Asilikali a ku Malawi ndi ogona tulo zitsilu zimalimbana ndi anthu wamba usayelekeze kuvala kabudula wa makaka ndiye amaonesa mphamvu zawo ati wavala unform yawo mbudzi
Ntanyiwa iweyo ndi number one radio yako timainyadira kom athu athawa ziko lili rawo kom kumeneko moto kuti buuuuu mumtimamo angokhuta mphuma lokhalokha km mulimba Ntanyiwa woyeee
Ankolo ku malawi kulibe a silikali akanakhala kuti alipo zikuchita galu ameneyo mukumuti chokwerayu atamukhazika kale pansi, koma nawo asankha kugwirantchito ndi chipani ayiwala makamulo awo ndi mbuzi za silikali za manu pansi ndi mbuyao chakwerayo tionana chaka cha mawa onse amene akupha ndi chakwera tikhaulitsa boma ili lapita olo ataopseza motani zosatheka
Kodi inu apolice ndi asilikali ntchito yanu ndi chiyani kumalawiko? Kodi mukuyang'anila zika Zanu zikuphedwa Kodi inu ndinu apolice opanda ntchito pamodzi ndi iwe wa mkulu wa asilikali utule Pasi udindo coz your usiless man dammit asilikali inu achilungamo menyani nkhondo please
Chopweteka kwambiri ndi choti ndalama za nkhani nkhani zikuthela kulipira anthu a kunja amene zomwe akuchita mudziko lathu phindu lake opindula ndi ochepa
Inuyo mulungu adzingokuonjexelani moyo wautali basi ,chifukwa mukutimvetsa kukoma
Koma iweyo pokhapa pot awagwila ndakuimikila manja mwamba athuo agwidwad
Akulu akulu mukulankhula koma sitikumva 😢
We won't fear anything even as Zambian s were coming in Malawi guys to fight that evil man chakwela
Akatula udindo chakwerayo, azibale ake onse azachotsedwe ntchto. Galu watitopetsa
May God bless you comrade Ntanyiwa
I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa.
Koma chakwera wandikwana one day ndi kupedza people they call gringo
Komaso Mr ntanyiwa musalore Kuti anthu 8 amene agwidwawo asatuluke Ayi kufikila chakwela atule pansi udindo komaso dziko la South Africa asawapange rilizi Ayi kufikila lamampho atamuzenga mulandu chakwela
umakwana mtanyiwa tikuziwa zambili amalawi ambuye azikupasani moyo wautali 🎉🎉🎉🎉
Asilikali a ku Malawi ndi ogona tulo zitsilu zimalimbana ndi anthu wamba usayelekeze kuvala kabudula wa makaka ndiye amaonesa mphamvu zawo ati wavala unform yawo mbudzi
Mademo akayambire kumamfumu hotel komweko tiyeni tonse tikasokhane popo pa mfumu hotel ku ma room achulidwawo osaopa
Asilikari anthu ntchito yao ndi kuchinda mahule mutchesi umu😂😂
Umwa chani
Ntanyiwa iweyo ndi number one radio yako timainyadira kom athu athawa ziko lili rawo kom kumeneko moto kuti buuuuu mumtimamo angokhuta mphuma lokhalokha km mulimba Ntanyiwa woyeee
Nice mr ntanyiwa
Pano malawi ndi North Korea 😭😭😭
Apolici a malawi a kuzishipisa
Umakwana ya mtanyiwa tili nawenawe my brother
Apapa ndatanganidwa kuwerenga nkunvesera😂😂
Anthu nonse amene mukudana ndi nthanyiwa mitungati zoswera malambe inu zikukusangalasani mmene akuyendesela dzikoli gule wanuyi achoke alibe phindu
following you sir
kom mukutivetsa kukoma ndikapanda kuva uthenga kuchokela kwainu sindipuma bwino kod mudarikuti mosemunja
Anthu akumalawi umbuli, anachotsa peter, ati wabwino chakwera, pano akufuna peter yemwe uja, mmalawi wanzeru sakuyenera kupeleka vote ku president yemwe analephera kale, votelani atsopano osati apeter muthalika
Ankolo ku malawi kulibe a silikali akanakhala kuti alipo zikuchita galu ameneyo mukumuti chokwerayu atamukhazika kale pansi, koma nawo asankha kugwirantchito ndi chipani ayiwala makamulo awo ndi mbuzi za silikali za manu pansi ndi mbuyao chakwerayo tionana chaka cha mawa onse amene akupha ndi chakwera tikhaulitsa boma ili lapita olo ataopseza motani zosatheka
Ma activists athu musakhare chete kunoko akumangidwa mwachisisi mudziwe zimenezi, anthu osatchuka panopa Ali ku area 30 guyz,
Limpopo FM ineyo ndimachedwa Ku ntchito kuti ndimvere basi nkhani ZANU mumandidalitsa ine ndi m,ngoni weni weni more fire inuyo a Mr Ntanyiwa
Kuti muone ku mcp kuli anthu osaoneka bwino okhaokha pamaso ndionyasa ndi mtima momwe
Chonde AMalawi asatiphimbe maso BOMA ilili osalivera tiyeni pansewu week yamawa osaopa gayz 💪💪🛶🛶🏹🏹⚒️⛏️
Ndipo chakwera tidzachita kuotcha pamoto chifukwa chankhanza akuchitazi
Mumakwana
Zachamba basi dikilani 2025 vote yanu ndiye nuclear power osati zabibi zanuzi
nkhanga zaonaaa
Ntanyiwa woyeeeee
Comredy mtanyiwa tikufuna number yanu tizipephela Nanu mulungu azikudalisani kwambili ndipo azikutetezani kulikose komwe mukuyenda
❤Zowona acc muthu ameneyu AChoke
Chakwela ofuna adibwe kanyenya basi
Nde inu mukuganiza kut olo patabwera peteryo zinthu zingasinthe foundation ya Malawi kuvuta konseko ndi chipani Cha udf olo mutatani Malawi sazasintha
Ukanakhala kut mwina ukutiwuza munthu wozamuvotera koma nawenso ukumpangila peter kampen choti uziwe peter nayenso atatitopesa kale sitikunfunanso
Tisayembekezere kuti tingamve munthu wakuphayo kuti ndine ndapha mayz ?
Munona kt wakupha kufufuza chifkwa chomwe wina wafera koma atapha ndiyeyo ?
Mayankho ndiomwewa omwe tikumayankhulawa coz action ikuchitatu kuoneka yokha ndipo mwachindunji monga kumangidwa anthu then kulowesa zigawenga nde ngt akusakidwa anthuwa kuti aphedwe nde nkumat ena omwe adafa aja anafera zina ?
Mcp mukali kuyalukirayalukiratu
M C P -- Malawi Congress Party
M C P = Malawi Chikangawa Party 👹👹👹🔨⚒️⛏️
Asilikali Aku malawi ndi asilikadzi.west Africa asilikali sakunyengelela kulanda boma
Anthu amenewo ngat agwidwa aphedwe ndinthu cifukwa iwowo anabwela kuzapha
Boss mbuyomu munatiuza kuti athu aku German ofufuza ndege aja anali okonza miseu lero muti ndi aku butcher which is which
Big man?
Mwatukwana president 🤣🤣🤣🤣th-cam.com/video/WRDkQ8s_34k/w-d-xo.htmlsi=PkGoYsuJRKSW0v4p
Mmmh
Kodi inu apolice ndi asilikali ntchito yanu ndi chiyani kumalawiko? Kodi mukuyang'anila zika Zanu zikuphedwa Kodi inu ndinu apolice opanda ntchito pamodzi ndi iwe wa mkulu wa asilikali utule Pasi udindo coz your usiless man dammit asilikali inu achilungamo menyani nkhondo please
Ambuye tithandizeni Malawi waipa
Zoonad amalawi azimai tizingoyang'anira nyasizi bvuto azimai timatengrka ndi kathu kochepa
mademo mpanga komweko ku lilongwe ayi mkanya
Hahaha AAA, Malawi poison party, Wanthu anawa votera dala, bolani ife tiri kutali zina ukamva zina Leku kamba anga mwala.
😂😂😂😂😂 zabwino zonse wachita bwino wagwidwa tiakonzere konkuno
If what comrade is saying is the truth,then Chakwera must be the worst president in Southern Africa.
😂😂😂😂
Malawian kuwopa too much that’s why amakonda kulepheresa mademo so don’t tell us ngati muziwona zoti sizingatheke zochita mademo! Aaa why amakonda kulepheresa mademo
Limpopo FM ndi 1
😂😂😂
MCP Pamtumbo pawo ndithu
Chakwela ndikanankhala kuti ndimatha ufiti ndinakamchosa ineyo manyi akee anthu
Chitsilu chichakwela ndi family yake yonse ambuye tichotseleni munthuyi😊
Koma Malawi walowa chibwana chakwera anapita ku sukulu koma?pano akusekedwa ndi anthu akunja omwe
Koma chakwera anthawa wauyouyo mbwiyache.
It's time to figh now,osagona
Ku Malawi aku shooter ma movie rekani amenyane
Asilikira akumalawi ndi wopusa.
Chakwela ndigalu kwabasi
8:30 musova mcp ,mulithawa dziko mukulifuna
Ndichoipadi ichi chigawenga chabechabe
zinamizanani pano pa limpopo kwachwera ali pheee kukozanyasi zomwe inapanga dpp . alikuti anthu omwe agidwa aaa opusi mtanyiwa
Iwe mutuwako suyenda ngati akutuma a mcp anthu akufinya ndi chakwera wakoyo ngati akupasa ndalama ulibe manyazi wekha otsutsa pano aaaaaaaa ona kolowera
Following
😢😢😢😢😢😢😢😢
Chopweteka kwambiri ndi choti ndalama za nkhani nkhani zikuthela kulipira anthu a kunja amene zomwe akuchita mudziko lathu phindu lake opindula ndi ochepa
Ndipo kwambili eni dziko kumangosaukirabe
Number yotumizila zinthu kwantanyiwa plz
Atanyiwa pathako pako
Yess
Zowonadi mchutsuludi chimenechi
Inu amenewo mungodziyankha nokha muli phee kugwiritsidwa ntchito ndi agaluwo 🥺mxieuw
Achakwera vomelezani😂
Am waiting good news not bad news 😔😔😔😔😔
Chakwera atha ngati Idi amin sizimuthera bwino ndithu.
Ndikut mambodza akowa Pali ine no comment ndizopusa zakozo tithana phwanga galimoto uma user ija nditha kukutumizira komaso pachikwangwani umakonda kucheza paj okay
Mwapemphedwa kutu mupange comment?
😢
Mbudzi iwe uthana ndindani usawone ngat ndife ogona wamva panyo pako
Chigawenga iwe chimunthu chopanda phindu chitsilu ulibe manyazi mulungu akukanthan
Anthu achoka Kuti iwe nawendimbuzi kwambiri ukukofuna kusokoneza amalawi ,chifukwa amalawi ndiopepera kale ndiye azikuvera nyasi zako sata yako
Paja ninakuwuza kale kuti upite kumalawi mabodza akowo mtanyiwa yiweyo niamene ukumasokoneza anthu infe timapeleka ulemu kwa boni kalindo osati mbuziyiweyo ayi
Muyiyambe muwone utsi ntanyawa Ali kunja athawa ataba mbuzi kumalawi
Chikamabodza chabwela zotani kukamwa ngati manyi
Pain MCP
Dzidyani za magazizo. Mulungu akulangani nkhuku inu
ukatelo watumidwa nda nzako akuphawo
Ndichoipadi ichi chigawenga chabechabe