GURU LINA LONYASIDWA LAWOPSYEZA A PRESIDENT CHAKWERA LERO KUTI ACHOTSE PA MPANDO A ZIKHALE NG’OMA

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 9 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 51

  • @munashemoyo4190
    @munashemoyo4190 28 วันที่ผ่านมา +6

    Kumkuyu iwe galu kwabas iweso ukuyenela kuchoka sutha ntchito ai mbalame yenyen gwape

  • @jacomw5797
    @jacomw5797 28 วันที่ผ่านมา +7

    Kunkuyu amazitenga dolo poyankhula while ku immigration zinthu sizikuyenda

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 28 วันที่ผ่านมา +2

    akunkuyu ndi a chakwera chonde muwuzane kuti pantumbo pa chamanu zitsiru za anthu lino ndi dziko kapena mudzi wakwanu boma la zitsiru zokha zokha

  • @Yoxym
    @Yoxym 28 วันที่ผ่านมา +3

    Achoke 💪💪💪💪💪💪💪💪

  • @user-ii2sh1mz3r
    @user-ii2sh1mz3r 28 วันที่ผ่านมา +1

    I think the problem we have with our president is , ali soft kwambiri , and ali ndi chifundo kwa even ma ministers ,so chimene ayenera kuziwa church ndi dziko ndi zosiyana ,Iwo asamanyengerere munthu Kaya akuoneka bwanji,

  • @ChristopherMakamo-ky4pq
    @ChristopherMakamo-ky4pq 28 วันที่ผ่านมา +3

    Apule achoke basi

  • @amosmuluwane4182
    @amosmuluwane4182 28 วันที่ผ่านมา +1

    Azimaywa amazipangitsa okha akasankhidwa palibe chomwe amachita mwachitsazo phungu wa ncheu bwanje North akhala paunduna zaka zonsezi koma dela lake ndilovesa chisoni pamudzi omwe amachokela mayi amenewa school idasasuka denga Chaka chatha koma mpaka panopa school iyi sinakhomedwe amene mumadutsa pamudzi wa akaiya kupita ku balaka kapena kugolomoti mundivomeleza phunguyi ndi nase chaola ndoko

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 28 วันที่ผ่านมา +3

    Ma passport a fake a Nic Chakwera

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani5697 27 วันที่ผ่านมา

    Koma pamenepa pothandiza school President Chakwera timuyamikire osamangosusa zili zonse chifukwa cha ndale pena zabwino kumayamika so zonse munthu sangakhale 100%

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi 28 วันที่ผ่านมา +1

    Chikangawah party ichoke basi

  • @BillyKalambo-jx3vf
    @BillyKalambo-jx3vf 26 วันที่ผ่านมา

    Vuto si zikhale ng'oma koma galu uyu otchedwa Chakwera tiziti iyeyu sakuona kuti immigration zinthu sizikuyenda contract angapereke kwa mwana wake Chenjela Nick ndi makutu akowo okhala ngati bowa masiku akuthera mbuzi iwe

  • @ibrahimalfred6539
    @ibrahimalfred6539 28 วันที่ผ่านมา +1

    Achosedwe watikwana galu ameneyo even chakwera achokeso sitifuna .. futso koma zikhale ng'oma azalola kuti achoke si nankha mcp yakwawo nankha kkk

  • @user-wd9yd1bg9n
    @user-wd9yd1bg9n 27 วันที่ผ่านมา

    Anthu sakuziwa zimene akufuna it's straight forward isue chajwera achoke basi

  • @VictoriaWilly
    @VictoriaWilly 27 วันที่ผ่านมา

    Kunkuyu nayenso achoke, onse achoke akuononga dziko la Malawi. Tatopa ndi boma labodza ili

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 27 วันที่ผ่านมา

    Apm akubwera kudzakonza dzikoli tazunzika mokwana 4yrs ngati 400 yrs?

  • @user-fy7qk6kk5s
    @user-fy7qk6kk5s 27 วันที่ผ่านมา

    Chakwerayonso achoke palibe chichita iye panopa chilichonse ndichosokonokera

  • @Dickies-mk8cd
    @Dickies-mk8cd 27 วันที่ผ่านมา

    Ufune oti uwapusitse Chakwela wamva

  • @DalitsoAlufeyo
    @DalitsoAlufeyo 28 วันที่ผ่านมา +3

    Ndipo zoona

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 28 วันที่ผ่านมา +2

    boma la zitsiru zokha zokha ili zigawenga

    • @MillyKachepa
      @MillyKachepa 27 วันที่ผ่านมา

      Chikangaws😂😂😂

  • @MosesMkandawi-e2v
    @MosesMkandawi-e2v 23 วันที่ผ่านมา

    Palibe chomwe akuchita zikhale ng'oma pakuti iye ndi chakwela ndi zigawenga nde akuba okhaokha safusana kuti chithu ichi wachitenga kuti pomwe ose ndi akuba,,, koma chomwe amafusana ndikuti kodi ichi unakaba kuti bas,, ndee chakwela sangamuchotse zikhale ng'oma pakuti zonse zimene akupanga iye amapanga limodzi ndi chakwela Kuba kupha katangale akupangila limodzi

  • @PatrickChagaka
    @PatrickChagaka 27 วันที่ผ่านมา

    Awatu palibe chomwe akupanga boma lawoli onse ndizitsiru zokhazokha zikhaleyo sangasokoneze zinthu payekha alipamodzi

  • @user-ev4or2kg4z
    @user-ev4or2kg4z 28 วันที่ผ่านมา +2

    A CDED please now take things seriously
    Please we are suffering like God created people from to suffer

  • @PanganoChilambe
    @PanganoChilambe 27 วันที่ผ่านมา

    Ok, kondi munthu angapite kusuku ya ukachenjede asanate ku pulaimale? izo ndindale zaku Malawi mukafu kupitiriza kumba mumatenga omphunzira amenewa why thandinzo yanuyo siyambe muchipatara olo kundende,ku pulaimale? Osatimvetsa mutu ife Malawi timudziwa musateye ndalama zoti ana amasiye asamalike ndeye nkhumbo langa ngati Malawi. Koma ndati mudziwe kuti mawa silero.

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 28 วันที่ผ่านมา +1

    Bora pamenepo achokedi saziwa ntchito amalawi tikuvutika

  • @MirriamKambale
    @MirriamKambale 27 วันที่ผ่านมา

    Boma mpaka kumapanga passport ya feki?Nigerian mmodzi kumaposa boma la malawi?coz feki passport yopangidwa ndi Nigerian individual ilibwino kuposa yopangidwa ndi boma la Malawi.

  • @KawawaIbrahim
    @KawawaIbrahim 27 วันที่ผ่านมา

    Kodi chifukwa chani maudindo kumangopasana anthu oti saziwa ntchito

  • @AREFRIEDNELSON
    @AREFRIEDNELSON 27 วันที่ผ่านมา

    😂😂😂😂 ndalama kulibe nanga zomwe akuba m'boma akuba kkuti ndalama zoooooo tatiwuzani

  • @user-fg1me1un8p
    @user-fg1me1un8p 28 วันที่ผ่านมา

    Keep it up comrades atule pansi udindo

    • @MoosahChikwakwa
      @MoosahChikwakwa 27 วันที่ผ่านมา

      😂😂😂😂, Achoke Achoke!

  • @NosparPalamelagee
    @NosparPalamelagee 27 วันที่ผ่านมา

    Iweso kumkuyu uchoke

  • @user-wi9pe2hz7e
    @user-wi9pe2hz7e 28 วันที่ผ่านมา

    Enanu mkumat boma nd lomweli kma likulephera kukonza zinthu shame😢

  • @MarthaBango
    @MarthaBango 27 วันที่ผ่านมา

    Anthu amatopatu amafika poti topi 😂😂😂😂

    • @PatrickChagaka
      @PatrickChagaka 27 วันที่ผ่านมา

      😂😂😂😂😂

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r 27 วันที่ผ่านมา

    Ayende basi aaaa atikwan

  • @watsonmhango8794
    @watsonmhango8794 28 วันที่ผ่านมา

    Boma la Chakwera zavuta ndithu 😂😂😂😂😂

  • @JamesGondwe-l6b
    @JamesGondwe-l6b 28 วันที่ผ่านมา

    Boma, limapanga chidodo kwambiri, pop anga ziganizo.

  • @sparkdymon3429
    @sparkdymon3429 28 วันที่ผ่านมา +2

    Achoke kamajeketi zikhale Ng,oma foseki Thabo chakaka nayeso alibali ya MCP sakutithandiza ayi nayeso foseki

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo 28 วันที่ผ่านมา +2

    Kamajekete apite 😮

  • @kingthymus4613
    @kingthymus4613 28 วันที่ผ่านมา +1

    makosana😋😋😋😋

  • @user-re7fo3be2z
    @user-re7fo3be2z 28 วันที่ผ่านมา

    Achoke kumene

  • @thomasbodo4099
    @thomasbodo4099 28 วันที่ผ่านมา +2

    Boma lalephera so mkuyu asamati president razarus mphamvuzo tinangomubwereka osati adzitumbwanazo apa

    • @JafalihMitawa-u2d
      @JafalihMitawa-u2d 28 วันที่ผ่านมา

      Mmmh nawesotu uzilankhula bwino wava, alindi mphanvu basi Chakwela.

  • @user-bg5oe1sl8n
    @user-bg5oe1sl8n 28 วันที่ผ่านมา +1

    😂 ndpo live

  • @AllieJonassi
    @AllieJonassi 28 วันที่ผ่านมา

    Achakwela awombeledwe

  • @PatrickMailos-j6u
    @PatrickMailos-j6u 28 วันที่ผ่านมา

    Athutu amanena kuti mcp sizithu

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 28 วันที่ผ่านมา

    Musanapange upload muzimvera kaye zinthu zanuzi, this is very unprofessional.

  • @LasieMolebatsi
    @LasieMolebatsi 28 วันที่ผ่านมา +1

    Anyamuke

  • @adamabiyen5079
    @adamabiyen5079 28 วันที่ผ่านมา +1

    Bolan pamenepo