Bon Kalindo Response To H E Chakwera's SONA.

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 8 ก.พ. 2024
  • His Excellency the President Dr Lazarus Chakwera was at Parliament in Lilongwe to make his State of the Nation Address (SONA) and here is what Bon Kalindo had to say about it.
    Olemekezeka a President Dr Lazarus Chakwera anali ku Nyumba ya Malamulo ku Lilongwe kukakamba nkhani ya boma la dziko lino (SONA) ndipo izi ndi zomwe Bon Kalindo ananena pankhaniyi.
    Note: We Apologize, we mentined in the intro that Bakili Muluzi TV had a copy of the but it turns out they too do not have the full copy. Tikayipeza we will post it or tikupatsani Link kuti nanunso muyimvele.

ความคิดเห็น • 120

  • @nyasavoicebox
    @nyasavoicebox  5 หลายเดือนก่อน +5

    Note: We Apologize, we mentioned in the intro that Bakili Muluzi TV had an Audio/Visual copy of the SONA but it turns out they too do not have the full copy. Tikayipeza we will post it or tikupatsani Link kuti nanunso muyimvele. If you would like get the PDF version please email us at nyasavoicebox@gmail.com and we will make that available to you.

    • @ChrispinMpando
      @ChrispinMpando 5 หลายเดือนก่อน

      😊😊😊😊😊

  • @munashemoyo4190
    @munashemoyo4190 5 หลายเดือนก่อน +8

    Ine ndye saname president uyu amandinyasa zed since kulowa boma mbudzi

  • @ephraimkadamika
    @ephraimkadamika 5 หลายเดือนก่อน +1

    Mwana owopsya kwambiri ❤❤ the Dc

  • @GRACIOUSKENAN
    @GRACIOUSKENAN หลายเดือนก่อน

    The king master, the DC bon kalindo

  • @gladysbonongwe1038
    @gladysbonongwe1038 5 หลายเดือนก่อน

    Thank you Mr kalindo

  • @user-is5dl7np9g
    @user-is5dl7np9g 5 หลายเดือนก่อน +4

    Ine ndiye chakwera wandikwana😮😮

    • @giftdulamkalenga7344
      @giftdulamkalenga7344 5 หลายเดือนก่อน

      Ndipo opha, chakwera pano angakhale herooo

    • @user-jk8sh7fh2d
      @user-jk8sh7fh2d 5 หลายเดือนก่อน

      Empty brain

    • @user-jk8sh7fh2d
      @user-jk8sh7fh2d 5 หลายเดือนก่อน

      Koma analidi m'busa uyu ? Fuso zikupeleka pic yanji ya azitumiki achauta. This is are bad people not all 90%bad 10 are good.

  • @Bkathira
    @Bkathira 5 หลายเดือนก่อน

    Nice one Mr DC waiting ma Demo

  • @user-dt8nr1zx6e
    @user-dt8nr1zx6e 5 หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤❤❤ Bon kalindo
    Mawu amenewo

  • @BunayaJafali
    @BunayaJafali 5 วันที่ผ่านมา

    Bon!!!!! Kalindooooo 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @user-xo5mq7wl7t
    @user-xo5mq7wl7t 5 หลายเดือนก่อน

    A KALINDO KEEP IT UP

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 5 หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤❤❤ mr bon kalindo

  • @MphatsoDuncan-gh2vc
    @MphatsoDuncan-gh2vc 5 หลายเดือนก่อน +1

    Fire

  • @oliviamphande1900
    @oliviamphande1900 5 หลายเดือนก่อน +1

    Waiting ma demo Mr bon kalindo

  • @TiyaMtete
    @TiyaMtete 5 หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤❤Mr bon kalindo

  • @charlurquhart5788
    @charlurquhart5788 5 หลายเดือนก่อน +1

    Akanakhalako anthu ten kumalawi ngati born kalindo pano kumalawi kutasintha akapange kwa mache ximenezo galu ameneyo

  • @user-pu3sb2xw6z
    @user-pu3sb2xw6z 5 หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤Kalindo

  • @dingim1234
    @dingim1234 5 หลายเดือนก่อน

    Those who don't value their words, will never value your wishes.

  • @user-jp2qg2ww7r
    @user-jp2qg2ww7r 5 หลายเดือนก่อน

    Dc❤❤

  • @user-mk7fh5ml8s
    @user-mk7fh5ml8s 5 หลายเดือนก่อน

    Umakwana DC❤❤❤

  • @thefather007
    @thefather007 5 หลายเดือนก่อน

    🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉the dc!!!!!!!!!!!!!!!!!!!! Umakwanatu

  • @charlurquhart5788
    @charlurquhart5788 5 หลายเดือนก่อน

    ❤born kalindo ndikukanika kupta kwathu kumalawi chifukwa cha Boma iri mmm ai

    • @user-vm7iz6oz6r
      @user-vm7iz6oz6r 4 หลายเดือนก่อน

      Ngakhareso ine mmm galu uyu

  • @user-jw5rx9ze8k
    @user-jw5rx9ze8k 5 หลายเดือนก่อน

    The DC ❤

  • @PreciousHenderson-qc1hq
    @PreciousHenderson-qc1hq 4 หลายเดือนก่อน

    God guide malawi🎉❤

  • @IsaacPhakaya
    @IsaacPhakaya 6 วันที่ผ่านมา

    Mwanaa opsa kwambili Bon kalindo

  • @user-qy5sh4di7t
    @user-qy5sh4di7t 5 หลายเดือนก่อน

    Iya

  • @user-xv5pr3ji6w
    @user-xv5pr3ji6w 5 หลายเดือนก่อน +1

    A chakwera zikufunika musazike ndithu inuyo nthawi yanu yatha,.. ine patrick nampota, South Africa

  • @giftdulamkalenga7344
    @giftdulamkalenga7344 5 หลายเดือนก่อน

    Dc plz come tulusa ndodo

  • @HildatoweraMhango-et4mz
    @HildatoweraMhango-et4mz 5 หลายเดือนก่อน +1

    Pa campagn ndi chilima anatiuza kale kuti adzamanga airtell yabwino

  • @user-oo5bx1rl3j
    @user-oo5bx1rl3j 5 หลายเดือนก่อน

    Nkhani yaikulu a bwana president Boni Kalindo monga athu amene mukutiimilira ifeyo anthu osauka. Ndimaona ngati kuti akawakana mai Mary Navitcha kuti akhale leader of opposition; ndimaona ngati kuti inuyo ndi gulu la Malawi First. Mungopita ku court kukatenga injunction chifukwa MCP ikuwadelera a Malawi kwambili. Kulibwino parliament imeneyi ingoimitsidwapo. Chifukwa anthuwa akuwatola a Malawi ngati alibe tsogoleli monga inuyo bwana Boni Kalindo. Thanks mr President Boni Kalindo

  • @ThandieWaMalungaseda-rd1bg
    @ThandieWaMalungaseda-rd1bg 5 หลายเดือนก่อน +2

    Chilungamo chenicheni

  • @AlickNdeketeya
    @AlickNdeketeya 5 หลายเดือนก่อน

    Ku gaza

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 5 หลายเดือนก่อน +1

    Tidya chizungu chachakwera chaka chino

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 5 หลายเดือนก่อน +1

    DC ndimunthu wachilungamo anthu wotere ndi amene akufunika ku parliament

  • @user-ec3xh4pc6t
    @user-ec3xh4pc6t 5 หลายเดือนก่อน

    Wawa ambwiye

  • @abdulirichard260
    @abdulirichard260 5 หลายเดือนก่อน

    viva D.C. ❤❤❤

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 5 หลายเดือนก่อน +1

    Chakwela mulungu adzamulanga kwambili chifukwa athu akuzuzika ndipo athu akufa ndi njala

  • @HappyMwase-w7f
    @HappyMwase-w7f 11 วันที่ผ่านมา

    szilimbino dzikolawola

  • @PrinceMapemba-fn4cw
    @PrinceMapemba-fn4cw 5 หลายเดือนก่อน

    One day will bath together at state house 😎😎😎

  • @PreciousHenderson-qc1hq
    @PreciousHenderson-qc1hq 4 หลายเดือนก่อน

    Viva malawi Viva malawi

  • @AllanCharlesNgona-wm5xs
    @AllanCharlesNgona-wm5xs 4 หลายเดือนก่อน

    Mr kalindo ❤❤❤😂😂😂😂😂😂😂😂 neco

  • @custommantchombe-rn1oo
    @custommantchombe-rn1oo 5 หลายเดือนก่อน

    The kalindo DC ....Umatha

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r 4 หลายเดือนก่อน +1

    Koma chakwera amalingalira kt azafa ndikukakuman ndi fum ya mafum?mm koma ukuxuza ndithu

  • @user-qw4pk7wj8i
    @user-qw4pk7wj8i 5 หลายเดือนก่อน +1

    Ndithandizeni guys liu lot DR wakuti limatanthauzanji anzathu mumatha kuona dictionary

    • @user-to8pv7ph9g
      @user-to8pv7ph9g 5 หลายเดือนก่อน

      It stands for Doctor, mainly used in health field like physician,or with phd.just an abbreviation like, Mr which stands for mister.

  • @paulpaseli6310
    @paulpaseli6310 5 หลายเดือนก่อน +1

    Achakwela tikufa ndi njala komwe tikupita basi musala nokha

  • @JonesChingaya-yf4gg
    @JonesChingaya-yf4gg 5 หลายเดือนก่อน +3

    Mbewu iyiyi ya Chakwera yi isazabwerenso yatizunza ngat tili mu chipani chimodzi.

  • @eliasmgala8469
    @eliasmgala8469 5 หลายเดือนก่อน

    Akuluwa ndale zawalowa kwambiri. Angokhala leader of opposition basi

  • @user-qm1qb2jp4s
    @user-qm1qb2jp4s 5 หลายเดือนก่อน

    Ndipo chakwera palibe chilipo ine ndie wa kwa gwanda chakuambayo ndi bodza kwathu sanaikeko nseu DPP ndi lomwe idzakonze nseu

  • @BrazioBauleni-sq9pu
    @BrazioBauleni-sq9pu 5 หลายเดือนก่อน

    The DC more fire sonayi ndi manyaka

  • @peterkuliyanimbewe
    @peterkuliyanimbewe 5 หลายเดือนก่อน

    Moto kuti buuuuuuuuu kalondo yemweyooo

  • @johncassimu5433
    @johncassimu5433 5 หลายเดือนก่อน +1

    Ine chakwela ai ndi mbudz

  • @user-ny3it3jp9l
    @user-ny3it3jp9l 4 หลายเดือนก่อน

    Hy

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 5 หลายเดือนก่อน +1

    Chakwera kukamwa kobwafikako

  • @tiunzanenganimunomwaafrican
    @tiunzanenganimunomwaafrican 5 หลายเดือนก่อน

    🎉 Ndiye wina aliyese😂akulira naye❤ chakwela olo kufusa mwana amangotu kwana kuti ansavele virus ya chakwela ayenda ndi kurangura zonsa kwana Oro kakebe ka feteresa.🎉😂❤

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x 5 หลายเดือนก่อน +1

      😂😂😂😂😂Ndipo aliyense anadi akudana naye Akumamutukwana coz chaufiti wake

  • @ronexmcdonald8742
    @ronexmcdonald8742 5 หลายเดือนก่อน

    The DC

  • @user-gh1yc3mu5r
    @user-gh1yc3mu5r 5 หลายเดือนก่อน

    Umakwanira the DC

  • @lawrencetenthani5547
    @lawrencetenthani5547 5 หลายเดือนก่อน

    Or iweyo Kalindo ndichani unapangako uli MP kwanuko. Leave Chakwera alone tidamuvotera tokha

  • @user-qd2uy9fp9v
    @user-qd2uy9fp9v 5 หลายเดือนก่อน

    Bwana kuyakhula kumeneko kwa nzeru awawa akufunika ku pita koko atulukeko si ana ife

  • @BrightNkhoma-xz4bg
    @BrightNkhoma-xz4bg วันที่ผ่านมา

    Kod .mesa anat akalephera 2 years azatula pas udindo?? Tinenekut akukwanisa kusatula pasi udindowu?

  • @kennethkaunda3636
    @kennethkaunda3636 4 หลายเดือนก่อน

    Mumaona Ngati achimwene aakulu ndi wazisuzo munya muona

  • @user-jk8sh7fh2d
    @user-jk8sh7fh2d 5 หลายเดือนก่อน

    Kwa ine zomalandila ndalama za ulerezi si zabwino kwen kwen, chifukwa zimapwetekesa anthu ozilimbikila pa okha chifukwa ndi pamene misonkho imakwela kwambili ovutika amakhala ozilimbikila uja olandila za ulere sadandaula coz nzaulele. Program imenei ndingakhale osangalara itakhala only okalamba bsi not aliese and big problems amalembana pa chibale anthu ake ndi omweomweo choncho nzosakoma.

  • @storytambala6088
    @storytambala6088 5 หลายเดือนก่อน

    Chakwera usanamize anthu kuti, ungamange njanji yoti sitima iziyendera magetsi. Pakalipano, ikulira boma la south africa anthu atadula mawaya onse a copper mu njanji ikutha 3yrs pakali pano madera ena kulibe sitima zonyamula wanthu. Ndiye ukawanamize anthu lero, tamawopa Chakwera kumwambaku kuli mulungu udziwe kuti, unayamba bwino koma tsopano utha udyo.

  • @georgemponda
    @georgemponda 5 หลายเดือนก่อน +1

    Speech yagalu uyu(chakwera) its copy and paste speech ya president wa South Africa 🇿🇦 😂😂😂😂

  • @jonathanmbewe4246
    @jonathanmbewe4246 5 หลายเดือนก่อน

    Nyengo yakutswakutswa

  • @AlickNdeketeya
    @AlickNdeketeya 5 หลายเดือนก่อน

    Chakwera ndi batile linja lizigona Pa charge basi

  • @davietembo7935
    @davietembo7935 5 หลายเดือนก่อน

    Don't talk about Kalindo for everyone here in Malawi is able to see .Ifetu ndi anthu akuluakulu tikuona zonse bwana though mukusapota manyaka

  • @josephMandala-hk4xs
    @josephMandala-hk4xs 5 หลายเดือนก่อน

    Kodi a Boni K Alindo ndiotani ?Is he a Malawian or Mozambican

  • @IdritsaHanudan-dg3gi
    @IdritsaHanudan-dg3gi 4 หลายเดือนก่อน

    Ndpo chaakwela sukunya sunny wako

  • @user-qw4pk7wj8i
    @user-qw4pk7wj8i 5 หลายเดือนก่อน

    Kod uyu chidzungu chake chakut bible courage yomweyi kkkkkk Kom chisoni kobs

    • @user-qv4ko6ps4j
      @user-qv4ko6ps4j 5 หลายเดือนก่อน

      Satanic, imamusintha munthu mu zambiri ndipo English yi ndi silang ya pansi pa nyanja

  • @evansevas119
    @evansevas119 5 หลายเดือนก่อน

    Kalindo asakupusitseni amalawi choti mudziwe palibe chingasinthe mavuto wabe adzapita patsogolo chimene akufuna born kalindo ndichakuti boma limene likubwelalo lizamuganizile udindo winauliwonse akadzatelo simudzamuwonaso wapita basi mavutowabe adzati tsalila yinu ndiyene

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o 5 หลายเดือนก่อน

    A kalindo even u mp unakulephelani anakuchosan mukanakhala kut anthu akwanu mumawathandiza bwenzi sanaku choseni pa u mp leave our president alone ,jealous lakuvutan mumafuna unduna

  • @fridaymtembo1304
    @fridaymtembo1304 5 หลายเดือนก่อน

    Akafuse nyamilandu akati azamanga 5star hotel mu nthawi yowonjezela zimene akayesa kuti Malawi wa lero ndi wa zana anthu ndiwokwiya ndi anthu opusa onga wawa

  • @user-ce6hy6tp7e
    @user-ce6hy6tp7e 5 หลายเดือนก่อน

    Kod inu amalawi muli pati paliposo mukangonyoza zili zonse mwatan kod nanuso mitu yanu sikugwira ntchito pitani uko ndi chakwera wanuyo machende ake, bon kalindo ndi katundu payekha ife tili ndi abon kalindo

    • @user-qv4ko6ps4j
      @user-qv4ko6ps4j 5 หลายเดือนก่อน

      Dikila ndi wa tukwaneno zenizeni, mboli zanu,machende anu,nyini zanu, mikongo yanu ,kuda ngati kuseli kwa tchende nonse otsutsana ndi bon kalindo ,chakwela galu wa munthu, nankhumwa mwana wa mbuzi okakamila kuyamwa galu chakwela koma munya campaign ikayamba mpamene muone mkwiyo wa a Malawi,,,,,machende anu nonse ! Chakwela kukamwa ngati mpheto, mkazi wako kukamwa ngat kumtumbo agalu inu mwatizunza kwakwana manyi anu

  • @user-pe7lo1fe9b
    @user-pe7lo1fe9b 5 หลายเดือนก่อน +1

    Tikufera chizungu

  • @user-vl5on2lj8b
    @user-vl5on2lj8b 5 หลายเดือนก่อน

    Chakwera inachuluka ndi jerasi nkhwidzi kupangira APM koma kunena zoona walephera kusogolera wanthu

  • @charlurquhart5788
    @charlurquhart5788 5 หลายเดือนก่อน

    Cionse akulandila machende ache galu amenei achoke bs

  • @user-mk4lo7bd6f
    @user-mk4lo7bd6f 5 หลายเดือนก่อน

    Iwe ukusowa zolakhula kagone nichamba cakocho

  • @georgednthala-wh3pf
    @georgednthala-wh3pf 5 หลายเดือนก่อน

    Kuyanba kuwapatsa150k simwano, bcoz amadikila apange budget through parliament bcoz thy needed a gud amount of money. Iwe ili ndi nsanje whatever speech angayankhule u criticize it bcoz u want to deal with the president posakupatsa udindo m'boma

  • @user-fs1ox7ou1b
    @user-fs1ox7ou1b 3 หลายเดือนก่อน

    Chisilu ichi

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 5 หลายเดือนก่อน

    Chimangoziwa kuyankhura chisiru chi boza basi mbuzi ya munthu. Nthawi yako yatha basi.

  • @MathewsKamphambe
    @MathewsKamphambe 5 หลายเดือนก่อน

    Komatu amene akudyelela misokho yathu ni azathu akumwela koma izi anena ABorn Kalinndo nizosaveka kodi anapeleka Fredy ndi a boma ? anthu amafa ninjala ninali boma liti ?inu mukulimbana mokho ku DPP kwanuko .ukuwuzani kuti mukakhale kwina mukana kuzolowela kundila zawulele

  • @user-nc4vi1jt5g
    @user-nc4vi1jt5g 5 หลายเดือนก่อน

    Abonikalindo akachoka achakwera chakachamawa amene abwereyo simudzayimililanso nkuyamba kutukwana ndikungokuonani mulungu akadzatisunga tidzakusekani

    • @user-qv4ko6ps4j
      @user-qv4ko6ps4j 5 หลายเดือนก่อน

      Iwe ndi chitsilu eti! Bon satukwana koma kutsuka bodza la boma

    • @user-nc4vi1jt5g
      @user-nc4vi1jt5g 5 หลายเดือนก่อน

      @@user-qv4ko6ps4j tachenjera ndiweo mudamuchotsa apm lelo mukulankhula zachakwera mukusonyeza kuchenjera kodi kumuitana munthu kuti mbuzi sikutukana?

    • @user-qv4ko6ps4j
      @user-qv4ko6ps4j 5 หลายเดือนก่อน

      @@user-nc4vi1jt5g chokaaaaaa iweso mbuzi

  • @ChristopherKabanga
    @ChristopherKabanga 5 หลายเดือนก่อน

    timayembekeza kut tikumva kuti akalindo athandiza anthu 50 pakuwagawila chimanga aaa zokamba ulibe mbava yamunthu

  • @user-kr1kg5hy9l
    @user-kr1kg5hy9l 5 หลายเดือนก่อน

    Zokotani mfumu.

  • @nellikkmwenda7087
    @nellikkmwenda7087 5 หลายเดือนก่อน

    Achakwela ndi aboza

  • @PSTPerivoli-xd1ot
    @PSTPerivoli-xd1ot 5 หลายเดือนก่อน +1

    kodi umangosusa zilizose basi? ziyamikilani zinazi akulu ifet tikuonako ubwino winawake

  • @lawrencetenthani5547
    @lawrencetenthani5547 5 หลายเดือนก่อน

    Kusokoneza Parliament ukalowera kuti ndipo khomo lake litilo.

  • @user-xs3pk1vp8i
    @user-xs3pk1vp8i 5 หลายเดือนก่อน

    Kalindo ngwakufuntha akufuna ndalama wakavuka uyu zaziii

  • @user-xs3pk1vp8i
    @user-xs3pk1vp8i 5 หลายเดือนก่อน

    Kalindo chilichonse kutsutsa mmmm asatipusitse mutu wake sulibwino akuluwa

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o 5 หลายเดือนก่อน

    Kalindo has nothing and doesn't know anything chitsiru Cha chabechabe

  • @user-rk3uo5fs6g
    @user-rk3uo5fs6g 5 หลายเดือนก่อน

    Am failing to get your argument. U trash the SONA and same u recommend the SONA to the extent kuyitchula yokongola and mwayichekenera kuti can induce maiko akunja kuti apange support. Nkhani ikukambidwayi Ndi commenting on SONA is totally different. I expected you analyzing the SONA and isolate issues of great important and bring alternatives that can help to shape the situations. Waste of precious time

  • @johnchicoti
    @johnchicoti 5 หลายเดือนก่อน

    Bon kalindo adazowela kubwebweta kungomuzolowela basi alibe ninzelu zomwe ngati iweyo Ali plasntent wawanthu osawuka bwanji suwathandiza anthu osawukawotu

  • @ziyamporoma377
    @ziyamporoma377 5 หลายเดือนก่อน

    IMF, world bank, European union komanso the whole donor community is fully behind the president's economic policy...
    Anthu amenewa sapanganawo zandale so give credit where its due.
    Iweyo Kalindo what do u know about economy?
    Your audios are just a source of entertainment basi osati muzinamapo apa 😅😅😅

  • @user-og3dp9di7e
    @user-og3dp9di7e 5 หลายเดือนก่อน

    Kalindo mmmmm kumangotsutsa zilizose, ulire ndiweyo ,chifukwa chakwera akuwinaso,

  • @robertharawa9203
    @robertharawa9203 5 หลายเดือนก่อน

    The most useless guy in Malawi is Bon Kalindo after realising whatever problems the Malawi are facing what have you done to the people of you area to areaviate some of these problems do you really see what your friends like Bushiri are doing to help the poeple of this country but they have never been here to talk the nosense you talking about here

  • @user-cw8ue6qp8w
    @user-cw8ue6qp8w 5 หลายเดือนก่อน

    Kod inuyo a born kalindo ndiy tivotele ndan koz mukutisokonedza ndiy mwina muine inuyo

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r 5 หลายเดือนก่อน

    Akalindo ndiwopusa komaso chamba chamvuta

  • @PSTPerivoli-xd1ot
    @PSTPerivoli-xd1ot 5 หลายเดือนก่อน +2

    i think bon kalindo you just opposes for the sake of opposing!! see things with positive lens! akulu kususa kwanu nkopanda nzeru

  • @user-lc9bm6li6z
    @user-lc9bm6li6z 5 หลายเดือนก่อน

    Ndiwopusa kwambiri uyu

  • @peterkuliyanimbewe
    @peterkuliyanimbewe 5 หลายเดือนก่อน

    Moto kuti buuuuuuuuu kalondo yemweyooo

  • @AhmadumkomaTambala-lr9gp
    @AhmadumkomaTambala-lr9gp 5 หลายเดือนก่อน

    Nasongoleyi ayende byake biiiiii