A Chakwera Ndi A Mutharika Onse Ndi Olephela - Samuel Lwara

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 21 ส.ค. 2024
  • On Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara says neither His Excellency Dr Lazarus McCarthy Chakwera nor former president Prof Peter Mutharika are fit to rule this country. They are both failures.
    Pa Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara wati Olemekezeka Dr Lazarus McCarthy Chakwera kapena pulezidenti wakale Prof Peter Mutharika sayenera kulamulira dziko lino. Onsewo ndi olephera.
    #Malawi

ความคิดเห็น • 208

  • @hamiltonsolomon3756
    @hamiltonsolomon3756 หลายเดือนก่อน +5

    Samuel you are right ✅ 👌....Chakwera ndi Muntharika...tiwaona zintchito zawo....Onsewa olephwera we.Need New Blood....Mkulu uyu akalankhula chilangamo....zoona zokhazokha......More Fire 🔥 Samuel...👍👍👍👏👏👏👏👏👏

  • @Mahmoodwargison-op2gm
    @Mahmoodwargison-op2gm หลายเดือนก่อน +10

    Vuto munthuu akalakhula ngamo mumamuda kma chilungamo chimawawa keep it up nr Rwala

  • @SarahMusama-eu7wt
    @SarahMusama-eu7wt หลายเดือนก่อน +9

    Ofcz munthalika failed somehow but these one eeeh aonjezaa

  • @OMEXTWAIBU
    @OMEXTWAIBU หลายเดือนก่อน +1

    I'm really agree with you Samuel , keep it up and don't fear. True true big.

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 หลายเดือนก่อน +1

    Chilungamo chosatenga mbalin keep up the good job, zitseguleni mitu mbuli zimene zimavotera atsogoleri olephera, 80% ya anthu ovota ndi mabulutu, akufuna Chakwera olephera kubweretsa Mutharika olepheranso.

  • @MasterMwandira-q8v
    @MasterMwandira-q8v หลายเดือนก่อน +3

    Ndizoonadi. APM, CHAKWELA, awa ndi anthu olephela, bwanji tiyeseko afford nawoso tione kulephela kwao

  • @BrightPhiri-bt6ev
    @BrightPhiri-bt6ev หลายเดือนก่อน +5

    Apa mwalankhulapo za nzelu lero.peter is not a solution to our problems tinamuyesa kale

  • @DIRECTORJARVMACK
    @DIRECTORJARVMACK หลายเดือนก่อน +1

    Ndizoona onse ndi olephela koma devaluation mmmmmmmm ndiyopweteka kwa achinyamata ogwila maganyu ife APM my vote

  • @anniedennis7127
    @anniedennis7127 หลายเดือนก่อน

    That's very true , only a patriotic Malawian cannot vote for failed leaders Chakwela and muthalika.

  • @FrancoKaunga-rq2ki
    @FrancoKaunga-rq2ki หลายเดือนก่อน +2

    Mr lwara you are number one! Apm and chakwera same what's up group both are fools. Malawi is a cursed country leader ship is worse.

  • @GiftPhiri-tt7nn
    @GiftPhiri-tt7nn หลายเดือนก่อน +6

    Chipani cha dpp bingu anapanga chitukuko kwambiri and ndimachikonda koma president amayenera kukhala wina ku dpp ko , sankhani president wachinyamata ife tikamuvotela , dpp bola singafanane ndichakwera koma ma president tiyese atsopano

    • @VeronicaChirwa-ct4os
      @VeronicaChirwa-ct4os หลายเดือนก่อน

      Mwayankhula bwino kwambiri, anthu amadana ndi chilungamo

    • @haneefmuyaya7472
      @haneefmuyaya7472 หลายเดือนก่อน

      I prefer, Muthalika ataimanso ndi Atupele,
      Zikhiza kukhala bwino, akazatopa, mwana azapitirize,
      Koma zomatenga anthu isaziwika bwinozi,
      5yrs it's not a joke guys

  • @MenciaMadex
    @MenciaMadex หลายเดือนก่อน +1

    Apm my vote 2025

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy หลายเดือนก่อน +1

    Pa Peter pokhapo ndie wapenga Peter sungamufanizilire ndi chakwera APM akufunika than any one

  • @user-si7po9sd5i
    @user-si7po9sd5i หลายเดือนก่อน +2

    Unaonako dpp ikugula fertilizer ku butchery,kwatsala iweyo akumange mpamene utadziweno kuti pakati pa awiriwa Pali kusiyana.

  • @user-wi9pe2hz7e
    @user-wi9pe2hz7e หลายเดือนก่อน +1

    Apm amalize term yake munamulandila nsanje upresident l support Dpp 100%

  • @user-ee6be5kl5o
    @user-ee6be5kl5o หลายเดือนก่อน +1

    Lwala Mutu wako sakugwila waoneka kale omwe amasankha ndi anthu iweyo sungafanizile Mutharika ndi chakwera , Mutharika anthu amasangalala kwambili kuposa pano ndi chifukwa anakuthamangitsa mnyumba ya Malawi housing, iweyo ziyankukula zako zopusazo amalawi Peter Mutharika wooyee

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h หลายเดือนก่อน +2

    Ndinu achitsilu alwara sungafanizile MCP ndi DPP aaaaa anyamata alipo muboma akupanga chani

  • @user-si7po9sd5i
    @user-si7po9sd5i หลายเดือนก่อน +4

    Pena pake nanuso Mr Lwara mumaganiza moperewera kwambiri,inuyo mungafanizire Peter ndi chakwera? Like seriously?

    • @TheresaKuluwemba
      @TheresaKuluwemba หลายเดือนก่อน

      Kkkk mwina akufuna aime iyeyo kukhala president kkk

  • @Emmanuelmw603
    @Emmanuelmw603 หลายเดือนก่อน +3

    mutharika akuwinaso mufune musafune.....APM my vote ✊

  • @MosesTangwe
    @MosesTangwe หลายเดือนก่อน +1

    Naweso larwa izi ife ai. chifukwa a Peter mutharika sungafanizire chakwera never. Pali zambiri zomwe simungafananitse

  • @YNOTGEORGE8
    @YNOTGEORGE8 หลายเดือนก่อน +3

    Yes Mr Lwarwa thus fact APM thus not a solution

  • @user-ti2ct8ts8d
    @user-ti2ct8ts8d หลายเดือนก่อน +3

    Iwe mutharika ungafanize mbudzi ngati chakwela? Iwenso ndi kape kwambiri

  • @isaaczuze
    @isaaczuze หลายเดือนก่อน +5

    Kodi a lwara muli mbali iti
    President wanu pano ndi mdani
    ....jnutu mwasowa kolowera ..
    .mmene chakwera waonongela zikoli mungayerekeze ndi apm....inuyo mukukhala ngati mbuli bwanji
    Mmene peter amasiya upresident katundu anali pati.....iweyo lwara wangosowa kolowera .....osachita support Enock chihana bwanji monga wakwanu.....usiletu kuyankhula za peter......amalawi chiyembekezo chimene tasala nawo ndi peter

  • @spargomw
    @spargomw หลายเดือนก่อน +1

    Akulu ngat Mfundo zakutheran ndibwino kukhala osayankhula kalikonse, inuyo pangan Alliance nd Lyton Mangochi muyambitse chipani chanu coz apapa mwaonetsaso uchitsiru ofanana nd Lyton Mangochi.

  • @user-st6bt5vv9c
    @user-st6bt5vv9c หลายเดือนก่อน +1

    Lawala is looking for chihana but AFORD alone can't win how old was mandera both are candidates let them exercise their freedom

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w หลายเดือนก่อน +1

    Bola APM kusiyana ndi chakwera, nthawi ya APM zinthu zinaliko bwino kusiyana ndi chakwera.

  • @QueneteCatundulo
    @QueneteCatundulo หลายเดือนก่อน +3

    Asowa choyankhula awa

  • @TypexTikita
    @TypexTikita หลายเดือนก่อน +1

    Lwara zopela zomwe walankhula za APM chifukwa munthu wanzeru sangayerekeze mavuto tilinawowa ndi APM

  • @AlfredSteven-v9m
    @AlfredSteven-v9m หลายเดือนก่อน

    Yes ur right koma mukananena oyenera muzipanimo

  • @OweniMalokooweni-es9qx
    @OweniMalokooweni-es9qx หลายเดือนก่อน +3

    Ndipo kwambii timufuna atupele mulunzi😊

  • @JumaKachala
    @JumaKachala หลายเดือนก่อน +1

    Koma.lero ndee mwayankhula zopepelatu
    Peter angafanane ndi chakwera

  • @PeterPhiri-di1ux
    @PeterPhiri-di1ux หลายเดือนก่อน +2

    ndimakupanga follow koma lero wangomunyoza muthalika panya pako ndipo ndakutuluka

    • @lucianogeoffrey4275
      @lucianogeoffrey4275 หลายเดือนก่อน

      Atumidwa awa, akuona ngat titha kusankha iwowa

  • @user-fm8ed7eo3i
    @user-fm8ed7eo3i หลายเดือนก่อน +1

    Inu ndiye mu kuwona owina ndi ndani, plz musapange zoti wina mungomuioitsa mbiri koma mudzilankhula kuti zinthu zisinthe. Pano tikufuna kuti tisinthe dziko ndiye osinthayo ndi APM zisiyeni zikhale chonho

  • @samsonhavenoyayshonga2609
    @samsonhavenoyayshonga2609 หลายเดือนก่อน +1

    Koma pa ma President onse mu Malawi yemwe aliko bwino kuposa onse ndi Mutalika.

    • @RitaDickson-ls7ol
      @RitaDickson-ls7ol หลายเดือนก่อน

      Palibe zabola apa change position peter and chakwela out 2025

  • @user-nd9cm3yl7e
    @user-nd9cm3yl7e หลายเดือนก่อน +1

    Muthalika satukwana muthu olomodzi ndiwante ndele zd

  • @user-iu6mr5xu6r
    @user-iu6mr5xu6r หลายเดือนก่อน +1

    Kodi bambo Lwara, amene afuna nzake pakati pa Peter ndi Saulosi ndani? Khalani ndi cipani canuco. Kuposa kunena zopusa ngati cidakwa. Kodi wanzeru? Nanga ulikuti ndipo ukutani?

  • @RitaDickson-ls7ol
    @RitaDickson-ls7ol หลายเดือนก่อน +1

    That is true Peter ngati anachoka pampando analephela tiwoneko zna asatinamize agogo l love your point keep it up mr🙏🙏🙏

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma หลายเดือนก่อน +1

    Ulibe mfundo nzimayi pachinyero chako dppp ikulowabe m,boma panyero pako

  • @VuyolwethuMbabani
    @VuyolwethuMbabani หลายเดือนก่อน +1

    Iwe uzilimbana ndi chakwela otsati Peter ngati wapasidwa ndalama ukazibwedze uyaluka komanso uchita manyanzi 2025

  • @marcuswalker2613
    @marcuswalker2613 หลายเดือนก่อน

    Mbuli iwe Mtumbuka opanda mfundo atakulanda nyumba ndiye wowowoooo. Ndale zako zilibe tsogolo "mark my word"

  • @GRACIOUSKENAN
    @GRACIOUSKENAN หลายเดือนก่อน +8

    Ndiyambe chochi,Neleson mandela uja sanalamulire dziko ali otha msinkhu??
    chikhala kuti peter anthu akumuda bwezi kumaliro kuja anthu akumulira kut ayimile??
    so iwe ukamat peter ayi what do you mean so tayimilatu iweo tione ndi mkamwa modambanamo aaarrriii.
    iwe do you compare chakwela nd peter,chambaaa chani,ngat sukufuna khala usavote uzidya soya peices bass kumpotoko ndi atumbuka azakowo bwanji? pita ukooooo

    • @Littlefair7
      @Littlefair7 หลายเดือนก่อน

      Akunena zoona, koma mbuli ngati inuyo simungaone.

    • @user-es4jt6ds8m
      @user-es4jt6ds8m หลายเดือนก่อน

      Ayi osanena Kuti stumbuka pliz zichepezo tseka Chikamwa icho

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili หลายเดือนก่อน +9

    Lwala wayamba kukhumudwitsa wanthu chakwera ungafanizire ndi Apm?

  • @user-si7po9sd5i
    @user-si7po9sd5i หลายเดือนก่อน +5

    Mr. Lwara is a chaotic person, he wants people to applaud whatever he says, Mr. Lwara learn to be quiet sometimes, you are missing the point

    • @MacphersonJuma
      @MacphersonJuma หลายเดือนก่อน

      opepela uyu mbuzi ya munthu

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 หลายเดือนก่อน +1

    Peter mutalika ndi simungayerekeze ndi Chakwera. Vuto amalawi timaziwa kuyankhula koma mopanda zeru. Mcp udf ppp dpp mukhale pasi muone kuti kodi ndichipani chiti chimwe chapangapo zabwino muona kuti dpp inayesesa. Chinthu chimozi poti mutalika wakalamba koma still ali ndi zeru . Chilima sanawinise dpp. Dpp nditimene anayitana chilima. Chilima anawinisa mcp ndiyime isamanyade .

  • @MaryChavula-jz3di
    @MaryChavula-jz3di หลายเดือนก่อน +1

    Lwara ndi wa ganyu sasamala za amalawi akungifuna kuti amupatse ndalama koma APM sangamupatse ndalama n'gooooo ozavotela APM ndife amalawi akumudzi amene tikudziwa ubwino wa APM tikufuna feteleza ontchipa ife

  • @user-iu6mr5xu6r
    @user-iu6mr5xu6r หลายเดือนก่อน +1

    Inu ndi munthu amene amanena zinthu zimene sadzidziwa. Munapha zipani 9 kukhala ndi kusunga MCP. Lero mulalata?

  • @MarriamBakalie
    @MarriamBakalie หลายเดือนก่อน +2

    Wayambatu ku khota tidana nawetu uziyankhula za chakwela nt APM wamva machende ako galu

    • @DeliaKaduya
      @DeliaKaduya หลายเดือนก่อน

      😂😂😂😂 yomweyo galu iweee

  • @MaryChavula-jz3di
    @MaryChavula-jz3di หลายเดือนก่อน +1

    Mulilanaye APM chomwe timadziwa APM sanaluzepo ndewu akamamenyana 1 to 1 kukanikana ndiye mubweletse 1 to 5 ndiye 5 a wine muziti m'modziyo walephela? Anthu adyela Inu tandiyankheni alwara komanso kamenyedye ka m'modzi uyo sikanasithe 40 pelesenti ndiyomweyo anapezanso pa 1 to 1 mulila ndi APM 2025 APM boma

  • @BertharrySecurity
    @BertharrySecurity หลายเดือนก่อน +1

    Mnthalika inde analephela Koma anayesesa, kusiyana ndiwomwe alipowa

  • @StevenDastan
    @StevenDastan หลายเดือนก่อน +1

    Apm ndimunthu wankulu kwambili kuliphika dziko lino

  • @user-dp7bc7yy6s
    @user-dp7bc7yy6s หลายเดือนก่อน +1

    Alwala mwayamwa tikutulukani mwayambaz,inu nthawi ya DPP mungayerekezere ndinthawi inu.
    Inu nthawi ya DPP anthu amamangidwa chonchi or kukwera kwazinthu zinafika apa?
    Njara,kusowa kwamankhwala mzipatala,kukwera kwa zinthu mungayelekeze ndinthawi ya DPP

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili หลายเดือนก่อน +4

    Apm my vote

  • @jonas-xh4hz
    @jonas-xh4hz หลายเดือนก่อน +1

    a rwara zikambani zanzeru musiye kuyankhula zopusa zanuzo

  • @user-ln3zx6wo4w
    @user-ln3zx6wo4w หลายเดือนก่อน +1

    As itikut peter alibwino koma tikut apm alikobwino kusiyana ndi chakwera basi

  • @user-xd1cm7tm7t
    @user-xd1cm7tm7t หลายเดือนก่อน +2

    2020 mumanenaso Chocho kut alowe anyamata lelo bwanji

  • @EllahChikwatu
    @EllahChikwatu หลายเดือนก่อน +1

    Iweyo suzakalamba omwe anakubala nd sikana wina nyamata sibwino kwanu kulibe agogo

  • @OsmanPatrick
    @OsmanPatrick หลายเดือนก่อน +1

    Machende ako iwe abambo akowo

  • @ibrahimbamusi109
    @ibrahimbamusi109 หลายเดือนก่อน +1

    Lwara tikutulukatu ali ndi chibwana

  • @DesmondKanguwe
    @DesmondKanguwe หลายเดือนก่อน

    Reality yowawa...odana ndzomwe ukunenazi sadziwa zomwe akufuna

  • @user-or7ng3fj8f
    @user-or7ng3fj8f หลายเดือนก่อน +3

    Ndiwe kapolo wamundu Peter again in 2025 🔥

  • @user-zx3pz2wy1j
    @user-zx3pz2wy1j หลายเดือนก่อน +1

    Kodi osalephela ndi ndani ngati ukutiso peter ndiwolephela iweyo wachitapo chiyani ?

  • @SofiyanoMayuni
    @SofiyanoMayuni หลายเดือนก่อน +1

    Peter ndiwabwino

  • @retirementtoafrica
    @retirementtoafrica หลายเดือนก่อน +1

    Nkhani yodya mabanzi ndiyovuta, chilungamo chimasowa ndikumagoyankhula mozungulira opanda solution.

  • @HendresonLubano
    @HendresonLubano หลายเดือนก่อน +1

    Kuyambila pano usazanyozeso muthalika ndimunthu watendele

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma หลายเดือนก่อน +1

    Galu nzimayiiwe athu anzeru avotera dppp pitamuthalika amayesetsa kuti athu tizidya chakwera anabwera kudzaba njara yavuta km muthalika zakudya zimatsika ntengo

  • @KennyPhiri-zg1kr
    @KennyPhiri-zg1kr หลายเดือนก่อน

    Peter anayendesapo analephera chakwera walephera you are true pezani wina

  • @Samu-q3z
    @Samu-q3z หลายเดือนก่อน

    Apm ❤❤❤❤

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 หลายเดือนก่อน +2

    Ndiwe galu Kwa basi mbuzi DPP fertilize wunaliko mapassport analiko makhwara amapezeka muzipatara ndiye zingananane Ndi MCP kagwere wuko

  • @user-lw4hw9ce4w
    @user-lw4hw9ce4w หลายเดือนก่อน

    Chi luwara ndichimbuzi APM will win you can't compare with chakwera suka ng'undu

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d หลายเดือนก่อน +1

    Abambo inuyo timakukondani panopa tisiya kuvela ma odio anu inu satana ameneu chakwela mungamufanize ndi peter muthalika muthu salephela kukhala ndi zofooka koma peter muthalika anali muthu oyesesa ndipo akatengaso boma adzalamulila bwino kwambili chifukwa wadziwa zomwe amalawawi amafuna Moyo wautali adad ❤❤

  • @user-nd9cm3yl7e
    @user-nd9cm3yl7e หลายเดือนก่อน +1

    Wanamaiwe sudziwa ndale

  • @kondwanbanda2671
    @kondwanbanda2671 หลายเดือนก่อน +1

    Alekeni anthu akasakhe okha

  • @lucianogeoffrey4275
    @lucianogeoffrey4275 หลายเดือนก่อน

    Mwayambatu uchitsiru madala. Muthalika ndi Chakwera you cant put then together. Ya Chilima ija timakupangani support koma mwayamazi ayi

  • @frezarphiri3480
    @frezarphiri3480 หลายเดือนก่อน

    Iwe luwala iwe APM siwungamufanizile ndi chakwela ayi iwe watanikodi

  • @Mahamudu-q6b
    @Mahamudu-q6b หลายเดือนก่อน

    ❤❤ zowona

  • @paulmanyamba5437
    @paulmanyamba5437 หลายเดือนก่อน +1

    Ndichifukwa achichotsa ntchito ndiwamisala wakutumayo akupusitsa koopsa 😂😂😂

  • @user-hd7wq2yc6m
    @user-hd7wq2yc6m หลายเดือนก่อน

    A Lwara ndinu odwala mumutu nzeru mulibe ukuganiza kuti anthu angasithe maganizo awo pazimene ukuyankhulazo Inu a Lwara mukufina kisokoneza anthu Malawi muno iwe nzeru ulibe ndiposo anthu asakumvere iyayi foseki mahala ulije ulichindere chomene palije zakusintha Peter wayomenge ndiposo wazamuwina u activist wa iwe Lwara ngwauzereza mwawanthu ngati iwe Lwara ndimweikunanga Charu Chaalawi foseki ulichindere so iwe unamahala Lwara? Vyakuyowoyeka vyako vikuchita kuwonekerathu kuti ndiwe miulwali mumutu zimene ukuyankhula ndizonyoza sopano ndalere zonyozana monga mumene ukunyozera iweyo, anthu sangakimvere aMalawi simuwaziwa iweyo anasukusula ,ulichindere chomene ndicho chifukwa ukunyoza mafumu ghakuno kwithu ku Mzimba ngati nawe uli mongonl .ikuchimanya chiyowoyero na chikhalidwe chachingoni iwe foseki zako uwaleke wazakayime wene Peter Mtharika uzamuvota ndiwe chlmunthu chasanje ichi wati iwe ungalingananayo zeru Peter? Ulichindere

  • @samsonhavenoyayshonga2609
    @samsonhavenoyayshonga2609 หลายเดือนก่อน

    P M munthu odziwa kulamulila munthu wanzeru akuziwa ,Larwa udakiwe

  • @VuyolwethuMbabani
    @VuyolwethuMbabani หลายเดือนก่อน

    Udani wako ndi a Peter usasokonedze nao anthu omukonda Peter Ife Peter ndi chiyembekezo chathu usiye kuyankhula manyi

  • @MaxwellSakwata-wb8ep
    @MaxwellSakwata-wb8ep หลายเดือนก่อน +2

    We never voted out APM may be you did.....

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 หลายเดือนก่อน

    Iwe ndi mbuzi leave Apm alone you can't compare ndi chakwera kupusa....

  • @VincentNgabuhvincent
    @VincentNgabuhvincent หลายเดือนก่อน

    Ada awawo Samuel Lwara mumuuze ma chende ake palibe chomwe wakamba chamzeru wamva ukalimbana ndi DPP poliyako wamva iwe ndy ndindani.
    kd nanunso Amalawi munthu kungoti wangobwera ndi ka audio kake bs mungoti that's true km akukamba zopanda munthu Amalawi mulibe mzeru kwa amene mungoyamikira zopanda pake zausichilu bs.
    MCP ukafanizire ndi DPP mutu wako ukugwira iweyo kd nthawi imene APM anali pa mpando kd ena inu timakuziwani kd chifkwa nthawi zina APM munangokhala chete chifkwa zinthu zikayenda bwino ngakhale zimavuta km sangafike pa mbudzi iyi chakwera .
    Samuel lwara machende ako mpaka uzafe ndiza DPP kuipa kwake ok.

  • @EmmanuelMaxon
    @EmmanuelMaxon หลายเดือนก่อน +1

    Iwe aliyese akavota yekha usati nyase usamat amalawi sakufuna dpp uziti iweyo sukufuna koma ine ndikufuna zako zimenezo mesa chilima anadziwa ndale chifukwa cha apm

    • @michaelkallyz2425
      @michaelkallyz2425 หลายเดือนก่อน

      Auzeni koma awa. Khala ngati ntawi yaPita analikuLwanda

  • @user-qg4it7my9n
    @user-qg4it7my9n หลายเดือนก่อน

    Akulu fodya tamazimisiraniko a peter simungafanizire ndi mbuzi ya mu2 ngat chakwera

  • @EllahChikwatu
    @EllahChikwatu หลายเดือนก่อน

    Iweyo olo ungafanane nd APM ,,,,, ku pepera bas cisiru lwara

  • @MastonWatson-g7g
    @MastonWatson-g7g หลายเดือนก่อน +4

    Iwenso mmutu mwako nzeru mulibe nzeru chakwera ungamufanizile ndi mutharika? kape iwe wosowa chonena.

  • @chifundocharles2348
    @chifundocharles2348 หลายเดือนก่อน +1

    Nyamata wa chilima wasowa kolowera kkkkk

  • @SheenahMwalabu-iz3pr
    @SheenahMwalabu-iz3pr หลายเดือนก่อน +1

    Ndipo a samuel lwara mumandiwaza nsaname kkk everytime ndikamamvera ma audio anu ndimamva sugar 😂 ndimafuna ndikumvelani daily cz mumabudula mpunga wanyama, kamba simugawa. Izizi akunena apazi akutsutsa amadya thewera lamwana 😅😅😅

    • @user-qp8kh2hj9o
      @user-qp8kh2hj9o หลายเดือนก่อน +1

      Zoona ine munthu uyu ndimafuna kumamumvera daily fact ndiyomwe akunenayi😂😂😂😂

  • @HarrisonMwanga-xy4sc
    @HarrisonMwanga-xy4sc หลายเดือนก่อน

    100% light show ndi olephela.tiyetsele,utm UDF or afford.amagona,ali pa mpando.ziko,amayemdetsa,ndi chisale.ndi,amayi akunyumba kwao.just, remember akazi awo,amachita kupita ku reserve bank kumangotenga, ndalama kumeneko,atiudza za change for what corrupt our nation? that's sheet 'we can no sitting here watching this happen.amalawi,kodi,timadziwa akamati democracy?tili kutali,ndi chitukuko mu ziko lathu.

  • @ExcitedBreakingWaves-oh3zb
    @ExcitedBreakingWaves-oh3zb หลายเดือนก่อน

    Auzeni zoona bwana

  • @Spaw-BTheGogoBoy
    @Spaw-BTheGogoBoy หลายเดือนก่อน

    Lwala nde tivotere ndanino kulephera kulitu ma stage stage enawo nde ndi zero

  • @user-jj3oo6jh1l
    @user-jj3oo6jh1l หลายเดือนก่อน

    Mr samuel.pachimanga choola timasankhako.kt ichi ngankhale chili choola km.ndinkhonza kukazinga nde anthu tikuona kt bola peter

  • @user-xe9hp2tc4t
    @user-xe9hp2tc4t หลายเดือนก่อน

    IWE NDIWE GALU ASEEE NDIPO PAMSANA PAMBWIYAKOO UKHAULA IKAWINA KAPEE IWEE

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of หลายเดือนก่อน

    Apeter ndiye ndiokanika bola namkhumwa osati peter aaaa ngati zili chotcho basi alipowa angopitiliza

  • @AlfredSteven-v9m
    @AlfredSteven-v9m หลายเดือนก่อน

    Mwangolongolora 18 min osanenapo oyenera anthu tigwire ziti ndiye

  • @JamesMalango
    @JamesMalango หลายเดือนก่อน +1

    Akulu awanso,,,,

  • @isaaczuze
    @isaaczuze หลายเดือนก่อน

    Lwara ndichisilu alibe mfundo zomveka bwino kaya akufuna chiyani kaya
    ..amati ndiwa mcp....chisilu cha munthu

  • @user-fq4kv8dj4t
    @user-fq4kv8dj4t หลายเดือนก่อน

    Koma peter ungamufanize ndi lazalo ukunama zikatere nde kt basi kulibe wabwino

  • @blessingmanda
    @blessingmanda หลายเดือนก่อน

    change the system, anyone who has been who is who will be the president of malawi nothing has change and will change eccept if the system is changed. scrap the constition book

  • @OMEXTWAIBU
    @OMEXTWAIBU หลายเดือนก่อน

    APM wakalamba akapume, akakhala akungozikodzela ndiye angalamule ndani? Kwake kunatha petulo tiwone zina, munthu osadziwa kulankhula kkkkkk akagwele ndi family party yakeyo, Tiyeni amalawi tiyese Atupele ❤