Jomo wamukana Bon Kalindo

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 21 ส.ค. 2024
  • "Count me out" says Jomo

ความคิดเห็น • 21

  • @FachiMalilima
    @FachiMalilima 12 วันที่ผ่านมา +2

    Winiko spresident nanu okuti angasinthe dziko, osimtha dziko simukuwaona, winiko amangoying'alula boma likamalephera kugwira ntchito

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 11 หลายเดือนก่อน +2

    Well done Jomo, mademo a Winiko mutu wake ndi kumanidwa udindo kwa Kalindo.

  • @PrinceKachimanga
    @PrinceKachimanga 12 วันที่ผ่านมา +1

    a JOMO INU...NDINU A MANTHA CHABE😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @BlessingsmadalitsoShumba
    @BlessingsmadalitsoShumba 12 วันที่ผ่านมา

    Ayiso ajomo nanu 😅 mumaikonda inu mcp kuti izivutitsa anthu

  • @katalamajames4947
    @katalamajames4947 11 หลายเดือนก่อน +1

    ndiposo jomoyo machende amake iye migodi yoyitani ndichaniso osasaka ndzochita bwanji chifukwa choti sanapite kuxool mkona akufera migodi yoitanira nanga mene wakulira yeyu azinena dzoyitanira ndi mbuziso imeneyi eti

  • @harrymbelenga8614
    @harrymbelenga8614 2 ปีที่แล้ว +2

    More fire nkharango

  • @mphatso2976
    @mphatso2976 11 หลายเดือนก่อน

    Mene wayakhulila jomoyo mwaona bwaji mau ake dimagulu ugulisa amalawi didalama olomene akuonekela sagakane ndalama jomo upeleke ulemu kwa anthu opephape diwechisilu sukuziwa chimene ukuchita ufela zani

  • @MozesKamwambi-iu4ox
    @MozesKamwambi-iu4ox 11 หลายเดือนก่อน +1

    Ver good magyz

  • @PeacefulWildFlowers-sl8er
    @PeacefulWildFlowers-sl8er 7 หลายเดือนก่อน

    I am warning you 😂😂😂😂

  • @lyiemax
    @lyiemax 11 หลายเดือนก่อน

    That's a big warning, take care don't involve mademo ndi zautsilu za achina Jomo

  • @ThandiePotah-qq6ox
    @ThandiePotah-qq6ox 8 หลายเดือนก่อน

    Mulungu adalitse malawi

  • @JonesChingaya-yf4gg
    @JonesChingaya-yf4gg 6 หลายเดือนก่อน +1

    Iwe Jomo usalowese chibwana, MCP ikumwaza ndalama kugula anthu m'malo mochita zomwe analonjeza lero a Malawi ambiri akuvutika iwo ali busy kugula anthu kut azinyoza DPP pali nzeru pamenepo??????

    • @manuelmalunga8763
      @manuelmalunga8763 3 หลายเดือนก่อน

      Ndipo zoonad koopsa zedi Jomo ndiofoira zedi

  • @user-lt3xl7cv5n
    @user-lt3xl7cv5n 6 หลายเดือนก่อน +1

    Kodi akalindo dziko la malawi mukufuna kuyambitsa nkhondo, alomwe inu mumadzitenga ngati ayani? Mmalawi muno muli mitundu ya anthu ambiri mbiri koma kumanvela alomwe wokha, boma simudzalionaso ndi umbuli wanuwo

    • @JonesChingaya-yf4gg
      @JonesChingaya-yf4gg 6 หลายเดือนก่อน

      Ukamati alomwe ukutanthauza chani? Pafika zinthupa akuvutika nd alomwe okha, sugar wakwerera alomwe okha? Iweyo suziwa kut alomwe ambir anavotera boma ili koma palibe cha nzeru ikuchita. Mind your mouth.

    • @LuciusMaison
      @LuciusMaison 7 วันที่ผ่านมา

      Iwe ndiye ndani kakapetheee ngati iwe

  • @user-wz8jo7fj2b
    @user-wz8jo7fj2b 9 หลายเดือนก่อน

    Zoona d big

  • @DanMhone-iw6xg
    @DanMhone-iw6xg 6 หลายเดือนก่อน

    Koma kunyasaland kwavuta

  • @manuelmalunga8763
    @manuelmalunga8763 3 หลายเดือนก่อน

    Chakwera ndi MCP Mulungu azakuweruzani yekha

  • @mederinausain6913
    @mederinausain6913 11 หลายเดือนก่อน

    Kkkk

  • @AndrewDamson
    @AndrewDamson 11 วันที่ผ่านมา

    Ur lie