ไม่สามารถเล่นวิดีโอนี้
ขออภัยในความไม่สะดวก

HOT CURRENT 14 JULY 2024 |

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 13 ก.ค. 2024

ความคิดเห็น • 97

  • @patrickndojime1632
    @patrickndojime1632 หลายเดือนก่อน +8

    Go on Guy's we wait to see the changes in Malawi eeeee from Bakili muluzi up to know am in RSA because of politics of Malawi throwing as away not thinking of coming back to home eeeeeeeeesh

  • @Yungjoe786
    @Yungjoe786 หลายเดือนก่อน +6

    Chilima was assassinated that's the truth what more do u want to hear?

  • @user-lj8ug5lq8c
    @user-lj8ug5lq8c หลายเดือนก่อน +2

    Guys keep it like this ,this is Hot current we know from those days congratulations

  • @JamesIngeni-ku3qj
    @JamesIngeni-ku3qj หลายเดือนก่อน +2

    Manganya ndi mcp anapha chilima.

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6e หลายเดือนก่อน +3

    Usi si wa UTM. Munamuwona muja amarandira udindo muja? UTM yachita bwino kuwaturuka.

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 หลายเดือนก่อน +2

    Ngozi ija singozi ngozi ,,komanso yonse taona ndimafinso

  • @BambordKabambe
    @BambordKabambe หลายเดือนก่อน +6

    😂😂😂😂😂 chaka chino ndi CHONG'ALURA

  • @JohnNjerenga
    @JohnNjerenga หลายเดือนก่อน +1

    Kkkkk akut ipondeni fadha

  • @paulpaseli6310
    @paulpaseli6310 หลายเดือนก่อน +1

    Apa ndiye mwabwelatu chilungamo chimenecho

  • @EstherChimombo
    @EstherChimombo หลายเดือนก่อน +1

    🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥💯💯

  • @InnocentnMbale-zq8pk
    @InnocentnMbale-zq8pk หลายเดือนก่อน +5

    Times muziwe kuti chilima agwila bwanji ntchito ndi chakwela mu 4years

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 หลายเดือนก่อน +2

    Masapota a UTM tonse tatuluka ku mgwirizano Chifukwa tinkasapota Chilima.Usi alibe masapota.

  • @user-oh9bh1cl3b
    @user-oh9bh1cl3b หลายเดือนก่อน +1

    Well spoken guy's adzimva akawalalawa

  • @clintonhodda9830
    @clintonhodda9830 หลายเดือนก่อน

    Walephera Chakwera kulamulira kuchedwa 4yrs ndipo akhala akungodandaula DPP mmalo mopanga ziganizo msanga

  • @OrtonKabbichi
    @OrtonKabbichi หลายเดือนก่อน +2

    Sizachilendo olo pa ngozi ya ndege ija anachedwanso kukafufuza ayambe kuchotsa ameneo onwe amaenera kukafufuza za ngozi ya ndege

  • @patricksinyala1345
    @patricksinyala1345 หลายเดือนก่อน

    Mtsukuluzi ukulankhula mopusa, kufooka kwa Ussi kunayamba Chilima alimoyo. Ndipo. Chilimma anali atamuzindikila Kale Ussi ukathyali wake.

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h หลายเดือนก่อน +3

    Inu ussi siwa UTM 😂😂😂😂ameneuja ngawa MCP

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 หลายเดือนก่อน

    Chakwera so asamale zomwe wawona Nzake wa kwa merica zija zichitikanso kuno.

  • @symonmakata938
    @symonmakata938 หลายเดือนก่อน

    Changucho chiyambile pa kafukufuku wa ndege inapha chilima kenako the public ikhala ndi changu

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4v หลายเดือนก่อน +3

    Dziko ndilathu osaonesa kutopa azibambo ipondeni thawi ino palibe kuopa ng,alulani basi ng,ambani

  • @user-jk8sh7fh2d
    @user-jk8sh7fh2d หลายเดือนก่อน

    Usi atha ngati nankhumwa sure, olo kuthesako akufuna kukhaulisa manganya coz anamuziwa kuti uyu sitili limozi ndi wa mcp.

  • @JohnmarkNazombe-hi9xd
    @JohnmarkNazombe-hi9xd หลายเดือนก่อน

    Dziko nkumasawukaaaaah!!!!!!!

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 หลายเดือนก่อน +1

    Masapota ake ati omwe atsatire Usi ku MCP. Musanamizane palibe yemwe angavotere MCP true member wa UTM

  • @EfeloYovita
    @EfeloYovita หลายเดือนก่อน

    ngati bola Allience latha ndibwino kukhala opanda president cs chakwela polowa m boma unali mgwilizano maka utm inali ndimavoti ambiri kuposa mcp we must have emergency presidental election

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg หลายเดือนก่อน

    MCP yayambitsa nkhondo yoopsa yokha amalawi sangasangalale nazo izi
    Zotsatila results zangozi kuli ziiiii mpaka pano what do you do

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma หลายเดือนก่อน +1

    Keep it up Guy's ife ndalama tidya koma sitidzawavotela talira kokwana sife opusaso pano

  • @MPHATSOKALUWA-lm2uy
    @MPHATSOKALUWA-lm2uy หลายเดือนก่อน

    Akuchedwa Nd pule yomweyo😂😂😂😂😂

  • @imaculadaAndre-ns1py
    @imaculadaAndre-ns1py หลายเดือนก่อน

    Fiti ndifiti basi awa sangaulule chilingamo kwao ndikunama basi koma ife chilingamo tinachipeza kale

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 หลายเดือนก่อน

    Akuti mbwexe😅😅😅😅😅😂😂😂

  • @catherineKalinga-m4c
    @catherineKalinga-m4c หลายเดือนก่อน +2

    🤩

  • @AishaChipande
    @AishaChipande หลายเดือนก่อน +2

    Chakwela azuzula bwanji pomwe iyeyo anaphaso muzake

  • @EsnartMbalale
    @EsnartMbalale หลายเดือนก่อน

    Ipitilile ndiyabwino coz ikulakhula mosatenga bali

  • @imaculadaAndre-ns1py
    @imaculadaAndre-ns1py หลายเดือนก่อน

    Tamusiyani maganya abakhala komweko adzatiuza zenizeni abawatola zifukwa adzapange sewelo mutu wake chakwera anapha zake chifukwa chaudindo

  • @OfwaMwambila
    @OfwaMwambila หลายเดือนก่อน

    Alot of people re in marriages that ended a long time ago but due to kids u re forced to still living together that's what I think was the case of SKC&usi.

  • @StiveKantiki
    @StiveKantiki หลายเดือนก่อน +1

    Akuyambisa kuchedwa ndi achakwela ndipo ife tinalakwisa kumuika munthu onamizila ubusa Ngati uyu pa mpando

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 หลายเดือนก่อน

    Mbwelera zokha zokha za mcp kkkkkkk koma pankuku!!!!!!

  • @BestonStima
    @BestonStima หลายเดือนก่อน

    Mcp ivutika chifukwa isanalowe m'boma amalawi ankaopa nkhanza za mbiri yawo
    Lero in their 4yrs rule patuluka nkhanza.
    Do you think they can reign???????????

  • @robertnambazo9936
    @robertnambazo9936 หลายเดือนก่อน

    President osaziwachomwe akuchita he is so relaxing President President uyu ndi bubu shatapu zake

  • @SteveKanongwa
    @SteveKanongwa หลายเดือนก่อน

    Koma ma guys inuo hahaha munatopa nalo dzikoli simufunaso zachikape

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h หลายเดือนก่อน

    Manganya ndi wa mcp not utm

  • @johnmhango9405
    @johnmhango9405 หลายเดือนก่อน

    Briefcase parties end just like that.

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 หลายเดือนก่อน

    Uyakhura za chidodoyo ndiye ili mbudzi yoyambisa chakwera samasata zinthu that’s y anyamata ake angomisewera basi.

  • @SteveChapola
    @SteveChapola หลายเดือนก่อน +1

    A mcp chipani chokupha

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 หลายเดือนก่อน

    Sitizalola report. Wonder you are very Intelligent than pankukuyo

  • @GodfryMalishe
    @GodfryMalishe หลายเดือนก่อน

    Salute u guys 😂

  • @MPHATSOKALUWA-lm2uy
    @MPHATSOKALUWA-lm2uy หลายเดือนก่อน

    How many meetings manganya has been attending?? Can he allow to apart from the alliance coz it's obvious manganya it's won't allow

  • @peterchikwakwa8476
    @peterchikwakwa8476 หลายเดือนก่อน +1

    Eeeeeee yankhulani guys ❤

  • @lukedumbula2724
    @lukedumbula2724 หลายเดือนก่อน

    Very true wonder and jona, a PULE akuchedwaa

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w หลายเดือนก่อน

    Pa nkhani yochedwetsa chitukuko, tingomuchotsa next year basi, sali fit Chakwera to be a President.

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 หลายเดือนก่อน

    A Usi si president wanthu,,munthu mkazi wake tamuziwa polumbilitsa mkumazitama kuti ine sindinayendepo ndi mkazi wanga,,muthuyu angayendese chipani

  • @RafiqueChibwana
    @RafiqueChibwana หลายเดือนก่อน +1

    You guys u don't share kamba here really keep it up guys kkkkkkkkk

  • @JaphetSakala-pq4fl
    @JaphetSakala-pq4fl หลายเดือนก่อน +2

    Kuchokela pa ifa ya VP chilima kufikila pasiku la mavoti UTM ILI PA TOP ONE. or Dpp ndi mcp ita phatikizana. UTM IKUTENGA BOMA TIZAIPEPESA NDI VOTE.

  • @SheenahMwalabu-iz3pr
    @SheenahMwalabu-iz3pr หลายเดือนก่อน

    Lero munabweratu a jonah kkk wonder akuti back to sender eee Chakwera dzimvere mumtolo

  • @JuuuKomba
    @JuuuKomba หลายเดือนก่อน

    Eni ake a UTM ndifeyo ovotafe Tatupu ndife awowo dyela Paolo asaleko tilibe nawo film

  • @PartsonKamkuzi
    @PartsonKamkuzi หลายเดือนก่อน

    Osawopa ayi a malawi ambiri tikuyang'anira inu kut muziyakhura mosawopa apa

  • @CosimassShyman
    @CosimassShyman หลายเดือนก่อน

    Wakulu andevu zamwayi amayankhura Chichewa cha boo

  • @YamikanChirwa
    @YamikanChirwa หลายเดือนก่อน +1

    Ng'alula iwe

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂😂 anyamata inu mwandisangalatsatu chikufunika ndichimenechi osanyangerera kulankhula chilungamo kubandaluka basi sizoopaso ayi

  • @user-mj2te7vl6p
    @user-mj2te7vl6p หลายเดือนก่อน

    Kaya DPP kaya ilibe ndalama iwinabe 2025

  • @user-rd9pd9hr2l
    @user-rd9pd9hr2l หลายเดือนก่อน

    Inuyo munabwera ngati coming 🔥

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo หลายเดือนก่อน

    A pule ayamba kupemphera ku CCAP kamutu kataya

  • @joneskalitsilo6556
    @joneskalitsilo6556 หลายเดือนก่อน

    Exactly Wonder bambo wanzelu amakonza mavuto amu nyumba mwake not kutuluka nkumakadandaula panja or kubwalo kuti mnyumba mwanga sitikudya ana anga sakuvala bwino, sitikudya bwino! Nde ana Inu muzivala bwino, muzidya bwino, ukuganiza kuti anawo azitenga kuti?

  • @peternashyo9850
    @peternashyo9850 หลายเดือนก่อน

    Nkhaniyo ndiyoona, a President akugona kwambiri pachiongolero, dziko silingatukuke ai

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 หลายเดือนก่อน

    Anaphedwa ku Mwanza aja ndiochepa.pano ayesetsetsa kupha ambiri.athakati sadzasintha.Malawi Congress of Perishers

  • @DarlingtonMaya
    @DarlingtonMaya หลายเดือนก่อน

    Gyz mmmatha

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y หลายเดือนก่อน +2

    MCP ndi Yakupha

  • @PartsonKamkuzi
    @PartsonKamkuzi หลายเดือนก่อน

    Iwe pankuku osamayakhura mowopa apa

  • @BENSONRANGWANI
    @BENSONRANGWANI หลายเดือนก่อน +1

    Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach

  • @MuhamadYassin-ye4hn
    @MuhamadYassin-ye4hn หลายเดือนก่อน

    Mumakwana mabigi

  • @Amos-tr6ro
    @Amos-tr6ro หลายเดือนก่อน

    Koma makosana inu MMM mwanditha keen on on our behalf

  • @jackmambo2638
    @jackmambo2638 หลายเดือนก่อน

    Kod amaphang’ombe ali kut😂😂

  • @user-cf9yz3ei5o
    @user-cf9yz3ei5o หลายเดือนก่อน

    Did. Mcp ask Afford

  • @StiveKantiki
    @StiveKantiki หลายเดือนก่อน

    Aganizq bwanji mwakuya kuposa anthu zosatheka ubongo unatha chifukwa ankadya zopasidwa Za chaulele

  • @user-tg7ni7wh2c
    @user-tg7ni7wh2c หลายเดือนก่อน

    Eeh 😂

  • @johnmhango9405
    @johnmhango9405 หลายเดือนก่อน

    A kaliati ndi a njawala nzokonza izi, akufuna apange handpick Kabambe, can't you read between the lines? Typical of atsogoleri a dyela.

  • @user-fd1tu6ku1r
    @user-fd1tu6ku1r หลายเดือนก่อน

    Emusipi ofunika isale yokha. Anthu woipa awa

  • @frankdomingo1109
    @frankdomingo1109 หลายเดือนก่อน

    Decisiveness palibepo

  • @yusufjab786
    @yusufjab786 หลายเดือนก่อน

    Ndipo inuyo kumeneko mumaitha 😂😂😂 akuchedwesa ndi chakwera

  • @user-cf9yz3ei5o
    @user-cf9yz3ei5o หลายเดือนก่อน

    You. are. wrong. it. Is. People. at. the. grassroots. who matters not individuals

  • @PartsonMdeza
    @PartsonMdeza หลายเดือนก่อน

    🤣🤣🤣 iponden fadah kkk

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn หลายเดือนก่อน

    Ofufuza ngozi akuti, khoswe akakhala pakhate sapheka

  • @SteveChapola
    @SteveChapola หลายเดือนก่อน

    Asiyeni atuiuka chifukwa chake achakwera apha chirima ndipo ndizoona

  • @lastonmasoatenganji-bs5gf
    @lastonmasoatenganji-bs5gf หลายเดือนก่อน

    Osamayiwala ku mudzi kaamba kokomedwa ndi maidyaidya chifukwa tsiku Lina amadzakusandutsa mtsamiro wa mfumu ikadzamwalira.

  • @michealchaomba9761
    @michealchaomba9761 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂 President wake utiyo mukudikira kuti azuzuleyo

  • @MarthaBanda-ye4pt
    @MarthaBanda-ye4pt หลายเดือนก่อน +1

    Koma Wonder Ati kukura mtima 😂😂😂😂🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥uyatseni basi ng'alulani basi

  • @user-ru4px8os2v
    @user-ru4px8os2v หลายเดือนก่อน

    Anthu ake ndi chimwendo banda,howeh mkaka,zikhaleng'oma ndiomwe akuyenela kuchoka

  • @ThandiMbewe
    @ThandiMbewe หลายเดือนก่อน

    Musamamuzile zochita president, yekha samawona???

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus หลายเดือนก่อน

      President wake uti
      Ma comments 100 wa MCP yekha .chita manyazi😅😅

  • @SteveChapola
    @SteveChapola หลายเดือนก่อน

    Chakwera ndiwofoka koma kumagaanthu chimenecho ndiye chitukuko.chake

  • @NdazionaKumcheza
    @NdazionaKumcheza หลายเดือนก่อน

    Ine dakalira malemu za chipani tizitaye uko aaa

  • @YusufuUsumani
    @YusufuUsumani หลายเดือนก่อน

    agaluwa alilimosi ndi chachera

    • @JudithMaida-ug4oi
      @JudithMaida-ug4oi หลายเดือนก่อน

      Mumatiimilira big hands for you

  • @PartsonKamkuzi
    @PartsonKamkuzi หลายเดือนก่อน

    Osamayakhura ngat akupatsani za lent kung'alura basi ukuva iwe ndevuzamwayi !!

  • @user-ql8nf2vb8s
    @user-ql8nf2vb8s หลายเดือนก่อน

    Inu a times muyang'ane mgwirizanou kuchokela mmbuyo inunomwe mumaunikira mgwirizanou mmene umayendela chilima asanamwalile asiyeni ausi ali ndigululawo odya zake alibe mulandu

  • @MuhamadYassin-ye4hn
    @MuhamadYassin-ye4hn หลายเดือนก่อน

    Mumakwana mabigi