Sitiopa wokupha thupi koma timaopa mulungu amene amapha thupi ndi mzimu. Ondikumbila dzenje agwelamo yekha. Mulungu wa Daniel, shadreck, mishel and abdenego will protect onse amene mayina awo Ali pa list.
Oh Lord have mercy on us Malawians Tipulumutseni ambuyeeeee ............Mbuzi ikakondwa kwambiriiii amalonda alipafupi la 40 likudzaaaaaaaa list mwayikayo ikhala yanuuuuu anthu akupha amagazi m'manja inu
aziwombere yekha lazalo wa ku kasiya ndi a zinzake onse, kuyambila zikhale, chimwendo kukunyu ndi agututu a thakati onse a congress. BRR brrrrr pha pha pha, comarde mumakwana boss.🤣🤣🤣🤣🤣🤣
Muwamve Mai kaliyati mmene anayankhulira kumaliro a LUCIUS BANDA kumuyamikira president kut ankamuthandiza Lucius,pomwe Lucius wavutika kwambiri mmoyowu.i will never trust politicians.kulira konsekuja,lero akufuna alemerere pa imfa ya chilima.Amai awawa apapa ndiye azionongera mbiri .Akufuna awanamize aMalawi.
Koma Chakwera zoti kuli Court la ICC lomwe limathana ndi ma President aku Africa akuziziwa Mr President becareful kunali ma President a mphavu kunjaku koma anaphedwa enaso anali okondedwa ndi anthu awo osati inu
Mr Chikangawa Chakwera Bp yakwera kale kuti muulura chani 😅😅😅😂😂😂😂yomweyo galu iwe
Osamasowa antanyiwa please 😊
I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa God bless you all the time.
Loud n clear from Johannesburg
Sitiopa wokupha thupi koma timaopa mulungu amene amapha thupi ndi mzimu.
Ondikumbila dzenje agwelamo yekha.
Mulungu wa Daniel, shadreck, mishel and abdenego will protect onse amene mayina awo Ali pa list.
Koma ndaseka ngati zabwino 😂😂😂 athu onsewo akaphedwa nde iwo adzawina zisakho Kom hahahaaaaa chakwera akunama kwambiri kumwamba kukanena kuti kwatha ndi kwatha basi paribeso zoti apha muthu wina a ntanyiwa dzikoli silachakwera ndalama sizingamupindulire komaso paribe zoti anga gure chipani paribe yemwe afuna achoke komaso akaliyati sangalore mudzina layesu ndikuti patibe zoti muthu anga gure chipani awo akalandira ndalama ndizawo za kunyumba kwao and olo apatse ndalama kakiyati olo adzalandira koma chilungamo chisitha chimakhalabe chilungamo ndinaonera esau ndi abere choipa chitsata mwini MLUNGU WATHU SALEPHERA
We are here already comrade ✌️
Zakwanitsa tate akuona zonse
Yehova akuona chilichonse afa yekha
ose amene ankufunna kuphedwa mulungu salolla mashall Allah bless you always
The best Radio station in the world. Big up Comrade
Good morning, welcome back tinakusowani tinayamba kudandaura
I salute Comrade ntanyiwa,, ndiye titani Comrade amalawi tiyen titengen gawo tipemphere kwambiri
Koma kukhala anthu Ku Malawi. Koma chakwelà azatha ngati ma curtain.
I ❤ this program
Comrade am 100% support u always ing'alure fadah
Koma dziko lathu tinalozedwa bas zoona kumuopa chakwela kamuthu kamodzi tiyen tipange ngat ku Kenya please zausilu zikuchitikazi
Pemphelo rathu ndichida chomwe timangonjesera adani zenje akuwakumbira athu onseo agweramo onse akupereka mayina awathu osarakwa imfa akunenayo atamwalire ndiwo 2025 isanafike mulungu akuona
Oh Lord have mercy on us Malawians
Tipulumutseni ambuyeeeee ............Mbuzi ikakondwa kwambiriiii amalonda alipafupi la 40 likudzaaaaaaaa list mwayikayo ikhala yanuuuuu anthu akupha amagazi m'manja inu
Ntanyiwa wadzuka bwanji kumeneko ifetu tilibwino ndithu tiye nazoni
Ndikamava kanyimboko ndiye ndimasangarara ndimazdziwa kuti chirungamo chirimunjira
Muzina la yesu christu achakwera kungopha modzi muziona ndithuuu😭😭😭😭
Angozinamiza anthu onsewa Mulungu sangalore kuti aphedwe.
You are our head lamp Mr Mntanyinya tipempha mayiko ena atithandize kuchotsa president okuphayu
long live Mtanyiwa here in capetown i support you❤
Amalawi kumudziko tadzukani mumchotse chakwelayo......dziko silake
Lord have Mercy
Waying'alura kuno mtanyiwa
Atchela kumawa nkhangazaona anyanayo
We love you comrade ..tell us more
We're always with you buddy Ntanyiwa.♥️🔥🔥
😂😂😂😂😂 nde mcp itsala yokhatu nanga anthu osewo akawapha ku opposition kudzakhala ndan mcp muzitenge bwino zithuzi vuto mwakhalitsa padzuwa muli kotsutsa😅😅😅😅😅😅😅😅
Long liveNtanyiwa
Comrade ntanyiwa ..great man ft kalindooooo
My gracious heavenly Father have mercy on Malawians
Okhesa mwazi yehova sakondwera naye olo nyama ikatero
Mulungu amapereka Chicano paizo
I salute you comrade!
GOD bress u Mr mtanyiwahhh!!
Antanyiwa nlipo abale osamasowa chonchi
Iwe chakwela Mano kuyipa ngati nyemba ya pa nyini ya Monica wako uyo usatibowe ife
Mtanyiwwa ulemu wanuw mulungu adalise wina aliyese astaguffllal yha Allah thallah brother
Timakunyadilani Mr Mtanyiwa koma za anthu ogwidwa pa Bedbrig Ili pat naosotu akanapita Maliro kwao kumalawi iya
Ndipo galu ameneyo siomuchula kuti mr iyayi chakwera akufuna amalawi atani 😂😂😂
aziwombere yekha lazalo wa ku kasiya ndi a zinzake onse, kuyambila zikhale, chimwendo kukunyu ndi agututu a thakati onse a congress. BRR brrrrr pha pha pha, comarde mumakwana boss.🤣🤣🤣🤣🤣🤣
Achakwera ku state house atawako posachedwapa
Muwamve Mai kaliyati mmene anayankhulira kumaliro a LUCIUS BANDA kumuyamikira president kut ankamuthandiza Lucius,pomwe Lucius wavutika kwambiri mmoyowu.i will never trust politicians.kulira konsekuja,lero akufuna alemerere pa imfa ya chilima.Amai awawa apapa ndiye azionongera mbiri .Akufuna awanamize aMalawi.
Iiiii ndiye atipha tonsetu
Am just a Malawian but my president is Traore..on my DP😅😅😅
Nice 👍 nndinakusowani
Amtanyiwa bwanji Kodi odio sikumveka bwinotu
WHEN YOU ARE PLAYING THE MUSIC OR OTHER VOICES WE CAN NOT HEAR CLEAR PLS TELL YOUR TEACHINIAN
Koma mulipo a Ntanyiwa, mulibwanji kumeneko
Mukamachedwa kupanga post timakhala ndi nkhawa
Kut chachitika chan
Lipopo support ❤ 💙
Apa bet bridge aja awafinye especially waku MALAWI athane naye ndi opusa
Mmmmmmm ayi zagawana ku mitunduzo ayi....usatinamize ingonena zoooyenera kunenazo....timakutsat Ra mwachidwi...km zotigawanisazo sitilora...tonse nda Malawi ndipo palibe adzatigawanisa
Zosatheka athu APHA Aja sanakwane BaiBulo Linati okumba zenje agwelemo yekha ndiiiiiiithu amene watenga gawo lokupha athu amenewa agweramo okhaaaaa ambuye invani simunawalenge athu Kuti azuzike paziko pano inu mukule Ife tichepe
Mr Chakwera pamtumbo panu ndinthu
Nsembe yomwe inapelekedwa zaka zapitazo ya ufulu chakwera waipangisa expire akufuna mwazi wina otchuluka
Komatu kulimbana ndi aNtanyiwa kuzipusisa ndithu. Awa ndi akatundu omangidwa ndizitsulo. Mbambande.
anthu onsewo awakwanitsa koma Mulungu wake waliyenseyu aaaa
Palibe so kuphedwa apa Inu ambuye akukutetezerani a ntanyiwa ndi azinzanu onse timakuikizani mmapephero
Koma Chakwera zoti kuli Court la ICC lomwe limathana ndi ma President aku Africa akuziziwa
Mr President becareful kunali ma President a mphavu kunjaku koma anaphedwa enaso anali okondedwa ndi anthu awo osati inu
Lipopo ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤❤❤❤
Okupha nayeso azafa... palibe kuopa mcp ndi azitsogoreli ikagwere
God is able
a comrade yobu 13;13 yakhulani mosaopa
futi yomwe akufuna aphere azawo apita ndi iwoo mulungu simunthu
Ing'alureni fadah
Mulungu sichejemu auzeni
❤❤
Tinakusowani Boss
🎉🎉🎉🎉🎉🎉
💥💥💥💥
Nthatha za njaladi
Zosatheka osewo kafu olo atalimbikila bwanji
👍👍👍👍🤝🤝🤝🤝👍
Chilango
Koma chakwela eeee
Komatuu tili pa ululu eeeeee
MCP or chakwela si mulungu agalu amenewa atikwana dzene 2025 kwatalika dzedi asanephe anthu ofunika MOTI PAKANGOFA MUNTHU WINATSO CHILIMA NDI ANTHU 8 AJA AKWANA chifukwa ife amalawi sitimakhulupila kuti MCP yokupha timati yakele yija iyi ya wong"ono ung'onu KOMA PANO ALIYETSE WAWONA YEKHA KUTI MCP YAMAGADZI NDINTHU
Wina watukwana chakwera uku 😂😂th-cam.com/video/WRDkQ8s_34k/w-d-xo.htmlsi=r_3Qm9tNpQwXfR0D