LIMPOPO FM WITH COMRADE NTANYIWA USIKU wathawu

แชร์
ฝัง

ความคิดเห็น • 83

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 3 หลายเดือนก่อน +3

    Mr Chikangawa Chakwera Bp yakwera kale kuti muulura chani 😅😅😅😂😂😂😂yomweyo galu iwe

  • @MikeKanyaza-bm5tp
    @MikeKanyaza-bm5tp 3 หลายเดือนก่อน +3

    Osamasowa antanyiwa please 😊

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 3 หลายเดือนก่อน

    I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa God bless you all the time.

  • @CostanceLalli
    @CostanceLalli 2 หลายเดือนก่อน +1

    Loud n clear from Johannesburg

  • @meganabigail-ye7fw
    @meganabigail-ye7fw 3 หลายเดือนก่อน +1

    Sitiopa wokupha thupi koma timaopa mulungu amene amapha thupi ndi mzimu.
    Ondikumbila dzenje agwelamo yekha.
    Mulungu wa Daniel, shadreck, mishel and abdenego will protect onse amene mayina awo Ali pa list.

  • @GanizaniKamvazaana
    @GanizaniKamvazaana 3 หลายเดือนก่อน +3

    Koma ndaseka ngati zabwino 😂😂😂 athu onsewo akaphedwa nde iwo adzawina zisakho Kom hahahaaaaa chakwera akunama kwambiri kumwamba kukanena kuti kwatha ndi kwatha basi paribeso zoti apha muthu wina a ntanyiwa dzikoli silachakwera ndalama sizingamupindulire komaso paribe zoti anga gure chipani paribe yemwe afuna achoke komaso akaliyati sangalore mudzina layesu ndikuti patibe zoti muthu anga gure chipani awo akalandira ndalama ndizawo za kunyumba kwao and olo apatse ndalama kakiyati olo adzalandira koma chilungamo chisitha chimakhalabe chilungamo ndinaonera esau ndi abere choipa chitsata mwini MLUNGU WATHU SALEPHERA

  • @JosephHill-fy1bb
    @JosephHill-fy1bb 3 หลายเดือนก่อน +6

    We are here already comrade ✌️

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj 3 หลายเดือนก่อน +1

    ose amene ankufunna kuphedwa mulungu salolla mashall Allah bless you always

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 2 หลายเดือนก่อน

    The best Radio station in the world. Big up Comrade

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 3 หลายเดือนก่อน +1

    Good morning, welcome back tinakusowani tinayamba kudandaura

  • @PreciousChlima
    @PreciousChlima 2 หลายเดือนก่อน

    I salute Comrade ntanyiwa,, ndiye titani Comrade amalawi tiyen titengen gawo tipemphere kwambiri

  • @VaseleMsiska
    @VaseleMsiska 3 หลายเดือนก่อน +2

    Koma kukhala anthu Ku Malawi. Koma chakwelà azatha ngati ma curtain.

  • @simonpaul6567
    @simonpaul6567 3 หลายเดือนก่อน +1

    I ❤ this program

  • @DaitonKabila
    @DaitonKabila 3 หลายเดือนก่อน

    Comrade am 100% support u always ing'alure fadah

  • @RaheemMogoya
    @RaheemMogoya 3 หลายเดือนก่อน +1

    Koma dziko lathu tinalozedwa bas zoona kumuopa chakwela kamuthu kamodzi tiyen tipange ngat ku Kenya please zausilu zikuchitikazi

  • @BraghtYohane
    @BraghtYohane 3 หลายเดือนก่อน +1

    Pemphelo rathu ndichida chomwe timangonjesera adani zenje akuwakumbira athu onseo agweramo onse akupereka mayina awathu osarakwa imfa akunenayo atamwalire ndiwo 2025 isanafike mulungu akuona

  • @MebleNgulinga-hi6rg
    @MebleNgulinga-hi6rg 3 หลายเดือนก่อน

    Oh Lord have mercy on us Malawians
    Tipulumutseni ambuyeeeee ............Mbuzi ikakondwa kwambiriiii amalonda alipafupi la 40 likudzaaaaaaaa list mwayikayo ikhala yanuuuuu anthu akupha amagazi m'manja inu

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg 3 หลายเดือนก่อน +1

    Ntanyiwa wadzuka bwanji kumeneko ifetu tilibwino ndithu tiye nazoni

  • @SamukLungu-zg7fl
    @SamukLungu-zg7fl 3 หลายเดือนก่อน +1

    Ndikamava kanyimboko ndiye ndimasangarara ndimazdziwa kuti chirungamo chirimunjira

  • @PreciousChlima
    @PreciousChlima 2 หลายเดือนก่อน +1

    Muzina la yesu christu achakwera kungopha modzi muziona ndithuuu😭😭😭😭

  • @modestamhango7737
    @modestamhango7737 3 หลายเดือนก่อน +1

    Angozinamiza anthu onsewa Mulungu sangalore kuti aphedwe.

  • @JamesDaud-jz7uq
    @JamesDaud-jz7uq 3 หลายเดือนก่อน

    You are our head lamp Mr Mntanyinya tipempha mayiko ena atithandize kuchotsa president okuphayu

  • @AbdullahBnp-l8m
    @AbdullahBnp-l8m 3 หลายเดือนก่อน

    long live Mtanyiwa here in capetown i support you❤

  • @MustafaAbdullah-pb5zv
    @MustafaAbdullah-pb5zv 3 หลายเดือนก่อน +1

    Amalawi kumudziko tadzukani mumchotse chakwelayo......dziko silake

  • @sulleahmnyimbili1362
    @sulleahmnyimbili1362 3 หลายเดือนก่อน +1

    Lord have Mercy

  • @AnusaNkhoma
    @AnusaNkhoma 3 หลายเดือนก่อน +1

    Waying'alura kuno mtanyiwa

  • @sparkdymon3429
    @sparkdymon3429 3 หลายเดือนก่อน +1

    Atchela kumawa nkhangazaona anyanayo

  • @Nelsonmatenda
    @Nelsonmatenda 3 หลายเดือนก่อน

    We love you comrade ..tell us more

  • @DaveDambo
    @DaveDambo 3 หลายเดือนก่อน

    We're always with you buddy Ntanyiwa.♥️🔥🔥

  • @louismagongwa
    @louismagongwa 2 หลายเดือนก่อน +2

    😂😂😂😂😂 nde mcp itsala yokhatu nanga anthu osewo akawapha ku opposition kudzakhala ndan mcp muzitenge bwino zithuzi vuto mwakhalitsa padzuwa muli kotsutsa😅😅😅😅😅😅😅😅

  • @SydneySibande-z6k
    @SydneySibande-z6k 3 หลายเดือนก่อน +1

    Long liveNtanyiwa

  • @DarwinBobot
    @DarwinBobot 3 หลายเดือนก่อน

    Comrade ntanyiwa ..great man ft kalindooooo

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 3 หลายเดือนก่อน

    My gracious heavenly Father have mercy on Malawians

  • @LouisKanje
    @LouisKanje 3 หลายเดือนก่อน

    Okhesa mwazi yehova sakondwera naye olo nyama ikatero
    Mulungu amapereka Chicano paizo

  • @mathewsmdzanja3276
    @mathewsmdzanja3276 3 หลายเดือนก่อน

    I salute you comrade!

  • @GiftMlinde
    @GiftMlinde 3 หลายเดือนก่อน

    GOD bress u Mr mtanyiwahhh!!

  • @PetroMatias
    @PetroMatias 3 หลายเดือนก่อน +1

    Antanyiwa nlipo abale osamasowa chonchi

  • @CharlesmakveliNyirenda
    @CharlesmakveliNyirenda 2 หลายเดือนก่อน +1

    Iwe chakwela Mano kuyipa ngati nyemba ya pa nyini ya Monica wako uyo usatibowe ife

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj 3 หลายเดือนก่อน

    Mtanyiwwa ulemu wanuw mulungu adalise wina aliyese astaguffllal yha Allah thallah brother

  • @MerryWayson
    @MerryWayson 3 หลายเดือนก่อน

    Timakunyadilani Mr Mtanyiwa koma za anthu ogwidwa pa Bedbrig Ili pat naosotu akanapita Maliro kwao kumalawi iya

  • @MariamJaffali
    @MariamJaffali 3 หลายเดือนก่อน

    Ndipo galu ameneyo siomuchula kuti mr iyayi chakwera akufuna amalawi atani 😂😂😂

  • @originalblack100
    @originalblack100 2 หลายเดือนก่อน

    aziwombere yekha lazalo wa ku kasiya ndi a zinzake onse, kuyambila zikhale, chimwendo kukunyu ndi agututu a thakati onse a congress. BRR brrrrr pha pha pha, comarde mumakwana boss.🤣🤣🤣🤣🤣🤣

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja 3 หลายเดือนก่อน +1

    Achakwera ku state house atawako posachedwapa

  • @cynthiakananji1608
    @cynthiakananji1608 3 หลายเดือนก่อน

    Muwamve Mai kaliyati mmene anayankhulira kumaliro a LUCIUS BANDA kumuyamikira president kut ankamuthandiza Lucius,pomwe Lucius wavutika kwambiri mmoyowu.i will never trust politicians.kulira konsekuja,lero akufuna alemerere pa imfa ya chilima.Amai awawa apapa ndiye azionongera mbiri .Akufuna awanamize aMalawi.

  • @MeliaMichael
    @MeliaMichael 2 หลายเดือนก่อน +1

    Iiiii ndiye atipha tonsetu

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus 3 หลายเดือนก่อน

    Am just a Malawian but my president is Traore..on my DP😅😅😅

  • @kondwaniwhite2871
    @kondwaniwhite2871 3 หลายเดือนก่อน

    Nice 👍 nndinakusowani

  • @HusseinMoffatt-mi1fl
    @HusseinMoffatt-mi1fl 3 หลายเดือนก่อน

    Amtanyiwa bwanji Kodi odio sikumveka bwinotu

  • @leonardjika2100
    @leonardjika2100 3 หลายเดือนก่อน

    WHEN YOU ARE PLAYING THE MUSIC OR OTHER VOICES WE CAN NOT HEAR CLEAR PLS TELL YOUR TEACHINIAN

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma 2 หลายเดือนก่อน

    Koma mulipo a Ntanyiwa, mulibwanji kumeneko

  • @ZionekaMember
    @ZionekaMember 3 หลายเดือนก่อน

    Mukamachedwa kupanga post timakhala ndi nkhawa
    Kut chachitika chan

  • @JummahNelson
    @JummahNelson 2 หลายเดือนก่อน

    Lipopo support ❤ 💙

  • @LeonardMhone-cg1tk
    @LeonardMhone-cg1tk 3 หลายเดือนก่อน

    Apa bet bridge aja awafinye especially waku MALAWI athane naye ndi opusa

  • @CharlesPhiri-ds1rk
    @CharlesPhiri-ds1rk 3 หลายเดือนก่อน

    Mmmmmmm ayi zagawana ku mitunduzo ayi....usatinamize ingonena zoooyenera kunenazo....timakutsat Ra mwachidwi...km zotigawanisazo sitilora...tonse nda Malawi ndipo palibe adzatigawanisa

  • @AgathaJerard
    @AgathaJerard 2 หลายเดือนก่อน

    Zosatheka athu APHA Aja sanakwane BaiBulo Linati okumba zenje agwelemo yekha ndiiiiiiithu amene watenga gawo lokupha athu amenewa agweramo okhaaaaa ambuye invani simunawalenge athu Kuti azuzike paziko pano inu mukule Ife tichepe

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d 3 หลายเดือนก่อน

    Mr Chakwera pamtumbo panu ndinthu

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 3 หลายเดือนก่อน

    Nsembe yomwe inapelekedwa zaka zapitazo ya ufulu chakwera waipangisa expire akufuna mwazi wina otchuluka

  • @kamwazabonomali825
    @kamwazabonomali825 3 หลายเดือนก่อน

    Komatu kulimbana ndi aNtanyiwa kuzipusisa ndithu. Awa ndi akatundu omangidwa ndizitsulo. Mbambande.

  • @AminahMussah
    @AminahMussah 3 หลายเดือนก่อน

    anthu onsewo awakwanitsa koma Mulungu wake waliyenseyu aaaa

  • @ElizabethKazambwe
    @ElizabethKazambwe 3 หลายเดือนก่อน

    Palibe so kuphedwa apa Inu ambuye akukutetezerani a ntanyiwa ndi azinzanu onse timakuikizani mmapephero

  • @ZionekaMember
    @ZionekaMember 3 หลายเดือนก่อน +1

    Koma Chakwera zoti kuli Court la ICC lomwe limathana ndi ma President aku Africa akuziziwa
    Mr President becareful kunali ma President a mphavu kunjaku koma anaphedwa enaso anali okondedwa ndi anthu awo osati inu

  • @JummahNelson
    @JummahNelson 2 หลายเดือนก่อน

    Lipopo ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤❤❤❤

  •  3 หลายเดือนก่อน

    Okupha nayeso azafa... palibe kuopa mcp ndi azitsogoreli ikagwere

  • @RobertFegstone-v3g
    @RobertFegstone-v3g 3 หลายเดือนก่อน

    God is able

  • @JogaJoseph
    @JogaJoseph 3 หลายเดือนก่อน

    a comrade yobu 13;13 yakhulani mosaopa

  • @MissiPhiri-h3w
    @MissiPhiri-h3w 3 หลายเดือนก่อน

    futi yomwe akufuna aphere azawo apita ndi iwoo mulungu simunthu

  • @EvanceKasankha
    @EvanceKasankha 3 หลายเดือนก่อน

    Ing'alureni fadah

  • @edmorswalley6663
    @edmorswalley6663 3 หลายเดือนก่อน

    Mulungu sichejemu auzeni

  • @VanessaGwangwa
    @VanessaGwangwa 3 หลายเดือนก่อน

    ❤❤

  • @PatrickMtira
    @PatrickMtira 3 หลายเดือนก่อน

    Tinakusowani Boss

  • @AminAbbasi-xc4qk
    @AminAbbasi-xc4qk 3 หลายเดือนก่อน

    🎉🎉🎉🎉🎉🎉

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg 3 หลายเดือนก่อน

    💥💥💥💥

  • @ChiefJustin-cl8jl
    @ChiefJustin-cl8jl 3 หลายเดือนก่อน

    Nthatha za njaladi

  • @Jasonnyatwa
    @Jasonnyatwa 3 หลายเดือนก่อน

    Zosatheka osewo kafu olo atalimbikila bwanji

  • @PetroMatias
    @PetroMatias 3 หลายเดือนก่อน

    👍👍👍👍🤝🤝🤝🤝👍

  • @LouisKanje
    @LouisKanje 3 หลายเดือนก่อน

    Chilango

  • @ArnoldBinali
    @ArnoldBinali 3 หลายเดือนก่อน

    Koma chakwela eeee

  • @Uncle_B265
    @Uncle_B265 3 หลายเดือนก่อน

    Komatuu tili pa ululu eeeeee

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 3 หลายเดือนก่อน

    MCP or chakwela si mulungu agalu amenewa atikwana dzene 2025 kwatalika dzedi asanephe anthu ofunika MOTI PAKANGOFA MUNTHU WINATSO CHILIMA NDI ANTHU 8 AJA AKWANA chifukwa ife amalawi sitimakhulupila kuti MCP yokupha timati yakele yija iyi ya wong"ono ung'onu KOMA PANO ALIYETSE WAWONA YEKHA KUTI MCP YAMAGADZI NDINTHU

  • @mipeacemakermw9501
    @mipeacemakermw9501 3 หลายเดือนก่อน

    Wina watukwana chakwera uku 😂😂th-cam.com/video/WRDkQ8s_34k/w-d-xo.htmlsi=r_3Qm9tNpQwXfR0D