Komabe ndikukhulupilira kuti mwini wake sakadakhalanso ndi maganizo obwelelanso ku chipani cha dpp. Kuli aford udf konso ndi zipani zina. Think twice .f,
Mhuuu aaa ine nkhani ya a Chilima omandivetsa chisoni mukayankhura kungotchurapo a Chilima sindipilira Loma kututsa misozi naso manga basi ndipo ndimati adaferanjiii? Mzimu wawo uziusa mu ntendere mpaka kumuvula kohala maliseche mhuuuu Malawi mchiyani?
Mmmm a Malawi chonde tengani Maiwa ngati mtsogoleli wa dziko la Malawi, ali ndi mphatso yaikulu Kambili. Kuchokela ku Zambia 🇿🇲
Zakhala bwino kutuluka mumgwirizano, congrants utm and dpp my votes
Hh😊i
A UTM mwachita bwino kutuluka alliance yanu mmmm inali yakupha
Ng'ona zizidyana zokhazokha tsopana😂😂😂😂😂😂 Ngat ali Chauta yemwe wakuuzan kut mutuluke, tingoti Alemekezeke Yehova coz ku Tonse mukadatha Psitiiiiiiiii. Atsaleko Manga yekha ku Tonse'ko😂😂😂😂😂
Mwafita bwino ❤❤❤❤❤❤❤❤❤
😂😂😂😅 wakwanika bale
Apa nde aonetsa kuti ndie mafanadi oganiza BHO😅😅😅😅😅
💥
Mwachita zimene mwini wake wa chipani SKC akadachita akanakhala kuti alipobe Ambuye akudalitseni utm senior leaders
Congratulations faz for SKC
mwachedwa nazo zinthu anthu inu. munawonerera muvi kuti ukuloweni m'maso ndipo lero ndizi chipani ichi sogolo kweni kweni silikuoneka
I'm just saying all the best mwachita bwino ndithu akhaleko okha akanganyawo
Job well done 😅😅😅😂😂😂😂atsaleko adzidyana okha okha yomweyo mr Chikangawa 😅😅😅😂😂😂
Dpp my vote😂😂
Zikomo UTM pothetha mgwilidzano umeneo ndi anthu akuphawa
Perfect breaking news 🎉🎉 i love it keep up ❤ utm
Mai kaliyati mwachita bwino kutuluka allance ndizomwe ndimadilira zikomo ndamva bwino kuchoka Kwa mavaphire sianthu away taonani mmene ikungwera kwacha sangakwanitse kuyendetsa boma
UTM for life ❤
Zosangalatsa kwambiri changa chikunkhala chisoni mmmmm imfa imandiwawa
❤nw i can able to go home n start support our country
Ken msonda azalowera kuti ngati MCP yaluza 2025?
Very good very good very
Nde ndiwe mtsogoleli nkumawopa kukumana ndi anthu omwe ukuwasogolera pali zabwino pamenepa ndiyankheniko
Mwapanga zanthengo wapatari kwambiri
OLO MUTATULUKA ZILI NKANTHU😂😂😂
MOTO WAMAPESI SULIMBA
UTM for life from Zambia 🇿🇲
Mwachedwa inu mukadapanga izi nthawi imene Chilima adakali ndi moyo anthu amkakuuzani kuti mutuluke Alliance koma kusamva inu bwelerani ku Dpp basi
Yomweyo apapa ndiye ziribwino
We're a little bit happy now 🙏
Kaliati ndinu a experience ku ndale musalore Manganya kukupusitsani.ndiwazitsutso
It's not too late it's a united movement ❤
I can feel the pain inside her speech 😢
That's a brilliant idea
SKC forever in our hearts ❤❤❤❤❤❤
Mama mwayankhura nthaks
Very wise Leaders of UTM and all members, Leave crodiles alone to eat themselves,RIP Baba Saulos Chilima
Lululuuuuuuuuiuuuuu mwachita bwino kwasiya atombolomboyo a MCP aziphana okha okha. Very soon freedom is coming tomorrow mwachita bwino kutuluka . Lero ndigona bwino iiiiii infa ya Dr Chilima aaaayosaiwalika😭😭😭😭
Zathapo 🤗
Mwachita bwino kutulukamo mutonse mai Patricia kaliat mwalankhula bwino kwambili🎉👏👏👏👏
Kaliati morefire mai inuyo MULUNGU adzikudalitsani ine utm my vote
Strong woman .
Courageous.
Fearless.
Few we have .
kkkk kuteloko apa paseweredwa game kungoti apange gwilizano ndi DPP UDF ndi a FOD
Zili bwino ndinthu utm oyeee🎉🎉🎉🎉
Manganya ndi wa MCP, he is not a genuine member of UTM, Hon. Kaliati I salute you!!
look sharp 🎉
Utm motto ku buuuu
Ngati ifa yakwamulungu alemekezeke ngati ndiabusa chakwela mulungu adzaziona ngati falawo safelapo
Zikomo kwambili ndipo yehovah satitaya ife ayi anamalirs🎉
UTM standing for us youths too
Tikavote guys❤
Good decision
Muphese ma lawyer pano 😂😂😂
That's nice 👍
I like it 👍
Good idea
Achita bwino ndithu potuluka chipani cha MCP or blood part
Komabe ndikukhulupilira kuti mwini wake sakadakhalanso ndi maganizo obwelelanso ku chipani cha dpp. Kuli aford udf konso ndi zipani zina. Think twice .f,
Zoona nkhani ikumveka bwino ndithu palibe chifukwa chibwelera ku DPP
Nice potuluka mugwirizano
Chipani chikufunika mtsogoleri ochangamuka ngati SKC, akweni mukukwanira pa udindo upresident.
Bwererani komwe mudachokera congrats UTM
Ai zikomo kwambiri mwachita bwino ndithu ambuye adzikutsogorerani ndithu
Mukatuluka 2023 bwezi chilima alipo Lero Koma Palibe yomwe amaziwazamawa only God knows
Amwene...chilima samamva
Mary wachita bwino kuzisiya, ndalama anakamudyera iya
Good development
Mulungu wayankha the DC 💪 alandile ulem
UTM Moto kuti🔥🔥🔥
Mcp ikhale yokha, all the best
SKC made me to join politics
Osada nkhawa ninthawi ikubwera 2025 kwakhala minyezi yocepa mai
VERY GOOD KUTURUKA KUMANDAKO MMMMMMMMM🙌🙌🙌🙌🙌😢 R.I.P SKC 😭 😭😭😭😭
Mbuzi izi bwanji simukhatuluka chilima alimoyo cause chilima amakhala akunena nde mumadikilira alowe Manda Kaye mwadya unsi
Apa ndiye mwachita bwino, asaleko amagazi okhaokhawo, Chipani choipa chosamva madandaulo awanthu, ntchito kumanga, kupha anthu osalakwa agalu a MCP
Mhuuu aaa ine nkhani ya a Chilima omandivetsa chisoni mukayankhura kungotchurapo a Chilima sindipilira Loma kututsa misozi naso manga basi ndipo ndimati adaferanjiii? Mzimu wawo uziusa mu ntendere mpaka kumuvula kohala maliseche mhuuuu Malawi mchiyani?
Osabwelelanso ku DPP please
Macheal utsi asapiteso Ku UTM please guys
Salute UTM osaopa osatopa osafooka
💔💔💔💔🤪🤪🤪🤪😭😭zosangala mwachita bho kwambili osaopa
Atsaleko ekha wazisudzoyo
Mwabwela inuyo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥💪🏾💪🏾💪🏾🇲🇼
Mwachita bwino manganya simunthu nsiyeni
Akuluakulu achipani basi omwewo? Tizipani tinati koma guys
😂😂😂😂😂😂 skc woyee 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥💯💪💪💪💪
Apa ndiye DPP 2025 wooo
Yebo chomene mwawanthu 😅❤MWN
Manganya ndiwa mcp,mayi Patricia kaliat congratulations for your speech
Mwachita bwino till limodzi
Ndpo zachita bwino kwambli osatopa osaopa osafooka
Tili momo UTM tikavotabe basi kya tikaluza kya tiwina tilimomo ife
Good decision.
Chipani cha utm chachinyata
No alliance nkhan yabwino mai kaliat anthu akupha achoke Malawi siwawo
Mbbambande UTM awawa asiyeni apange zawo
Bon kalindo uja wosadzamuphweketsa
Ndikatundu womanga ndi mawaya
Yes I wish chilima had done it in July 2022
Koma osabweleraso ku dpp
Ndipo maganizo abwino amenewo ndthu, ndiye chomwe akuyenera kupanga achipan cha UTM nchoti agwire ntchito nd a DPP ndipo zinthu zizayenda bwino even awo sazakhalaso nd mphavu
Great move
Good decision sitiopa kmaso kufooka 😳😳😳😳😳😳😳😳😳😳😳😳😳
Amai takulandilani inu mwabwela
Mwachita bwino mwatulukamo atsale ndi chikangawa waoyo
UTM you have to move manganya
Akweni zabwino zonse osaopa
Mungotenga thomu mpinganjira asogolere chipani tizawina 2025 basi
Kkkk km amai awa
Komati inu a UTM kudzinthetsa mwadzi nthetsako mutiphetsa amatitu akamawona inuyo amalimba mtima koma apa eee tikuntha bas
Utmost for life
Well done come out of tonse alliance