa Ku ntchito kuti ndimvere basi nkhani ZANU mumandidalitsa ine ndi m,ngoni weni weni more fire inuyo a Mr Ntanyiwa

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 2 วันที่ผ่านมา

    Kuti muone ku mcp kuli anthu osaoneka bwino okhaokha pamaso ndionyasa ndi mtima momwe

  • @IssahAluba
    @IssahAluba 2 วันที่ผ่านมา

    Chonde AMalawi asatiphimbe maso BOMA ilili osalivera tiyeni pansewu week yamawa osaopa gayz 💪💪🛶🛶🏹🏹⚒️⛏️

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 2 วันที่ผ่านมา

    Ndipo chakwera tidzachita kuotcha pamoto chifukwa chankhanza akuchitazi

  • @NisharChibisa
    @NisharChibisa 3 วันที่ผ่านมา +1

    Mumakwana

  • @AugustineIshmael
    @AugustineIshmael วันที่ผ่านมา

    Zachamba basi dikilani 2025 vote yanu ndiye nuclear power osati zabibi zanuzi

  • @PartsonMdeza
    @PartsonMdeza วันที่ผ่านมา

    nkhanga zaonaaa

  • @BrunoChakukuma
    @BrunoChakukuma วันที่ผ่านมา

    Ntanyiwa woyeeeee

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023 2 วันที่ผ่านมา

    Comredy mtanyiwa tikufuna number yanu tizipephela Nanu mulungu azikudalisani kwambili ndipo azikutetezani kulikose komwe mukuyenda

  • @Bonisiwentamo
    @Bonisiwentamo 3 วันที่ผ่านมา

    ❤Zowona acc muthu ameneyu AChoke

  • @JamesIsaac-zi4kb
    @JamesIsaac-zi4kb 2 วันที่ผ่านมา

    Chakwela ofuna adibwe kanyenya basi

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o 2 วันที่ผ่านมา

    Nde inu mukuganiza kut olo patabwera peteryo zinthu zingasinthe foundation ya Malawi kuvuta konseko ndi chipani Cha udf olo mutatani Malawi sazasintha

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o 2 วันที่ผ่านมา

    Ukanakhala kut mwina ukutiwuza munthu wozamuvotera koma nawenso ukumpangila peter kampen choti uziwe peter nayenso atatitopesa kale sitikunfunanso

  • @user-vu4cz1mt4f
    @user-vu4cz1mt4f 2 วันที่ผ่านมา

    Tisayembekezere kuti tingamve munthu wakuphayo kuti ndine ndapha mayz ?
    Munona kt wakupha kufufuza chifkwa chomwe wina wafera koma atapha ndiyeyo ?
    Mayankho ndiomwewa omwe tikumayankhulawa coz action ikuchitatu kuoneka yokha ndipo mwachindunji monga kumangidwa anthu then kulowesa zigawenga nde ngt akusakidwa anthuwa kuti aphedwe nde nkumat ena omwe adafa aja anafera zina ?

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili 2 วันที่ผ่านมา

    Mcp mukali kuyalukirayalukiratu

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona 3 วันที่ผ่านมา

    M C P -- Malawi Congress Party
    M C P = Malawi Chikangawa Party 👹👹👹🔨⚒️⛏️

  • @maluli5691
    @maluli5691 2 วันที่ผ่านมา

    Asilikali Aku malawi ndi asilikadzi.west Africa asilikali sakunyengelela kulanda boma

  • @YONA-v5o
    @YONA-v5o 3 วันที่ผ่านมา

    Anthu amenewo ngat agwidwa aphedwe ndinthu cifukwa iwowo anabwela kuzapha

  • @stanleychisasa4343
    @stanleychisasa4343 2 วันที่ผ่านมา

    Boss mbuyomu munatiuza kuti athu aku German ofufuza ndege aja anali okonza miseu lero muti ndi aku butcher which is which
    Big man?

  • @mipeacemakermw9501
    @mipeacemakermw9501 18 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Mwatukwana president 🤣🤣🤣🤣th-cam.com/video/WRDkQ8s_34k/w-d-xo.htmlsi=PkGoYsuJRKSW0v4p

  • @dorisbutao4227
    @dorisbutao4227 2 วันที่ผ่านมา

    Mmmh

  • @UsenLashid
    @UsenLashid 2 วันที่ผ่านมา

    Kodi inu apolice ndi asilikali ntchito yanu ndi chiyani kumalawiko? Kodi mukuyang'anila zika Zanu zikuphedwa Kodi inu ndinu apolice opanda ntchito pamodzi ndi iwe wa mkulu wa asilikali utule Pasi udindo coz your usiless man dammit asilikali inu achilungamo menyani nkhondo please

  • @jangiya03
    @jangiya03 2 วันที่ผ่านมา

    Ambuye tithandizeni Malawi waipa

  • @GetrudeBanda-sd1yf
    @GetrudeBanda-sd1yf 3 วันที่ผ่านมา

    Zoonad amalawi azimai tizingoyang'anira nyasizi bvuto azimai timatengrka ndi kathu kochepa

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 2 วันที่ผ่านมา

    mademo mpanga komweko ku lilongwe ayi mkanya

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 3 วันที่ผ่านมา

    Hahaha AAA, Malawi poison party, Wanthu anawa votera dala, bolani ife tiri kutali zina ukamva zina Leku kamba anga mwala.

  • @CaptainNyenga
    @CaptainNyenga 3 วันที่ผ่านมา

    😂😂😂😂😂 zabwino zonse wachita bwino wagwidwa tiakonzere konkuno

  • @shadreckphiri1799
    @shadreckphiri1799 3 วันที่ผ่านมา

    If what comrade is saying is the truth,then Chakwera must be the worst president in Southern Africa.

  • @BitonFred
    @BitonFred 7 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    😂😂😂😂

  • @ThokohPrescotKalonga
    @ThokohPrescotKalonga 3 วันที่ผ่านมา

    Malawian kuwopa too much that’s why amakonda kulepheresa mademo so don’t tell us ngati muziwona zoti sizingatheke zochita mademo! Aaa why amakonda kulepheresa mademo

  • @CaptainNyenga
    @CaptainNyenga 3 วันที่ผ่านมา

    Limpopo FM ndi 1

  • @walesbanda4959
    @walesbanda4959 วันที่ผ่านมา

    😂😂😂

  • @SeephyMfaume
    @SeephyMfaume 3 วันที่ผ่านมา

    MCP Pamtumbo pawo ndithu

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 2 วันที่ผ่านมา

    Chakwela ndikanankhala kuti ndimatha ufiti ndinakamchosa ineyo manyi akee anthu

    • @EllenPhiri-xt8pt
      @EllenPhiri-xt8pt 2 วันที่ผ่านมา

      Chitsilu chichakwela ndi family yake yonse ambuye tichotseleni munthuyi😊

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma 3 วันที่ผ่านมา

    Koma Malawi walowa chibwana chakwera anapita ku sukulu koma?pano akusekedwa ndi anthu akunja omwe

  • @ConfusedAstronaut-qv6wq
    @ConfusedAstronaut-qv6wq 3 วันที่ผ่านมา

    Koma chakwera anthawa wauyouyo mbwiyache.

  • @HappyMaolid
    @HappyMaolid 3 วันที่ผ่านมา

    It's time to figh now,osagona

  • @user-xi2vo4gc4u
    @user-xi2vo4gc4u 3 วันที่ผ่านมา

    Ku Malawi aku shooter ma movie rekani amenyane

  • @ConfusedAstronaut-qv6wq
    @ConfusedAstronaut-qv6wq 3 วันที่ผ่านมา

    Asilikira akumalawi ndi wopusa.

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg 3 วันที่ผ่านมา

    Chakwela ndigalu kwabasi

  • @PaulineKamwana
    @PaulineKamwana 3 วันที่ผ่านมา

    8:30 musova mcp ,mulithawa dziko mukulifuna

  • @CHIWSABINYAMBOSE
    @CHIWSABINYAMBOSE 3 วันที่ผ่านมา

    Ndichoipadi ichi chigawenga chabechabe

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 2 วันที่ผ่านมา

    zinamizanani pano pa limpopo kwachwera ali pheee kukozanyasi zomwe inapanga dpp . alikuti anthu omwe agidwa aaa opusi mtanyiwa

    • @HalisonSolomon
      @HalisonSolomon 2 วันที่ผ่านมา

      Iwe mutuwako suyenda ngati akutuma a mcp anthu akufinya ndi chakwera wakoyo ngati akupasa ndalama ulibe manyazi wekha otsutsa pano aaaaaaaa ona kolowera

  • @CharlesMateya
    @CharlesMateya 2 วันที่ผ่านมา

    Following

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 3 วันที่ผ่านมา

    😢😢😢😢😢😢😢😢

  • @user-td6qe4gr6w
    @user-td6qe4gr6w 2 วันที่ผ่านมา

    Chopweteka kwambiri ndi choti ndalama za nkhani nkhani zikuthela kulipira anthu a kunja amene zomwe akuchita mudziko lathu phindu lake opindula ndi ochepa

  • @FrankMulela-qt1wi
    @FrankMulela-qt1wi 3 วันที่ผ่านมา

    Number yotumizila zinthu kwantanyiwa plz

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko 3 วันที่ผ่านมา

    Atanyiwa pathako pako

    • @ShentrycChinoko
      @ShentrycChinoko 3 วันที่ผ่านมา

      Yess

    • @ShentrycChinoko
      @ShentrycChinoko 3 วันที่ผ่านมา

      Zowonadi mchutsuludi chimenechi

    • @user-yc3ik9dq3x
      @user-yc3ik9dq3x 2 วันที่ผ่านมา

      Inu amenewo mungodziyankha nokha muli phee kugwiritsidwa ntchito ndi agaluwo 🥺mxieuw

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz 2 วันที่ผ่านมา

    Achakwera vomelezani😂

  • @FatimanickisJaffer
    @FatimanickisJaffer 3 วันที่ผ่านมา

    Am waiting good news not bad news 😔😔😔😔😔

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 3 วันที่ผ่านมา

    Chakwera atha ngati Idi amin sizimuthera bwino ndithu.

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel 3 วันที่ผ่านมา +1

    Ndikut mambodza akowa Pali ine no comment ndizopusa zakozo tithana phwanga galimoto uma user ija nditha kukutumizira komaso pachikwangwani umakonda kucheza paj okay

    • @victorauwana7258
      @victorauwana7258 3 วันที่ผ่านมา +1

      Mwapemphedwa kutu mupange comment?

    • @NizigiyimanaChantal-c2p
      @NizigiyimanaChantal-c2p 3 วันที่ผ่านมา

      😢

    • @SoundmasterElectrical
      @SoundmasterElectrical 3 วันที่ผ่านมา

      Mbudzi iwe uthana ndindani usawone ngat ndife ogona wamva panyo pako

    • @MaryNyirenda-nq3mh
      @MaryNyirenda-nq3mh 3 วันที่ผ่านมา

      Chigawenga iwe chimunthu chopanda phindu chitsilu ulibe manyazi mulungu akukanthan

    • @LukaThawe
      @LukaThawe 3 วันที่ผ่านมา

      Anthu achoka Kuti iwe nawendimbuzi kwambiri ukukofuna kusokoneza amalawi ,chifukwa amalawi ndiopepera kale ndiye azikuvera nyasi zako sata yako

  • @user-tm3zh5zk4t
    @user-tm3zh5zk4t 3 วันที่ผ่านมา

    Paja ninakuwuza kale kuti upite kumalawi mabodza akowo mtanyiwa yiweyo niamene ukumasokoneza anthu infe timapeleka ulemu kwa boni kalindo osati mbuziyiweyo ayi

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko 3 วันที่ผ่านมา

    Muyiyambe muwone utsi ntanyawa Ali kunja athawa ataba mbuzi kumalawi

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko 3 วันที่ผ่านมา

    Chikamabodza chabwela zotani kukamwa ngati manyi

    • @FrancisDay-br7xb
      @FrancisDay-br7xb 3 วันที่ผ่านมา

      Pain MCP

    • @user-yc3ik9dq3x
      @user-yc3ik9dq3x 2 วันที่ผ่านมา

      Dzidyani za magazizo. Mulungu akulangani nkhuku inu

    • @AminahMussah
      @AminahMussah 2 วันที่ผ่านมา

      ukatelo watumidwa nda nzako akuphawo

  • @CHIWSABINYAMBOSE
    @CHIWSABINYAMBOSE 3 วันที่ผ่านมา

    Ndichoipadi ichi chigawenga chabechabe